M’mwambamu ndiye madzi alimo ndipo atsakamukamo ndithu — atero a zanyengo
Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwa nyengo m'dziko muno ya Department of Climate Change and Meteorological Services (DCCMS) yati kumwamba kudakali madzi amvula ochuluka kotero mvula yamabingu ikhala ikugwa m'madera ochuluka mdziko muno kufikira lachiwiri.… ...