
FAM yatchetcha ma bwalo asanu nthawi yothaitha
Bungwe loyendetsa mpira wa miyendo m'dziko muno la Football Association of Malawi (FAM) kudzera mu komiti yake, lakana kuvomeleza ndi kuika pa mndandanda ma bwalo asanu mwa ma bwalo oti ayambe kugwiritsidwa ntchito pomwe masewelo… ...