![water tap](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2015/10/water-tap-235x176.jpg)
Akweza madzi ku Blantyre
Ngati simufa ndi njala, ndiye mwina ludzu kapena kolera zitha kukuphani. A bungwe la Blantyre Water Board alengeza kuti madzi awo akwera mtengo. Mu chikalata chimene bungweli latulutsa, a boma tsopano awapatsa chilolezo choti madzi… ...