Siyani kuchita nawo ziwonetsero, zilibe phindu – a Malawi alangizidwa
Ngakhale kutenga nawo gawo pa ziwonetsero zili zonse uli ufulu wachibadwidwe, gulu lina lomwe likudzitchula kuti ‘Abwenzi a Atupele Muluzi', lalangiza anthu m’dziko muno kuti asiye kutenga nawo gawo ponena kuti sizikubweretsa phindu ku dziko… ...