Bungwe lowona za akatswili pa ukadaulo wa makina a ma kompyuta ndi zipangizo za makono la ICT- Association of Malawi (ICTAM) lati lili lokozeka kuthandiza ndi ukadaulo udziwi wawo ku bungwe lowona za anthu otuluka… ...
Articles By Mphatso Khutcha Richard
Phungu wa wa dela la ku mmwela cha kum'mawa m'boma la Salima a Mike Ng'ombe Mwawa awatulutsa m'nyumba ya malamulo ndipo ati adzabwere pa 13 malichi kamba ka kuyankhula zosayenera mnyumba ya malamulo mu zokambilana… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera ati ndi nthawi yabwino tsono kuti makolo azindikire za ubwino okhala ndi ana omwe akhoza kukwanitsa kuwasamala komanso kuwaphunzitsa ndipo ati maphunzilo kuti ayende bwino akuyambila pa zipangizo,… ...
Mighty Mukuru Wanderers Football Club has appointed new members in its supporters' committees to serve for a period of two years. A letter dated 21st February 2024 and signed by board secretary Chancy Gondwe states… ...
Bungwe lolemba nzika la National Registration Bureau (NRB) lati silisinthila a Malawi omwe akufuna kusinthitsa tsiku lobadwa chifukwa tsiku lobadwa pa chiphaso cha nzika ndilotetezedwa. M'malingana ndi chikalata chomwe bungweli latulutsa pa 19 febuluwale chotsimikidwa… ...
Yemwe anali m'modzi mwa akulu akulu ku chipani cha Democratic Progressive DPP a Uladi Mussa ndipo pakali pano adalowa chipani cha Malawi Congress (MCP) ati iwo atafatsa kuwelenga malamulo a chipanichi tsopano ali ndi mangongolomela… ...
Apolisi mu mzinda wa Lilongwe amanga amuna asanu ndi m' modzi chifukwa choba matumba a 78 a mtedza, akina osokera ndi ma sikelo oyezela okwana asanu, zonse za ndalama zokwana 10.8 miliyoni kwacha Malingana ndi… ...
Three Malawian youths who went to Israel to work in farms have been deported to Malawi after they ran away from their farms to seek employment elsewhere. This is according to Lions Recruitment Agency director… ...
Mtsogoleri wa mbali yotsutsa boma wa DPP kunja kwa nyumba ya malamulo a Mary Navicha, ati atengela ku nyumba ya malamulo nkhani yokhudza kalembela wa voti kuti akawunikenso lamulo logwiritsa ntchito chiphaso cha unzika poponya… ...
Yemwe wangosankhidwa kumene kukhala mtsogoleri wa aphungu otsutsa boma wa chipani cha Democratic Progressive (DPP) m'nyumba yamalamulo, mayi Mary Navicha akana kulankhulapo m'nyumbayi pa zomwe mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera analankhula pomwe amatsekulira mkumano wa… ...
Mcdolnad Nginde' Mtetemela has put pen to paper as head coach for newly promoted Super League side Creck Sporting Club. Creck Sporting Club, formerly Kawinga FC, have confirmed the appointment. The coach will be assisted… ...
Dziko la Malawi pamodzi ndi mayiko ena onse padziko lapansi lachiwiri pa 13 Febuluwale limakumbukira nawo tsiku la "Condom'' pamene akatswiri ati a Malawi ambiri sakutha kupeza mwayi wa makondomu mwachangu. M'modzi mwa katswili owona… ...
Atatsanzika Mark Harrison, timu ya mpira wa miyendo ya Mighty Mukuru Wanderers tsopano yalemba mphunzitsi watsopano ophunzitsa osewera mu timuyi yemwenso anaphunzitsapo timu ya Nyasa Big Bullets Nsanzurwimo Ramadhan yemwe kwawo ndi ku Burundi. Malingana… ...
Lilongwe based giants Silver Strikers have made their third signing ahead of the 2024 season, roping in Dedza Dynamos forward Charles Chipala. Chipala on 13th February completed his move to the Area 47 based team… ...
The first deputy speaker in Malawi's National Assembly Madalitso Kazombo has emphasized that Democratic Progressive Party (DPP) Members of Parliament's action of blocking the entrance of Parliament Building cannot intimidate the Speaker Catherine Gotani Hara.… ...