JB dragged to court


Joyce Banda

Fugitive former President Joyce Banda has been dragged to court, Malawi24 can report.

Joyce Banda
Banda: Taken to court.

According to reports, the former Malawi leader is being summoned to appear before court after successfully dodging the dock this far having lost the presidency.

According to court documents that we have seen, security company G4S through its lawyers has sued Joyce Banda led People’s Party (PP).

Among other possible defendants whom G4S has issues with is the former president, Joyce Banda, and other PP top dogs.

According to reports, the people are being sued for failing to pay G4S money for the services that the security company rendered.

61 thoughts on “JB dragged to court

  1. munthu aliyese osokoneza ayenela kumangidwa musamulekelele anthu apite kundende JB dyela ndi chuma kusawusa ntundu wa Malawi,she is selfish idiots JB she must go to jail

  2. munthu aliyese osokoneza ayenela kumangidwa musamulekelele anthu apite kundende JB dyela ndi chuma kusawusa ntundu wa Malawi,she is selfish idiots JB she must go to jail

  3. Kkkk koma government. Yolowera imeneyo? Tiziti mulandu ndiwina kt akabwera kudzayakha izi muzamuzengenso yanutu milandu, mumawopa kumuyitanisa nokha

  4. Tired with politics of Malawi, a peaceful country in disguise, full of evil and develish deeds, to hell with these sons of Satan who rule us instead of leading us

  5. Tired with politics of Malawi, a peaceful country in disguise, full of evil and develish deeds, to hell with these sons of Satan who rule us instead of leading us

  6. l foresee blood running in malawi ndale zomanganazi zachikale kodi mukumuopa mayiyu ngati ndi amene akukulephelesani to deriva nkhani ya chitukuko bwanji? pomwe okuba mukudya nawo limodzi hands off pa ama

  7. JB in real trouble. Will she come back with all these law suits?

  8. JB has a case to answer,not only to G4S but also to the Malawiwians for stealing public funds which could help to lessen abject poverty which has stagnated in them.

  9. JB has a case to answer,not only to G4S but also to the Malawiwians for stealing public funds which could help to lessen abject poverty which has stagnated in them.

  10. idiot calling Jb fugitive makes you fake journalist, the case against her is electioneering because we have 18 month to the election, only fools like you can’t see, milandu yazisankho iyi ilibe malire or mathero, pano tili kuyandikira Ku zitsakho ndiye ati asegule mulandu opanda pache ati kuputsisa amalawi, this case is to waste our tax payers money, pano DPP imanga wotsutsa aliyetse to black mail them, Joice Banda has all file against DPP and Bingu. Fool the fools

  11. idiot calling Jb fugitive makes you fake journalist, the case against her is electioneering because we have 18 month to the election, only fools like you can’t see, milandu yazisankho iyi ilibe malire or mathero, pano tili kuyandikira Ku zitsakho ndiye ati asegule mulandu opanda pache ati kuputsisa amalawi, this case is to waste our tax payers money, pano DPP imanga wotsutsa aliyetse to black mail them, Joice Banda has all file against DPP and Bingu. Fool the fools

  12. Kodi ife athu ndimaso,ngati ameneyi samangidwa!,kulibwino atsogoleri anthu asazanenenso kuti akuyesesa kuthana ndi katangale kuno kumalawi.Sibwino kupitiliza kunamiza amalawi omwe akuvutika mwazaoneni kuti mukuthesa katangale.yes mutha kunena momwe mungathele chifukwa mukudya ndalama zankhani nkhani zamisonkho yathu,koma muganizile yemwe akupeleka msonkhoyo kuti mapezedwe ake ndiwotani.Tsokatu munthu odyera amphawi.Jb akufunika ndithu.

  13. Kodi ife athu ndimaso,ngati ameneyi samangidwa!,kulibwino atsogoleri anthu asazanenenso kuti akuyesesa kuthana ndi katangale kuno kumalawi.Sibwino kupitiliza kunamiza amalawi omwe akuvutika mwazaoneni kuti mukuthesa katangale.yes mutha kunena momwe mungathele chifukwa mukudya ndalama zankhani nkhani zamisonkho yathu,koma muganizile yemwe akupeleka msonkhoyo kuti mapezedwe ake ndiwotani.Tsokatu munthu odyera amphawi.Jb akufunika ndithu.

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading