Dan Lu ayanika mimba ya mkazi wake pa m’mbalambanda


Oyimba otchuka mdziko muno ndi nyimbo za chamba cha Afro, wazizwitsa mtundu wa a Malawi pamene wakhala mMalawi mmodzi yemwe waika zithunzi za mimba ya mkazi wake pa Intaneti.

Anthu ambiri ati zomwe wachita oyimbayu ndi kunyazitsa chikhalidwe cha amalawi komanso kulaura.

Oyimbayu yemwe watchukanso kwambiri ndi nyimbo yake ya “Sweet Banana”, adalimba mtima kuyiwala chikhalidwe cha ulemu cha chimalawi pamene lachisanu adaika dzithunzi dza mkazi wake Emmie Kamkweche koma dzovula mimba yonse ili padagu pa tsamba la macheza lija la facebook.

Dan Lu wautsa mkangano pa Intaneti.

Malingana ndi mwiniwake Dan Lu, yemwe dzina lake lonse ndi Dan Lufani, poti iye adachilimika kuyimitsa Emmie iye wati ali tcheru kudikira kuti akhale bambo a mwana yemwe akumuyembekezerayo, pamene awiriwa akuoneka okondwa zedi ndi kuyimaku.

Koma malingana ndi anthu ena amene akhala akuikapo maganizo awo pa tsambali, akuonetsa osakondwa ndi mchitidwe umene oyimbayu wachita poti wayalutsa mkazi wake komanso wanyazitsa chikhalidwe cha ulemu cha chi Malawi.

Malingana ndi macheza a pa gulupu ya whatsap yomwe Malawi24 yawona, yomwenso Emmie ndi mmodzi mwa ma membala, zaonetsa kukwiya kwa anthu pamene anafunsa mafunso mzimayiyu chifukwa chimene achitira izi poti pali anthu ambiri otchuka ndi a ndalama zochuluka mdziko muno koma safika mlingo uwu, koma mkazi wa Dan amangoona ma uthenga ndi mafunso koma samayankhapo kanthu.

Gulupuyi yomwe ndi ya azimayi okhaokha, afunsa Emmie ngati mimbayi ili yoyamba ndipo kuti ndi ndani uyo adapereka malango kwa awiriwa pa tsiku la ukwati wawo womwe udachitika mchaka cha 2016.

“Koma kudziwika kuli apo koma abale ulemu ndi ofunika, ndi ndani adakulangizani koma?”

1,002 thoughts on “Dan Lu ayanika mimba ya mkazi wake pa m’mbalambanda

  1. chitsilu ndi mkaziyo. iye angamalolere zopusazo. akuziyalusilanji.

  2. nothing bad @ all its just celebuleting as wel to everybody did whn he pregnate his loved one n if w can see vry wel to tht picture vry z nothing wrong i see on it even my kids i can show them

  3. palibe vuto pamenepo akunyadila mimba ya nkazi wake kapena kuti akunyadila mwana wake azabadweyo mukanena za chikhalidwe munama ndi chiwalo chiti chobisika wachisiya pa ntunda? mimba sichiwalo chobisika and this z not old days evrythng now z changing evryday mukafuna Zachikhalidwe muzikapanga ndi oyimba akumuzi not Dan lu ndi oyimba wapa town ameneyi simungafanane zochitika.

  4. ayi zawonjeza ife kumalawi kwanthukono zimenezi kulibe ndipo ine ndili ndi dzaka 29,,,,ndikuyamba kuona malodza ngati awa..nde amati anthu akawona nde atani…iiiiiiiii ayi ndithu mamawo zina bwezi akukanako olo kufuna kutchukako….

  5. Kkkk ee mfiti zonnse zokudya makanda zikukha dovu koma ndiiithu! Simungaphwasule chomwe mulungu walenga mwaaaawuuupoooondaaaaa

  6. a dan amanu adakati aziyika pantunda mimba yako adakawatengela otani?uwu ndiuchitsilu tisakambe mokunyengelelani mwana wobadwayo adzakhala otani?adzahadzakha

  7. MCHAWA UYU MIMBAYI SIYAKE TIZITI MONSE MUJA SAMACHINDA KUTI IKAKHALE MIMBA YOYAMBA? APA MPAMENE NDAKHULUPILIRA KUTI ACHAWANU AKAKUZINGANI MBOLO KUBELEKA KUMAKUVUTANI.

  8. MCHAWA UYU MIMBAYI SIYAKE TIZITI MONSE MUJA SAMACHINDA KUTI IKAKHALE MIMBA YOYAMBA? APA MPAMENE NDAKHULUPILIRA KUTI ACHAWANU AKAKUZINGANI MBOLO KUBELEKA KUMAKUVUTANI.

  9. Kuyaluka kumeneko mn ine ndimakufilani mm km izi zokha ndiye ndizausilu pa ntundu wa amalawi ngati kuno Ku cape town south Africa ndiye sizachilendo km kumalawi mwawonjeza mn km ndimakufilan zandinyasa ndizomwez

  10. Kkkkkk kuteloko amayi akewo sakukhulupilira kuti atenga miracle mimba pakana kumangowawonesa ndi ana omwe heheheeeeee kma kuti Hoooooooooooooooh

  11. This is bustard, Malawi ndi Malawi,u can’t charge like America, if u want go to America u murder fucker ,u showing kinds bad example

  12. Palibe chifukwa apa yose bho man D……
    Ogwirira azimayi ndi a tsikana osamawayika pamtanda sanya bwanji??????kusowa zodzudzula eti

  13. Enanu mukutanthauza kt Dan ndiopambana kwambiri km iyeyo alibe umunthu ndipo anthu podzudzula samaopa maonekedwe kapena chuma ngakhale kutchuka km zonyasa zakezo asamaike pa gulu bwanji atenge nkukaonetsa mako ake ndil ankaziyo

  14. Ngati amafuna kuti tisayankhule pa zolaula zaozi sanakaika pa public platform, akanakaika kuchipinda. Sikuti pakudzudzula nkhalidwe woyalukawu ndi jealousy koma kumukonza kuti asazapangenso. I for one have got nothing to be jealous about Dan Lu, he has lived a shameful life. I appreciate his talent koma mwaganiza mopelewera. Ena mukuti culture yathu ikusintha nde tizingoona zomwe zizichitika, asa! Ine nde ndikhala mmodzi mwa amene titamenye nkhondo yoteteza chikhalidwe chathu. Aliyense amene wasangalala ndi photo imeneyi ndiwachimasomaso. A well behaved lady can’t expose her pregnancy like that. Under the control of someone but not God Almighty. Go ahead and prostitute your bodies like that but know that Mkwiyo wa Mulungu udzaweluza onse opanga zochimwa ndi amene amasangalala nzauchimo ndikuzilimbikitsa zauchimozo. Think about the Glory of God before you act, write and say anything. Dan Lu is so immature.

  15. Inu mungoti nyonyo apa chikhalidwe chake chiti inu mimbayo mwampasa ndinu? Simesa ndiyankazi wake chimizi chani, ngati simmamfila dan lu khalani ife timamfila he is our seleb and to a seleb thats wat ayenela kumapanga wachimizi khala ndichimizi chakocho we love u dan lu big up

  16. Malawians mind ur own business. This z life of celebs.maybe it was just a photo shoot featuring a certain magazine.mudziyamkhula m’mene mungatukurire dziko lanu instead of minding other pipos business.

  17. Akuziyetsa dolo coz wapereka mimba????mmidzimu mphwanga muli ma memba anzako ali ndi ana 11 koma samatumbwa choncho,,,,watch out

  18. tazilimbanani ndi george chaponda wakubelani ndalama za chimanga uja,musiye dan lu ndi sweety banana wake ndi sweety banana junior!muneneni momwe mungathele koma muzigonabe ndi njala

  19. Inu musamuykire ku mbuyo ndiwausiru uyu amadzimva, we r Malawianz not Americans, mwina ndikuyamba kupanga mimba, akunyaudira ndani? Chachilendo nchani apa? Ifeso timatha

  20. It’s time of division and union in specific divisions.Of the same feathers flock together.24:15 Joshua,life is full of choices depending on both spiritual and physical realms we are present.

  21. Ngakhale ndapeza nkhaniyi anthu muta commenter kale ineyo mbari yanga ndineneko Bambo Dan ngati chili chamba pepani mwayalutsana nazo komanso Mmene wapangila apapa mmmm ndukaika ngati umaganiza mwaumunthu, ndipo mwana angakupose , Iweyo chachilendo ukuona kuti ndichani chomwe wapangila zopusazi? ngati umaona ngati upitiliza kutchuka apa nde wapusa, Taona anthu ife osati nyasi zanuzo, kapena unadya chamba chambiri sumadziwa kuti u kupanga chani? Koma simudzachiza nokha akazanuwo uchitsiru wake umene mwaonetsa apau, bola mawa musawauze kuti ayende mbulandatu akaziwo, Muyaluka nazotu zakupezani mochedwa Eti ndinu Achitsili mwamva Abambo inu Dan

  22. Ziwanda bansi., uchisiru.,chamba,mowa,ma drugs,pansi pa nyanja/usatanic bansi…..thats stupid a dan ndi kachibwenzi kanuko nde mukuwawonetsa ndan…. alipo samaiwona mimba ….nde mukufuna ife tikaiwona mutitani mutilowetse? Munya mukawauze amene akutumaniwo..zamanyi.,…!

  23. inu aulemunu osangokhala bwanji mwangotengela matchasi bwanji mwinaso ndi olowola munasonkha nao pangani zanu mwanandiosowatu kena tizatokota za inu zachikale basi

  24. amalawi kusowa zochita ….chukukhudzani nanga chani ….mukhala ngati mimbayo wayitengela ku lodge bwanji ,mesa ndiyanyumba mwake……

  25. To be honest i see no problem with that plus they are not the first malawians to take pictures of the baby bum . Its art abale plus memories to their new born . Get a life

  26. Idk why most of yall fuzzing about those pictures anyway…..to some of us they are normal and we dgaf.. Koma enanu kuzitengela pa mwamba!!!! Malawians thou.. Am done with yal!

  27. Amalawi palibe nkhani APA,,,,kodi kungoonetsa mimba mwat nditchimo,,kkkkkkk zikusiyana pati ndikuiona ili munsalu?Zaziiii basi

  28. Time changes.Nthaw imeneyo makolo athu ankatiuza kut mwana amagula ku hospa but nat as of today .u cant cheat a child of ths generation.

  29. kodi anakwatira hule? eeeee ndikuvera pompa koma anachita bwino orongosoka ndi mahure omwewa or diamond anapangaso zotezo mkazi wakeso wa ku Uganda kumuonetsaso mimba pambalambanda

  30. A Malawi mmene Dan Lu mu nyimbo yake ya sweet banana kuti ”Umakwanitsakwanitsa”inali clear evidence that he practise what he sings!!Majority ya anthu omwe akulimbikira za culture dont dare to practice even abit.Its high time we embrace to precipitate what we preach.Malawians were just very good at formulating intelligent policies but we always fellow to summit them on ground.I remember one time when Bingu was ruling kunabwera ma officials ochoka mmaiko ena a SADC like Unganda,Kenya,Tanzania etc kudzaphunzira how FISP is run,mukaunika mmaiko amenewa njala ndi mbiri yakale chuma chawo ndikumakwera pa mene mphunzitsi malawi angoloshoka mu umphawi mkumati kodi mphepo ya elnino yo amangokatha ife tokha nanga Zambia inakolola bwanji oti wealther pattern is almost similar.Conclusion,lets practice what we preach,tisathamangire kudzudzula eni pomwe iweo chi log cha baobab tree chili maso mwako kuti neng’a!!!!

  31. Whether u say kut its uptown, ndi Celeb, ndi wandalama, wats our business, ndife achimidzi, we shud get a life bra bra bra,, shootin a photo with his beloved wife is not our problem, my concern z y showing us the baby bump like that? We all know wat it looks like. If he wants to create memories then thats simple, take a photo of his wife and save it in his handset. Why showing it to the whole world? Tikaona titani nazo?

  32. Mukuvutikiranji ndikungobwebweta apa,,,,,iyi ndimbali imodzi lomwe buku la chivumbulutso likufotokoza…masiku otsiriza…tieni tizingokoza mitima yathu

  33. Zonyasa,zonunkha ice kwathu kulibe zimenezi a Dan mukuzitenga kuti nawenso mkazi iwe ukungoselera zilizonse nonsense zanuzo ukooooooo

  34. ambuye yesu bwlan .athu.avutaa pamalawi . ambuyee athu akukuiwalan chifukwaa chan.moyo mumapelekaaaa ndinuuu. ambuyee chikond chanu chapamwambaa kwabax eeeeeeeee. thawi.yakusaziwaa mulunguu analekerelaaa

  35. Akuti “amalawi nsanje ikukuvutani” munthu ungapange nsanje ndi ziwandazo?
    Kuli Anjiru Fumulani,Mlaka Maliro,chizondi onsewa sima celebrity?
    Sanawapatsepo mimba azikazawo?

  36. Amalawi mumayamikila mzanu akamalakwa ndiye mumakondwa.apa dan wankoza?uyu muuzen kut walakwa ndipo linakakhala mayiko achiluya anthu awa anakalandila chilango chowawa ndi kupusa kwaoku.amalawi uwu timat uchitsilu obadwa nawo.

  37. Ma PLAIN
    ma plain
    ma Plain
    ma plain
    ma plain
    ma plain
    ma plain
    ZIKUCHITA KUONETSERATU KUTI APA PANAFA MA PLAIN.

  38. Is nothing to talk about ,,,,mimba yamkaziwake kodichimidzi chimakupwetekani eti guys ??????? Talowaniko maiko anzanu izi sizachilendo kwa anthu akunja guys be serious about this things ur posting big up Dan lu

  39. Amene akuti Dan lu wapanga zazelu apapa ndi chitsilu chamano kusi ngati mbuzi,anthu ngati amenewa amayenela azionesa chitsazo kwa anthu osati nyasi zopusazi.2 mkaziyo nayo nzelu alibe akavale choncho osazilemekeza mimba kungoyisiya pamtunda ngati fodya kukanengo poyitanila Malonda,respect ur self first then people will retain respect to u.

  40. Dan yu sikuti walakwisa ayi,izi ndi zomwe ma cerreb amachita ndipo ngati ndi ntchimo atha kukhululukilidwa, palibe nkhani apa,ntchimo koma ili wapanga Chaponda, nde ntchimo lalikulu loti nkovuta kukhululuka pokhaulisa ntundu wa a malawi ndi njala.EMMA & DAN keep it up,kwasala ka blue move mutioneseso,nanga tizingona mimba yokha?

  41. Azimayi enanu amene mukukamba nawo nkhaniyi mumavala motani mmiseumu? Mabere akumakhala pa mtunda yet you are condeming this? Be not the first to cast the stone!

  42. what Dan Lu has done is of course out of this country,, Koma guys lets be honest Malawi culture ikutha pang’onopang’ono,,anzanga amene mukukhala mu town mundivomereza ,,zimene akuvala atsikana ndi azimayi athu mtownimu is that Malawian culture? He is wrong yes but pliz dont over judge him coz nanunso mabvuto muli nawo munyumba mwanumo,,luk @ the way ur relatives or urself dressdoes that show someone coming from God fearing nation?amalawi tinatayika basi tivo,,

  43. nanunso a Dan timakuonani ngat ozindikila koma shaaaa!!!!!Chabwino komatu mwayaluka potengela chikhalidwe chakuno,ndinu munthu oyamba kupanga izi mu history.Koma sitsatila khalidwe mwayambali coz ndizacbwana hevy.

  44. End times. i wonder kuti abusa awo olo aku church atawona zimenezi anati bwanji. u celeb uli apo koma i dont thin anthuwa anapita kuschool. coz munthu oti anaphunzirapo sociology zimenezi sangachite. chitawonicho chili apo i think they need to go back to school to some concepts on how we shud live in a society. Ngatiso abusa awo ali ndi uzimu he shud counsel both of you.

  45. Za usavage bax umbuli si dhilu watokhala oyamba ndiye kubeleka amene mukut chimidzinu mimba xanu muzidzayenda nazo pantunda osangovomeleza kut we are malawians bwanj umphaw uli thooo muno kumafuna kukhala ngat anthu akunja andalama

  46. Pachikhalidwe cha mmalawi muno,mkazi olo atakhala ndi pakati zovala zinali kachikopa kongobisa maliseche,kodi ndekuti mimba imabisidwa pamenepo? Bwelelani mmbuyo a Malawi nde muzilankhula zopusa zanuzo,tsweeeeeee!!

  47. KUMAIKO ANZATHU NDIZITHU ZOLOLEDWA….KOMA PACHIKHALIDWE CHATHU SIZOLOLEDWA NDIYE CHONDE TIYENI TISAIWALE CHIKHALIDWE CHATHU

  48. Let the man be it’s his wife not your wife so why are you making a big deal out of it Tjooo my fellow Malawians please learn to mind your business…Just go get your boring wives pregnant so you can post it as for you Bitches who are talking shit it’s just because your jealous maybe Dan fucked you and dumped you some time back a Malawi muzafa yopolama maliro anu azativuta kuongola

  49. kungoti mkuluyu wakula moyo wovutika kwambiri.panopa angowona ngati ndi nthawi yake yoti athamangisane ndi dziko.ngat anafika pozola yelesa.

  50. Muzapanga comment zinthu zoti zijuchokera kwasatana amalawi ndichani???? Nawo adan lu panyapawo mwamva osamaika mimba zotoporazo pa air nudxabereka naxo slippers cox anthu anakhwima kunja kuno akhoza kukuchesurani uchitsiru mwapangawo

  51. Mmmh kkkk kma guyz amalawi tinapitadi mukati ayi poti anthu akumavura bola kuvurako cos sakuvura mimb yoti mulimwana ndichibwana chaxhikulu chimenecho sinsanjenso ayi kma kumumvera chisoni cox chinthu chomwe wanyamulacho sigaluyi kma munthu en akhoza kupeza nazo tsoka kti mmalo mobereka nkupititsa padera cox sikuti mulungu akusangalatsidwa Nazi zomwe wapangaxo enanu mukuti ndichimidxi amalawi mukuzinamiza nokha inunso bwanji mimba zomwe munali nazozo simunaike Pa air kuti anthu azione bwanji??? Takharaniko ndinzeru inu osamangiti poti mwasirira nkupanga comm

  52. Koma ngati uli u Celebrity ndiye kuyalusa nako makolotu. Basi makolo a Dan Lu ku mtima mbeee mimba ya mpongozi wawo ili pamtunda. Malaulo.

  53. Sanachite bwino zawonekelatu kuti osewo ndi mbudzi komaso mimbayo ndi ya ena ikanakhala kuti ndiyake akanamupasa ulemu dona wakeyo.Komaso samamukonda mkadzi wakeyo,kaya adziwona wakula watha.

  54. Paja a Malawi kudziwa kulankhula koma kuti mupange mukulephela, kudziwa kuzuzula koma kuti mukhoze mukulephela, this shld not be story kuti muchuluke nzeru, everything is for Dan just leave, takambani za cashgate, kuphedwa kwa ma albino, maizegate etc, inunso a Malawi 24 mutanthauza kuti inu nde achikhalidwe? Azikazi anu sakhala ndi mimba? Anthu sadziwa kuti mwawapatsa mimba akazi anu? Vuto anthufe timakhala busy kuona anzathu kuti akupanga chani kusiya zanu, what Dan has done can be much better than enanu mukuti fwi! fwi! Uyu wabwera poyela apa koma inuyo you can’t do it.Aaaaa a Malawi tasambani mmaso mukukhala ngati mwamugwira ufiti hiiiyaa! Ndapita ine

  55. forget about it this is no news you guys are doing far much worse thing when night falls, now write somethings that will help this miserable nation where all necessities of life are scarce ,you know sometimes i dont think chilembwe deserves credit for fighting against colonialisnm he was one hell of a stubborn fool who chased the british even before they had developed this country,we should have chased them now imagine how malawi would have been?

  56. Dan lu sanalakwise. muli buzy kumanena kuti akuyuza ma drugs komanso wataya chikhalidwe chachimalawi mmalo momaona zovuta zenizeni zoipa? mukukwatilana amuna okhaokha komaso akazi okhaokha, mukupha alubino komaso kumataya mimba nkumamunena munthu amene akunyadira mimba ya mkazi wake kuti wataya chikhalidwe? bravo dan

  57. I Love the self confidence in Mrs. Lu amwene thupi lokhwima ngati limenelo kulionetsa kugulu, timuyamikile mzimayiyu

  58. Makolo ndi akumpingo akuti chani?
    Tisamangoti celeb celeb apa zisanalongosoke…inuyo mwabalabalapo,mwakhalapo kapena akazanu kukhala napo pakati ndani anaonesa?kodi 21century ndiye tizitero?
    Mukati tikusiya mavuto athu ndiye kuti chani?.mavuto samatha tinawapeza tizawasiya..komaa izizi izi zikonzedwe zomaonesa chinjazi…anthu amabala at old age samapanga choncho.zalakwika…kukhala ngati zachilendo zamimbazo? Asaaa!
    Afunika mlango….

  59. Kd enanu mukut DAN ndiwandalama mukuganiza kt ndalamazo zimamuuza kt azivulana? Kmaso mahule ntchito yao ndi uhule ngat nkaziyo akufuna kumavula ngat mahule azivula choncho kmaso enanu nkaziyo mukumudziwa kt anakatengedwa my bar ndizosadabwitsa. Iwe ukt ndiwandalama kapena ndiozindikila uwelenge bibble uve zanowa mwina utseka MAU ako opusao

  60. Mimba imeneyo ndchta kulowa #FISI nde lero akamabwera poyera ndmimba yopeleka ine ndingodabwa,,,mudkre mwana wobadwayo Angozo enieni!

  61. Which malawian culture are u talking about coz zitenje ndi zinazo ndiye zochokela kwa azungu,if u thnk he z wrong u mst put a pic of our foregrandmothers wearing a chitenje during pregnancy or in anytym,

  62. What’s the matter with you people, while you just indulge in other people’s happiness. I don’t see it wrong, The couple is just jovial for their gift of the baby and then is this what you’ll condemn them. Your just pathetic. Useless writers.

  63. Culture is important please don’t take outside things especially in Malawi you like cope wat ever you see in south Africa you bring it in Malawi you don’t have your won culture Malawi change

  64. Iiiiiiiiiii koma anthu kumalawi muli ndi vuto moti mudzipanga zanu muli busy kukamba zazanu, ine ndesimkuona vuto linalililonse masiku ano ndimene waimvelera komaso ngati zikukuwawani musamaone mudzitsizina basi. Asiyeni apange zakufuna zamoyo wawo ma pics amenewa ndawakonda kwabasi ndipo ndasilira next time ndiine ndi hubby wanga nafenso tidzaika hiyaaaaaa. Inu mudandaula bwanji poti ndalama zomwe alipila photographer ndi mzawo data yomwe amagwiritsa ntchito ndiyawo komaso mimba ndiyake sanaike yanu zomwe mukuyankhulazo ndiza ziiiiiiiiiiiiiii

  65. Kkkkkkk wanzeru amangokhala chete nkungopsyinyira diso tikanena kuti ndizabwino ndi uchitsiru bwanji osamagwirana mimbazo mzipinda mwanu kkkkkk koma yaaa dziko lithe basi akatiweruze

  66. Bvuto lanu ndichani agalu inu tiziwalo tazipsyera ndikuda tikuyanikidwa mmatauniti bwanji mulibe nthawi yoyankhura zimenezo mkumalimbana ndi Dan Lufani bwanji

  67. Mmmm kayandife aphawi, kma ku mwamba kulibe kuti uyu ndi ochita bwino kapena osawuka,tonse tikakhala chimodzi-modzi ngati tichitabwino panopa madziko la pasi

  68. Imeneyi ndi imene munaona kuti ndi nkhani yoti mulembere mtundu was a Malawi? Mukanalemba z kubedwa kwa ndalama ,ogula chimanga zija the better. But wasting ur tym and resources writing this? U r all useless…

  69. Enanu mukulimbana ndi #Dan Lu kamba kawu mphawi munaka khala mulikathu sibwezi mukulemba phusi zanuzo, Chinaso kusayenda muthu ungo khala ku mudzi uko uziwa bwanj #Life muziyenda muziwona muthu wawonesa mimba mukuchita kutha mawu chochi nanga atawonesa zinaz mupitila kwawokoko eti?

  70. Pachikhaledwe cha amalawi
    ndi uchitsilu kapena kuti dan
    ndi ozelezeka mu zelu zache
    zotendelazi kumaziwona
    kenako ayenda mbolo pantunda mwiniwakeyo sinanga aliyese
    alindi mbolo kumango cop chili
    chose mupusa nadzo adan lu

  71. Kamuzu Banda ananena kuphuzila si school yokha mudziyenda muziona zimene anthu ena amapaga it not about cerebrity izi amapaga aliyetse ndipo amapita ma mall azimayi mimba ili patunda palibe chachiledo amalawi

  72. Kungot kumalawi kamuzu anatipangitsa kukhala ogona ndipake anthu amangolemba zomwe aganiza podziwa kut amalawi ambiri ndiwogona…

  73. Amalawife chikhalidwe chutionetsa umbuli pena pake dats y tili otsalira zina zilizonse sindikudziwa mukadzapita kunyanja kukaona mmene anthu amavalira akamasamba mudzalemba zotani . kungowonetsa mimba zowona ikhale nkhani ? shame

  74. Ano ndimasiku otsiliza zikuynla zichitike yesu watsala pang’ono kubwela azaweluze ziko lapansi.ndipo izi muzionazi zikuchepa muona zina zoposa zimenezo.

  75. musamuletse kunjoya dan lu, moyo ndi wake iye anjoya alichete chete anjoya alichete chete anjoya alichete chete. He knows what he is doing

  76. musamuletse kunjoya dan lu, moyo ndi wake iye anjoya alichete chete anjoya alichete chete anjoya alichete chete. He knows what he is doing

  77. Eeeeish Opita Kujando Ameneyu ! Hmmmmmm Ukufunik Kument Iwe Ndi Mkaziemweyo ! & Akakuvinilenis Litiwo Mwawnjeza Asease Mukuzimvacha !? , Hmmmm Usayalutse Achawa Mwanaiwe !!! Mapaziako Ndithu Kumeneulik !

  78. a Malawi mmalo mot tidzikambirana mmene tingathetsere umphawi basi busy kumakamba za munthu oti zake zinayera , kod mukut chikhalidwe nd miyambo ingat yomwe inasithidwa kamba kwa kusitha kwa dziko, be civilised guys and get life munakagonabe eet, komaso inu mmat a Malawi 24 mwasowa chochita? ngat nd choncho ubwere udzakame agalu kuno, as a matter of fact malawians learn to mind your business and some things beneficial #TeamDanLu

  79. Ine sindikuona vuto pa nkhani iyi, moyo unasintha and tiyenera kudziwa kuti zofuna zanthu sizofuna za anthu ena, kwa amene ayenda ndikudziwa moyo andivomeleza: moyo wa kumudzi ndi mtown ndiosiyana kwambiri and Dan lu, ndi celebrity, komaso ndimunthu yemwe zonjoya amazidziwa

  80. Chonde wina aliyese kuno kwathu akakwatiwa kapena kukwatila amapasidwa ulemu kusonyeza kt alindimwini ndipo ziwalo zina amakazionetsa kwa iwo okha awiri buc ,Vuto ndilot ena mwainu simumava malangizo ngakhale chikhalidwe chakuno kwathu kumalawi .Mabanja ongotengana opanda akuchimuna ndiso akuchikazi thats wy amat muzipita kumudzi kukaphuzila chikhalidwe kmaso vuto ndikobadwila kd nkaz waumunthu angavomele kumupanga zopusa ngat izi pagulu inu ovomeleza zopusa ngat izi ngat ndikukapempha kwa chitsilu chanuchi pitan chabe kokapemphako osat kuvomeleza zauchitsilu ngat izii

  81. zachita kuwonekerathu kuti inu a dan lu mukamuyanikaso mkaziwanu kokachira mwanayo kodi amalawi akazakuwonetsani mkaziwake akuchira mwana mwanayo wangotulutsa mutu make akumva ululv woopsa muzachilandira bwanji? tingothokoza malamulo amakhala kumeneko ndithudi akanazachita ichi. masiku omaliza kaya tsoka kwa okwanilitsayo.

  82. DAN LU CHAMBA CHA KWAMERECA,NIGERIA, MOZAMBIC NDI KUMALAWI CHAKUPANGITSANI KUYANIKA MIMBA YA KAMKOTA KANU KAYA GANJA WAKE NDI WADZIKO LANJI MWAVULA NAYE CHOTELE KAMKOTA KANUKA.

  83. abale banja mpaka pamenepo? mwati liri ndi ankhoswe limeneri? ndi ife tomwe aku word apart tawonanawo a Dan Lufani Kuvula malawi kumeneko nyasi zimenezi mwakazitenga kuti? koma dzina lamulumgu limatchulidwa mubanjamo?wina nkumati ena amayenda ndi panti yekha mtauni mu mahule anuwo mumawaona nokha kutaliko tikukamba apa ndi banjatu koma wavula amayi ako iwe!! mwati mkaziyo sanakamutenge ku bala koma uwu ndimuchitidwe wamahule osati inu amabanja kutukuka tinene uku malawi mukufikatu pa sodom ndi gomora ndife amodzi amalawi kuno si ku america kapena ku india kuno ndikumalawi mulumgu watifulatira and mzimu wanu ulikuti nonse mukusapota zoyipazi aliyese woti mzimu wamuchokera azatenga chinthu chonyasa kukhala chabwino CHENJERA IWE PULUMUKA NDIMOYO WAKO usachimwe poganiza.

  84. Kkkk mmm alawa! !!! Palakwika chani apa kodi mesa nkaziyo ndi wake? Kodi ngati mukutelo pa izi kuli bwanji mukanamva zoti Dan Lu ali wakhapidwa mutu kuchigololo ali muchipatala mukanakamba ziti??

  85. abale banja mpaka pamenepo? mwati liri ndi ankhoswe limeneri? ndi ife tomwe aku word apart tawonanawo a Dan Lufani Kuvula malawi kumeneko nyasi zimenezi mwakazitenga kuti? koma dzina lamulumgu limatchulidwa mubanjamo?wina nkumati ena amayenda ndi panti yekha mtauni mu mahule anuwo mumawaona nokha kutaliko tikukamba apa ndi banjatu koma wavula amayi ako iwe!! mwati mkaziyo sanakamutenge ku bala koma uwu ndimuchitidwe wamahule osati inu amabanja kutukuka tinene uku malawi mukufikatu pa sodom ndi gomora ndife amodzi amalawi kuno si ku america kapena ku india kuno ndikumalawi mulumgu watifulatira and mzimu wanu ulikuti nonse mukusapota zoyipazi aliyese woti mzimu wamuchokera azatenga chinthu chonyasa kukhala chabwino CHENJERA IWE PULUMUKA NDIMOYO WAKO usachimwe poganiza.

  86. ineso ndilondoleze ndikodzele peni penipo ibwele mimba ine nde azangovala bra ekha mimba pambalambanda ntaikumbatila nkulemba kuti ndaika nthanga zanga

  87. Tumizani aboma akamange waphwanya lamulo chikhalidwe mpaka liti?? Mudakauzabe Ana anu kuti mwana amagula eti?? Inuyo Pangani zanu naye apanga zake basi

  88. Zoti mimba ndiyobisika anakunamizani ndani?ndipo pali zifukwa zimene eniwake apangira zimenezi,woimba muchenjere naye azakuimbani nyimbo,zasanje ayi malawi nde zimene amapanga akunja ife tingalephere chifukwa,ngati mukusalira ndinu ife tikupita

  89. bola poti mimbayo ndiyake pankazake,achikhala ili ya wina ndichibwenzie mudakalankhula motani?zathupilake,zakezomwe izi!!

  90. Mmmmmmm é fool doth thnk h z Wise bt é wise man knws hmslf to b a fool!!!!! they r stpd indeed ine nde cndngasekerere nyasizo Entseeee!!!!!!!!!!!

  91. Palibe Cholakwisa Apa Bora Akanakhara Mkaz Wanu Zikanaveka Ndiye Pot Ndikaz Wake Zakuvutani Mlibe Manyaz Agalu Inu Achabechabe Osangolemba Za Chimanga Bwaa Chija Amat Agura Kuzambia Lili Bodza Chosecho Agura Momuno Ndiye Dan Lu Ndiufulu Wako Iwoso Ngat Akufuna Athakukapanga Bola Akhale Akaz Awo Muisova Khobwe Sinyemba Agalu Inu

  92. Malawi’s civilization,where is it?instead of finding lasting solutions eg to the cash gate and maize gate like other countries did to solve their problems eg Egypt they inverted shaduf machine that helped them doing irrigation, what can Malawi benefit from this immoral behavior u call it civilization????

  93. Pali chani APA anthu akuyaluka kuyenda maliseche ndiye muziti wanyozesa Malawi hahaha mwasowa zolemba eti yendani mizindamu muwone kuyalusa Malawi…kkkkkkk wamwa utobwa iwe eti

  94. The issue is ‘kulimbana ndi a x wife’ sipaja iwowo anakamba zambiri banja litatha, mpaka anati dan sabeleka,so this is to prove her wrong plus kumuwalira

  95. I think dis pple from Malawi z very schupit//am syng I think oky!!kod mwamuonera nkaziyo pano kulemera kuli ndi njira zambiri so dre z no one can judge afrnd hre undy de earth its only god//so some of u u r judging “Dan luu” y ?

  96. Wachita bwino akunyadila pakati pamkazi wake. Ndizonyadilitsa anthu akukwera achina sapitwa koma osatheka ena kumaliza mitengo kumwa gondolosi, mthubulo,zimswa ndizina zotelozo komabe osatheka

  97. To those ladies who are saying there is no problem with that have u ever done that before during your previous pregnancies? Or u are just saying coz dan lu is acereb?tisalankhuleso mopsapsalika apa zomwe apanga anthu awili awa ndikupepera kapena titi kuzerezeka kwenikweni. Alawula ndiwo kukhala ndimimba?zathu akamapita kuphompho ndi bwino kumubweza .ngati awili awa sakuwona vuto pa izi ndekuti mkutheka mitu sikugwira bwino ntchito . M

  98. Mmmm e’ fool doth thñk h z wise bt Wise man knws hmslf 2 b a fool!!!!! they r stpd indeed ine nde cndngasekerere nyasizo

  99. Amene zikumunyasa atseke maso asawone zachimizi basi ngati ena akuenda ndi pant malawi momuno kukakwela ndege mimbaso ndichani plz plz learn tu mind your on business

  100. What brother Dan Lu has done to his wife is morally bad ,and can not be encouraged in Malawian cultural platform, Any society has its own culture and social morals. There is every need for celebrities like Dan lu to help in selling Malawian culture to the world at large. Women in Malawi is
    the national asset every body should be proud of .

  101. dzikoy yinali yogona no wanda kt zili chonch nde anjatchuwa akapita nkumaona anjao openya nawoxo afuna kutionesa kuno.watinyasa bwanji!! Arthur Wachibwibwi Muongola Felix Nyirenda Foster Chibayeni Morris Jossia Ownery Tabia Juvinali Aubrey Ansomba Wamoyo Evance Njanji Winnie Mafunga

  102. Vuto lokwatira maHure .. Makolo akamatirangizatu penapake zimaoneka ngati akutikhomerera..lero ndizimenezi mukupepera kuyalusa makolo..

  103. Fuck you Malawi 24 im not even going to open it surely this is nonsense and so uncivilised very stupid u should rot in hell u and whoever else wrote such stupid articles let the man live tf?

  104. What’s wrong with that?Amalawi kuyalusa kuli pati?things are now changing. for example, kale kunalibe zoti amuna azipelekeza ku sikelonndi ma spouses awo.panopa timapita nkumakaimba ndi ma pregnant mothers .Ndiye munthu alekelenji kuwonetsa chikondi kwa wokondedwa wake.More over pamenepa he has demonstrated to others how to show love to our spouses. Mumafuna azibisa zoti Ali naye wake? MAHULE NDI AMENE ZIKUWAWAWA.MNZANU WAKWATIWA NDI mamuna WA CHIKONDI.ine kusilira.

  105. Ndatsatira macomment koma ndapeza kuti ambiri mukukondwa ndi khalidwe la mchawa mnzanuyu ndi mbuzinso zosadziwa kathu nkomwe, inu a Dan lu olo mutakhara nawo pafupi mungawatenge ngat mutu wawo umagwira boh? Tiaana tokulira mwa m’baluku mbuzi zeni zeni ngatinso mimbayo athira ndi iwo pomwe timabatile tidauma kalekale ndi chamba. anthu apeleka mimba mmidzimu osat kwa achawanso ayi! mwana wa Abusa?

    1. inu ndi dan lu mungafanane ?? zinazi osamangoyakhura ndi cholinga choti anthu akuveleni end khani imene ili apa ndi yamimba achawa yawakhudza bwanji ?? kodi iweyo kaya ndi nchewa kaya ntumbuka kaya mati alomwe what ever kodi amako anachita kusakha mtundu obadwira kapena anangozindikira kuti abadwira kumtundu wakowo. ndi kakhala ine sinasakhe nabadwila kuchiyawo ena amati mjomba ndipi ndilibe nazo vuto koma tichexere bwino ife zamitunduzi sitikonda kunyozana zili ngati chilema. uchiphwisi wakowo uwone kokapangila wava ndipo usayelekezeso kutchula zina lachichawa pano mboli yamako chupit mwana wahule sorrytu ndangotsuka nkamwa guys

  106. Malawi24 get a life.
    Zimimba zomwe timawona minsewumu bwanji simukamba kathu?
    Dan Lu ndi mkazi wake ndi anthunso ngati simukudziwa ziwani lero.

  107. Iyeyo iz it his 1st mariage? i think w nid reason bfore doing something, zitachitika kut mkaziyo wapita padera azanenaso? wwhat childish iz

  108. Kkkkkkk eeee malawi the warm heart of africa ???uzatitumizilenso live pic akubeleka nkaziyo man lu wayamba bwino ichi timati chitawuni anyamata ahipap??

  109. komatu ine or chitaunicho mkazi wanga sindingalore kuchita zopusazo .thupi la mkazi liyenera kupatsidwa ulemu.ndiye popeza akazi owatola ku pub nkhawa anapachika nde mapeto ake ndi izi

  110. Dan keep it up akutelewo sanayende ur true a hero palibe anawonesako luso losilika ngati ili ur the first kufa mwana ndi thawi osati coz of display the pregnass za ziii tizingosalila awonese che lufan asakufuna akakolope nyanja Ku salima

  111. Kkkkkkkkkkkkkkk Malawian are funny people what’s wrong but you give delivery woman mwachonsetu anyamata akubereketsa azimayi mzipatalawo

  112. Do u know why people(malawians) dont post pregnancy pics? Its because mwanayo sanabadwe ; Nanga atabadwa wakufa or kupitilira or kupanga miscarry muziti chani anthu mwawulutsa ku Dziko lonse lapansi? Malangizo kwa mayi a chiyembekezo ndi awa, pitani mukafunse malangizo okhuza masamalire a mimba kwa azakhali anu ; bambo Dan Lufani awongolereni akazi anu moyenerera mimba ndi chinthu choopsa mwina bwezi mukumati pano mukutsara kudya ndi kupembezera moyo wa mwana ndi mkazi wanu kuti achire bwino ; Langizo lomaliza muchite break kweee muyende mosamala musamusemphe mwana meaning khazikikani mwakula

  113. Akunama Dan palibe cholakwika APA iwe ukunyadila chomwe wanyamula mkazi wako Iwo akazi awo akakhala oyembekezela amawabisa go DAN GO ndakunyadila

  114. Ma celeb akumalawi ofoyra . Just bcoz diamond expose his wife pregnant on internet nawonso ati ayesele . Manyaka amunthu thats wy malawi sakutukuka copying everything just bcoz kuti usawoneke ngati osalira . Osangovomeleza bwanji level yomwe muli ? Diamond znt ur size . Wina ndi uyu just bcoz trump said that he will make america great again nayenso ati basi he will also make malawi great again kkkk malawi uzafa ndi mtima .

  115. Kodi mesa mimbayo ndi yake? Tsopano ife chikutikhudza chiani? Ifenso tili ndi akazi anthu, nawonso akazakhala ndi mimba kaya tizatani zizaoneka patsikulo

  116. Looking foward to the malawi in 2030 wen maybe news will be news and malawians will have better things to critisize and have contempt for rather than other ppos endevouirs.

    1. Blacks are not backward people they do things according to the black values the only problem is that you are comparing black people with Europeans which is not good let black people be directed by black values not European values we are black lets accept that we not Europe lets be unique and be happy with our culture lets avoid copying what Europeans do coz its according to their culture aswel lets accept the fact that we are black and we are Africans #pan-african.

    2. Stain Chigumula now thats a lie????? blacks especially from Malawi we always talk about Culture….. Things that agogo awo a agogo awo used to do in ignorance…. Be civilized, even every App or Cars keep updating, i remember kale even munthu wankazi akavala trouser kumayenda mu Town anthu amachita kumukuwa mostly ma Vendor ati hule……. Even a mini skirt mkazi ati asavale……. People please

  117. Bvuto lokwatila mmalo omwela mowa ndilimeneli kumuza ichi amangovomela mutu unabaiizika kalekale I tink mkazi wanzeru zake sakanalola kuvundukula mimba nkuisiya panja. Akanaibisa betele.

  118. mwaika ma comment omubakila nonse ndi zisilu inu olo mai anu anayamba atachita izi koma muli ndi uzimu inu? Kapena nanu ndi chiwanda ngat Dan lu osamaombela mmanja zilizonse agalu inu bwanji inu azikazanu simawaika pa air ? Tizit simunakwatile inuyo zonsezi ndi zosala ulemu ndi chikhalidwe ndie zofunika komaso munthu wa moyo aziganiza za umulungu nanga apa za umulungu zili pati?

  119. Aliyese alindichisakho chake chimene iyeyo akachita amati zilibwino ndeye athu tiyeni tichepetse kupanga zawina tizipanga zathu zimene zingatithandize Dan lu ndichisakho chake mlekeni

  120. mmh malawians know how to exaggerate… i see the comments are filled with hatred, Dan Lu has done something bad yes bt this is not how you can correct this, zalowapo nsanje apa tisaname though dan lu sandisangalasa…. ambilinu mukuyankhula zausilu apanu mumavulilatu maliseche bolaso apa, kwangosala siku loti muzayaluke lachi 40.

  121. Iwe mavutoakondi chani kulemba nkhani yolusa ngati imeneyi.. Mind your own business. Lembani nkhani zenizeni apa osati zopusa ngatiizi… He is a Celebrity what did you expect… hahahahahahahaha Pambalambanda pambalambanda chani..?

  122. Opañda nzeru inu mukubakila nyasi izi…….maiko akunja alindi chikhalaidwe chao kunoso chthu bwanji ngati munkoña kuti ndzofunika osawauza makolo anu aziika nyasizi APA…………usatanikiwo ntchito zasatana izi ife tikaona tiatan saziwa ñdani kuti anthu akakwatirana amanyengana mkupasana mimba kma mpaka ife tiziona apa…….mulungu simunthutu akuziwa wanyamula mkaziwakeyo Danyo???? Kenako azationesa akunyengana kuti tione mmene amapangila ziwanda zaozo…….Malawi wasochera

    1. AMEWO NDIYE MAWU, AMENE AKUKONDWERA AVULE AKHALE MALSECHE NGAT SAVULA ALI PA SOKA LOCHOKELA KUMWAMBA SINZELU ZIMENE WACHTA NZANUY AMENE MMUCHA INU DAN LU KOMA INE NDMUCHA WAKUMIDIMA SAONA.

  123. mmm koma amalawi uchimizi kulaula, walaula ndan apa dan luu tikunena tsiku ndi tsiku kut muziyenda maziko azanu muziona zomwe azanu amapanga mukutipasa manyaz bwa mukuona ngati mumawelenga nokha nkhan izi ziwan anthu akunja nawo amawelenga ndipo amakutengan umbuli chabe apa mimbayo ndi ya mukaz wake akanakhala wachibwez mukananena kut walakwisa mimbayo ndiyosonkhelana iiii apa pokha changamukan dziko likuchangamuka ili siyan kugona abale. mumalo molimbina ndi maizegate mukulimba ndi munthu osalakwa Dan luu pitilizan aman anthu ogona tulo awa akadalipo pa malawi inu imani ngangali ndikuziwa ikafika nthawi azazuka mutulo tomwe ali nato panopa

  124. Hahaha koma a Malawi vuto mchani inu apa musiyeni munthu ndi celebrity yake ndipo ali ndi ufulu opanga zomwe wafuna please tasiyani kumalonda amzanu mapazi mkumapanga zanu (I respect you brother man thts what we call romantic)

  125. Kkkkkkkk koma yaaaa pamalawipo!! Iwe Dan lu koma zikuyenda ndi alungusetse wakoyo kapena akuuzani choncho kusataniki wanuwo? Ndiyetu muyaluka umaleka bwanji kuonesa maliseche ako pa nthawi yomwe mumatulusa zomwe watupa nazo m’mimba khwevemulezo? Zauchisilu

  126. We are Malawians don’t adopt Europeans culture! Azungu ndi azungu ifenso amalawi ndi amalawi basi, please don’t lost our culture becoz of Europeans.

    1. iweyo wandisangalasa kwambiri. walemba in a western language on a western platform criticising western culture yet your name is in western language…. my friend you are so ignorant

  127. Zoona.ndi zomvetsa manyazi komaso chisoni kwambiri uko ndiye kutaya chikhalidwe chathu. My question which human right he had violented?why the human right are so quite about this sin?

  128. Inu amene mukuyamikira izi ndinu opanda nzeru,akhwakhwa ,agulugunyinda ,analikukuti ,akhaniwa nchifukwa chake Malawi ili panambala wani pazasataniki mkhalidwe wake umenewu kutengeka,,munthu wanzeru sunganene kuti Dan Lu sanalakwise ,,,imeneyo ndiye misalayo ,,mimba ndi chinthu cholemekezeka pachikhalidwe chachimalawi,,,tisanene kuti dziko linasintha,,,linasinthira ndani,,,zoterezi abale anga mwa ambuye tichenjere nazo izi titha kupereka mphamvu kuziwanda, because last minute always danger,,,,nawenso mkazi mkumalola chithunzi chako kuchiika pambalambanda,,iwenso Dan mkumaikadi ukumwetulila ,,,sitinganene kuti sakudziwa kuti mimba imalemekezedwa onsewa anabadwira kuti,,zotere amalawi tisamazisekelere,,,tizuzule molimba ,,,,osati jealasinso taonatu mimba I’ve osati zochezazi ayi ndipo anthu abereka koma sanachitepo izi,,,,pofunika banjali liyambepo kupemphera anziwe mulungu weniweni,,,,,,,, ,,,,,,,,,,,

  129. aa, nde kuti dan lu ndi mkazi wakeyo apanga zimenezo ndimtima wonse, nde mumutani? mum’mangisa? makapeso inu eti, umphawi wathuwu unatipundula bac, zilizose? chikhalidwe chake chiti?

    1. Ulemu wake utiwo anthu mukuyenda maliseche town umu…. Mimba ikakhala yako zimafunika kuinyadilira tatopa nkumangona ana pa fb mimba zake osaziona… Komanso zinthu zikusintha pano

  130. DAN si CELEBS koma ndi osaganizabwino iku mkusambula #MALAWI.akumuonetsa ndani mimba yamkaziwakeyo? Nde tikaona titani?? Sangajambulitse chithunzi cha mkazi chimimba chiliphwee mkuchiika pambalambanda potere mkumbwambwana.Inu azimai mukuti sanalakwitsenu mumaganiza bwinobwino?? Inuyo mumatani kumayenda ntawunimi muli chimimba kapena kuti muli ndi makati ngati uli u CELEBS?? munthu wochokera kukhomo kwa anthu sangapange zopusazi kutengera zinthu musakuziwa tanthauzo lake mapeto ake nzimenezi; anakuuzani kut munthu akakhala otchuka sasamala zachikhalidwe ndani?? NAYE MKAZI KHOSI GENEKELEEE CHIMIMBA CHILIPHWII NGATI NG’OMA YOFUNA KUKACHEZERA KUYIMBIDWA KU MLAKHO WALOMWE #ZIWANDA ETI??

  131. mwangosowa zolemba eti, azimayi ndi atsikana akuyenda matako pamtunda town osawalemba bwanji kuti akuyalutsa chikhalidwe, ndie mimba ndi matako choyalutsa ndi chani apa, ndaniyo sadziwa zoti mimba imabwera bwanji, za ziiii,

  132. Palibe chalakwika apa chifukwa. Sanawonesepo chiwalo cha chobisika ngati mukumuyenda maphazi ndiye.Mwayalukapo. Fuso nkumati nankha. Bwanji simuku blamer amene akumavina nyimbo zanu atavula malayamalaya ????????? komaso komaso atavala timasiketi tatifupi todhinda zobisikazo nakha ovinawo mukutiuza. .kuti si amalaw?????? Asass amalawi sibwino kumakhala busy kukamba
    Za mbaja la ena ayi

  133. Komaso palibe chikuwoneka kut ncholakwikai vuto la athu akuda ndichoncho mexa iyeyu akunyadira mkaz wake komaso iyeyu waima pachulu kukumanyitsani inu bwanji osaimaso ndi wanu kut athu amanye sanje bwanji athu inu Kkkkkkkkkkkkkk nde mukhaula aikaso china

  134. Koma iwe umalembawe koma kuchipatala munapitako ndi ndi mkazi wanu ku sikelo? Nanga munamvako zoti pano amuna azikaonelela kubadwitsa ana ku maternity ward? ukadzaona izi udzakomoka shuwa !!!! Akadakhala wachibwezi ukadatani. Upite ku joberg ukaone zolaula pali chani apa!!!

  135. Ndikupusa kuonesa mimba ya mkazi wako pa gulula anthu, lthink mwina mimbayo samaonesaife, mwina akuonesa anzakeakuja omwe anajoinanawo ujeniija.

  136. The man is so stupid as well as mad.He cant do that.What seed is he planting on youth?Thats so stupid.He needs deliverance before he completely went mad.These are the people TB Joshua needs.

  137. Abale satanayu akatigwila bongo sititha kuziletsa ndipo timaona ngati ndimmene zinthu ziyenela kukhalira uwu nduchitsiru ndithu ….mukamati masiku ano ndiena mukutanthauza zichani???: zinazi mzochokera kumidima chenjerani muzamva khwangwa ili mmutu zikanakhala zimenezo bwenzi dzuwa likusintha kolowera kapena kotulukila anthu amsiku ano tikufera chitauni kapena kuti kufuna kuchita zomwe anzathu anachitapo dziwani satana wakonzeka kusintha anthu oduduluka ndizanziko…omwe asakha kukhala adziko lapansi amadudulukila zanziko lapansi ndi zatsopano…. ziwani zinazi nzapansi panyanja

  138. Kungomumvesesa basi,wakhala zaka zambiri osatheka,so mwina akusangala kuti zathekadi/?anyway let’s hope sanainyamulw kunja.

  139. Malawians learn to mind your own business. Leave Dan Lu and his family alone….its his life, his pregnant wife….whats wrong with this nation kumangotchathuka anything zinazi tamangowanani basi osaikapo mlomo…..jelousy people

    1. Iwe fatsani bwanji iweyo ukukanika kuyika thupi lako panja??? I think uli mu chart chimozi ndi ka dan lu kakoko, u cereb nde kuti chani??? Bwanji ma cereb ena amapanga post azikazi awo amimba koma amakhala avala chobisa mimba yawo bwanj??? Mungokhala chete chifukwa ukuziwonesa uchitsilu wako

    2. Osati iweyo Ganizani Mkuchira ungokhala Chete chifukwa ukupanga behav ngati savage,muthu osowa chochita,iweyo osapanga zako zoti zikuthanize bwanji,

    3. By exposing his private life to us he has made it everybody’s business so I wonder why some people are saying we should mind our business-wake up Malawians don’t think adopting everything of the western culture or other cultures means you are cool,sometimes it may show ignorance & indecisiveness-it’s better to adopt only the meaningful & usiful things from other cultures & maintain the valuable aspects of our culture-One of them is respecting women & their body-especially pregnant women.

    4. I second Dan lu is a celebrity and we cant expect his lifestyle to be of Malawian average.
      Anthu you have passwords for your phones & mumasungamo zinthu zosayankhulika? tsopano apa mukuti culture culture …imakhala ili kut that time mukamapanga zanu zija?
      #Osamaiwala everybody chooses their lifestyle we are free to do so…dont impose your personal convictions on someone else..just let them be eeeh.

    5. malawians shld learn to mind their business? How? wen u put smthing out fo us to see ndye ndiye tipanga bwa? stop putting up stupid stuff ndye iwe mapala ukuti cha? ma zobaaaa ucnt deny wat u r ife ndi amalawi, pple do show such things kma atavala bho n it looks cook ndimosililisa not ths shittt

  140. Amalawi umbuli basi chachilendo ndichani APA kusayenda ndi kumene kukuyakhulisani mudakagonabe zithu zinasitha Malawi zuka aaaaa koma umbuli ndimatenda

  141. Tinene Kuti Mwina M’mimbamo Muli Yesu? Kumazitama Ndi #Usatana basi! ngati walemela azitaya ndalama munsewu osati kutukwana #Mulungu, Chimene Chili Mkatimo Akuchiziwa? Matama Otelowo Muzabala Mwalatu’,!,

  142. Wataya chikhalidwe komanso akufunika mapephero kuti amasulidwe, sakuziwa kuti ndiziwanda zimenezi zikungofuna kumuyalutsa basi

  143. Dan usawale apa mimba iyi mwiniwake alikunkhotakota mufusitse mkazi wako akuuza ngati amakukondadi.akuti iweyo palibe chimene umamupanga.

  144. A Malawi Tsamangoyamikira Zna Zlizose Nd Manyi Omwe,uselebu Siumenewo Kma Nd Umbuli Umene Acita Danzo Taona Maselebu Kma Sanapangepo Mbwelera Ngat Izi

  145. That’s the evidence of using hard drugs. Most musicians are famous for using hard drugs so no wonder what he is displaying on social media. Keep on following him next time he will post a display of his wife’s private parts claiming that she is the most beautiful lady on planet earth. Shame on you.

    1. Amene mukuthamangila kutchula private parts mukudabwisa…kapena tiziti ndizomwe mumafuna muone poti munazolowera kuona zimenezozo? #Get a life.tisamateroyi

    2. hahahahahahahahaha Nde mwati za drugs and pic zikugwilizana pati? I dnt see the connection.paliso nkhani apa? .

  146. Aliyense Ali ndi choice pa moyo,iwowo anapanga choice choyipa mimba pa mtunda ndi mene anayimverera amafuna attention kuchoka kwa anthunu ndiye who are we to judge them,let them leave their life to the fullest,zikungofanana ndi anthu ena amayika mabele pa mtunda.

  147. Paja mumafuna mzimai wamimba azivala chitenje mmabelemu ndiye kusekelera ine simkuona vuto bwanji atsikana amavala malaya oonetsa mchombo just because mmimbamo muli mwana ikhale nkhani

  148. Kkkkkkk chitsilu si mamunayi ayi chitsilu ndi nkaziyu kapena kuti agogowo, iyeyu sanalangidwe kwawo chifukwa mamuna sakuziwa kalikonse kokhuza mimba, komaso sakuziwa kuti chikhalidwe chapamalawi kuonetsa mimba yoti muli munthu ndi uchitsilu,plus kuyalutsa, ndikhulupililaso anayambitsa kuti aike pa air ndi amayiwo

    1. Mwangokhala ndi Sanje wakalamba Pati apa Emmie kuti akhale gogo get life pipo what’s wrongs with that its their baby and style why drinking panodo on another person headach

    2. Zinhle you’re right..but don’t start arguments with fools because they’ll drag you to their level and beat you with experience…

  149. Amalawi muli ndivito…. what z with ppo? This is normal and fine… proud of you for showing a good example.

    Mmalo moti muzizuzula azibambo okwatira amene amangochosetsa mimba za ana. Muli chilili kulimbana ndi Danlu who z accepting his baby mama in public proudly.

  150. Tisiyanise ma celebrate ndi ife osaziwika, look at foto of actress Toto Dinker pa page komaso mumene ama valira oyimba akunjawa aaaaa musiyeni inu munthu apange mumene wafunila

    1. No Wonder Satanizm Line Thats Y You Dont See A Problem There May Lord Guide U Wth Proper Knowledge Coz U Guyz Ur Out Of Mind

    2. Why are u judging him like that ngati iye wapanga zimenexo its his own business with his wife,plz amalawi let’s mind our own bussiness, zolozana chalazi sizingatithandize thus why tikumangosaukabe bcz tikumakhala ndi tym yolozana zala malo mopanga chitukuko

  151. Vuto si iyeyu koma umbuli u know pple from mangochi inu mix nanu olemba nkhani mwasowa zowauza anthu komanso mkanziyo mmmmh akuoneka ngati wamkulutu iiii paja ana amasiku ano sakuona size mixi zakucheza etiiii

  152. Pachikhalidwe chathu apa alakwitsa ndipo or kumene kuli makalo a Dan ndi Emmie ali ndi manyazi kamba koti pali mau oti akulu akulu ndi mdambo mozimila moto, komanso tiyeni a Malawi zinthu zikalakwika tiuzane mwachikondi osati mochita kunyoza, and zomangoti zili bwino pamene zinthu zisali bwino muzalangidwa nazo za eni.

  153. palibe vuto lilirose apa kodi anthu inu ndiotani tamayendani ntownmu muone m’mene azimayi akuvalira chimidzi too much a malawi iiih.

  154. Nde taonani ena ma comment awo momwe akubwelera maphunzo ndimaphunzo pali zotukwanira apa ?? dziwanda chani ??…pammalo pamene pakuchitika zoipa ndipamena anthu aambiri amathamangirapo coz satana naye akhala akupezapo ake pompo..akanakhala kuti Dun Luu wapanga post pic yosonyeza kut akulalikira mau a Mulungu anthu omwewa akusangalala ndizomwe wapangazi akanayamikiraso kusonyeza kut sakudziwa kuti ichi ndichabwino ichi ndichoipa chilichonse kwaiwowo ndichabwino sinanga wapangayo ndi Selebo,, kma tayesera kupanga nzanga opanda dzinawe kkkkkkk maphunzo azichita kukupeza ndiku inbox komww…..

  155. Za ma celeb mukhala ngati simubrowser ma celeb akunja bwanji ? Mkazi wa diamond uja bwa ? Ndi 20 centuary inu lekani uzimwale

  156. Nde mwana obadwayo dzina lake lidzakhalA ndani???kkkkk
    Chitauni chavuta ku Malawi anzathu ine kusilira malodzawo go diper

  157. Pali nkhani apa walakwa Dan ndi Emmi inu nonse amene mukubwebweta apa mimba simuiziwa , amene ankati alangizi amalangiza za mimba ndani zopusa basi ndi maboza nanuso a news ndi nkhani imeneyo kuti mpaka kukhesera thukuta chamba eti lembani za chimanga kuti chaponda ndi pitala anaba ndalama zohulira

  158. inu mafuna anakawonetsa chende nde mukanati wa iyitha eti ?? ndipo kuna kakhalara kuti kumalawi kuli khalidwe bwezi azimayi akuwonetsa mabwete townmu kulibe.. inu olemba nanu ndachitsilu mulibe zeru azimayi akuvula townmu osalemba zimenezo nde mukanene zoti dan wayalutsa mimba yakazake. mimba nkachaniso hhhhhhhhhhhhhhhhhhhhh mimba nde yomati ayalutsa chikhalidwe ha! mimba nkachaniso inu tagozisiyani ntchito zake zimuchitile umboni basi.

    1. Iweyo ndi 1 amalawi mmmmmmmmmmmm sitizatheka akazi amaonesa zoopsa mutownmu koma kukanena za danlu kkkkkkkjjkk kusowa nkhani eti asa auzeeeeeeeee naoso aike yao nsanje basi kodi alimaliseche nkoyamba kuona mimba kkkkkkkkkkk zaukape

    2. Ndiuchitsirube kma nsanje ndimimba zake zotoporazo taona mimba ife xoti ukhoza kupita naxo Ku photo shooting zauchitsiru basi nsanje yachani ndi agigowo ndinkaxinso ameneyo kapena chimbara zopusa

    3. My people are dying because of lack of knowledge, thus says the Lord. In last days, we shall see a lot, but you…..lift your cross and follow Jesus Christ everyday.

      Foundation determine the finishing of the structure, if we love God and do according to His will, our ways shall manifest likewise if we love things of this World, they shall manifest as well. The Prudent wife comes from the Lord, God bless us and give us heart to understand His ways in JESUS MIGHTY Name Ameeeen!!

      Greetings to my fellow Malawians.

    4. mundifufuza bwanji ndinu apolice kapena nda tukwana iweyo or ndatchula zina lamunthu ?? zingoku pweteketsani mutu, muziyamba zithu zoti muzimaliza mwava izi mukuziyamba apazi simungazi kwanitse.. kapena ukuwona ngati ine nde ndiope kuti iwe undifufuza a! iwe godwala eti ??? usachedwe dzina langa ndilomwe ukuliwona pamenepolo. ukachedwa ndi kupeze ndine mwana wachimidzi..

  159. Voto lake ndilimenelo,ukalitengela kwambili dziko pa chilichonse, umapango zofoyila kumaona ngati ukukhoza palibepo chogwila mtima kuvula mimba yamkazi wako kugulu aaaaa

  160. Dan Timakunyadra Umaimba Boo. Koma Uzpanga Zoganiza Bed Work Shuld Not Be Displayed. Mlemekeze Mkaz Wako& Uzpangangat Umachoka Ku Banja Lachi Khrst

  161. Go Botswana ur going to see Berry Heart a female musician on her DVD n CD covers put pics while nude..everybody has the rights..its non of our bussines

  162. Dziko linasintha talowani m’town mu mukaone nokha mmene azimayi a mimba akuvalira. Palibepo nkhani apa, azimayi akuyenda ndi ma pant, yet they drive their own car. Vuto lake mukutumiza ma comment kuchokera ku Nthalire, Euthini, Kabudula, Nambuma, Msundwe, Golomoti, Masaula, Nyezelera, Muloza, etc

    1. Tru uchimizi wakula apa mmmmmmmmmmmmmm mpaka nkhani pamenepa mimba zikuenda pambalambana munjilamu but …………..liv hm u guys iz it ur ccta or dd u add something kumimba ko nayeso ndimwambo ndilamulo lake mpaka kumulowera panyumba pake kukamuphunzisa mwambo ndiye mwachedatu kkkkkkkkkkkkkkkkkkkk muzanu alibe nazo alipheee kupha money

    2. Tsoka Kwa Ovomeleza Ntchimo Poyenda Ndi Dziko Ndibwino Kuoneka Otsalila Kusiyana Ndi Kukhala Mu Chain Cha Jablos Ambue Akuonen Mwapadela

    1. culture dsnt get civilised…if it ws so then we born in 90″s cudnt knw knw wat really culture is..dats morally wrong..yo mother hid yu for 9months , she nvr showed her belly to the public, somtyms u hav to think beyond measures..thisvis malawi nt niger not tz nor usa..we hv our own perceptions n ethics that we follow..

    2. Kod chukuvutan nchan??? Ndmmene waonera mwniwake mix mkax wakeyo. Inuso pangani zanu cz muwawata mene kungathere bt wont change anythn yah

  163. Dan Lu ayanika mimba ya mkazi wake pa m’mbalambanda
    By Mphatso Khutcha Richard January 16, 2017

    Guaranteed to Make You Laugh – 12 Funny Photos

    ?
    Oyimba otchuka mdziko muno ndi nyimbo za chamba cha Afro, wazizwitsa mtundu wa a Malawi pamene wakhala mMalawi mmodzi yemwe waika zithunzi za mimba ya mkazi wake pa Intaneti.Anthu ambiri ati zomwe wachita oyimbayu ndi kunyazitsa chikhalidwe cha amalawi komanso kulaura. Oyimbayu yemwe watchukanso kwambiri ndi nyimbo yake ya “Sweet Banana”, adalimba mtima kuyiwala chikhalidwe cha ulemu cha chimalawi pamene lachisanu adaika dzithunzi dza mkazi wake Emmie Kamkweche koma dzovula mimba yonse ili padagu pa tsamba la macheza lija la facebook.

    Dan Lu wautsa mkangano pa Intaneti.Malingana ndi mwiniwake Dan Lu, yemwe dzina lake lonse ndi Dan Lufani, poti iye adachilimika kuyimitsa Emmie iye wati ali tcheru kudikira kuti akhale bambo a mwana yemwe akumuyembekezerayo, pamene awiriwa akuoneka okondwa zedi ndi kuyimaku. Koma malingana ndi anthu ena amene akhala akuikapo maganizo awo pa tsambali, akuonetsa osakondwa ndi mchitidwe umene oyimbayu wachita poti wayalutsa mkazi wake komanso wanyazitsa chikhalidwe cha ulemu cha chi Malawi. Malingana ndi macheza a pa gulupu ya whatsap yomwe Malawi24 yawona, yomwenso Emmie ndi mmodzi mwa ma membala, zaonetsa kukwiya kwa anthu pamene anafunsa mafunso mzimayiyu chifukwa chimene achitira izi poti pali anthu ambiri otchuka ndi a ndalama zochuluka mdziko muno koma safika mlingo uwu, koma mkazi wa Dan amangoona ma uthenga ndi mafunso koma samayankhapo kanthu. Gulupuyi yomwe ndi ya azimayi okhaokha, afunsa Emmie ngati mimbayi ili yoyamba ndipo kuti ndi ndani uyo adapereka malango kwa awiriwa pa tsiku la ukwati wawo womwe udachitika mchaka cha 2016.“Koma kudziwika kuli apo koma abale ulemu ndi ofunika, ndi ndani adakulangizani koma?”

  164. Both Malawi 24 & Dan Lu Are Fools. If You Hear His Speech Why Are You Telling Us And You Lufani Why Have You Done This? God Cant Happy Your Speech So If You Are A Satanism Dont Bother Unbornbaby You Should Fear Blood Of God In The Name Of Jesus Amen!!

  165. Musiyeni eee nayenso ndi mmene wachimvera mumtima mwake nanga pali amene sadziwa mimba apa? Akunama iwe nyada ndi nthawi yako azaziwa bwaa?!!

  166. penapake panyo panu ko mw24…this is 2 personal 2 b news…musiyeni munthu inu simukuika za ma banja anu bwanji….nsete zanu bwanji

  167. Tisanamuyamikire munthuyu ngati wapanga zanzeru,,,ma cerebrity akunja amapanga zimene zili chikhalidwe chawo,,,nafenso amalawi tili ndi chikhalidwe chathu uyu ndi cerebrity wakumalawi n malawi nkazi wamimba amamupatsa ulemu,,,apapa Dan Lu waonetsa uchitsiru wake wonse,,ndipo anangotengana onse ndi mkazi wake anthu opanda mzeru,,,,

    1. nanga iwe ukumayankhula anzako kut achimidzi,nanga iweyo ambuyako aja mesa ali ku mudzi komweko andinso xmas ndi new year udali komweko.kumangoti uli town ulinso ku tchire kwa chabe chabe.

    2. Chiwanda, zapansi pansi panyanja akufuna kulaula dziko mtundu wa amai. Mai ake anamubisa miyezi 9, koma ngakhale tsiku limodzi bambo wake sanabwerepo kumtundu wa amalawi ndikuonetsa nyansi izi.

    3. Anthu inu ndi aja mumakhala zaka 10 muli mmanja koma kumangonyengana usiku usiku okha okha osamasukirana. Chalakwika ndichani apa? Mungalore kuti nkazi akuyamweni inu? Bwanji osayang’ana kumbali ngati simukufuna kuona?

    4. Anthu inu ndi aja mumakhala zaka 10 muli mmanja koma kumangonyengana usiku usiku okha okha osamasukirana. Chalakwika ndichani apa? Mungalore kuti nkazi akuyamweni inu? Bwanji osayang’ana kumbali ngati simukufuna kuona?

    5. Kumangoimbira mmanja zilizose
      Bwanji kodi amalawi? Eh Amene mukuti wapanga zabwinonu pansi pa mtima mukuziwa kuti muli inu simungapange zopusazi kma apapa muku sapota
      #Shupit

  168. Naoso asocialmeadia osamakana zinazi analipira zingati kuti mutengeke chonchi m’malo momatiuxa zamene nyengo iliri chaka cha2017 koma kumafatsa kutilaurira dziko ngati mukuyamba Inu akulu Akulu ngati inu ana anu akamawelenga aziti mchani stop to distloying my malawi plz

  169. nanu amalawi yakula ndi nsanje , walakwisa chani mimba ndi maliseche kodi , musiyen ndi yake akuinyadira ngat zakuwaw kakolopeni nyanja inu osapanga yanu bwa ngat mumantha ? palibe chachilendo or chodabwisa apa, kuzolowera ka moyo ka chimidzi muziyenfe kumadziwa maiko ena zomwe amapanga, lyk ku joz mwana wa xul amatha kukhala ndi mimba kumaonetsa azake bwino bwino opanda oyankhula amunaso kumaikisa pa public aliyesa akuona ngakhale sali yawo mimbayo , nde palibe chachilendo apa , mungokhala chete azitsiru inu ndi umbuli wanu , mesa mukuziyalutsa nokha kod , wavula kaziyo kut mwaona malitseche ake ? zikusiyana pati ndi azikazi anu amasiya ntchafu pa mtunda kumapita ku ntchito???????

  170. Amalawi palibe cholakwika2 pamenepo mkazi ndiwake mimba ndiyai awirio akudziwana kapena mkazi wake anabwela kuzakudandaulilani? Mxwieeeee mukanika kufufuza zachimanga apa basi fwiiii fwiiii fwiii mphuno zanu pa banja la eni iyaaaaa

  171. Kusowa khalidwe mai wachimalawi yemwe ndimuziwa ine sanga tele, chifukwa amachilemekeza chomwe wasedzacho tisataye chikhalidwe kamba kakuimba, sibwino yesani kusunga ngodya zinai.

    1. Iwe fatsani sindidanene zaiwe apa komanso lulu ndi mwana wapakwathu uneyakutandana ngangusaka nombe mmwej mkasalile wankwenu.

    2. Iwe fatsani sindidanene zaiwe apa komanso lulu ndi mwana wapakwathu uneyakutandana ngangusaka nombe mmwej mkasalile wankwenu.

  172. ana aku nigeria adachenjela kwambili ngt ana akujoni kuno ine ndikuziwa kuti akumupusisa ndi nzake uja kcee adaimba nae swt nthochi (banana) ana a nigeria amapusisa anzao kwambili even psquare adamupepelesa Akon mu chop my money so oimba athu ali pamavuto opusisidwa kwambili taona nao sindidaonepo mkazi wa pha

  173. Chimavuta a Malawi kukopera zinthu izizi zinapangika ndi Diamond ku Tanzania naonso awa eti ayesere ndizomwetu a Malawi zawanyasa bro

  174. Chimene ankafuna chitachika pamoyo wake ndekuti ndichimenechi afuna mutawona..kaya mimbayo sadapeleke ndiyeyo kwankaziwake monga mukukambila enanu izo ndizake palibe chotikhudza ife…ulemu umadzipatsa wekha munthu

  175. DIFFERENCE BETWEEN A EUROPEAN FACEBOOK PAGE AND A MALAWIAN FACEBOOK PAGE!! UK PAGE
    Hello Admin, my name is Keisha Brown, I am from Winchester, I love my husband so much and I can do anything to please him. But recently I am falling for his young brother who has come from Nottingham to stay with us, he’s so irresistible, what should can I do?plz help.
    *COMMENTS:*

    1. Chris James: I think u need to talk to a marriage counselor and see why there’s a sudden lack of interest in you for your husband.
    2. Sarah Waters: oh my dear, sorry about that. Have been in your shoes before, I had to wake up and face the fact that I am married.
    3. Michael Peters: well just remove your mind from him and make your husband do the things you like in his brother..

    *MALAWIAN PAGE:*
    Hi Admin. My name is Janet Lungu, I stay in Kanjedza, am married and my husband and I have a child, but recently his brother moved in to stay with us after he finished his studies at CHANCO. Quite frankly, I am falling for my husband’s brother! He is what every woman wud love in a man.. Plz help, what shud I do?

    *COMMENTS:*
    1.Stella Kaduwa: You are a disgrace to womanhood. Shame on you!!!
    2. Brenda Chikoti: Ndiye ife ukuti titani? Za uhule basi!
    3. Frank Mataya:Wakula watha usova.
    4. Maria Banda: Holy ghost fire..
    5. Mercy Phiri: Uzafa imfa yowaws kapolo iwe ndi ndata yakoyo ukufuna uzingowonetsa aliyense ndi mulamu wako yemwe. Mbuzii
    6. John Chowe: Galu iwe, osamangozikanda bwanji?
    7. Peter Nankhuni: Mongokumbutsana, Tottenham 2 – Chelsea 0. Ife kumva kukoma.
    8. Linda Magombo: Odi uko!
    9. Thokozani Mwale: u need deliverance ndithu. Accept Jesus now! Uzafa chopolama

    1. Mbuzi palibe comwe walemba . Wekha ukunena kuti european page ndye umafuna zikhale zofanana ? We differ in customs in many ways . Kape cosa cicomment cakoci

  176. Ngati ali dolo atiwonetsenso chipangizo chomwe angwiritsa ntchito popereka mimbayo. Other wise iyeyu ndi kape tisamusekere chifukwa amatha kuyimba. Woyimba ndi yekha kuno ? Iyaaaa!

  177. imwe mwe wanthu wakwenda nthumbo pawaka sono munthu wabudach ?wanthu wanyake nomahala yayi kkkkkkk nthumbo njake mleken myinu nkhukhumba kwake see!!

  178. haha koma anthu mulibe zochta et?pali nkhan apa mwayesa inu okanika kuyenda ndi akaz anu akangotenga mimba…ndpo chikhalidwe chake chiti bwanj akaz akumayenda atavala ma bam short n malaya oonetsa mchombo koma simukamba kut ataya chikhalidwe …mxiiiii

    1. hahaha@princess ndinali ndli mwana ndisanaziwe choipa ndichabwino nanga 2011 ndipano udikire mkatenga mimba ina 2020 ndizaika koma ine simkuona pulobulemu

    2. nanunso apa zugwilizana ndi dubai…ubwno wake nkhan ili apa ndiyaku malawi si dubai…mumkaleka kubadwira ku dubai ko kut muziona town yo…tilibe nawo ntchto

    3. nanunso apa zugwilizana ndi dubai…ubwno wake nkhan ili apa ndiyaku malawi si dubai…mumkaleka kubadwira ku dubai ko kut muziona town yo…tilibe nawo ntchto.

  179. Agalu awa kenako azationesa zomwe agalu amapanga akafuna kubeleka,Dan lu kapelekeni mkaziyo siwanu kkkkk mimbayonso siyanu

  180. Thats celebrity life dont blame him, Malawi what is culture nowadays…outside celebrity also do that to their fans, pa malawi chilichonse ndi ufit basi

  181. Thats celebrity life dont blame him, Malawi what is culture nowadays…outside celebrity also do that to their fans, pa malawi chilichonse ndi ufit basi

    1. Hy Mr..paumunthu wake inuyo mukudziwa kut sizabwino wapangazi..ndikaona dzina lanu ndikutha kuzindikira kut mwina ndi Muslim nzanga do u think kut pali kuopa Allah apa ?? comon broh osamapanga support zithu zofoila ngat kukunena kut ndiufulu wake kupanga izi ndizoonadi ndiufulu wakedi but remember kut ukamatsata zaufulu wako make sure usaphereso anthu ofulu wawo..apapa waononga Ufulu wa aanthu ambiri omwe amabisa mimba Kumalawi kuno..ngat sindinakuyakhuleni bwino khululukani….

    2. zikanakhala kut ndizabwino wapangazi mwinaso iyeyu asanapange oyamba kupanga ukanakhala iweyo coz ana ulinawo ndithu.. bwanji sunayanike mimba yako poyera kut anthu ayione ?? yako mimba unakwanitsa kuyibisa kma iyi nde yoyenera kuyanika poyera ?? mindset…

  182. Mkaziyu ndi wake akuyenera kupanga naye zonse angafune taona ambili ataikanso nawo ndi wachikondi wawo ali maliseche uyu chavutapo mchani

  183. Kkkkkkk mtengo wautali salozerana.zangoonetseratu apa kuti akuluwa satha ndipo sadzathanso.okumba fulu sachita phuma.kukangalika chonchi pa air koma apanira mphika alipheeee.kkkkk

  184. uku ndye tmat kuolokela pamatope mndato ukuwuona,,,azmayi amimba osewa amabsa iwe mkumavula pagulu zoona,,,,,,,? khala nd umunthu kd aliese azcta kudzwa kt umamwa #gondolosi

  185. Dan Luu amabeleka? mimba ya fisi iyi mkaona akupanga zopusa ife tili ndi ana ankhaninkhani mmidzimu komano pokhutitsidwa ndi ubeleki wathu sitipanga izi fuck……!!

  186. Dan, unamvapo mawu oti{miscarry}? Ngati n’chibwana, stop it. Mkazi wamimba timati {wodwala}. Two things can happen. Kuchila kapena ku mwalira. So watch out. Nanu azimayi, makolo anu anayamba apangapo zimenezi? Tamawakanirani amuna opusawa in strong terms.

    1. Why fear negative side? Zoona munthu wamoyo angamaseweretse mimba ndi ya mkazi wake. Azaziwa kuti ndimatenda amenewo ochilira ku hospital ngati m’chibwana.

  187. Palibe vuto apa inuuu!…koma akhale wakunja nde kumasirira ..musiyeni akunyadira katundu wake…inu mimba za akazi anu zili biiii ngati achule mungaziike pa air…mwagwa nayo chapweteka abwerere ku ma 1980..man Dan ali bho kashikena bwaaaa!

  188. Akukuwonesani nanga kuti iyeyo ntchito ku bed amayitha osati kumangokhala ndi nkazi ngati mlongo wako palibe cholakwika unless amene walemba khaniyi zimakukanika ku bed

  189. Kodi mwamuna oyamba kubereka ku Malawi kuno ndiiyeyu? I don’t think if this pregnant is for him. This is one sign of kusalowa mnyumba,ngati ili mimba yoyamba mbuyo monsemu samanyenga? Why he didn’t show us mimba zimenezo! Muzagulisidwa matewera mimba ya weni inu kupusa kwanuko mxiee

    1. Mpaka mumenyane chifukwa cha mimba ya Dan Lu? Musiyeni nkazi ndiwake, bwanji osaphulixa wanu? Iyeyo ngati sakuonapo vuto what’s wrong with u? Dan Lu ndi Celebrity, nkazi wakenso Emmie Kankweche Lufani ndi Celebrity inu muli mbuuuu.

    2. Nsanje mimba sichinthu choopsa kodi ndipost yogonana????????? Inuso muli ndizomwe mumapanga but coz u dnt hv nem dats y u dnt post mmmmmmmmm liv dem alone u ppo

    3. Iweyo ukuzitenga ngati dolo zizungu zolowezazo kuchokela mufilimu ukhale dolo sukanathawa pamalawi,zangosonyezelatu kuti unalezeka std8,ukhalila yomweyo yamaboza ngati siiwe muthu wammuna

  190. Man Dan Ndnu Otchukadi Mwava? Kungokulekani Amene Sanapelekeze Mkazi Ku Scale Ndamene Akuona Zachilendo Ana Okhaokha Awa Mimba Saidziwa Mmdani? Sanje Ku Malawi Sidzatha

    1. Iweyo umakonda zodabula not anzako uli ndi umboni anakunyengapo kuti uziwe samabeleka dis z not first child for dan he hv another one already mind ur business

    2. Ndiye kuti mkazi anamusiya (Thoko) amkakana izi eti? coz paja anamusiila mwana maybe that’s why anamusiya amafuna omamuyalutsa chonchi. congrats Thoko sunalole zoyaluka

  191. DAN APA SANACHITE ZINTHU NGATI MUNTHU WOZISAZA ngat mimba imeneyo si yake amayenera kukambiri mwa chisisi osat kumuyalusa chochi….

  192. Ndwmwayaluka ndinuyo??? Mudziwa bwanji mwina nkuyamba kunamizilidwa, kt ndiye wagwira ntchito imeneyo. Inu mukufuna asadzionetsele kt amagonana kwambiri

  193. Ndiyankhule motere amwene Dan nthawi zina ndibwino uchisilu kumausiya kunyumba zomwe mwapanga inu apazi ndi zinthu zopusa chamba kapena chani?

  194. mimba yoyika pa mbalangandayo ikhale imeneyi mmmmm mulibe mzelu munangokwatirana chifukwa chakuti aliyense anali neba wa mzake amkadutsa pa khomo la kwau dairy mulibe nzeru.Mimba yochititsa manyazi ngati iyi inu simunawone ngakhale nkhuku imabisa mazira kuti anthu asawone kufikira itabeleka ndiye inu mukanyozetse uchembere choncho.

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading