![Malawi Police](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2016/02/Lexten-Kachama-235x176.jpg)
Kachama sapepesa
Mkulu wa Malawi Police, bambo Lexten Kachama wamenyetsa nkhwangwa pamwala kuti iye, ngati yemwe anakhalapo pa udindowu a Peter Mukhitho, sapepesa kwa Jessie Kabwila. A Kabwila, omwe ndi phungu wa chipani cha Kongelesi anamangidwa pamodzi… ...