Champweteka chimanga Chaponda: Amuchotsa pa unduna paja


George Chaponda.

Atapulumuka kwa kanthawi, tsopano wagwa chagada George Chaponda.

George Chaponda.
Chaponda champweteka chimanga

Chikalata chochoka ku nyumba ya boma chimene wasayinila mneneri wa a President chalengeza kuti a President a Peter Mutharika amuchotsa Chaponda pa unduna.

Malinga ndi chikalatachi chimene a Malawi24 tachiona, a President ati atenga mphamvu zonse ndi ma udindo a unduna wa zamalimidwe.

Kunalowa chipolowe ku unduna wa zamalimidwe pamene nduna yake inapezeka kuti inachita utambwali.

Sponsored

207 thoughts on “Champweteka chimanga Chaponda: Amuchotsa pa unduna paja

  1. I will be glad if Chaponda is going to mention others in order to fire them all

  2. Kodi iwe chaponda mutu wakoo anakupondani amai ako uli mwana .??? Nakupangani amai ako pokumbeka chonchi chimutu chonyasa dengu latomato ku Ncheu. Amathamangira kuti bambo ndi amai ako. I mean time for sex masimmba amuthu

  3. Joseph. Mkasa ndi muthu chinzeleze ophunsa iye amafuna. Kungelera ndalama kapena kuti papsa tonola .mutu uja sugwirchito anawagwensa amai ake Ali mwana.wang’no Ali kumbuyo kwa amai kumunda

  4. Point! Play a song to this man called chaponda done by Joseph mkasa dedicated to him….
    Mr Mkasa backed up him with total mind but he forgotten that “chomwe wamkulu sakuchiina atakhala pansi…ngakhale ana ngati che mkasa ndi ineyo pandale or titakwera mumtengo…sitingachionenso.

    Mr mkasa can u just interprete that song as quick as u can paja simumachedwa kutembenudza.

    Shame! Malawi! Above all…the heavenly judgement is heading you…if u don’t repent!

  5. Peter and Chaponda are congruent. Look at them. They seem to be brothers from same parents

Comments are closed.

Discover more from Malawi24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading