Atapulumuka kwa kanthawi, tsopano wagwa chagada George Chaponda.

Chikalata chochoka ku nyumba ya boma chimene wasayinila mneneri wa a President chalengeza kuti a President a Peter Mutharika amuchotsa Chaponda pa unduna.
Malinga ndi chikalatachi chimene a Malawi24 tachiona, a President ati atenga mphamvu zonse ndi ma udindo a unduna wa zamalimidwe.
Kunalowa chipolowe ku unduna wa zamalimidwe pamene nduna yake inapezeka kuti inachita utambwali.
Sponsored
207 thoughts on “Champweteka chimanga Chaponda: Amuchotsa pa unduna paja”
Comments are closed.

I will be glad if Chaponda is going to mention others in order to fire them all
We are not vote Peter muthalika but he was stealing vote Malawi news.
Mkasa nayenso achotsedwe pa gulu la oimba
Kkkkkkkkkk
You can do what ever you want coz its your time, but dont 4get that it will become the time of others. Then you will feel pain when they will do things according to their time, time tell you’ll blve this
Kodi iwe chaponda mutu wakoo anakupondani amai ako uli mwana .??? Nakupangani amai ako pokumbeka chonchi chimutu chonyasa dengu latomato ku Ncheu. Amathamangira kuti bambo ndi amai ako. I mean time for sex masimmba amuthu
Joseph. Mkasa ndi muthu chinzeleze ophunsa iye amafuna. Kungelera ndalama kapena kuti papsa tonola .mutu uja sugwirchito anawagwensa amai ake Ali mwana.wang’no Ali kumbuyo kwa amai kumunda
Nkhope ya chapondayo ikuyenera kukhala nyapala osati nduna ya boma
Ammange ndikumulanda ma billion WO. Mkutigaila aliyense ma 5 handz tidye nao
Musiyeni adyeko ndalama za boma
La 40 lakukwanirani mdara. Tachiwoneni ngati achidyetsa manyii. Utimva kuwawa iweee
Point! Play a song to this man called chaponda done by Joseph mkasa dedicated to him….
Mr Mkasa backed up him with total mind but he forgotten that “chomwe wamkulu sakuchiina atakhala pansi…ngakhale ana ngati che mkasa ndi ineyo pandale or titakwera mumtengo…sitingachionenso.
Mr mkasa can u just interprete that song as quick as u can paja simumachedwa kutembenudza.
Shame! Malawi! Above all…the heavenly judgement is heading you…if u don’t repent!
Achoke
Lafika la 40 achimwene anga achaponda muziona mumaba nokha kkkkkkkj
Peter and Chaponda are congruent. Look at them. They seem to be brothers from same parents