Cama wants govt to set maize price

Advertisement
John kapito
John kapito
Kapito: Maize price should be set.

The Consumers Association of Malawi (Cama) has asked government to set low price for maize in order for people to afford the staple food.

Currently, a 50 Kg bag of maize is going at K5500 Kwacha at Agriculture Development and Marketing Corporation (Admarc) depots whilst vendors are selling it at the price of 13,000 Kwacha.

CAMA Executive Director John Kapito said government should set low price for maize and should make maize to be accessible to rural residents.

”There is need for government to set an affordable price for people to easily access it at an affordable price,” said Kapito.

Recently, government warned vendors who are buying more maize at the Admarc depots and selling at exorbitant prices that they will face the law.

Advertisement

14 Comments

  1. A CAMA,musatiphimbe kumaso akuikani big banzi mkamwa ndiye mukulephera kuyankhula.But kumbukirani kuti a Malawi siopusa pokusankhani kuti mudziwayakhulira pa mavuto ngati awa.Why nthawi yonseyi munali silent?Kodi si inu amene munali kutiyakhulira very powerful dzana lija mpakana zidachita affect wina kutsikira kuli chete?Kodi mavuto amene aja ndi alerowa akulu ndi ati?

  2. Sangasitse mtengo ndizomwe amafuna tiyiwala kuti ali ndi ma farm ndi nthawi yake yopanga profit ali ndi chimanga chambiri in his backyard

  3. kumalawi tilibe atsogoleri anzeru. anakakhala kt nanalipo sibwenzi chimanga chikusowa.just magine 50kg of maize ealy 2015 was at k2.5-k4000 nw at k10-k13500. nkumati amalawi ndmakukondani

  4. Our nation has no presedent, if there is, why is no paying any concern or attetion to such kind of big hiccups that vunilable malawians are moving through. He is just like a road sign, he dnt even stand and talk. Thanks CAMA for airing ur concerns about this, though it seems to be late but u tried ur better to waken up this mambumbani readership. Mr. U need to kill all poor villagers in dis dirty style?
    if it isnt, then what is this? I never seen a doomed presedent like u in this country. I wish u ld just die, u got no even a vission a bout malawi. God must show his wrathy agnst u, am very very sorry! hooooooooo! Am i dreaming?

  5. Zomwe ayankhula a Camazi ndizo-ona koma ngati ndi zo-ona kuti akumapanganawo ma secret metings ndi a Chakwera, amabungwe ena kuti alande boma aziwe sitimakhulupililanso, ndipo timawakaika ndi kale kuti amabungwewa ndi adyera kuyambira pa Bingu aziwe

Comments are closed.