Gift Manison, a 19 year-old Malawian man in Lilongwe city , has been sentenced to 15 months in prison with hard labour by the Dedza first magistrate court after being found guilty for the offence of trespassing on a burial place.
According to state prosecutor Sub-inspector Bauleni Namasani, the convict trespassed on a graveyard in the area of village headman Katsekaminga in Lilongwe where he stole a picture frame belonging to late Steve Chizala’s late mother.
In his judgement, first grade magistrate Symon Mwambo slapped the convict to 15 months in prison as a warning to would-be offenders.
Dedza deputy Police spokesperson Constable Cassim Manda said he is satisfied with the sentence.
“What the convict did was not only a breach of section 129 of the penal code but also a total breach of section 26 in chapter 4 of Malawi’s constitution,” Manda said.
Manison hails from Katsekaminga village, Traditional Authority Kamenyagwaza in Lilongwe.
Hahaha
kkkkkkkk koma umphawi sizithu mpaka pikitha fulemu ya pamanda
Wobayo ndi ntumbuka? Kapena chewa?
Zafika Povuta Kuzisaka Kwamtunduwanji Kumeneko Pena Khalani Ndi Umunthu
Kkkkkkkkk..zakuba zake aaaaa
Kkkkkkkkk..zakuba zake aaaaa
koma abalee3ee
koma abalee3ee
gyz mpaka kuba kumanda? ukacita ganyu bwaa?
Sanalakwe manio akufuna akakongolesere tchemba mwao,osamulakwila ai siyeni mu2yo kolesedw ndie kt cani apa anakatengaso mtandao akapange makasu ozalira or mipeni ma batcala ena mpeni tilibe
Akumubakirayo naye akuziwapo kanthu zao ndizimozi,aa bm limangoona kukana zaufiti munthu wazeru akabe kumanda km malawi tichitepo kanthu.
Achewa amavalila nyau zao,komweko ,kuli ngati ku office kwao .
umphawi wafika povuta munthu kusowa mtengo ogwila Malawi akumvesa anthu kupweteka
Zakumva kumvetsa mutu mulandu suchepa kukhala munthu osaba mkusagwidwa muliposo m’bomamo mukuti mwabisala koma la 40 lidzafika wakuba a mawa mudzakhala inu. chigwire nyanga kwa wina mawa ndiwe
umphawi wafikapo kumalawi
ku lilongwe kuno m`manda ndi ku dambwe palibe zachilendo
Palibe za shame on u apa, flamemuyo imangokhala yopanda ntchito in’yeyo alinayo ntchito sanalakwe kutola chopanda mwinicho
wabadi ndipo amumanga
Awanso ndiye awonjeza bwanji,,,,,mmmmmmmm
kuprison kwacani,apolic inu kusowa anthu owamanga eti,osalimban ndimbava zomwe zaba ndalama zakhanikhan bwnj
Section 184 ya penal code imaletsa kupezeka kumanda popanda authority choncho police yakwanitsa lamulo
mwina anatumidwa ndi sing’anga ku akakhwimire
Ntchito za achewa zimenezo munankhala bwanjimwe wanthu oipa imwe
Gyz u should 2 understand malawi wavuta & their is np way
Thats is fucken bush sheet
15 months for stealing apicture frame? Then the cashgaters must have 200months for every 1million.
Mmmmm guys, ndi nkhanitu yaikulu imeneyi. Tisaitenge mopepuka ayi! Amangidwe ndithu. Anthu ngati awa ndi amene amakonda kufukula mitembo ya ana ang’ono aja. 15 months yachepa, zaka zitatu bola.
wah baaa enewambo ku nyasakupotsa satana? shaaaa
Zili bwino.
Imagn
Katsekaminga Vg, TA Kamenyagwaza in Lilongwe. Really? Malawi 24?
Obim Chiboy Nonso
hmmm
wali ni probulemu ameneyo wakufunika ku mental
Just give him a corporal punishment basi.
Achewa kutukwana anthu akumpoto kwambiri,ndiye mwazionela,bwelani kukabwafu muzapitilize kutilimila fodya,kumeneko mwachulukana zitsiru zawanthu,fokolo muwuzane osatukwanaso atumbuka
Trespassing mlandu wake.kumanda pamalamulo nkolesedwa kupezekako wamba.zoona guys mukuti wabela ndani olo wadandaula ndani?Are u sure inu koma?shame on u all nzelu ngat mbavayo.
NDALAMA YAVUTA NAYE APEZEPO
Manison ameneyo am sure naye ndiwakumupoto sichoncho?kunyoza mpoto too much yet kwinako mumachitazodabwisa ngat zimenezo.Zoona mpaka kuba pikicha felemu kumanda eeee….man ulimo!!!
Akumwera omwewa Opanda nzeru!!!
#Pheshaj and Frank ndinu zitsilu…pali nkhani apa yoti munyozere anthu akum’mwera
Wanzelu ndiwe.Kufuna kuchuka eti???
Wachita bwino kukaba kumanda,kusiyana ndikuba mnyumba zawanthu,ndiye mukummanga,mlandu umenewo wamulakwira ndindani?
Mtembo kkkl
Akanakhala mtumbuka
Kkkk mpaka apa aaa
Ameneyu angazibe yekha mpata ataupeza
He deserv lyf in prison …he is stupid……
Ya ndi mlandu basi ngakhale uli ochepa
Akut framegate. Kkkkkk
kkkk mtima sunali malo pamene anali kumanda akamaona anthu akuyika maluwa kkkk
pali chifukwa pamenepo ????
Fucken people
Mayb he wntd 2sell da pictre frame. magulu a an2 oba mafuwa amenewa.
Zamkutu! Zalowa ndale. Abale nanga chilango chawakuba mafupa amunthu kufewa nakhwima cha wakuba frame?
Zamkutu! Zalowa ndale. Abale nanga chilango chawakuba mafupa amunthu kufewa nakhwima cha wakuba frame?
Kkkkkkkkkkk! Madness
Hahahaha,mpaka kukabera akufa?ufiti umenewo
Sanabe mesa atola chotaidwa kutchire
Kkkkkkkkk a picture frame ,l think he is mad.
Ndiwa zaka zingati ine Ku mpoto kuno matenanti apelewera
Ndi doro!kumapanga zosiyana ndi anthu,nanga kumangoba mmanyumba,mma office?kkkkkAMENEYU NDIOVUTA HEAVY!!
Nanunso apolice mudziona zomangira anthu ku malawi kuno kusowa zochita eti? Pali nkhani yoti munthu ndi kulowa pa OB apa or ma criminals atha ?
Nanunso apolice mudziona zomangira anthu ku malawi kuno kusowa zochita eti? Pali nkhani yoti munthu ndi kulowa pa OB apa or ma criminals atha ?
Kodi court anthu ake m’mesa amakhaka oti anaphunzira bwino, ndie angamagamule milandu yoti m’criminal law mulibemo? Komanso mutafufuza mwapeza kuti amugwira kumandako ndi apolice?Have some questions in your head and ask then judge.
Akuti mulandu wa framegate kkkkk. Malawi sadzatheka. Nanga pali mulandu pamenepa
Wabera ndani? Who is a complainant?
Ulipo mlandu,trespassing kumanda ndikolesedwa n inu mungakondwe restn place ya abale anu yoti munavutikila kukongolesa wina wake wakachochepo jst lyk that?nkhalani ngati anthu oziwa momwe manda ndi malilo timawalemekezela kuno.
Kkkkkk a Picture frame what for?I think he made
shaa! Achewa asowano chochita mpaka pamenepo mvula yagwayi osamakadzala fodya bwanji?shame
T/A Kamenyagwaza its in Dedza…not in Lilongwe…..kaya mwina ena andithandize di we have this TA in Llwe?
Bt Why?