![](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2024/07/IMG-20240716-WA0013-235x176.webp)
A Chakwera ayamikira atsogoleri a mpingo wa katolika ndi mayiko awo pogwira dzanja Malawi
Mtsogoleri wa dziko lino, a Lazarus Chakwera wayamikira mpingo wa katolika motsogozedwa ndi ma Bishop ake maka mayiko a Zimbabwe ndi Zambia ponena kuti mayikowa agwira dziko la Malawi pa mkono mnyengo za mavuto. A… ...