
Zativutanso!
A Malawi ali pakalikiliki kuthamangila ku ma okala kuti apeze nawo mwayi ogula shuga yemwe akusowa zedi mdziko muno.
Shuga wasala ochepa zedi mu magolosale aakulu ngati Shoprite, Peoples, Sana Cash and Carry komanso Chipiku.

Malingana ndi maripoti, izi zili chomwechi chotele kamba koti kuli mpungwepungwe pa nkhani za mgwilizano wa pakati pa kompani yomwe imapanga shugayu ya Illovo komanso makampani onyamula shuga kuchokera kumafikitale kupitisa mmisika. Koma a Illovo sanayankhulebe kalikonse pa za nkhaniyi.
Mu Shoprite mwachitsanzo munthu sakuloredwa kugula mapaketi opitilira asanu ndi limodzi (5) . Izi zaikidwa kuti aliyense aguleko shugayu yemwe akugulidwa ndi anthu mokanganiliana.
Izinso zapangisa kuti shuga afike pa mitengo ya K950 komanso K1000 kupyole mtengo ovomelezeka wa K750.
Mmene zililimu, pofika sabata la mmawa, shuga akhala atatheratu kamba koti mumagolosale ambiri watheratu.
Pakali pano bungwe lowona ufulu wa ogula la Consumers Association of Malawi (CAMA) lati kampani ya Illovo iyenera kunena ku mtundu wa a Malawi vuto leni leni la kusowa kwa shugayu.
IIllovo ndi kompani yokhayo yomwe imapanga shuga ku Malawi.
Anthu azisaporta tima small shop basi samapita ku sp kwanuko
Bola special akupezekabe pa mtengo wa k550
aaah koma nato suzathekaxo
Hahahahahaha ha Kaya amene amamwa Tea, hahahaha sugar k1000
zovuta kuteloko sugar ntengo wake weni weni ndi 750 koma yeah
Panja 2014 tikati ophuzila zakwanitsa wakhalapo kwa America ndiye rero ndizi maganiza kundetsa dziko ndichindu chobweka ngat kupalasa njinga tionana 2019 ngat zabereso galu amenowa ndalama zanthu zamisonkho mungodya muliphe inuwake ndikuvutika
My Malawi my nation where we are going? Don’t worry if your are born again belivers bible its explain already for the last days
Shuga gate
kkkkkkkk mbc news after the minister josephy mwananveka visited ilovo company,”sugar wa brown akusowa chifukwa anthu ambiri akumukonda”
tizigwilitsa ntchito waku zambia.uyo nyadanayeni amalawi kuyelekedwa No1
Vuto Ndi Awa Otsutsa Boma, Ndi Amene Akusowesa Shuga Wathu.
Kkkkkkkk mapaketi asanu ndi limodzi 5 ngakhale school ya atsamundayo ndi choncho.
Write a comment… Kuno ku Nkhatabay akupezeka wambili packet 750
Write a comment…
Welcome to Malawi
RIP in advance
ulendo wina wayandikila apo …don’t worry Malawi
Fuck malawi government.
Sugar ndi chani??…sinagulepo,akapezeka ku shoprite kokha?..
ife ku dedza tilibe problem. wa Mozambique basi
Kodi shuga amene timapangayu akupita kuti gayesi osabisatu shuga
Write a comment…
shaaa dziko mpaka lomasowa shuga mavuto sazatha basii
that y ndimangoipota
Anthu nonse omwe mukunyoza boma nkhani yasugar mitu yonu sigwila ayi. Sichinthu chachilendo sugar kusowa kumalawi
asanu ndi limodzi(5) kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
Aaa ndizingomwa juice wa Wakawaka k30 chikapu ndeeeee
Kkkkk, asanu ndi limodzi nkudzati (5)? Scribes! Hey!
Ife tikumagula wa ku mozambique pa lizulu @ k800
Apa guyz tea xitimwaxo mpak grand mmmmm km malawi waonongek bc
its time to learn how to leave without sugar, we can copy from China people.
Anthu enanu muli m’mabvuto akulu ganyu wabvuta. Kodi panyumba kapena ndinene kuti pabanja zinthu zogwilitsa ntchito monga mchere,sopo,macheso,suga ndi zina zikatha amauza mwana kuti akapeze zinthuzo?Mwina kwinako zimatero,koma kwathu kuno timauza amene ali oyang’anira pabanjapo kuti athe kutithandiza.Ndiye ena mukuti tisaloze chala boma kapena pulezidenti ndiye chabwino tasintha inuyo inu tipatseni kapena tulutsani suga anthu asabvutike nkulimbirana pogula.Paja zinthu zikavuta olamula amakhalanso otsutsa muja idachitira UDF atachoka Bingu nkuyamba chake chipani ndiponso DPP idalinso yotsutsa nthawi ijayi atakhala pa mpando mayi Joice Banda pomwe dppyo ndiye inkalamula boma.Zinthu zabvuta kumpanda madzi achita katondo.
mwina ayibaso Sugar kumeneko, nanga wasowa bwanji.
Ndiwo Ana A Munthalika Ulamuliro Tidauzolowera Sizachilendo(chimanga Chochuluka,ndalama Kusowa,malipiro Kuchedwa,ngongole Zambiri Ndi Kusowa Kwamafuta Omwe Asowaso Posachedwa)komabe Timakunyadirani Poti Ntidziwitsa Kuti Sukulu Sichotsa Uchitsiru Moti Ulemu Wanu
https://www.facebook.com/LCPMWOFFICIAL/?ref=your_pages
zintchito za diphiphi ndi kunda palibepo zachilendo apa!
Kkkkkkk mizimbe yatha ku farm
Let me eat zimbe Ku NCHALO kuno…mundipeza Ku KALULU or Ku area 4
It started like this with the late Big Kahuna nd now this young Kahuna is following the footsteps of the bro
Ife ndi abawa inu makape omwa sugar munya nayo pamodzi ndi uyo wakhala pampando
kkkk dziko lauhu panopo likukoma kwambili chili chonse chiku sowa apa ndiye zayang’ana kungolo
Kkkkk km boma ili iiiii tizingwira sitinati next mafuta agalimo km amene anatilozayo ndifitindi
apezeka weekend Yamaha bona latelo
Bullets ikwapura ambwenu mbwenu kumpoto bb woyeeeeeeeee!!
Kukhala m’malawi ndikulimba mtima
Many people r politicizing the issue of sugar scarcity.People who r pointing fingers at the president and his gvt r doing so coz of their negative attitudes towards the president.I know that people who r politicizing this issue r MCP and PP supporters.One word to u is that no matter how u spoil the image of the president,u shall not win the elections.Munyenyedwa kwambiri ndipo muzanamanso kuti mwaberedwa chisankho.Game simuzaiwona.For ur own information,shugayo wayambano kupezeka.Pezani nkhani ina yokamba
Kaya ndi bambo ako iwenso udziwe kuti nthawi yake yolamula Malawi afuneasafune izatha ndithu.
Ai peter ndi boma kale tu
Ife kuno ku Nu sizitikhuza za kusowa kwa sugar coz wambiri zeediiii akubwera kuchoka ku Moshiko
mulibwino kuno ndi k1150
Kwaaaaa kkkkk who care
kaya timwelalimozi juwisi inendamuzolowela mukut sugar mukanat mages ife tikanadandaula chifukwa mitembo ikananunkha mzipatalam
Hehehehe!!!koma bodza liriko shuga wambirimbiriyu? PaNyOPanU
Pachema
Kodi sugar amene timagwiritsa ntchitokumalawi Amachoka kuti Moti akulowetsaso ndare ndishuga yemwe Koma Malawi uzasinthaliti Zilizonse Ndale Eiiish
guys ndindani amagula ma packet 6 apa? chosecho ambili timagula oyeza wa K100 koma ma comment okhao kkkkkkkkkkkkkk
kwasala mafuta agalimoto kut asowe
kodi anthu mumasiya kukupita nkhani mumaikhotetsa chifukwa chiyani?Peter amagwira ku ILLovo? mwangodana naye akukulamulanibetu musova.Ngati anabera simunapite naye kukhoti bwa?munali kuti?wabwino mudzampeza kuti? Mudzandifunse,Mcp yopha anthu,Udf yodula mabere kuChiradzulu Pp yodula ziwalo.Ali mwana ndindani yemwe samaona ?Ndinu womvetsa chisoni etiii? shamefull
panja piter iwe ndi bambo ako?
amayi a Dpp kkkkkk
No she is saying the truth.Scarcity of sugar hs nothing to do with Peter
Nde DPP yapha ma albinos angati
And who killed Njaunja and Chasowa, if your party doesn’t kill. Shupit!!
Shut up ur fucken mouth,we dnt tok abt the past
Shut up ur fucken mouth,we dnt tok abt the past…Nosense!
vuto si iwe koma mutu nzeru zero,umafuna amalawi aririre nda ,kodi tikamati mtsogoreri akutandauza cha? athu ena chithupi kungokula nzeru kumanja,stupid !! u must shut yo fucken mouth
Agalu inu a dpp
Unaiwalaso dpp yopha albino.Boma lilindimphavu pamalonda ndi chifukwa kuli nduna yazamalonda sikuti imangoyang’ana makapani aboma okha ngakhale Illovo ndie akuyenera kulowelererapo.Iwe ukuganiza kuti a Malawi tonse tingapite ku Illovo kukadandaula??????????
Kodi A Malawi Mudzapenya Liti? Kodi Simudziwa Kuti President Ntchito Ina Ndikupanga Overlook Ma Company Akuti Akugwira Bwanji Ntchito, Mwaiwala Atasowanso Sugar Mu 2012 Zinatengera Joyce Banda Kulamula Kuti Sugar Apezekenso Nde Muli Peter Amagwira Ku Ilovo? Ngati Ma Kampani Sakugwira Bwino Ntchito Dziko Lingatukuke Bwanji ? President Akuyenera Kuchitapo Kanthu
Mutayeni ndiwamisala uyu.
komatu tinawaona olemekezeka a mwanamveka akuyendera sugar factory pa tv ndipo anapanga confirm kuti sugar ayamba kupezeka. nde iwe kadet ukuti boma sizikulikhuza bwana mwanamveka amakataniko ku ilovo ?
yah neeeh!
Mbuzi ndi mabulutu ndi eochuluka pa nyasaland
kkkkkkkkk koma nallia …. u dnt kno meaning of Head of state go back to school
Inakakhara Mthawi Ya PP, Vuto Bwezi Ali Amayi, Koma Poti Si Iwo Vuto Si Pitala.
PAMNYERO panu mayi inu zoti dziko lavuta sukudziwa ??
Its now personals estate for idiot mthalika
Wina zulo wagula belo lonse
Hahaha ma paketi asanu ndi limodzi(5)
Kodi amatilembela nkhanizi ndi akumalawi kapena ndi ma foreigners?
Kkkkkkkkkkkkkk
Ine ndiye zandikwana za sugarzi kodi amakatenga kunja kapena Ku nchalo
Ife kuno Ku zambia sugar Ali mbweee,moti banja lakwathu silikufola nao Ku shopriteko
Akapezeka afika k1000 tsopano. Koma ziliko
Kkkkkk wavuta wamkojo wa mbunzi
Malawi at 52 zovetsa chisoni
Zim father of nyasaland
Ngat nzimbe yatha nde mumati apange bwaa
No wonder, that’s DPP Govt…
A Malawi tinazipalasila tokha makala amoto pa zisankho za mu 2014…
Nde tiliradi ndipo sitinati
vuto losankha anthu oipa, opondereza, adyera komanso ankhanza kuti atisogolere ndi limeneli…
Next is fuel…
Eeeee akuti Amalawi tavuta kwambili Illovo yaganiza zoyamba kupanga pack mphendo zamzimbe Muma packets tizingofinya tokha…. so bad
kikikiki bola inu mumamwa thiyi ine nde handimudziwa anta
If i bring another factory from mocambique goverment won’t complain?ngati zinalili za frozy muja?
Paja sugar factory ili ku sanjika ndi ku new state house etii…. by the way magetsitu atsiya kuthimatu… world bank has resume….kkkkk izinso Lembani mosindikiza ndithu
so u r happy bcoz world bank yabweranso bro tidalira mpaka lit
I need to be schooled if at the moment we have alternative to that….. standing on our own it’s gradual thing not kungozuka lero
Typing
Tizingotengana banja lonxe aliyenxe adzikagula muwiri iyya
kumalawi mumamwa tea ndinu opezako ndalama. ife tilibe nazo ntchito zimenezo olo atasowa kwa zaka ten. timadya nsima mamawa komanso pena kukazinga chimanga.
Chinthu Chikalakwika Koma Kunyoza Kokha Kokha.World bank yapanga suport budget mwakwiya sugar wasowa pamsika mwakondwa kwambiri amalawi mwatani? peter mukumunyoza mwina 2019 azalowanso m,boma.
koma ngati factory siikukwanitsa mulingo wa anthu amene amagwiritsa ntchito,let the Mozambicans to bring in there more sugars
Stupid!!Onama Inu Lero Lomwe Ndinali Kogura Ndakumana Ndi More Than 10 Pple Atagura Ma Bale A sugar Each In Limbe So What Do U Want To Say Idiots
A Illovo amapanga zotiyesa,akufuna anene kuti mzimbe zinauma? panopa madzi ndi ambili sugar akumasowa nanga october ndiye bwanji? koma malawi bola nyasaland ija.
zanu ife tikumwa waku Mozambique
za ziiiiii kod kusowa kwa shuga ikhale nyimbo???? not all of us can afford to have tea gyz,,,,,,kaya kwa mene amamwa tea wo zao zimenezo
kkkkkk
Mu chipiku yapa ginnery corner wayamba kupezeka,10 packets
One to blame is not Government but Illovo. Illovo started before Peter Mutharika even before Bakili Muluzi. Why you blame innocent person. Think before you comment
The government is industry regularator and over seer and is also to blame.Why the government hold ministerial of industries? They are at the helm!
Which means we must blame Malawi Government not the leader coz leader himself can’t handle all the matters
One Question, Who is the reader of Malawi Government? @ #Maff_Sinjan-
To say the fact without fear or favour mr #MUTHALIKA is failure!
The guy maff is ignorant of the facts, just leave him like that
?? ?? ? ? ? lol Limbie Addison you can say that again! nkhani ilimuchichewa iyi osango commenta chichewa bwanji kufuna kuyaluka basi
Peter Mandevu, not reader but leader
To Limbe Addison. Am not here to fight with anyone. What you should know is that Facebook is for charting not swearing each other. If I talk something wrong to you Just forgive me and you are the first person to talk like that. We just put a comment about our Government not friends. So mind your tongue.
@maff.. husband spend salary kumowa kufika pa den alibe kanthu kumapanga blame APM….. maganizidwe opusa basi.kkkkk
@ Erick, tizingowakhululukira popeza sadziwa kusiyana kwa mtsogoleri ndi boma
koma tu zinazi let’s take our feelings aside n think ….I don’t think its the duty of a president kuwona kuti sugar alipo nyumba mwanu or Ku shop rite …illovo is not a govt department… The main problem with us is this monopoly capital companies like carsberg mW..illovo etc …if we had other companies in the sugar industry we couldn’t b this worry… Right now what’s needed is for illovo to explain to its customers not pres must explain to illovo customers no no ….
Ena nkhani ya sugar ailowesa ndale.This shortage of sugar has nothing to do with Peter Mutharika.Ena mukhoza kumanena kuti he is a failure.Maybe u hv to find other reasons to name him a failure not this sugar issue.Mind u wayambano kupezeka pano shugayo.
Maff the moron!
Did you say “charting”? What does that mean?
Check in your dictionary If you have.
sugar wasowa tili mu ulamulilo wa ndani wa “peter” tiyenera maso anthu kuyang’ana kwa iyeyo, nanga ma company ena mukuwanenawo angawayitane ndindani oposa goverment nanga government yo akuyenda ndindani president, nde zosezi ndi gwero lake watch ur taque dis guy is a failure dat’s all palibeso chifukwa chumuyikila kumbuyo ameneyi eish !!!
Kodi Pali President yemwe anakwanirisapo zofuna as wanthu? The answer is no. Ziko latthu langokkhala losauka basi. Ngakhale patabwera mogoleri wina tizalirabe mpaka kale. Chofunika ndikumangopemphera kuti tizipeza chakudya cha lero osati tea ayi.
kodi illovo is a gvt/ pvt company? am confused
Ine sizikundkhudza kwathu timamwa phala lamatsukwa
The banana Nation with its unendless problems!
Chosecho zikupangidwa momuno muziko kaya
Koma yah
dpp boma !
Don’t worry that’s Malawi
Mchele nd diluuuuuu ,,osat zinazi zanthu owelengengaz iyaaaaaaaaa
Kwathuku ngakhale atazalamulilandani sikuzathekanso kubwelela chikale ndipo amene akumakakamila kuzalamula apa akungofuna njilayoti anthu azizawatukwana Ooo Allah chonde chonde chonende lipangeni zikolathu la Malawi kuti lisazafike pamavuto ngatimmene inalili Zimbabwe muma 2003 eshiii izindiye zinanso zozilimilatu zimenezo
950 Kwacha Paketi Imodzi Ya Sugar??
Ndiye Malawi ameneyo,magetsi kuvuta,sugar kuvuta mpilaso utivute aaaaa Maalawi wanga wathelatu.
Koma mwafasako kwanuko
We are yet to hear from Illovo what is the problem!!?
Pangatalike bwanji we shall hear the cause for this becoz others are saying illovo wanted to finish white Sugar which was remaining at their warehouse.
Illovo has given its version of the story, when the trade minster paid them a visit some days ago.
They have doubled their effort soon the market will be flooded, like here in Lilongwe both brown and white is everywhere now.
Malawi Pakana Kusowa shuga eee………
Malawi 24 just has nothing to write about.
Dpp woyeeee! History pamenepaja nkuzangozibwerezanso yokha shaaaa
Asanu ndi imodzi total nkukhala 5????
Malawi si zava , sugar upangidwa Malawi momwemo koma osapezeka eshiiiii
Tsoka amene amakonda tea
Tsano meepa ochewa fe nde mtita? Mmafu kt mgulise malo nkapezeko kanga ka belo ka shuga da pa chiweru…khwesi
They are exporting it,pajatu campaign ikununkhira apezeretu money
bora mchere ukupedzeka zinadzo kaya
baaaaaaaaaaaaad mpaka kuika mulingo
Ndiye Ku Malawi kumeko
oh Ididn’t know kuti ASANU NDI LIMODZI = 5
A DPP ndichocho.
Kuti lero lomwe mupite ku Zambia mukamupeza shuga wa ku malawi pamene amalawi akumusowa shame!!!!!!!
Imeneyo ndie DPP back in days 2012…..nxt ndimafuta
nde malawi ameneyo kkkkk shame
Zayambiranso za mkuluwake zijatu kkkkkk kenako mafuta kkkkkk boma iloooo!!!! Zilibho mulungu wakwiya ndi anthu obera mavoti chilichonse chikuyang’ana kukhoma ngati Ahabu m’baibulo kkkkk
JOZ AKUPEZEKA WAMBILI MOTU MUWAPASE AMALAWI MUKUTUMIZA KUNO KKKKKK
kukhala Mmalawi nkulimba ntima
Many comments here are are based on assumption, ask us who work here @Illovo
Tell me more about this fracas. What is the reason behind this sugar problem?
we are all ears
Ngwazi the problem is that they underestimated the sugar thereby exporting more and some sold locally to major companies like Calsburg, chibuku, universal etc, the stucks for local consumers is empty. However this years production has started last week and it will hit the market soon. For us we have already started consuming
Ock #Willy_Mandala_Matwanje
Okolopa kuchimbudzi uyu musamumvele angadziwe chiani
Thanx Limbie Addison
Thanx Limbie Addison
Ndipeza anyamata 5 aliyese ndimupatsa ndalama yama paketi 4 ndikatero bello lakwana
Takolora zolima zathu tasanja,tea amwedwe basi apo biiii wakumchalo komwekotizikangodya mizimbeyo ngati machine opangila sugar apenga.
kkkkkkkkk
hehehe koma zodandaula za anthu sungazimvetsetse,ife tikati tamwako madzi otetha ndiye kuti tapungula nsuzi wanyemba kapena nsaula.Breakfast yathu ndichimanga chokazinga mulunena za sugar thuni eiiish athu mulujoya atiiii???
Chifukwa chake ndinasamukila ku mozambique kuthawa manyiwooooo
Sugar wayamba kupezeka tsopano vuto limeneli linalipo chifukwa choti Factory inali isanayambe kugayamzimbe pano inayamba
Hell nyasaland
Ndibweretsa wanga kuchokera ku south Africa
Dont worry fellas akubwera pampano
Apezeka pali ponse tikupanga wa nyawani pano
Kenako timva kuti cardiac arrest yagwira munthu
There z something behind musayiwaletu paja zinachitikanso 2012 atalowa mayi joyce banda sugar anapezeka ndipo anatsika mtengo ndipo a illovo ananena mu chikalata chomwe chinalembedwa kuti anachita dala chifukwa president wa nthawi imeneyo ankachita demand ndlama za pa dera zopitira kunyanja ndi dzina zotero so lets expect hard times again
That’s very true, the commodity became scarce the time we were about to lose bingu. I was in mzuzu that year and it was 1 packet per buy(characterised with queues) in Peoples @K800/1kg packet from something like K350. We all know what followed later.
Kodi enanu mukunyoza boma pa khani ya sugar boma limapanga sugar? Muzikhala serious mukamayakhula zithu.
Ok
Akulu boma litha kuyankhulapo ndilomwe limapeleka ma licence! Bwanji za magetsi mmaloza chala boma, limapanga magetsi! Nanga akati unduna wa ma factory, boma liti ndi ma factory mu cingerezi boma NRI over seer and industry regulator work up!
Mbuzi ya Munthu sakuziwa chilichonse,
Iwe omvetsa chisoni kwambiri
Muziganiza osamaztenga azeru atalowa joyce banda bwanj sugar unayamba kupezeka boma likuzwa kathu
Illovo is private company,if there is any problem is for Illovo not government,,Escom is a government company if theres a problem is for govrnment…This is for Illovo to sult out.
Mmene ankaxowa mafuta nthawi yabingu muja,,boma ndilomwe linkapanga?
Akuluwa andimvetsa chisoni ndi coment yaoi yopepera
Evance Charlie you need to be schooled, Government is a esponsublr to regulate issues of national importance, its like you don’t know, Government have 15% shares in Illovo,65% belongs to Malawians and 20% is for illovo .We have Ministry of Industries, should we say Ilovo can’t listen to the orders made by the minister? You need to go back to school and learn much how things work.
Evance Charlie wandimvesa chisoni bwanji! Anthu enanu zinthu zikamakhala chontchi, zimakusangalasani eti? Kodi kumakhala kukonda chipani? Tamakhudzidwani ndi za mu dziko anthuni
pali athu ena ngakhale ku family yakwawo ,akuluza nawo ,u must think wise ,amalawi apo ayenela kufusta astogoreri awo ,some important questions sugar uja timagula allikuti ,mbuzi zina pamenepo zikuti eti ,boma limapanga sugar ,iwe ndiwe garu yeni yeni
forgive him cause he was commenting while his brain was upside .
Ameneyu osakutaya and amvere radio ngati Ali nayo, Boma latulutsa press statement pa za sugar, nanga apanga izi kaamba ka chiyani? Umbuli a Evance changamukani!
Chisoweleni cha sugar pafa anthu angati
kaya kwamene amati akapanda kumwa tea amakhala ngat aotcha mzikitiwo ife unatilimbatu.sunday ndmacheza ndi brother wanga frm Dwangwa tnakumana ndimoz mwa omwe amapanga nawo sugar ku Dwangwako,ndikumufusa kut kod akulu takambani y sugar akusowa chonchi????? ali mbale sugar tinapangatu okwanilatu mpaka amasowa pokhala komano vuto,kunabwera Vice president waku Tanzania ndpo anagula sugar oculuka zedi mot anacita kulesesa amafuna asese yense.nde kupezeka kut wina yemwe analipanja amasowa maloyo ananyowa ndi mvula mot alibiiii sangathe kupitisa pa nsika,koma nkhani yaikulu ndiyakut sugar anagulisidwa ku Tanzania.SHAME!!!!!!
Atiuze zoona ndithu
Kukhala mmalawi ndi kulimba mtima.
Ine ndagula mopanda kukanganira ndi wina.White sugar ndiye ali ponseponse
tamamwanikoni super midori.
In January 2012 we had the same crisis and four months,,, we experienced the state funeral, lets wait what happens in Sept!
Maganizo ausatana amenewo… sindinu satana koma maganizowo brother….kkk
May the same Lord who 4give others 4give U bro
Umakwans willado
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkmmmmmmm ife ndi a nsima
ayi zachita bwino amphunzirepo chimphunzinso a #ILOVO zoti anthunso akunja amagwiritsa yemweyo sakuziwa? nthawi zonse mumangopanga zinthu zoyerekeza~mumayetsa makoponi? tiye nazoni munva kuwawa …..!!!
musazanamizidwe kuti kunja amagwiritsa illovo.that is a big lie.kunja kwake kuti.? munthu ukakhala kuti sunatendepo umangonamizidwa chilichonse ndithu.
a #damien zoti mumagwiritsa ntchito grade 3 simumaziwa? inu mumagwiritsa ntchito ma residures grade 1 and 2 simungamununkhe inu a #malawi… go and make some enquiries den u come back with a tangible report not diz….!!!
inu a #damien zoti sugar mukugwiritsa ntchito kumalawi ndi grade 3 mumaziwa? ok nde ufufuze kuti grade 1 and 2 amapita kuti simungamununkhe a #malawi or pang’ono ataa!! ngati ukufuna ma umboni a izi ndikuyankhulazi utume atola nkhani ndizayankha….!!!
life goes on and on waiting for our time
Kkkkkkkkk
kwali
Our sugar is produced locally and with a local supply of raw materials. How come now this scarcity. I can see that the current government doesn’t care for its citizens at all. They are failing their mandate to provide essential services to the people.
my men govt diesnt not peoduce sugar, but illovo.here at illovo there was a machine breakdown for three month now.oti machine ayamba kuyenda dzana.uasamangoblamer boma Zilizonse.
This government is useless
Bwana Damien Jhala..I did not say that the government produces sugar. Re-read my comment and understand it better. It is the government’s responsibility to ensure the availability of all basic human needs to every citizen of the country one of which is food in which sugar falls under. It not only Illovo that produces sugar in Malawi as far as I know. Did the machines also break down in the other sugar producing companies? It is again government’s responsibility through the Department of Trade and Industry to convince foreign investors to come and invest more such industries in the country if the current ones cannot meet the quantity and requirements.
Ndi Vuto Limenelo?Tea Mukumwa Nokha Anthu Okuba Ndalama Zamisonkho Yanthu,asowe Ndithu Tifanane
ife tayamba kudya phala lamchere kuti tirizolowe
Inenso Ndingoyamba Kudya Phalalo
kkkkkk koma mbwiyake mukwanisa inu
kkkkkk koma mbwiyake mukwanisa inu
Kkkkkkkkk knotu akupezeka wambiri ocokera ku malawi konko n anthu akuno amamuknda kwambiri
Kuti kumeneko bwana Coss?
Ngakhale asamapezeke kumene palibe angamwalile .
Eiiiishhh chabwino palibe Ambuye ndionetse(Wendy Harawa)apa tikuzionadi
çry for my beloved country Malawi
Realy ??!!!!!! Zoophya
Kuli frozzy
palibe vuto, tiyi akumwa ndi anthu ochepa kwambiri.
Kkkkkkk after all we have our own factories which produces Sugar in the country shame!!!!!
Ametero amenewa ku banja kwao
Boma la pitala palibe chodabwitsa apa. Otsatila ndi fuel.
Wakhala Nd Fuel Kusowaso Palibeso Nthawi
Ndiribe problem ine
bola mu shoprite pamene muchipiku muwiri basi
sizachilendo izi I remember 2012 zinalikoso
Ndiye zikutathauza chiyani?
Ndiye zikutathauza chiyani?
Zimayamba chonchotu paja kenako munva fuel wasowa… Umangodziwiratu ??
Next is heart attack
Ndiye zikutathauza chiyani?
Ndiye zikutathauza chiyani
Zikutathauza kuti boma la bisa sugar kuti mawa akapezeka adziti dziko luyenda bwino
OK
Nothing new
zayambanso
Asanu ndi modzi (6)
kkkkkkk
Kufunaso kukweza ntengo kkkkkkkkkkk mayi Malawi ukupita kuti
again????/?