A Mutharika alalatira Zodiak, awuza a Malawi kuti iwo ali bwino

Advertisement
Peter Mutharika

Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika dzulo analankhula ndi atolankhani a dziko lino masiku asanu chifikileni mdziko muno.

Mtsogoleriyu anafika mu nyumba yomwe munali atolankhani akuoneka wanyonga kusiyana ndi mmene amaonekela lamulungu atafika ku Malawi kuno.

Iye atafika kutsogolo anaimika manja ake awiri mmwamba ati chitsimikizo choti anali moyo komanso wangwiro. Pamene anafika lamulungu ku Malawi kuno, a Mutharika amakanika kugwilitsa ntchito dzanja lawo lamanja zimene zinapangitsa ambiri kuganiza kuti mkuluyu anadwalikadi.

Peter Mutharika
A Mutharika; Alankhula za u moyo wao.

“Ine ndili bwino, ndinaonedwa ndi madokotala amene andiuza kuti ine ndili bwino ngati ka mnyamata ka zaka makumi atatu (30),” anatero a Mutharika.

“Ngati ndinali ndi vuto, inali nyamakazi basi. Ndinapita ku chipatala kumene anaganiza zongondibaya ka jekiseni basi, ndi kamene kamapeleka phuma lamulungu lija ku dzanja langa la manja,” anatero uku azimayi akuimba nthungululu.

“Monga mukudziwa, nyamakazi siipha munthu, kapena mwina ku Zodiak,” anaonjezela.

A Mutharika ananena kuti atolankhani a ku Zodiak anachulutsa mabodza ma za umoyo wawo, ena kutchukitsa kuti atsamaya kumene.

Iwo analangiza wailesi ya Zodiak kuti isinthe mawu ozitamilira kuchoka ku ‘Zikachitika mumvera kwa ife’ ndi kukhala ‘mabodza mumvera kwa ife’.

A Mutharika anaonetsa mkwiyo wawo ndi anthu a Zodiak pamene anamudula mtolankhani wa Zodiak asanamalize kufunsa mafunso. Mtolankhaniyu, a Tereza Ndanga ananena kuti ali ndi mafunso atatu, koma atangofunsa funso limodzi, a Mutharika ananena kuti mtolankhani wina afunseko funso.

Anthu otsutsa a Mutharika ena apitirizabe kunena kuti a Mutharika akudwala ndipo dzulo anamwa chabe mankhwala a mphamvu kuti aiwaleko matenda awo.

Koma anthu ambiri amene anaona a Mutharika dzulo atsutsa zimenezi ndipo ambiri atsimikiza kuti mkuluyu ali bwino.

Kupatulapo nkhani ya umoyo wawo, a Mutharika anayankhukaponso za kuzimazima kwa magetsi ponena kuti boma lawo likubwela ndi njira zatsopano zoonela kuti vuto limeneli lithe.  

Advertisement

194 Comments

  1. Ubuli Wathu Amalawi Mukuyangana Zalelo Maiwali Amayi Akudyabe Ndalama Zathu Mpaka Lero Ubuli Basi Musiyeni A Piter Azitafunenso Nanga Zomwe Akubisa Mukuzidziwa Ukapanda Kugwira Ntchito Udya Maudzu

  2. Chonde musanapange COMMENT mutsegule linkyo, muwerenge bwino nkhaniyo kenako nkupanga COMMENT…..Sinawerengepo pomwe paonetsa kuti Mutharika walalatira a Zodiak. Tifune kaya tisafune, ndimtsogoleri wathu ndipo akuenera kvlemekezedwa. Ndimadabwa ndi inu amene mumafuna mzanu atamwalira, dziwani kuti nthawi ya Mulungu palibe angaithawe. Munthu akabadwa amadikilira tsiku loti amwalire ndipo ineyo, a Mutharika komanso inu amene mumapha munthu ndikamwa tonse tidziwe kut tidzafa ndithu. Tiyeni tipereke moyo wathu kwa Mulungu, popeza kut tonse tikudikira tsiku laimfa yathu

  3. musalalate kwatola nkhani komàno inuyo mmutumo abongololo akuyendà bwiño ñgati ngakhaleso inuyo nokha dzoti mukulakwisa tsimuoña àyi ŹBS imakamba dzoona ifeyotu timati tikutsakha munthu wabwino tsitikaziwa kuti tatenga wakhunyu ukulimbanatso ndi bakili wulowatu bale wakopano alikuti bwiñotu samuka tadziwa kuti watopa çhoķapo munthu opanda dźelu I we fack

  4. Watsala Pang’ono Kufa Mleken Kumeneko Ndkuphupha Ndifa Mbale Wake Amkatan Mesa Amkabisaso Atafa Apetulowo Ndagalu Muwauzeko Kt Akaptliza Akufa Ngat Khuku Yachitopa Amapta Kuchpatala Chakunja Kumalawi Kuno Kulibe Chpatala Akachita Mutu Ngat Papaya Losapsa Ctngasekelele Zmenezo

  5. Bisani matenda koma maliro tizanva.kkkkkkkkk Osamunyoza President mesa ndinu mnamvotera Anthu unumukun sangarasa OK mnaiwara mumene anakuwuzilan Bingu kuti wamangakare ramba mkapezana panjir mpompo ndikutengatso mubarewake Osadanda mnaziyamba nokha?

  6. zikungowonekeratu kuti zbs chidzimidzi chilipodi kwa atolankhani a ku zbs,sichina ayi ndi chifukwa cha ma collage omwe angoti bweehwa.Kodi munamuwona kuti mtolankhani woti kwinaku amagulitsa mbatata kwinaku akuti ndi mtolankhani,tikufufuzani kuti kodi school yake mudaphumzilakuti.

  7. Osama uza anthu anu zama #buzi ngati simuku dwala amwene mukangomwa ka power drag kaja sumava kupweteka or uta vulala kaja ndiku enda ndi didi basi ndiku manyang.wa polankhula zodiak imanena chilungamo zomwe yawona simanama kapena kuikapo chining.a

  8. If you are sick accept it my leader, just ask God to heal you and if you are not Thank God it is well with you,we better talk about blackouts and poverty here not this I guess

  9. Mr President panja boma lanu mwati muzimanga koma pa speech yanu mwayakhula mopepela kuti simunaka choka ku America komwe muli ndi madotolo aluso ku bwela.kuno ku mudzi kusonyeza .kuti simudalila ma dotolo omwe tili nao ku mudzikuno kodi ndi chifukwa chake simusamala kuti mudzipatala mulibe makhwala okwana? komaso mwati muli ndi miyoyo yoposa 9 kkkkkkk i dont think my boy angayakhule zimenezo kunena mosabisa munayakhula ngati mbuli chifukwa moyo muyelekedwa naowo umatha ma seconds

  10. President my foot, y cnt he just admit he was sick. After kupezako bwino nkumathera mau chonchi? Shame, he shouldn’t 4get it wasn’t de last he gets sick. What will he say if it happens again? He is a human being just like everyone else 4 God’s sake, asathe mauyi.

  11. a zodiak amanena zoona nanga bwanji bwana munkapereka moni ndi dzanja la Ma mzere kumavomereza zinazi ife timakhulupirira zomwe amatidziwitsa

  12. Zodiak is the most best radio station malawi has, while petulo is the most worst president malawi has. this is the fact.

  13. Okay , guys ! Ndilibe nthawi yotukwanizana ndi zitsiru zoti zilibe ndi value yomwe , sindikufuna kubwenzera poyankhana ndi zitsiru zoti ngakhale kwawo achievement yomwe amadziwa ndikutukwana , iwe ngati chilichamba dziwa kuti uzafa imfa yowawa heavy ! Ine sindingalimbane ndi galu osaseta pokunya ngati iwe , ine ndi malimbana ndi azitsogoleri opusa andale ngati Chakwera Lazaro , osati onunkha kumaliseche ngati iwe , ukweche uli thoo , pachakuti pa amako wamva iwe .

  14. Zodiack is the best radio station in Malawi & this President he don’t know what he is talking, it means he was just eating our money in America he wasn’t sick what a joke ,staying in America the whole month for nothing

  15. Iwe ukunena azako uchitsilu uwona ngat ukulakhu zazelu mbuzi yamano musi iwe wailesi imaenela izinena zoona alephele kulakhula chifukwa kuli muthalika iyeyo ndindani Tienela tiope mulungu yekha basi

    1. Iwe panyapako ndi PITALA wakoyo wamva? ukuna ngat ndi nthawi yomaopana? Ngat Ndinu Pachibale Ndi Pitalayo Muuzane! Azitiopseza?

  16. Pofuna kukhala akatswiri pa utolankhani, ZODIAK yafika pa ukazitape waboza ndi kusinjirira nkhani zikachitika. Lero a president aonesa mikono yao yonse kuti ndi yamphamvu, ZODIAK bwanji manyazi?

  17. Nthawi toopsyezana inapita ndi Kamuzu , zoti ukakhala pansonkhano kumachita mantha kudzuka kuti ukazithandize kuopa kutibulidwa ndi ndodo, A president anthu a nowadays ndi aziwindi ndie polalatapo kumayang’ana mkhope zozilalatira , ZBS chinkhazikitsileni Radio imeneyo yakhala ikukhala pa No1, that’s means Chilungamo chilipo choyankhula zoona zokhazokha. Mafusowo azibwerabe mukuona kuti tikukondwa kumangodya ndalama zaboma Ku America mwapita mwapitanso mukuona ngati mukumapita ulere?As a citizen om Malawi palibe kungokhala pansi ndie tizionelera zimenezzo No pakalakwika tikhonze muzimvera zokamba za anthu omwe anakupatsani chimpando chaulemelero wa umphawio

  18. ZBS u r100% right,enawa anangokhala akumwera sangaone okha kuti chilungam nd chit coz amangodziwa kuombera mmanja chinthu chopanda mano mkamwa.stupid apm n dpp

  19. Eish!!!! Zinatovutanso apa eeeeeti? mpaka… lha lha lha kulalata?? Asaaaah Munatomuputatu Munthuyu eeeeti ? munatomutengamo Asaaaaaah kkkkk

  20. Zodiak yalakwisa chiyani. ndichiti chomwe ZBs yalankhula chaboza ine ndimankhulupilila Zodiak. Zikachitika timanvela kwainu. More fire Zbs Ilove all

  21. Iwe Peter Ndiwe Wabodza Wailesi Ya Zodiak Ndiyokhayo Mdziko Muno Imanena Zoona Ndipo Zaumbon,Ukaloze Galaxy Kuti Muzichangamuka Ngati Atola Nkhani A Zodiak Kuti Yakoyo Ikhale ‘Zamaboza Mumvera Kwa Ife Galaxy Fm’

  22. Mr president mwachita bwino makape amenewa amasokosa ngat kut iwowo ndi achilungamo komaso they lack experience in the ground of jonalism moti ayi ndi kupatula zimenezi apule uhav done the ryt thing

    1. Muziyankhulatu ngati muli ndi azibale anu aja akuvutika kumuzikotu, dont just focus on the prevelege u gain frm the party as an individual…tsegulani maso amalawi

    2. Mutatokota mbuz inu ndukuuzeni media is the dangerous weapon if it is not well control it can ruin the image of the ruling boma over al for the secand tym uhav done the ryt thing chabwino enanu mumakamba za skul ndinatopa nayo pano

  23. Zitsiru zosaphunzira ndi zimene zimaima pa mbalanganda kutukwana President , uchitsiru waukulu upite kwa anthu onse amene alemba ndemanga zowo zotukwana President , uchitsiru wina upite kwa Azodiack , polemba ndikufalitsa nkhani za uchitsiru zabodza . Uchitsiru wina upite kwa mambala wina othawa Mulungu uja , Lazaro Chakwera , galu wa munthu ndi chipani chake cha mwazicho , Uchitsiru wina upite kwa masapota onse a MCP bladifulu zawo amla shatapu kkkkkkkkkk iya nanga tiname hahahaha , Uchitsiru omaliza upite kwa inu nonse amene mumasapota wailesi ya Zodiac . Mufune musafune , Peter Muthalika ndi tate wa Dziko la MALAWI . Pomaliza yemwe aku ndifuna andipeze pa no iyi mawa : 073 488 8515. Futsek ZANU nonse otukwana President !!!!!!!

    1. Nanga iweyo wadziiwala bwanji iweyo ndiee chitsilu chomaliza ndi ndi pitala wakoyo mbunzi za anthu abakha apusi akalingondo anyamu abwanoni mbewa achule aka mchimbudzi atondido makoswe ineso ngati ukundifuna .no yanga ndi080000007

    2. Iweyo chitsilu , peter chitsilu pompano upite ukanyambite kumatako kwa peter yo coz ukuoneka kut ndiwe mbuzi bakha ngati zakuwawa nane undipeza pa # iyi 0717801007 panyo

    3. Uyunso ndiye khwangala wachabe chabe. Ukuyiwala uchitsiru wakowo. Pali nkhani yoti nkumamvomereza Pitala wakoyo? Iweyo unaphunzira chani, chimene ungatitsegule nacho mumimba pakali pano galu wachabechabe iwe? Umawona ngati kuti ndi za ufumu zimenezi? Iweyo ndi pitala wakoyo, nonse ndinu zitsiru zachabechabe, zosaganizira miyoyo ya wanthu ku Malawi.

    4. Chitsilu choyamba ndiweyo zaönetselatu potukwana makolo ako chifukwa ndamene amakonda kwambiri zbs upambana wina aliyese mmalawi..eeishi ndinayiwala chinyani peter wakoyo mabuzi yake…mmmm ndikudziwa kuti waphya mtima umwe kaye madzi kenaka uniyimbire pa 074225 4474 pls

    5. Panyero pako nawe ukuyakhula ngati unavota wekha bwanji pamtumbo zikutipweteka zomwe akupanga pulezidenti wakozoo Azodiak alakwitsa chani timamuona ife akupeleka moni nddzanja lamazere ndye mbuzi ngati iwe #Evance Mazango ukufuna utiuuze chani panyero pako kachikena uchitsilu ochoka nawo kunyumba kwanu umenewoo mbuziii

  24. pitala niozelezeka ekha ananena analakwitsa posanena komwe anariri ndipo ekha wanena anagwala ndie zbs anamapati?Ago tulapasi udindo mavoti anachita kuba esewakuba amalandila chilago ambendela analandila wakhala ndiwe kenaka chilima basi nose muchoka mwatizuza fonya kugula mwakaniso mumati wmapeza maiko ena oti agule koma mpakana 5s pa kg zisanachitipo galu iwa wachabechabe ndie chitsilu china chizitsutsa!

  25. Mmmmmmmmm ZBS ndi radio yokhayo yomwe imanena zooneka ndi maso ndipo zimakhala zaumboni, iye osalalatira ajawa amaletsa kuti iyeyo akudwala aja bwanji? Koma alangizi a president mukufuna kumupepeletsa mtsogoleri wathuyu eti?

  26. Ndamuona bwampiniyi akuchita mantha ndi Gospel Kazako panja akuyambisa chipani chake ndi Marthews Matemba kkkkk.dikira 2019 iziona.siokhawatu pali ambiri akuyamba zipani zawo achina Bu*****.uisova

  27. apa ndiyekuti munthalika ndi a zodiac onse ndionama popeza munthalika wati anapita kucipatala komwe anangomubayako ka jackson ka nyamakazi pomwe azodiac anati munthalika akuoneka kuti akudwala pogwilitsa ntchito mkono wa mazere zomwe zikudabwitsa anthu [0:1:odwala ndiye Amafuna sing’anga ngatimunthalika sakudwala amakabaitsa jackson wa chiyani wakalera kapena?anene bwino ngati amakatenga wakalera ndiye kuti zodiac ndiyonama koma ngati ali wa nyamakazi zodiac siyabodza ndiye kuti alindi ukadaulodi ofufuza bwino nkhani zomweamatidziwitsa]azimayi nanu nthungululu zilizonse ndinu omwe mukuononga dzikoli mumuimbira munthu nthungululu choseco akulankhula zopusa iya musinthe simudziwa komwe kumachoka ndalama yomwe mumakagula soap yemwe akweza mtengoyu

  28. Akulu awawa mumati apitalawa sure saganiza ngat munthu wankulu zodiak sidanene zabodza imanena zimene inkaona ndimaso komaso zimene tonsefe tidawona tsono asabisala pa chipande ngat akubaidwa jackson oti atha kugwira ntchito for some hours ayamike kuti zikutheka amene mumamvera kaya kuonera dzulo press conference ija wazodiak uja anamudulilanji mafunso ena komaso kumudula nfunso asanamalize? Ena aja amadikila kut afunse then mkuyankha koma sizinatero ndi wa zodiak thats selfish

  29. kkkk misalatu iyi apeter ufunika kuzomba kumento sungalalate za phwisi chonchi mmalo molakhula zanzelu mkamwa ngat pa chipululu mopanda mano kkkkk wabadwa kumene

  30. ZODIAK imaenera kuyankhula molemekeza mtsogoleriyu,kodi or titapanga chani pano ndi nthawi yaiye 1 mtsogoleri @ a tym,kupanda,kudziwa malemba kuliraku ndie sikudzatha.vuto siiye koma nthawiyi ndiyomwe timaenera kudutsamo.tiyeni tinkonde mtsogoleri wathu ndiyemweyu!!!!JAH BRESS OUR LEADER!!!!!

  31. Matenda amupengesa ameneyo.. Kumango lalatila wina aliyenda nde anthu azikuwopani inuyo ngati mukufuna anthu akupatseni ulemu zipatseni Mr pulesidenti.. atolankhaniwo akugwila ntcito yawo..yomwe anasayinila ngati matewo afika poyipa nde ingobwelalani ku USA kwanuko muzikakhala udindowo siyani mmanja mwa amene alibwino bwino osati muziwopyeza azicimwene ndi masistezi athu wo kumeneko mwatikwana bad..Tagwilizanani ndi otsutsawo chifukwa ife comwe tikufuna ndicitukuko osati zongolalata zanuzo…ngati zikulakwika anthu akuzuzulani satopa ayi..ndilathu zikoli tinacitanso kukuvotelani kuti mutilamulile basi mukufuna mpaka tiziganiza zoti Tambala wakuda alowe m’boma?? Tayesa bho dziko lathuli man tikudalila inuyo basi…Mulungu akudalitseni man Peter you still my President of REPUBLIC OF MALAWI.

  32. Kodi anayikitsa mano mkamwa?? Kumayankhula ngati mbuzi yopanda mano kusi bwanji,,Nanga Zbs yalakwaso chani.He is trying to blaspheme us kuti amalawi asamuyankhuletse za ndalama zankhankhani zomwe adaononga ku USA koma ndale indeed is a dirty game.Munthu akudwala mmalo moti ayang’ane kwa Ambuye basi nganganga ndi za dziko la pansi.

  33. Yaa,$ even if i were information minister i wouldn’t have allowed stupid ZBS reporters to attend the conference.

    1. You must be sick in your head. People like you are the overzealous cadets aimed at destruction. Why shld people not ask independent questions. What gives you the right to waffle stupid utterances like these. If all presidents can be asked all questions why shld our own president not. What gives you the belief that the president is only yours? This is foolishness at its best

  34. Zodiak has no handclappers, bootlickers and brainwashed joirnalist like mbc as this mtchona wished it could be. I see no reason of castigating zodiak as they reported nothing bur truth!

    1. Media should strive for professionalism.they don’t have to report on rumours that is not in their code of conduct.or might lose their credentials.

    1. Munthu ameneyu sitisiya mumafuna tiyamikile Ochokwera.Ayi sali Boma ndiwotsutsatu simukudziwa mavuto anayambira ndi Kamuzu Banda sadzatha mpaka Yesu adzabwee mwava man.Inu osataya nthawi pangani zanu zikuthandizeni

  35. kusowa usogoleri wabwino nkuluyi chifukwa a Zodiak zina mwa zomwe amakamba zinali zooneka ndimaso ,kupereka moni ndi zanja lamanzere and afotokozanso okha akuluwa zavutoli ndie sindikuona cholalatra atolankhan apa

    1. Sure bro nanga mwa atolankhani atengamo chani mwalo moti azikalalatira a escom kut azigwira ntchito molimbikira osati izi akukambazo

    2. kodi ameneyu akufuna aziwopseza anthu ndi zanja lake lamazerero??ngati akufuna kuti anthu asamalakhule atibwezere mavoti athu

  36. Zolalatiranazo ngati ana aang’ono zichepe. Kodi dziko limenelo, ndi la ambuyake? Foolish President. What has he done since he was elected as a president of Malawi?

    1. mpaka foolish president. . ufulu wa mayankhulidwe umenewo.? ufulu wanuwo mulibe nawo udindotu chonchi akakuitanani ku police muziti president wankhaza….

    2. Inuyo ngati mumagwadira munthu, mavuto ake ndi omwewo. Munandiwonapo ndikutamanda munthu mnzanga? Nchifukwa chake mukumavutika, sayizi yake yomweyo. And musamandilembere ma msg ayi. Muwona nokha zimene zitachitike muma foni anuwo, ngati mundilembere dala ma msg anuwo opanda nawo kuganiza.

    3. Chifukwa cha mantha amalawi tidzingovutikabe kupembedza munthu olengedwa ngat inunomwe mmalo momapembedza mulungu…muli abwana zinthu zili bwino kunyumba kumakangoseteka milomo ndi njala kusowa chakudya dzitsiru amalawi

Comments are closed.