Chiyanjano Mbeza
Patadutsa maola oposa 24 apolisi chimangileni mkozi wa nyimbo, Chiyanjano Mbeza pa mlandu omwe sukudziwika, achibale ake ati mpaka pano sakudziwabe polisi yomwe m'bale wawoyu akusungidwa. Mbeza yemwe amajambula nyimbo munzinda wa Blantyre, anamangidwa madzulo… ...
Bon Kalindo
Omenyera ufulu wa anthu Bon Kalindo yemwe wavekedwa unyolo mowilikiza pakatipa wati zithu zambiri ndizosokonekera m'dziko muno kamba koti dziko lino linapita kwa agalu. Poyankhula mu pologalamu ya padera yomwe yaulutsidwa pa wayilesi ya Zodiak… ...
Malawian Economist Dalitso Kabambe is aspiring for president
Dalitso Kabambe yemwe wangolowa kumene United Transformation Movement (UTM) kuchokera ku chipani cha Democratic Progressive (DPP), wati chipanichi chiyembekeze kuti chilandira alendo ankhaninkhani kuchokera ku zipani zina. Kabambe yemwe adali mkulu wa kale wa banki… ...