Mnyamata wina yemwe amayankha mlandu kale, wamangidwaso kachiwiri pamodzi ndi mzake wina yemwe amafuna kukamupatsira chamba chomwe anachibisa munkhwayira tsiku lakumva mlandu. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa Polisi ya Zomba, a Patricia Supuliano, oganizilidwa awiriwa… ...
Malawi 24 news logo
Njobvu imodzi mwa ziwiri zomwe zinatuluka m’nkhalango ina m’boma la Dedza, yapha mayi wa zaka 45. Watsimikiza za nkhaniyi ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Dedza, Beatrice Jefita, yemwe wazindikira malemuwo ngati a Volontina Yonasi… ...
Lazarus Chakwera president of Malawi
Mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera, lero ali m’boma la Kasungu komwe watsegulira nyumba ya Tobacco Commission yomwe yamangidwa posachedwapa komanso akuyembekezeka kutsekulira nsika wa fodya ndi kuyendera nyumba za asilikali zomwe zikumangidwa.  Izi ndi… ...
Private Schools Association of Malawi (PRISAM), has offered a full scholarship to an 18-year-old boy who was on the verge of dropping out of school as his parents could not manage to pay for his… ...