Boma latsindika kuti limanga mabwalo amasewera a Bullets ndi Wanderers

Advertisement
Quadruple dream alive for Bullets as they reach Castel Challenge Cup final

Boma latsindika ku mtundu wa a Malawi kuti limanga mabwalo amasewero a matimu a Mighty Mukuru Wanderers komanso FCB Nyasa Big Bullets mu mzinda wa Blantyre.

Nduna yoona za achinyamata ndi masewero mdziko muno a Uchizi Mkandawire ndi omwe atsindika za nkhaniyi.

Ntchito yomanga mabwalo amasewerawa alengezedwa koyamba mchaka cha 2020 koma idayamba yayima kaye. Kotero ndunayi yatsindika ku mtundu wa a Malawi kuti ntchitoyi iyambiranso mpaka kufika poti yatha moyenera.

Boma lanena izi kutsatira lonjezo lomwe mboyomu lidalonjeza kuti limanga mabwalo amasewerowa.

Advertisement

One Comment

Comments are closed.