Bizarre: Newborn child speaks

Advertisement
Malawi24.com

Pandemonium rocked in Mangochi when a new baby spoke to request for a porridge.

According to reports published by one of the local radios on its Facebook, a baby born last night asked his mother to prepare him prepare so he could eat leaving villagers in shock.

“TA Makanjira whose area boarders the Mozambique place where this is alleged to have happened says he also instructed his subjects to abide by the instructions” said ZBS on its post.

According to the report by the media house, the baby died hours later.

Advertisement

84 Comments

  1. Kodi olemba nkhani mumangolemba zakumva kapena mumawona chimene chachitikacho?
    Basi mukango kumva inuyo nthawi yomweyo mwafalisa ndicho chamba chimenechi poti kuli technology kale kulibe technology timazikhalila pheee..
    Koma panopa lokha boza fokofo.

  2. Tili mmasiku omalizadi! dzulo mpomwe ndinawerenga nkhaniyi! zodabwitsa nzoti kuno ku Tanzania mwananso wabadwa ku Mtwaka wanena kut aphike phala la ufa wa kondowole (ufa wa chinangwa) mudzi wonse umwe akapanda kutero kubwera mvula yomwe iwononga zinthu!

  3. Mwana wanga weni-weni wakumwetsani phala kkkkkkk or ukadakhala mkodzo mukadamwa

  4. Makolo ake sakamudyesa Ali ndimimba yake bambo anali ankhanza asanabadwe mwanayo izizokuchika kumalawi konko Ku mzimba amai wina wabeleka Ana 4 nthawi imodzi Ku mchinjinso Ana 4

  5. Izi ndizamasiku osiliza kulinso nkhani ina yodabwitsa ngati imeneyi. Akuti ku sobi kwatuluka mzimai ndipo wayenda panyanja amalawi24 tafufuzani mutiuze zoona.

Comments are closed.