
Daring thugs on Monday stole a gun from a police officer as she was guarding World Vision International office premises in Thyolo district, Malawi police officials say.
The thugs injured the officer during the robbery and she is receiving treatment at the district’s hospital.
Police identified the officer as Elida Kusakala who was guarding World Vision International offices in the district.
Reports show that the thugs attacked the police officer as she was doing rounds in front of the building with two other officers.
It is said that these criminals tied up the guard who was watching over the premises but it is not known whether the thugs had planned to steal at the institution.
Kadadzera said that it has also been established that the thugs went away with the officer’s gun. He said they had not yet arrested anyone on the matter saying investigations are still underway.
125 thoughts on “Thugs steal a gun from a police officer”
Comments are closed.

Iwe sumaba?
Iwe sumaba?
Boma lachitetezo Dpp wo eeeee! Ine niribe polobulemu kikkkkkkkkkk koma ku Malawiiii
umangoziwilatu.
umangoziwilatu.
achita bwino
Zolembana kudziwana!!, zimenezo ife zitsatikhudze thananazoni nokha, coz ife munakanika kutilemba ntchito poti si abale anu!!
Zolembana kudziwana!!, zimenezo ife zitsatikhudze thananazoni nokha, coz ife munakanika kutilemba ntchito poti si abale anu!!
People in thyolo are living in fear there is no security, anthu angophedwa every weekend
People in thyolo are living in fear there is no security, anthu angophedwa every weekend
Sitimanewani tija tija timeniti? Upolice omalemba tiyana ta 17 year poti ndimwana wachemwali anaphiri basi ena ali ndi paper labwino anamaliza geri 2010 mpaka pano no job koma awa kuwatenga mayeso a 2014 asanatuluke eeee dziko ili kaya
Sitimanewani tija tija timeniti? Upolice omalemba tiyana ta 17 year poti ndimwana wachemwali anaphiri basi ena ali ndi paper labwino anamaliza geri 2010 mpaka pano no job koma awa kuwatenga mayeso a 2014 asanatuluke eeee dziko ili kaya
Amagona ameneyo
Kkkkkk…..my mother land
kkkkkk
kkkkkk
Bvuto si iye,kma omphunzisa ndi omulemba.zolembana kuziwana, mwati mkazi,zithera komko.
Bvuto si iye,kma omphunzisa ndi omulemba.zolembana kuziwana, mwati mkazi,zithera komko.
Iyenso amaba
zolembana sunday we hav strong citizens here koma tilibe yo disha abalenso tili kuti tingapeze vep zimene then we have to train them how to be a police officer …kkk its part of training
Ntchito za ana amunna ndi amuna basi zimawonekelatu nthawi yowumba madongo mkazi samaumbapo mfuti koma wa muna