
Veteran Christian broadcaster who used to host gospel programmes on state broadcaster MBC, Pastor Fletcher Kaiya, has said that homosexuality is not a sin.

In a media debate that was followed by Malawi24, Kaiya told the host Bayana Chunga that homosexuality is not a sin.
“There are two sides to this issue. For men who choose to marry other men, that is a sin. However for men who are born attracted to other men, it’s not a sin,” said Kaiya.
He later quoted a verse from the book of Romans arguing that God created homosexuals and therefore there was a need to love them.
Kaiya further said that homosexuality wasn’t a foreign concept. He argued that it has always been happening in Malawi only that it was not mentioned in public.
a #KAYIYA, mwatikhumudwitsa
NGATI NDI UMPHAWI AKAIYA, PEZANI NJILA INA YOPEZELA NDALAMA IYI YOKHA AYI. NDINU MUNTHU WAULEMU WANU KOMA MUPUSE CHIFUKWA CHA NDALAMA?
Is not sin to those in one boat
ambuye bwerani
Bho bho
May the God torment u 4 ever
Yahwe angoyan’gana…adzakukanthani ma gay nonse pamodzi ndi Kaiya
Todayz of freedom of expression any one can say anything h/she wants
ur so stupid fretcher,upastor anakupasa ndani iwee go to hell with ur fucken gays
akuvomerezayo akakwatire bambo ake tiwone ngati zingatheke msanamizile mulungu akuwona sanagone ali maso ndithu akungokuwona mzadabwa siku lomaliza!!!
zopusa zokhazokha basi. ndichanikodi a malawi?!!!
it hs shown that some ppo who r cald pastors bcoz of their education r nt really true pastor bt wat they uz iz wat they learnt,bt holly spirit is the best teacher,u pastor dnt confuse ppo,ambiriwa mphamvu ya choonadi munaitaya kale.
it hs shown that some ppo who r cald pastors bcoz of their education r nt really true pastor bt wat they uz iz wat they learnt,bt holly spirit is the best teacher,u pastor dnt confuse ppo,ambiriwa mphamvu ya choonadi munaitaya kale.
Stupid paster. If u r a real paster tell us a verse n a chapter abt homosexual{stupid tolerance}
Stupid paster. If u r a real paster tell us a verse n a chapter abt homosexual{stupid tolerance}
Nchifukwa chan nkului walankhula mopusa chonchi? Akaiya timaona ngat ndimunthu wa mulungu kma xaoneka kti ndi satana atate akathen athu oipawa achoke nxiko muno asatisochelese ife
Nchifukwa chan nkului walankhula mopusa chonchi? Akaiya timaona ngat ndimunthu wa mulungu kma xaoneka kti ndi satana atate akathen athu oipawa achoke nxiko muno asatisochelese ife
Ziko lilikumapetodi eeeeeee mmmmh manyi wekha
Til Mmasiku Maliza Ndie Tieni Tisankhulupilile Muthu Alietse Komatikhulupilile Malemba Buku Lopatulika.
Ponena chilungamo anthuwa aphedwe basi
ai gahena ikadzadza ndithu.ife timakutengani ngati m’busa wabwino kma nyalugwe wachabechabe ndithu…inu a fake pastor ndikakuonani ndikumafuna kusanza mxm
Anthu amenewa nd amene akupangisa kuti Malawi asalandile mvula yabwin malemba akuti ngati wotsogolera wa mudzi aopa Mulungu mudzi umeneo uzakhal odala koma ngati saopa Mulungu mudzio uzakhal otembereredwa nde apa tiziona nafeso mmalo moti tilape ay tiganize bwino
my dear brothers and sisters, the problem with such pastors is actually not to have gone to Bible schools but its due to lack of the Holly Spirit alipo ambiri ndipo ngati salapa the hell is waiting 4 such pple,may God have mercy!!!
we fletcher ulikupusa iwe….wakavuka??????
Akunena za Akaiya! Anakalamba Ndi nzeru zomwe! Period!
From Old Testament to New testament homosexuality is sin.Pastor Kaiya you better resign now as you work under devil
Sorry so much iwe ka Kaiya osamasewera (kulimbana) with GOD! Ndi zibwana ukuchitacho. Ngat ungapitilize, kayaaa?
My living God created two living things amale and afemale to mate then multiply how come amale and amale shame????
God created a male and a female to mate then multiply so how come amale and amale so malawian how can you do that shame????
Ifeel sory for him, he is gone into the devils hands after serving God for a long time.
Uzeleza peradventure
Uzeleza peradventure
Mwana wa satana ameneyo
Mwana wa satana ameneyo
Ifetu sitiopa mbuyako Satan abwana athu mulungu
Ifetu sitiopa mbuyako Satan abwana athu mulungu
Ufiti wamako
Ufiti wamako
Great fool, he should be the first to provide his ass
If it is nt asin….y God him self nt create aman or awoman alone?? Tsoka kwa okwanilitsa malemba
Pastors pastors!
comment reserved, chifukwa ndingayambe kulankhula pambali pabwino ndikupawona ndithu.
Kufuna kutchuka eti?
Wa satanic Ameneyo musiyeni
Pastor….aaaa zankutu
Ng’oooo!,you have writen in water ng’ooo!,so you satanic pastor,you thought people would agree with your evil views?Why do you want to be a sign of last days by making people realise people will love money than love among themselves.If I may visit your home,won’t l get a wife there?what about children?dont you have?were they born from a man?was God foolish by creating Adam and Eve?If what you have said is right,God would have just created two men in the beggining rather than individuals of different sex!!TAKE NOTE:the Hello is waiting for you,you can never decieve malawians,WE ARE NOW AWAKE,these are not 1940’s!
Ngati kayiya wanuyo akutelo mumfuse kuti anatulukila kuti pobadwa.nanga nhifukwa chani anakwatila nkazi osati mamuna?komaso utumiki wake ndiwaboza.
This pastor need to read Leviticus 20vs13 if he is indeed true pastor you pastor go to hell
rude! mr kaiya, my God wat a sin thing, ife sitilora kuti tilangike chifukwa cha munthu mmozi we kip on saying no to homosexual. and knowingly even dogs and goats knows It is a sin according to the Holy Bible and Holy Koran and
it is a crime according to the laws of our beloved nation.
In the Holy Bible (ROMANS 1:18-32, 1 CORINTHIANS
6:9-10, 1TIMOTHY 1:10) it is punishable by death,
What a pastor.
God may have mercy upon us. I think Poster KAIYA has a problem, is having a some demons in him.
God may have mercy upon us. I think Poster KAIYA has a problem, is having a some demons in him.
Moti akaiya mukaona mwendo wa mamuna nzanu mumatota?????
Ukulimbana ndi Mulungu wa makamu,kkkk koma abusa enawa,zako izo
Mxiiiiii
Mmmm oky
Go to hell ur stupid pastor
chikhalibwe cha agalu athu wopusa nose amene mumanyengana muli wofanana ziwalo ndpo
Bvuto lili ndi anthu enafe ndi loti timakhulupilira abusa koopsa mwinanso kuposanso bible,,to be honest mulungu atati atilozere axibusa enieni zoti 10 angakwane ndakayikiratu,,,,can u imagine a man who calls himself a pastor nkumati mathanyula si uchimo? which Bible does he use? am not righteous koma dis Fretcher is as bad as devil himself, ,last days inde;indeed
Those are the feck pastor ,that the bible said already sorry to the people prezing god under him .I Jindex never accept a very open sin like stupid guy unless they give birth .vyamthondwee pastor ameneyo
I will be praying n my home to avoid spiritual pollution
Inetu nchifukwa chake nimasilira ma islamic countries komanso chisilamu sindimafuna kumva zanyasi ngati izii
Iwe Kaiya u bastard i will shoot u
akufunika awelenge Leviticus 20 vs 13, azindikire pa zomwe akuwauza anthu a Mulungu, let God forgive him!
“There are two sides to this issue. For men who choose to marry other men, that is a sin. However for men who are born attracted to other men, it’s not a sin,” said Kaiya…… By this it is the same with people born with physcal challenges we always accommodate them mosiyana ndi oti wakadulidwa mwendo or kuphuritsidwa maso kokaba. MALAWI24 could clearly present Pastor Kayiya opinion kuti it has 2sides even give the quoted verses in Romans because you were following it…..Its apity that Pastor kayiya has got all the insults resulting to how the article has been headlined
i still see no justification to this bra! homosexuality is never in born, naturally God created a woman for man. its so unfortunate that a man of God would even suggest that other people are attracted to those of same sex by nature.
Blessings with due respect…ziri ngati mmene anthu amabadwa ndi chilema…..all the people who are born with degrees of disability; crippled, blind, death were created by same GOD who created those that are whole! The way we clothe naked mad persons its the way these should be treated! Mmene sitingamulore wamisala kumapha anzake coz ndi wamisala its the same way we should help people who have same inclination to same sex that they should live a normal way not promoting such behaviour. Aliponso amene during sex action with their wives does fellatio and cuningulus (sucking each other private parts) which I just think kut homosexual does the same. Go deep on eunuchs in the Bible– people who choose not to marry. They are also strange people isnt it?
Blessings with due respect…ziri ngati mmene anthu amabadwa ndi chilema…..all the people who are born with degrees of disability; crippled, blind, death were created by same GOD who created those that are whole! The way we clothe naked mad persons its the way these should be treated! Mmene sitingamulore wamisala kumapha anzake coz ndi wamisala its the same way we should help people who have same inclination to same sex that they should live a normal way not promoting such behaviour. Aliponso amene during sex action with their wives does fellatio and cuningulus (sucking each other private parts) which I just think kut homosexual does the same. Go deep on eunuchs in the Bible– people who choose not to marry. They are also strange people isnt it?
fotseki,,
kkkk
People like you need to go to hell and burn for eternity mr pastor
Chamba cha ex pastor
Ndi mwana wa Hule uyu! Alidziwira kuti Bible? Ku Bar?
a busa akaiya mukabadweso kachitatu, shame to you!!!!!
Is he a pastor or a magician?
My fellow brothers and sisters,kod pamenepa pastor ndani pakati pa Mr K Nsonda ndi Mr F Kaiya?
YOU MUST BE VERY STUPID FLETCHER KAYIRA NEVER CALL YOURSELF A PASTOR ANY MORE. WE DONT NEED PEOPLE LIKE YOU IN MALAWI & DONT FORCE PEOPLE TO INSULT YOU.
Hahaha zimatero ukadyesedwa chi bans
Man of goat will be like “homosexuality is not a sin” you need deliverance satanic pastors before you die a miserable death.
He iz a member of illuminati
Last days warning izi mbusa akuikira ndemanga anene verse lake baibulo tilione ,Ndipo masiku akudza kwake ayandikira konzeka kale linseli za u gay zinali kuti?
I knew it. That mother fucker was only on air for money. he is not a fuckin man of God. All gays they luck love. How wud one love fellow man up to intimacy? That’s not love its insanity.
Kodi Kaiya ameneyu ngwampingo wanji?Pitala wamugula kuti azinena zimenezi nzina la Devil eati?chabwino takumvani abusa…nde mukathese banja lanulo ndikukufunani ndikukwatireni muzikataya nkhoko payard mwamva..?
It is a sin
let God be God dont do his judging for him …if every sin is equal then gays are no different than liars and adulterers which am sure most of us at one point have been but that doesn’t mean we should be sent to jail. iam not saying its right am just saying no man should imprison another for their short comings
choka choka choka kafere uko kaiya
Abusa ophunzitsa zosangalasa munthu osat Mulungu…..adagwa amenewo pa maso pa Mulungu olenga kumwamba ndi dziko lapansi… osawamvera… Dyera ndi dziko lapansi….abusaaaa, mwaiwala nkhan yaSodomu nd Gomola….?
Za sodomu ndi gomora zinanditopetsa. Kambani za lero. Maiko ololeza mchitidwe umenewu alipo ambiri. Tiuzeni limene linaona zonga izi ndi liti? Ine ndikuona ngati Malawi akuona armageddon chifukwa chosowa chilungamo pa nkhani monga imeneyi
wanja zambiri iwe usatinyase
A Kaira akufuna allowance ya ma Donner Mutu wao unasiya kugwira ntchito
Go to hell kaiya
ZAYAMBIRA PATI AMALAWI ??
A tiwo ndi amenewa akutalutsa malawitu kuno ku south africa
Satanic
Kachilombo kotchedwa mathanyula kanabwela ndindani aaaaa,…wamathanyula no molllll
who iz dat friking pastors am sure god will punish him
if this is true may God forgive him
Eish Kukalamba ndiubongo omwetu uku waliyiwala bible nthawi yomweyi.Abusa Werenganiko Romans Chapter1 Muyambile Verse27,ndiye Mutiuzenso.Paja Kumudzi Nkuti apastor?kkkkk mufunse Ken Nsonda Irespect Him Though he consetract on politics but he doesn’t forget za m’bible.
God punish him
May the lightning strike dis idiot pastor
Wea malawi z going
Your are the first Pastor since l was born to say that,maybe you are also one of them because none supports something without being part of it,you dont deserve to be a Pastor in Malawi
Pastor Kaiya ziwani kuti mulemela inde koma mudana ndi Mulungu
bullshit
Fletcher Kayia udzafa imfa yowawa ndipo MULUNGU sandakukhululukira zochimwa zako
sidzachilendo so called pastor talking such kind of blasphemy. He is munthu chabe wa mulungu koma ndi mtumiki wa satana. GO TO HELL PASTORLESS!!!!!!!!!!!!
Za chamba basi ma pastor ake sinunomwe mukusanduka njoka aja angakukhulupirireni ndi akazi anu ndi ana anu za m mbwererazi
mmmmmm mabodzatu awa…. i watched the said program on TV sananene kuti homosexuality is not a sin ayi….. He said to be attracted to afellow man as it can be to opposite sex is not a sin but to do the thing is a sin… thats what he said… mabodzawo
You are doomed. What is sin then?
Let’s just wait n c how he will b punished, GOD IS NOT A MAN
From the quote in the article, Its like he is misquoted!
Read it. Lies.
Hey u Pastor u fool ov dhem go to hell. ..
lichikhala Kale bwezi ntawatukwana pastor kaiya kuti pamtuzu pao kudaa…..koma ndidatembenuka..
Nawoso akufuna ndrama nde azitisandukira
Nawoso akufuna ndrama nde azitisandukira
tili kumapeto anthawi zoona
tili kumapeto anthawi zoona
Mbuzi ya pastor…
Mbuzi ya pastor…
God created Adam and Eve NOT Adam and Steve!
God created Adam and Eve NOT Adam and Steve!
Kkkkkkk ndichifukwa ndinasiya kusatila MBC
Kkkkkkk ndichifukwa ndinasiya kusatila MBC
ineyo ndwochimwa, kma na uyu pastor kaiya ndwochimwitsitsa
ineyo ndwochimwa, kma na uyu pastor kaiya ndwochimwitsitsa
flersher panya pako. ngt usaononge mbili ya achrist. bible lit lomwe ukuwelenga kut mathanyula si uchimo?
flersher panya pako. ngt usaononge mbili ya achrist. bible lit lomwe ukuwelenga kut mathanyula si uchimo?
This is unbelievable words from the Pastor.I think he is in the wrong field and he is playing with God
This is unbelievable words from the Pastor.I think he is in the wrong field and he is playing with God
mukumuputa mulungu wamakamu wamphanvu zonse muzafa imfa yowawa
mukumuputa mulungu wamakamu wamphanvu zonse muzafa imfa yowawa
koma kut tifufuze abusawo nkazi wawo ndimamuna nzawo?kapena ali ndinkazi ubusa wina ndiongofuna kusokoneza anzawo ndithu
koma kut tifufuze abusawo nkazi wawo ndimamuna nzawo?kapena ali ndinkazi ubusa wina ndiongofuna kusokoneza anzawo ndithu
zomvesa chisoni kwambili mpaka azibusa kumati kukwatilana amuna okhaokha sintchimo
zomvesa chisoni kwambili mpaka azibusa kumati kukwatilana amuna okhaokha sintchimo
You are not a pastor go to hell
You are not a pastor go to hell
bwanji iyeyo osakwatila mamuna mzake??? Holy ghost fire!!!!!!!!!!!!!!!!
bwanji iyeyo osakwatila mamuna mzake??? Holy ghost fire!!!!!!!!!!!!!!!!
Fleisher zawuve ife ayi pati kapena kolani bible liti zopusa ife ayi usamuka
Fleisher zawuve ife ayi pati kapena kolani bible liti zopusa ife ayi usamuka
Fleisher zawuve ife ayi pati kapena kolani yi
Fleisher zawuve ife ayi pati kapena kolani yi
He who says homosexuality is not a sin is a homosexual and a sinner. What a shame, mbusa kupusa kuposa mbuzi? aaaaa
He who says homosexuality is not a sin is a homosexual and a sinner. What a shame, mbusa kupusa kuposa mbuzi? aaaaa
If Its Not Asin Why Bible Limati Kale Anthu Amchitidwe Umenewu Mulungu Amawaononga?? Inu Mapastor Musatisochelese Ndimasiku Omaliza Awa.Chilungamo Chimakukanikan Akaiya
If Its Not Asin Why Bible Limati Kale Anthu Amchitidwe Umenewu Mulungu Amawaononga?? Inu Mapastor Musatisochelese Ndimasiku Omaliza Awa.Chilungamo Chimakukanikan Akaiya
If its not a sin, what is it?
If its not a sin, what is it?
Amati kunyoza mtumiki wamulungu mkulakwa koma na uyu yekha deserves chitonzo.
Amati kunyoza mtumiki wamulungu mkulakwa koma na uyu yekha deserves chitonzo.
kuulutsa mau pa radio sikuti ndi m’busa akagwele adya za ma gay zambiri kufuna kusocheletsa anthu zidalinso chomwechi nthawi ya Lot sodomu ngati adawonongedwa mchitidwe wake omwewu
kuulutsa mau pa radio sikuti ndi m’busa akagwele adya za ma gay zambiri kufuna kusocheletsa anthu zidalinso chomwechi nthawi ya Lot sodomu ngati adawonongedwa mchitidwe wake omwewu
Ohhhh mama Malawi wataikilanji? tinkadira Iwe
pastor are u serious
According to which bible or quran?
why satan
Thats why i dont trust these so called pastors, zoona man god kumalimbikisa za mathanyula?
This guy is trying to confuse as with his bad ideas. What he should know is that there will never be reward to those who turn their against JAH. He is not aware that homosexual is satanic ideas, it’s quite evident that he is also a GAY although he has been married to a woman.He thought that AZUNGU will give him a lot of cash for saying this foolish statement. Their thinking capability is below that of a DOG. SHAME ON U BAD PASTOR.
mkana mulungu sakutipasa mvula coz of agaluwa
futsek
Kkkkk. He want to build his Church and buy a jet through American donors
abusawo anenadi mauwo kapena mkungonama?sindikukhulupilira,ngati pali voice or video clip download it
Kodi Mbuye wanga Mwagona??? Nanga Why mukumpatsa satana Danga mpaka chonchi? Plz Do something Papa we are crying to you ndipo tagwada pamapazi anu Papa.
Babylon agwe..fire
That’s what happens when even those who claim to be men of God gets defiled with Homosexuality money from the west… #praying_4_Africa
flecther kaiya you are in the wrong field
Pali mipingo ina ndiya anthu ina ndiya Mulungu.bcoz Mulungu anatilenga ndicholinga choti tizichita chifunilo cha Mulungu.ndiye ma pastor mukuwanenawa ndiwoti anayambisa mipingo yawo osati ya Mulungu.Pano dziko ladzadza ndi usatana chifukwa cha ma pastor onyenga ngati amenewo.tsoka mtunda ndi nyanja poti oipayo watsikila konko.YESU anapelekedwa chifukwa cha ndalama.Aneneli ose kunalibe mneneli ophuzila koma amangozozedwa ndi mphavu ya namalenga.pamene Aneneli alero akuchita kupitalila ku sukulu ngakhale alibe umulungu mutima mwawo.one of them iz Mr kayiya
Its very sad and worrysome that the highly acquired honour this so called pastor enjoyed had gone this easy way for we had now know his master,LEVITIKO amanena momveka bwino mosafunikira wina kulalikira kuti ichi Mulungu anyansidwa nacho…,who are we to justify this sin!
AS REVALATION 2:4-5 SAYS THAT “koma ndili nako kotsutsana ndi iwe,kuti unataya chikondi chako choyamba. Potero kumbukira kumene wagwerako nulape nuchite ntchito zoyamba koma ngati sutero ndidzaza kwaiwe ndipo ndidzatunsa choikapo nyali chako kuchichotsa pamalo pache ngati sulapa”. Pastor kaiya lapani
I can’t believe that a fellow pastor can say homosexuality is not sinful! May be I am dreaming!
Pastor amene kuyankhula zopusa choncho ine mpaka nditatulukamo church kumapita kuthu ndithu ndipo bola kukapemphela ndekha osati osati kukhala pa mpando church kumamvela ma pastor ngati awa
Fake
Itink Fletcher some how goes crazy .He is so stupid .kukanakhala bwanji makola ake akanakwatiwa ndi mwamuna mzake kapena mkazi mzake akanabadwa iyeyo . He iz a real fool
He is a Big fool.
Pastor Uyu Ndi M’dzukulu Wa Satana. Bt Why Dis 2 U Malawi.Ndatsimikiza Kt Umphawi Umacititsa Ucitsiru.Akhala Pang’ono Atiwuuza Kt Ngat Mukufuna Chinthandizo Muziyenda Maliseche.Dziko Langa Malawi Usayiwale Mulungu.Boma And Other NGOs Awavumatitsa Obama M’kamwa Ndicifukwa Chake Akumazembazemba Pa Nkhaniyi.We Say Malawi Ndi Dziko Lowopa Mulungu Nanga Uku Ndikuwopa Mulungu Kapena Satana?Dn’t Late Our Poverty 2 Do Us Apart With Our God.
ubusa wa pa radio fwakafwaka
ameneyu ndi pastor wa satanism angoleka kufalitsa maprogram pa radio
Anthu anja akumasathuka joka ndinu eti
Sionse ot Ambuye Ambuyd azalowe mufumu wakumwamba.Apa nde zaoneselatu kut dis greedy pastor ‘ll yield notin @ de end.He ‘ll ganishin teeth in de hell.Maonekedwe auMulungu koma mphamvu yake adaikana.
maluz a muswa ameneu,what a sham to 2 u, u so called a paster….PASTER OF A DEVIL!!! paster ochititsa manyaz iwe.chonsecho2 ali ndiana komanso mkaz kunyumba
Nchikhala ndi truck makamaka road master,pastor wa chambayu nakammangilira kumbuyo mkumamkwakwaza,kapena kumuyendesa grinder pamimba.UZAFA NGAT GALU pastor iweeee
أنا حصلت على 3000 طلب صداقة
احصل انت ايضا على آلاف طلبات الصداقة من بنات و اولاد
ومن جميع الدول العربية والاجنبية
الشرح من هنا ==> http://www.talabat.ga
which GOD is he saving?
That’s why you are turning into a snake
Nonses full of satanism
For Almighty God and his people is a sin but for devil and kaiya is not!! we are ready to kill all gays!
Amakonda ndalama! he is so greedy! pure satanic fake pastor!
Achende ake busa ameneyo!
Abusa asatanic amenewo! akusocheletsa anthu so why Almighty God punish gay people during Lot time?
zacibwana zmenezo neyeso aligulu lawochita
Ndimafuna nditadziwa funso lomwe linachititsa kuti ayankhe choncho?
Mulungu analanga mzinda wa Sodomu ndi Gomola chifukwa chani abusa a KAIYA? l wonder if at all this pastor went to bible school. Or he was just appointed by his fellow church members after being the oldest member in the congregation. Open up people this is the clear testimony that we are in the last days. Lord have mercy on us.
If it’s reported by #Malawi24, am 100% sure its twisted. These guys are a disgrace to the media fraternity. They have this tendency of fabricating and twisting stories to gain attention, they are total SHAME!!!
The deeper secretes of Satan.rev 2v24.
pachakuti pako iwe m’busa onama fletcher kaya kwinako ndani fisi iwe unya manyiii uona okonda ndalama iwe suzipezabeeee
iiiiiiiiii km nde wamtukwana2 angokuchimwisapo apo
Usamalimbana ndi zitsilu no guda.
Victor tell us the tru,,, anati chani pastor kaiya?
Indeed the devil is showing himself throuhg his chosen ones who once claimed to be gospel gurus but now the devil is even controlling them, I used to admire yu. Mr kayiya but now yu have just shown malawians that yu sold your soul to the devil. don’t let money make yu lose your diginity and morals
Kkkkkkka pastor
Wophenga
Aaaaà ma pastor achamba
U fake pastorz plz dnt spoil dis innocent name_ inu mwna ndmang’anga !! Dead Kaiya
I watched the programm yesterday on Times Tv. He didn’t realy mean what is being said here, the reporter has just twisted his words.
Maybe hes homo himself lol
mchitidwe wake umenewu nde mvula ikagwe mulinchibwana ..ofunika kulapa ..tiotche gay aliyense ngati wakuba
Azibusa enawa Eeee , kma ndi wa mpingo wanji ameneyi satanic chani ? Ine zopusa ayi ndngadye deal mwa mamuna nzanga kkkk imeneyi mbuzi ndithu eshhhh so sad
Mbuzi,,,,kangaude wa pastor. Ur speech will lead u to judgement
Ubusa wakunyanja umenewo omwa magazi
Ubusa wakunyanja umenewo
what a public shame dear pastor! kani ubusa wanu unachokera kwa mdierekezi? ha aaa! agalatiya opusa! kwatirani mwamuna mnzanu lero musudzule mkazi wanu uja chifukwa mwaledzera, mwachita chigololo ndi mwamuna inu. sindidzamvereranso programme yanu ngakhale ulaliki wanu wonyengawo! abusa ozungulira mutu ndi umphawi komanso adyera ngati mvimvi!
Abusa ana anu akuwerenga zimenezi? nanga akuti bwanji pa zimenezi? mwadalitsa angati amuna okhaokha chiyambireni ntchito? izizi anakuuzani abambo wanu, ambuye wanu kapena? ndikulangizeni ine mwanamwana ine? sioyenera kukhala apongozi anga inu? shutup musadzaneneso zimenezo.
end of days
Ameneyu ytisatayenthawi ndikumutchula kut poster cifukwa sakukwanila ngakhale pa ubusa waziweto ziwandaso zilibwino cifukwa ziwanda zimamudziwa mlungu koma uyu ndiosocheletsa nkhosa a ambuye evil suppoters ana anjoka
Take care bcz they will decieve even the choosen ones thats why God destroy sodom &gomora. Shame!!!
Take care bcz they will decieve even the choosen ones thats why God destroy sodom &gomora. Shame!!!
mapastor enanu munaitanidwa ndi satan et read leviticus 20vs 13 4rm de holy bible den say your opinion again
Eeesh….. “4 God So Lovd De World & He Gav Hs Only Bgoten Son That Who Eva Blv In Hm Shall Not Perish Bt Av Evalastng Lyf” God 4gv Dem, 4 Dey Not Know Wat They Do. These R Last Dayz Indid, Mpaka A Pastor.
this man must retire with immediate effect. wadya zamabugwe uyu. zimutsata zimenezo.
sure sir
sure sir
Imodzi mwa mbuzi za abusa ndi imeneyi. Voertsek! Mwana wa galu!
if sex is not done correctly is. a sin what more fucking each other anuses????
the man is bankrupt understand him
I don’t want want to see him again at MBC tvm
Who is this pagan pastor .Iz he from ndirande,lunzu or where.Ope not from the ocean.
haha last daez indeed tsoka kwa okwanilitsa ,maremba
Leviticus 20 vs 13. Romans 1 vs 26.
mac hende…………..
I cannot buy what the so called pastor said, look it is absolutely not true for a person to born attracted to a woman, I can only agree if that person starts to be attracted to a women as he grows. If this happens it means that the person is possessed with evil spirit and he requires total deliverance. God did not create a man to be attracted to his fellow, then god purpose of woman is null and void, I don’t think if god can contradict himself
Kayiya nayenso ndi gay
Poti ndidiso limawerenga nkuona zilizose koma nkhaniyi ikanandidutsa. Kuuma mtima kwanji kulankhula izi
The pastor says the truth that Homosexuality isn’t a sin but rather a small thing that hen puts together with other devious thing becomes a sin. A sin is combination of many devious thing. However the pastor has justify his status as a man of Gd if he really is!!!
I think its not a sin to FEEL like that, but to express and live it is a sin.
wowww i nvr thot malawian pastors ar lyk ths fr real tht devil z at wrk bt gud pipo out thy let nt ths pipo decive us coz tht son of man z on th way cumin so b careful
mulungu akukhulukire find out what was the progarm was
If is that so y u didn’t divorce ur wife then ukwatire brother wako 4sek with ur rubbish…………. U deserve to die wava I we chi China pastor including u america
My own pastor,heyy chilema chimenechi cha mandevu vs mandevu,tsuna vs tsuna,chabwera liti?ndithu ndisitha mpingo,mbambadi.
total madness according to bible.
it was a sin, it is a sin and shall remain a sin according to my HOLY BIBLE which is the infalible word of God!
Thats Why Mulungu Watikwiyira Osatipatsa Mvula,bt What Has Come Over You Pastor,ndikakukhulupiliran Kom Aaa Manyaka Enieni Bt You Need To Know That Musocheletsa Ambir, Mulungu Atikhululukire As A National
those who mate with the same sex or animals have their own judgement including those who are surppoting them.
Zakumuziwa mulungu ameneyo komaso ndikumudziwa ndiwa satanic musavele
i will comment on ds issue in two yrs to come
An2 ngat inu ndiofunika Mulunguo paekha kuzakuchoxan zwanda zanuzo… Cz t xmx ndzazkulu hvy…!! Eh. Mundpaxe verse mu bible. Ymwe inalembedwa nyax zmezo… En muambe mwakwatra anada man lyk u en u guys shud bear chldrn or els u wl danc d muzk pastor. GOD shud purnish uuuu lier.
pastor ameneyo ndichisilu akufuna ndalama ku azika lima uko kapen ngat wasowa chochta abwere ndixam pasa chochita.
Don’t worry he will perish
dats nt true, ufiti basi. dats wi call (END OV DA DAYZ)
The last dayz
If dats the case GOD would av never created EVE…..stop cheatin ppo….tiuzen kapena ndi verse it yomwe imaloleza mathanyula!!!zixilu,..kukomedwa ndi ndalama….
We should better believe that this kind of pastor ruled by beast from devil. Can’t we see our selves evil on this?
ANENERI ONYENGA AJA MWAYAMBA KUZI ULULA NOKHA APA
ngati tchimo ali kugonana ndi nkazi popanda ukwati nde inu mwati. sodomo its not a sin koma langizo kwa a khirisitu nde mwati muzitsatilabe chi khirisitu coz your pastor and even pope betrayed you so think deeply
Malawi was there long time ago why today we should move on with rubbish things, it’s not everybody is rich, it’s not every country is rich we must stay as we used to stay , Malawi will never be like America, Malawi wil never reach where SouthAfrica has reached accept that our country is poor with their poor leaders n life wil move on, I don’t support the idea homesexual is a sin, even don’t they respect that, even cows they do respect that ,Dog male has got feelings in a female dog to respect what God has created each n everything with their purpose, Ass is for kubibila not for useless things why can’t that pastor go to church with bra or skirt?
Demeti yambani kukwatiranako i wil b d first to kill u wit my bare hand i dnt fear anytin apart frm God
this idiot will die with his stupidity
Ndithu Akaiya Zavuta Apa Mwawalodza Kut Asinthe Zonena Et?Munthu Wa Mulungu Wapanga Bwanji?Wapenga Ndi Bible Et? Tisiyire Bible Ana Tione Kut Tipange Nalo Bwanji,mot Akaiya Munakwatilana Ndimwamuna Mnzanu?Zotitengela Kokatiyesa Ife Ayi,Takana Ndimwaz Wa Yesu Fire! Fire! Fire!
Kodi akupatsani zingati
This kind of pastors must go to hello
Bola Chauta Akadalenga Galu Kusiyana Ndi Ndichitselekwechi Tisamale Abale Anga Asatisocheletse Ano Ndi Omalizadi Masiku Anthu Ngati Awa Ndiwo Akubweletsela Ng’amba Namalenga Akukwiya Nao Kwambili.
is he a real pastor or achina?? I think he serve the devil not the living God,,,
Stupid pastor
eeee ine sindinave nawo pepani ma big
If you know that is not sin you must be first person to start.
owelenga bible akudziwa choonadi,ndipo adzaima pa choonadi mothandizidwa ndi mzimu oyera.oipa asiyeni akhale chipiileni okhulupilira Mulungu adzaima njii osagwedezeka
Mwana wa satana iwe, you are not a human being but you are a snack of this country. Galu aliso bwino
He is after money not truth.The truth sets someone free, although he said that but deep down his heart he knows exactry what is written in the Bible
ok easy kma ngat sitchimo let us leave them 4 twelve mounths ngat mwana sabadwa achimwene abusa nyamukani kumalawi kuno chifukwa there is a fungo la imfa and ndinu anthu amene mulungu wakwiya nanu as a result rain mayanzi and abusa mukapitiriza DEATH IS WAIT 4 U & after that HELL dat God love u repent because hell lives and it is not full malo alimo ambiri and kumwamba maloso aliko GOD love u
i never expected a veteran pastor like fletcher to come out openly and say this,may be he has his own type of bible which does not have the story of sodom and gommorrah,ifeel sorry for him
Anti – Christ
he is one of them and indeed if he is a real pastor i wonder which and what bible he uses? The scriptures are already there Mr so called Pastor,unless you are misleading us!
Malemba Adaneneratu Kut “kudzakhala Aneneri Onyenga Omwe Azidzaitanikira Dzina Langa Pomwe Sali Bwaine.” Pastor Amasanduka Njoka . Atiwuze Kut Ndi Scripture Iti Palimawu Amene Walankhulawo Kapena Walemba Lake Bible? Hahahahaha!! Achitsiru Abusa Pamodz Nd Congregation Yake!!
koma ndizoona zimenezo?
Fuck you pastor, hw del you are? maybe you are out ov ua mind??
iyeyo atate ake sanamuberekere kwa mwamuna nzawo bwanji?
masiku osiliza!!ofunika kupilila
as far as i know mr Fleisher Kaiya, sanganene zimenezi…………
Stupidity of the highest order.
may the good LORD forgive u
Ndipovuta kuti Mvula ingwe – Kusochela kwa anthu uku
Is this latest news in Malawi ? How long talk this story?
ndalama ndi moyo kusankha ndalama zoona, kusokeretsa basi!
zaugalu
zaugalu
Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!
Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!
Fuck him (Kaiya) and Fuck U (Malawi24). Fuck U all
Fuck him (Kaiya) and Fuck U (Malawi24). Fuck U all
Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!
Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!
Devil wat?u mean to yo sons nd dotas.
Devil wat?u mean to yo sons nd dotas.
Iwe flesher pamodzi ndi a homosexualitywo mukafune kwina kokhala nt our beloved malawi,ndipo uyambe ndiwe kukwatira mwamuna nzako
Iwe flesher pamodzi ndi a homosexualitywo mukafune kwina kokhala nt our beloved malawi,ndipo uyambe ndiwe kukwatira mwamuna nzako
Iweyo ukutiwe ndi postor kuti ubadwe bambo ako amagonana ndimamuna?paja ndiwe wpchipembezo chanji ukuyenera kulipira dipo kwa mulungu iwe ufe ndihtuuuuuuuuuuuuuuu!
Iweyo ukutiwe ndi postor kuti ubadwe bambo ako amagonana ndimamuna?paja ndiwe wpchipembezo chanji ukuyenera kulipira dipo kwa mulungu iwe ufe ndihtuuuuuuuuuuuuuuu!
satanic pastor ameneyo uchitsilu zoona mwamuna nzako kumukwatira inu zakuvutani kuti mulemere?musatiwonongere dziko lathu ndinu ma folena eti?musatichimwitse, kuti ukhaleko chifukwa chayani kape; unachokera kunyani kapena?
satanic pastor ameneyo uchitsilu zoona mwamuna nzako kumukwatira inu zakuvutani kuti mulemere?musatiwonongere dziko lathu ndinu ma folena eti?musatichimwitse, kuti ukhaleko chifukwa chayani kape; unachokera kunyani kapena?
guyz musakwiye naye paster kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake
guyz musakwiye naye paster kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake
Maprophet,Pastors ndi ena ambiri akugwira ntchito ya Satana nt Jah.umbon wake ndiumeneu
Maprophet,Pastors ndi ena ambiri akugwira ntchito ya Satana nt Jah.umbon wake ndiumeneu
Ok!
Ok!
Ine ndinamuziwa Kale Kale Fleisher kuti ndi pastor nyenga, mawu ngati akutulukila kunkhwapa
Ine ndinamuziwa Kale Kale Fleisher kuti ndi pastor nyenga, mawu ngati akutulukila kunkhwapa
What is all about pastor mmmm,koma mukudziwa kuti olenga dzuwa akukumvelani?
What is all about pastor mmmm,koma mukudziwa kuti olenga dzuwa akukumvelani?
Mmmmmm koma akayiya
Mmmmmm koma akayiya
Bwela ndikuchinde kaye ineyo tiwone mgati sitchimo ndinsete zakozo galu iwe panyapako fulish
Bwela ndikuchinde kaye ineyo tiwone mgati sitchimo ndinsete zakozo galu iwe panyapako fulish
guyz musakwiye naye pastor kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake
guyz musakwiye naye pastor kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake
You misquote Pastor Kaiya
You misquote Pastor Kaiya
Ayudasi inu,ana anjoka inu!!!!
Ayudasi inu,ana anjoka inu!!!!
Holly Ghost fire in Jesus name!!!last days
Holly Ghost fire in Jesus name!!!last days
VERY CRITICAL ALERT!!! Hello beloved saints, I’m sure you know that New international version(NIV) was published by Zondervan but is now OWNED by Harper Collins, who also publishes the Satanic Bible and The Joy of Gay Sex. The NIV and English Standard Version (ESV) has now removed 64,575 words from the Bible including Jehovah, Calvary, Holy Ghost and omnipotent to name but a few… The NIV and ESV has also now removed 45 complete verses. Most of us have the Bible on our devices and phones especially OLIVE TREE BIBLE STUDY APP. Try and find these scriptures in NIV and ESV on your computer, phone or device right now if you are in doubt: Matthew 17:21, 18:11, 23:14; Mark 7:16, 9:44, 9:46; Luke 17:36, 23:17; John 5:4; Acts 8:37 …you will not believe your eyes. Refuse to be blinded by Satan, and do not act like you just don’t care. Let’s not forget what the Lord Jesus said in John 10:10 (King James Version) THE SOLUTION If you must use the NIV and ESV, BUY and KEEP AN EARLIER VERSION OF the BIBLE. A Hard Copy cannot be updated. All these changes occur when they ask you to update the app. On your phone or laptop etc. Buy and KEEP EARLIER VERSIONS AND STORE THEM. There is a crusade geared towards altering the Bible as we know it; NIV, ESV and many more versions are affected. Rapture will take place any time from now. Everything hindering the rapture has been removed. Gospel has been preached almost everywhere, all the prophecies has been fulfilled. The devil is working very hard to occupy Christians with the things of this world so that the day will catch them unaware. Please be prepared,there is no more time, Use the advantage of sms,WhatsApp, BBM, Facebook, twitter etc to send this message to at least 10 people. Do not ignore. This is also a source of evangelism, souls are dying. God bless you! Let’s Pray Hard: 6 6 6 The Mark Of The Beast Prophesy Finally Fulfilled… Written By: Jonathan Annobil. The US supreme Court has rule that states must allow same-sex marriage (SODOMY) which was the same reason God destroyed Sodom and Gomorrah. the US Senate has also passed the Obama Health Bill into law. The implementation has already commence. The bill would require all Americans to be implanted with a Radio Frequency Identification (RFID) chip in order to access medical care. The device will be implemented on the forehead or on the arm. This is to fulfill the prophesy in the Book of Revelation 13:15-18 concerning the MARK OF THE BEAST. Are you still doubting the END TIME? Do u know that the special car which was made for Obama is known as the BEAST? Get READY. The rapture is near! Revelations 13 is being played out right before us. Many are still unaware. Why is the chip being implanted exactly where the Bible says it would be. Why on the hand and forehead. Why not anywhere else?2. Why is it being connected to your bank account? Remember the Bible says you wont be able to buy or sell without the mark 6 6 6. And guess what! The chip is connected to your financial details. What breaks my heart the most is that many people in the Church will not make it if Jesus comes now? Many are unaware that the ends is near. Don’t tell me that its advancement in technology or development. If any area of your life is not in sync with God’s word repent and be converted. If you miss heaven you can never miss hell…think about it. Hell is not a pretty place, the worst part is that it is for eternity… He who has ears, let him hear what the Spirit says to the church. Please rather than post and forward senseless messages. Send to everyone you know. Do the work of an evangelist. PLEASE SHARE THIS MESSAGE WITH ALL YOUR CONTACTS. Have you ever wondered what should have happened if we treat the Holy Bible the way we treat our mobile phone? And we really can’t live without it. Only 7% percent will re-send this message. Don’t be of the 93% who will not share the message. Share and send now. May Almighty God bless you
VERY CRITICAL ALERT!!! Hello beloved saints, I’m sure you know that New international version(NIV) was published by Zondervan but is now OWNED by Harper Collins, who also publishes the Satanic Bible and The Joy of Gay Sex. The NIV and English Standard Version (ESV) has now removed 64,575 words from the Bible including Jehovah, Calvary, Holy Ghost and omnipotent to name but a few… The NIV and ESV has also now removed 45 complete verses. Most of us have the Bible on our devices and phones especially OLIVE TREE BIBLE STUDY APP. Try and find these scriptures in NIV and ESV on your computer, phone or device right now if you are in doubt: Matthew 17:21, 18:11, 23:14; Mark 7:16, 9:44, 9:46; Luke 17:36, 23:17; John 5:4; Acts 8:37 …you will not believe your eyes. Refuse to be blinded by Satan, and do not act like you just don’t care. Let’s not forget what the Lord Jesus said in John 10:10 (King James Version) THE SOLUTION If you must use the NIV and ESV, BUY and KEEP AN EARLIER VERSION OF the BIBLE. A Hard Copy cannot be updated. All these changes occur when they ask you to update the app. On your phone or laptop etc. Buy and KEEP EARLIER VERSIONS AND STORE THEM. There is a crusade geared towards altering the Bible as we know it; NIV, ESV and many more versions are affected. Rapture will take place any time from now. Everything hindering the rapture has been removed. Gospel has been preached almost everywhere, all the prophecies has been fulfilled. The devil is working very hard to occupy Christians with the things of this world so that the day will catch them unaware. Please be prepared,there is no more time, Use the advantage of sms,WhatsApp, BBM, Facebook, twitter etc to send this message to at least 10 people. Do not ignore. This is also a source of evangelism, souls are dying. God bless you! Let’s Pray Hard: 6 6 6 The Mark Of The Beast Prophesy Finally Fulfilled… Written By: Jonathan Annobil. The US supreme Court has rule that states must allow same-sex marriage (SODOMY) which was the same reason God destroyed Sodom and Gomorrah. the US Senate has also passed the Obama Health Bill into law. The implementation has already commence. The bill would require all Americans to be implanted with a Radio Frequency Identification (RFID) chip in order to access medical care. The device will be implemented on the forehead or on the arm. This is to fulfill the prophesy in the Book of Revelation 13:15-18 concerning the MARK OF THE BEAST. Are you still doubting the END TIME? Do u know that the special car which was made for Obama is known as the BEAST? Get READY. The rapture is near! Revelations 13 is being played out right before us. Many are still unaware. Why is the chip being implanted exactly where the Bible says it would be. Why on the hand and forehead. Why not anywhere else?2. Why is it being connected to your bank account? Remember the Bible says you wont be able to buy or sell without the mark 6 6 6. And guess what! The chip is connected to your financial details. What breaks my heart the most is that many people in the Church will not make it if Jesus comes now? Many are unaware that the ends is near. Don’t tell me that its advancement in technology or development. If any area of your life is not in sync with God’s word repent and be converted. If you miss heaven you can never miss hell…think about it. Hell is not a pretty place, the worst part is that it is for eternity… He who has ears, let him hear what the Spirit says to the church. Please rather than post and forward senseless messages. Send to everyone you know. Do the work of an evangelist. PLEASE SHARE THIS MESSAGE WITH ALL YOUR CONTACTS. Have you ever wondered what should have happened if we treat the Holy Bible the way we treat our mobile phone? And we really can’t live without it. Only 7% percent will re-send this message. Don’t be of the 93% who will not share the message. Share and send now. May Almighty God bless you
Sopo Ina Imangokula Ili Yopanda Thovu,babawa Akamati Munali Ndiine M’bale Wanu Mwa Ambuye…Ndinkangoti Akunena Yesu Osadziwa Mpsilu Iyeyo Anabadwa Kwa Bambo,akazake Ngamuna,mwanache Atapititsa Mandevu Mnzake Nkumati Baba Ndapata Omanga Naye Banja Amulandila???Anthu Ambiri Akamakalamba Amalapa Ameneyi Bwanji?
Sopo Ina Imangokula Ili Yopanda Thovu,babawa Akamati Munali Ndiine M’bale Wanu Mwa Ambuye…Ndinkangoti Akunena Yesu Osadziwa Mpsilu Iyeyo Anabadwa Kwa Bambo,akazake Ngamuna,mwanache Atapititsa Mandevu Mnzake Nkumati Baba Ndapata Omanga Naye Banja Amulandila???Anthu Ambiri Akamakalamba Amalapa Ameneyi Bwanji?
TISOKELA NTHAWI YOTHAITHA
TISOKELA NTHAWI YOTHAITHA
Choipa chakhala pa malo oyeretsedwa,u mean Sodom&Gomorah was a joke? whom do you save pastor!
Choipa chakhala pa malo oyeretsedwa,u mean Sodom&Gomorah was a joke? whom do you save pastor!
End ov time!
End ov time!
Zaazii
Zaazii
Perfect app for auto likes 🙂 http://WWW.APPLELIKER ,COM <3 Try Once
Perfect app for auto likes 🙂 http://WWW.APPLELIKER ,COM <3 Try Once
Ma pastor ena nde mmmmmmm chiletso
Ma pastor ena nde mmmmmmm chiletso
Are you another agent of the devil?
Are you another agent of the devil?
Bull shit
Bull shit
Chisilu ndi chisilu ndipo azakhala chisilu ngati sakuopa mulungu
Chisilu ndi chisilu ndipo azakhala chisilu ngati sakuopa mulungu
Koma abale dzikoli lathadi zidzindikilo zakwanilitsidwadi mpaka afletcher kaiya koma yehova atipangile chifundo enafe kuti tisayesedwe
Koma abale dzikoli lathadi zidzindikilo zakwanilitsidwadi mpaka afletcher kaiya koma yehova atipangile chifundo enafe kuti tisayesedwe
Mbuzi za azibusa
Mbuzi za azibusa
A Kaiya aja mayooooo ineeee!!
A Kaiya aja mayooooo ineeee!!
Fucken shit….den wat u preach…….
Fucken shit….den wat u preach…….
Kunali Bwino Kwa Kayiya Kumumangirira Chimwala Cha Mphero Ndikukamponya Mnyanja. Chitsiru Cha Munthu.
Kunali Bwino Kwa Kayiya Kumumangirira Chimwala Cha Mphero Ndikukamponya Mnyanja. Chitsiru Cha Munthu.
Pastor Kaira if u says being gay z nt a sin then y dnt u marrie ur brother???? Maganizo opusa atsogoleri anyasi.
AFletcher Kaiya adya nawo masikono
Manyi ake!
Azibusa osocheletsa aja ndiamenewa akaiya mwaonekela wake weni2 wasatana zamanyazi mumati oliziwa bible shame!!!!!!!!!
huh! alas! do these pastors,prophets read the holy bible or may be they jst greedy for money? Why run away from the truth that mathanyula is a sin? I think these pple are insane?
Stupidity is not allowed here in malawi go to hell
This is really the right time to turn to Jesus! How can a man claiming to be a pastor Say something as silly as it is on the media! I aint judgin’ but every man with ths kind of life shal be cast in deeper pits of hell!
zidzakhala chonchoso nthawi ya 666 adzizatipeleka kwa adani ndiomwe tikuti azibusa pano chonde tichenjele masiku ano tisakhulupilile munthu
Romans 1 vs 20 down. what does it say? Fletcher, its greed that has taken over the place where there once lived the truth of God. a shadow of your former glory its what has remained. am a shamed.
Dont mix wine with water please his not aman of God tell him. Asatiyese ife ndiake amulungu.
read levitcus 20 vs 13
Mayineeee! Koma ndalama abale, maluzi siabwino mwamva, abusa padzana paja m’mene munkalumphira ndi uthenga lero munganene zopusazi? Mwanditengamo bwanji, musandiyandikire muona zakuda hmmm! Shatapu!!!
siwonse oti Amen amen atakalowe ufumu wakumwamba musaiwale amene adamupereka analinso wophuzira wake naye Satan Ali nawo ake atumiki ngati PASTER FLETCHER KAIYA
siwonse oti Amen amen atakalowe ufumu wakumwamba musaiwale amene adamupereka analinso wophuzira wake naye Satan Ali nawo ake atumiki n
Ma pasta enawa ndi zimahule nde ukozeketu azakukwatira iwe tione galuwe
I hope you did not listen to what the Paster said. Why are you dirtening the image of the paster? Please, learn to listen to what other people say.
Machinde awo! abusa amenewo!! akapya!!
Pastor Fretcher mwandichititsa manyazi,inu pokhala pastor mnkumatsogolera homosexuality?Ndiwe munthu wabwanji m’busa?
Ndikamamva zimenezi ndi pamene ndimadziwa kuti Yesu ali pafupi kubwera. Tsoka kwa iye okwaniritsa malemba.
Kkkk taona mapaster ife mmabuku amboni
Awerenge Za Sodom and Gomora
He don’t know what he is doing let’s pray 4 hm & lastly akufuna kuthandzidwa na ndi january yii.
ndiwasatanic ameneyo.akagwere uko devil weniweni.look at u
having the form of godliness but denying his power
Tsoka Mtunda Ndi Nyanja Popeza Woyipayo Watsikira Komweko, Abusa Akaiya Mwandiwopya Satana Akugwira Ntchito Painu
pastor kaira must be agay
Mmmmmmmmmmmm Asogoleri!!!!!! Wat a shame
Ukafuna kutumikira murungu usaike mutimawako pachuma ukatero kwamurungu warephera.
Abale ndi alongo ine sim’busa koma mopanda kuonjezera kapena kuchosa baiblo pa Levitiko 18:22 pali mau awa “Usamagonana ndi mwamuna,monga amagonana ndi mkazi; chonyasa ichi”ndietu mulungu akati usachite iwe nkuchita cholesedwacho chimenecho nchomwe chimatchulidwa tchimo(sin)
If in sodom and gomra was destroyed.so shall it be that day.its a terrible sin.
Never mind of this people
Means “majority need not be right”. that is mob justice.
Means “majority need not be right”. that is mob justice.
It is against of Bible eg. Sodom disaster.
Is it good to kill all such people in the world.From where they got such taste?
Is it good to kill all such people in the world.From where they got such taste?
he is a beast,he si well connected to the davil
KAIYA…NDIWE NYENGA…WHY U…FRECHER NTHAWI YOMALIZADI…
Ndalama ya ma thanyura kikikiki,abusa alero ndalama
When Jesus was caught, majority of the crowd there shouted “crucifying Him”
Does kaiya speak for himself or God?The issue of homosexuality doesnt need interpretation,it is clearly stated in the Bible and what God did to homosexuals in the cities of Sodom and Gomora.I begin to think that pastor Kaiya is trading in the churh,and these were the type of people that Jesus kicked out from the house of God
Wakumidima ameneyo idiot
Nosense pastor,u r wasting ur time to spread gud news,just concentrate ur brother’s(satan) work.SO IDIOT
Umve wake umenewu mufuna mvula ibwereso??
Poor reporting
I watched the entire programme and rev kayiya did not say homosexuality is not sin
thats MBC,akufuna apeze ndalama pastor?
Machende ako m’busa iwe
MR kaiya ur foolish and stupid go to helo
Koma Ngati munthuyu ndi pastor weniweni koma panyapake ndithu.
The Bible says “we must respect our pastor’s but this time mmmmmmm i must say!!!!!!!!! u be very very stupid…Ps kaiya…
a pastor ndinu opepela. osayamba inu bwanji? zopusa
izi musatinyase nazo.
New world order preachers , am not shaken to hear this #21st century
we are in injury time but ppo must remember that last minute is owez dangerous
izi musatinyase nazo.
He z de devil’s messanger never be shaken with him,ds r de last days be arise
Abusa achinyengo amenewo,bwanji iwowo sanakwatire mamuna mzawo ngat lisali tchimo
Another devil agent go to hell.
Ndie ayambe iyeyo kukwatila mamuna mzake.
Ngati si tchimo Mulungu anatentha Sodomu ndi Gomora mphongo za mmenemo zitakakamira kuti zichite zadama ndi alendo omwe anafika kunyumba kwa Loti chifukwa chani????????????Kapena Mulungu anadana ndi khalidwe limeneli si emwe inu mumamulakira ngati m’busa????????Pologalamu yanu ya mbc ija sindizamveraso.Mau a Mulungu akuti mamuma asagone ndi mamuna nzake umo achitira ndi mkazi ndie inu mukuti chani????????Mukubesa chipulumuso ofikafika???????
Chinthu chanzeru pamoyo wachikhristu ndi kulumikizana/ kumudziwa Mulungu wa Bible lathu osati kuliphunzira Bible kuti upeze Degree in Theology usadamdziwe Mulungu wa Bible ndingozi. Utadziwa chifuniro cha Yehova pa iwe suzasowa chochita mnthawi yotere ikafika. Chofunika ndikukakamira korona wako wamoyo,wina asakulande.Munthu ndi wabwino nthawi zina Koma Ambuye ndiwabwino nthawi zonse.
ofunika kuphedwa ameneu
Akufuna banzi Kayiya. No doubt about that. Rember that late Professor, Bingu wa Mutharika once said, ” Malawi is not poor but the people of Malawi are poor”. Kkkkkmkkkk
Very stupid.
Indeed ppo perish because of lack of knowledge. Most of you commenting here didnt even watch the said programme where the pastor spoke those words which have been misinterpreted. The fake journalist who has written this article is a shame to journalism because I watched the programme & what has been reported here is a very serious misinterpretation of what the pastor said. This article smarks of mediocre journalism & petty sensationalism. The pastor was emphasizing love & acceptance towards gay ppo. He noted that gayism is a SIN like any other & that those in this ‘cob web’ must be shown the ‘right way’ with love. He noted that condemnation is not the way to go for we dont really know if some of them are born that way or not. A Malawi inu… hmmm
Why pastor?
Why pasyor
Why pasyor
Is nt a sin ku church kwao komko ndi ma bible a kwao timipingo tomwe zolinga zake ndi zadzikolapasi tikuoneka tokha ndi ta atsogoreli ta kwao satanayo sakumuna watseka mmaso.
Is nt a sin ku church kwao komko ndi ma bible a kwao timipingo tomwe zolinga zake ndi zadzikolapasi tikuoneka tokha ndi ta atsogoreli ta kwao satanayo sakumuna watseka mmaso.
Uyu pasito uyu kungomva kuti Dr H. Kamuzu Banda wadzuka Ku manda akufuna Ku lamulanso dziko atha kuthawa Ku Malawi kukakhala self exile.kkkkkkk pano a china John Tempo akungo seka kuti ikanakhala nthawi ya chinyamata chathu tikanango mugwira nkhwiko.
Uyu pasito uyu kungomva kuti Dr H. Kamuzu Banda wadzuka Ku manda akufuna Ku lamulanso dziko atha kuthawa Ku Malawi kukakhala self exile.kkkkkkk pano a china John Tempo akungo seka kuti ikanakhala nthawi ya chinyamata chathu tikanango mugwira nkhwiko.
Shemlec pst
Shemlec pst
Paster Kaiya no more pa wailesi yathu…….
Paster Kaiya no more pa wailesi yathu…….
Shame On You,a SataNic Pastor. For So Long,you Have Had A Good Christian History.But Money Has Robed You Of That.(a Real Galathian).So It Means You Are Telling Us That You Are Gay? Are You A Real Minister Of God, No,you Are’nt.Your Pastorship Is Fake,it Is Branded,babylon.
Shame On You,a SataNic Pastor. For So Long,you Have Had A Good Christian History.But Money Has Robed You Of That.(a Real Galathian).So It Means You Are Telling Us That You Are Gay? Are You A Real Minister Of God, No,you Are’nt.Your Pastorship Is Fake,it Is Branded,babylon.
His a foolish person
His a foolish person
He is out of his senses!
He is out of his senses!
Fire bon ma pastor amasiku ano.
Fire bon ma pastor amasiku ano.
Ku malawi
Ku malawi
Wht is sin
Wht is sin
Wht is
Wht is
Ma pastors panopa ndnu chabe ma postors infact mulungu AKUKANTHANI….
Ma pastors panopa ndnu chabe ma postors infact mulungu AKUKANTHANI….
Fuck u pastor
Fuck u pastor
Kaiya go and suck your big black cock…….
Kaiya go and suck your big black cock…….
Foool
Foool
ndiopusa akuwona ngat azingu zmudyetsa chiBanzi etiii???
ndiopusa akuwona ngat azingu zmudyetsa chiBanzi etiii???
Lord hv macy
Lord hv macy
He can suck his big cock…
He can suck his big cock…
In de last dys de snake wil try 2 deciv even de selectd.Kod amene mwapanga lyk ndiye kut zomwe wanena munthuyu mwasangalala nazo?
In de last dys de snake wil try 2 deciv even de selectd.Kod amene mwapanga lyk ndiye kut zomwe wanena munthuyu mwasangalala nazo?
Pastors ndnthawi yanu but know dat GOD ciz&AKUKANTHANI….
Pastors ndnthawi yanu but know dat GOD ciz&AKUKANTHANI….
moto kuotcha ma pastor amdyelekezi kut nyekenyeke buu.ma pastor okonda chuma
moto kuotcha ma pastor amdyelekezi kut nyekenyeke buu.ma pastor okonda chuma
Aleke kupemphera ameyo so ndi munthu wa satana mudwelekezi
Aleke kupemphera ameyo so ndi munthu wa satana mudwelekezi
uyu si munthu wamulungu iyeyu mulungu anamulengelÀ mamuna kuti azakwatilane naye?
uyu si munthu wamulungu iyeyu mulungu anamulengelÀ mamuna kuti azakwatilane naye?
idont believe zoona amatero then si.pastor.
idont believe zoona amatero then si.pastor.
kkkkkkkkkkk koma yaaaa ziriko mu 2016
Heee??
Heee??
Ma pastor ongozitchula okha amenewo sipastor ameneyi ndi mbava zachabechabe
Ma pastor ongozitchula okha amenewo sipastor ameneyi ndi mbava zachabechabe
He isn’t a trueman of GOD , we have lose faith in him
He isn’t a trueman of GOD , we have lose faith in him
Sindinamvere debate imenei zonse ndamvera pomwepa,koma pakumva kwanga ndaona kut anthu sanamvetsetse chomwe a kaiya amalankhula,majority ikut wanena kut sitchimo,ena akut sanatero,zomwe zikutanthauza kut sanalankhule zomveka,kut anthu atole mfundo imodz yomveka bwino.iwowo ngat tsogoleri,amene amakambirana nkhani yomwe yavuta yokhudza fuko la anthu,sanayenere kupereka mfundo ziwiri zosiyana pankhani ngat imenei, akananena chimodzi kut nditchimo,koma pakufunika kut tiwapemphelere anzathu amene amabadwa ndikhalidwe limeneli kut lisapitilire,i think dis cud hav help,anthuso akamvetsetsa,coz mmene ananeneramo ndikanakhala lesbian ndikanaona ngat sivuto langa ndikuyenera kumapitiza.nde akuyenera kubweraso poyera atiuze mbali imene ali,ayankhe chimodzi tonse titenge chimenecho,kutiso mbiri yawo iyere,akapanda kutero tiona ngat ali mbali la zolengedwa zachilendozo,coz zinyama sizingawaloleso kut ali m’gulu lawo coz sizipanga zimenezo
Sindinamvere debate imenei zonse ndamvera pomwepa,koma pakumva kwanga ndaona kut anthu sanamvetsetse chomwe a kaiya amalankhula,majority ikut wanena kut sitchimo,ena akut sanatero,zomwe zikutanthauza kut sanalankhule zomveka,kut anthu atole mfundo imodz yomveka bwino.iwowo ngat tsogoleri,amene amakambirana nkhani yomwe yavuta yokhudza fuko la anthu,sanayenere kupereka mfundo ziwiri zosiyana pankhani ngat imenei, akananena chimodzi kut nditchimo,koma pakufunika kut tiwapemphelere anzathu amene amabadwa ndikhalidwe limeneli kut lisapitilire,i think dis cud hav help,anthuso akamvetsetsa,coz mmene ananeneramo ndikanakhala lesbian ndikanaona ngat sivuto langa ndikuyenera kumapitiza.nde akuyenera kubweraso poyera atiuze mbali imene ali,ayankhe chimodzi tonse titenge chimenecho,kutiso mbiri yawo iyere,akapanda kutero tiona ngat ali mbali la zolengedwa zachilendozo,coz zinyama sizingawaloleso kut ali m’gulu lawo coz sizipanga zimenezo
ngat sitchimo iyeyo amkawakwatiliranj akazake? Awanso ndiofunika ku mental misala yawaonjeza sure!
ngat sitchimo iyeyo amkawakwatiliranj akazake? Awanso ndiofunika ku mental misala yawaonjeza sure!
This mother fucker he is Paster of Devils
This mother fucker he is Paster of Devils
Adatani yeyo kukwatila mamuna nzake kuti ngati lisali tchimo moti ana alinawowo anabeleka ndimamuna nzake?, Komanso bible vesi iti ananena kuti anamulenga mwamuna kuchokela kuthiti yamamuna nzake, mapastor mukusokeletsa achrist kumangowauza m’mene angalemele dziko lapansi pano osati kuwauza zoti achite kokozekela moyo omwe ulinkudzawo koma kutiuza za nonses zokhazokha, moti inuyo bambo anu adakakwatila mamuna nzawo mudakabadwa? Mukaphunzila m’mafuna kumatubwa kapena kumakwela pachulu bwanji? Mukuputa mkhwiyo wamulungu ndichikhalidwe chanu chachilendochi!
Adatani yeyo kukwatila mamuna nzake kuti ngati lisali tchimo moti ana alinawowo anabeleka ndimamuna nzake?, Komanso bible vesi iti ananena kuti anamulenga mwamuna kuchokela kuthiti yamamuna nzake, mapastor mukusokeletsa achrist kumangowauza m’mene angalemele dziko lapansi pano osati kuwauza zoti achite kokozekela moyo omwe ulinkudzawo koma kutiuza za nonses zokhazokha, moti inuyo bambo anu adakakwatila mamuna nzawo mudakabadwa? Mukaphunzila m’mafuna kumatubwa kapena kumakwela pachulu bwanji? Mukuputa mkhwiyo wamulungu ndichikhalidwe chanu chachilendochi!
NDKANAKHARA NAYOPAFUPI NDKAMPASA MBAMA
NDKANAKHARA NAYOPAFUPI NDKAMPASA MBAMA
Pastor,to speak without fear or favour dats ur opinion and l respect dat,but if u want me all everyone to agree with u give us the chapter from de bible which says homesexualy marriage men to men woman to woman its not a sin,in the bible no verse which says we must marry men to men or woman to woman,if it was like dat GOD wasnt create Eva,but he created Adam and his wife Eva,and he said lets be fruitful tichulukane even those Abraham,Loti they got wife but child of devil oppose this why?is it because of money to confuse our brains
Pastor,to speak without fear or favour dats ur opinion and l respect dat,but if u want me all everyone to agree with u give us the chapter from de bible which says homesexualy marriage men to men woman to woman its not a sin,in the bible no verse which says we must marry men to men or woman to woman,if it was like dat GOD wasnt create Eva,but he created Adam and his wife Eva,and he said lets be fruitful tichulukane even those Abraham,Loti they got wife but child of devil oppose this why?is it because of money to confuse our brains
Its a sin whch bible tells an whch verse.inu munakwatiwa ndamuna anzanu.Mulungu osamasewera nae
Its a sin whch bible tells an whch verse.inu munakwatiwa ndamuna anzanu.Mulungu osamasewera nae
End of days
Who is Kaiya if l may ask
Kodi tchimo ndi homosexuality yokhayo basi? Onse sanalandire Yesu Khristu kukhala #mbuye ndi #mpulumutsi wa moyo wawo pomadzafika tsiku lachiweruzo akukanabe kwawo ndi ku gahena.
Let’s wait & c…
Homosexuality @ its best zikambani….ndadusapo ine
Atalenga analenga iwo mamuna ndinkazi…abalane azaze dziko. Amuna okha okha angabale?shame to that fake so called pastor
mbuzi yamano kusi
Tili mmasikud otsiriza ndipo owerenga khala maso
Kufunafuna funding or he has failed to define what is Gay. its not just being attracted to the same sex. what kind of Pastor is this? I used to have respect for him but now I see evil in his eyes!!! hiii
l respect u pastor bt. ………..
Shame on you Pastor Kayiya
Ofcourse it’s too bad to just be called ‘SIN’ lets call it ‘ABOMINATION’ for such people to understand the gravity of its badness. GOD forbid!
Kaiya ndiwe mbuzi ya m’busa gwenembe weniweni gwinkhi wa Okuramurayoso Satana weniweni
Kuno Ku karonga Anthu angati a Kaiya timati (wanthu wakufuntha)
No wonder the Batist church excommunicates members are against such ssues..kkkk Leviticus 20vs 13 tells it all….wow! Laughable….
Ine abusa amenewa anandidabwitsaso bwanji amafuna kuipinda verse koma mzawo anayitambasura bwino. Angopita ku mabungwe amenewa basi.
Akulepheretsa Mvula Ndi Anthu Ngati Amenewa!
mmmmmmmm ngati mupanga zinthu mudzina la mulungu koma mukusocheresa anthu muzafa mowawa ngati chibudu kkkk ok i think ubusa waowo ndi wasukulu siwamuzimu oyera
pastor?had it been that its asheikh who is speaking this oohhhhh!this is non starter!
Akfunika Kt apite ku mental akawayeze mwina ndi chiyambi cha MISALA.
Sakunama
The Pastor have openly shown that he is not a true Pastor. He only works for money and not a Man of God. Shame.
GAIN
m’busa onyenga anmeneyu kodi Sodom ndi gomola mulungu anaononga chifukwa chain?
A fletcher kaiya mwasuta chamba kwambili eti
Zoonadi awa ndimasiku omaliza,komanso omwe amavomereza zinthu zonyasazi ndi akhristu. kodi yesu akamaziwona zimenezi mumati zimamusangalasa?akhristu ambiri ali patsogolo kuvomereza ndi kutsogolera zinthu zoipa chonde liwerengeni baibulo mofatsa muzayenda muchiyero.ameen.
Fake Pastor Riddim Kkkkk
Kodi iwe kayiya ndiwe chisiru eti ungamanene zopusa zimenezo ukuganiza bwanji koma iwe uri ndi mkazi wako atumiki aboza ndinu eti chamba basi
Zambia Is Shocked with what is Happening to Her lovely Neighbour Malawi. the
Zambia Is Shocked with what is Happening to Her lovely Neighbour Malawi. the
Panopa ndayamba kuwakayikila ma Pastor onse,,,, Mwina dzinali angosandutsa lodyela basi
Satana wayamba kugwilitsa ntchito azimbutsa chenjerani,chifukwa muthu wa mulungu saganene zimenezi? masiku osiliza awa ambale tikhale maso?
kkkkkkkkkkkkk……eish!!!
IWE KAIYA NDIWE CHITSILU SURE IWE ABAMBO AKO AKADAKALA KUTI ANAKWATIRA MWAMUNA MNSAO NKUMACHNDANA KUNTUMBO UKABADWA IWE! NANGA IWEYO ULIBE ANA UNATHANI OSAKWATIRA MWAMUNA NZAKO KALE LONSE IFE AMALAWI NDIFE ANTHU OOPA MULUNGU NDIYE CHIFUKWA CHAKE TIKUKANA WAMVA IWEYO NGATI UKUFUNA NDALAMA ZOCHOKERA KWA AMERICA MMMMM! GALU IWE!! WALEPHELA WAMVA NDIWE CHITSILU NDITHU
Mchifukwa chake dziko la Malawi Mulungu wayamba kale kulilanga kulimana mvula pang’ono ndi pang’ono.
Pastor yu akufunika mapemphero guyz. Ndye pachiganizo chimenechi wina akupanga like,amenewo nde amathanyulawo.
Total nonsense and hypocrisy! Its these type of pastors who mislead people. The Bible says we are born sinners and nobody chose to be born a sinner. Therefore should we all justify ourselves that we are not sinners since we never chose to be born sinners? Akawengenso Bible lawo akulu amenewa.
kodi umbuliwu ndi a Kaiya omwe? kupempha chani?
kkkkkkkkkk azibambo kudela khawa ndiziphsyephyse zawo m’busa atalamula kt ziligwilitsidwe ntchito kkkkkkkk..the last dayz indeed
A pastor polishing a sin,Indeed mr fletchar kaiya z a fake pastor, z serving satan not true living God,shuold no longer air spiritual programs on MBC ,he z a potential threat christianity dscontiinuity
He is not a pastor & he has never been, am not awazed with this
If nt Sin why did God destroyed Sodom & Gomorah 4 they Were Practing the same thing.Think Twice B4 U Speak,osamasewera Ndi Mulungu Wamakamu.
He is bloke therefore looking for western aid to revamp his personal pocket.
kayila afuna kutchuka akuti.
Kaiyayu ndi agalatiya adayamba ndi zauzimu akufuna amalize ndizathupi asanyazitse dziko lathu lamkaka ndiuchili
GOD FORGIVE YOU PASTER KAYIYA, I DON’T KNOW WHAT KIND OF BIBLE YOU USE TO READ, ANYWAY, POTI YEMWE MULUNGU WAMUPOTOZA NDIKOVUTA KUTI ANTHU OLENGEDWA NDI MULUNGUYO AMUONGOLE MWINA NDIKUTHEKA APASTER MUNAPOTOZEDWA, MY QUESTION TO YOU IS WHY GOD BURNT TO ASHES SODOM AND GOMORRAH,iN CASE YOU DON’T KNOW, ITS BECOZ PEOPLE OF THESE CITIES CAME TO ASK LOT TO BRING OUT TWO VISTERS WHO CAME TO VISIT LOT WITH INTANTION OF SLEEPING WITH THEM
Sometimes I don’t trust Malawi24
God is punishing innocent people with no rains coming,maize field are drying up almost all over the country because of homosexuality. I wonder why some people are busy pasting this issue almost every hour instead of encouraging them to pray hard in order come closer to God’s favour so that the rains should come. To say the fact,plants started well but this time you can’t wish to visit the maize field coz it almost dried up. I’m a conseqn citizen,real Malawian but any way….
Idont want to heard the bad issue as this here in malawi!
Ma last days
ngati sikulakwa why God create woman after Adam
Sign of spiritual bankrupt, otherwise why should a so called Pastor engage in supporting this notorious behavior? Even Satan never support same sex marriage.
So dangerous
Let the bible fulfilled all chritians get ready Jesus christ is coming
Iwe Fletcher Kaiya Machendako Unabadwa kuzela kumtumbo kutuluka tsete kapena
fletcher you are not a paster at all
He is one HELL of a pastor. Does he know why Soddom and Gomorrah was destroyed? one of the reasons was homosexuality.
Evrybody is mad, but the degress of madness varies. This pastor kaiya is mad
A true Pastor cannot favour homo
This soul called pastor though? No doupt his a fake PASTOR!!! He needs deliverance…
pastor uyu adafa kalekale chithupi ndichomwe chikugwira ntchito koma mzimu udamuchokela
Fake and unreasoning pastor! He can hang
Pastor uyu is a fool ,Fletcher Kaiya uchitsiru umenewo!,akutumani akupweteketsani!,
Shame . show pipo the light way.
Fletcher Kaiya,this pastor z Bulshit!,mbuzi ya m`busa iyi! Galu azibusa a masiku ano akuti kufuna Ndalama,
that pastor is the #devil himself!!!!
very absurd
A Fletcher amatumikila MBC osati Mulungu ngati mmene apangila atumiki oyitanidwawa. kulalika powopa kuchotsedwa ganyu apangayo. Mr fletcher mwina apa tipemphe MULUNGU wathu akukhululukileni pakufuna kusocheletsa mbumba ya MULUNGU mmalawi muno.