“Homosexuality is not a sin,” says Pastor Fletcher Kaiya

Advertisement
Tiwonge Chimbalanga & Steve Monjeza are a gay couple who were arrested and jailed to 14 years in Malawi

Veteran Christian broadcaster who used to host gospel programmes on state broadcaster MBC, Pastor Fletcher Kaiya, has said that homosexuality is not a sin.

Pastor Fletcher Kaiya
Pastor Kaiya: Homosexuality is not sin

In a media debate that was followed by Malawi24, Kaiya told the host Bayana Chunga that homosexuality is not a sin.

“There are two sides to this issue. For men who choose to marry other men, that is a sin. However for men who are born attracted to other men, it’s not a sin,” said Kaiya.

He later quoted a verse from the book of Romans arguing that God created homosexuals and therefore there was a need to love them.

Kaiya further said that homosexuality wasn’t a foreign concept. He argued that it has always been happening in Malawi only that it was not mentioned in public.

Advertisement

1,317 Comments

  1. NGATI NDI UMPHAWI AKAIYA, PEZANI NJILA INA YOPEZELA NDALAMA IYI YOKHA AYI. NDINU MUNTHU WAULEMU WANU KOMA MUPUSE CHIFUKWA CHA NDALAMA?

  2. it hs shown that some ppo who r cald pastors bcoz of their education r nt really true pastor bt wat they uz iz wat they learnt,bt holly spirit is the best teacher,u pastor dnt confuse ppo,ambiriwa mphamvu ya choonadi munaitaya kale.

  3. it hs shown that some ppo who r cald pastors bcoz of their education r nt really true pastor bt wat they uz iz wat they learnt,bt holly spirit is the best teacher,u pastor dnt confuse ppo,ambiriwa mphamvu ya choonadi munaitaya kale.

  4. Nchifukwa chan nkului walankhula mopusa chonchi? Akaiya timaona ngat ndimunthu wa mulungu kma xaoneka kti ndi satana atate akathen athu oipawa achoke nxiko muno asatisochelese ife

  5. Nchifukwa chan nkului walankhula mopusa chonchi? Akaiya timaona ngat ndimunthu wa mulungu kma xaoneka kti ndi satana atate akathen athu oipawa achoke nxiko muno asatisochelese ife

  6. ai gahena ikadzadza ndithu.ife timakutengani ngati m’busa wabwino kma nyalugwe wachabechabe ndithu…inu a fake pastor ndikakuonani ndikumafuna kusanza mxm

  7. Anthu amenewa nd amene akupangisa kuti Malawi asalandile mvula yabwin malemba akuti ngati wotsogolera wa mudzi aopa Mulungu mudzi umeneo uzakhal odala koma ngati saopa Mulungu mudzio uzakhal otembereredwa nde apa tiziona nafeso mmalo moti tilape ay tiganize bwino

  8. my dear brothers and sisters, the problem with such pastors is actually not to have gone to Bible schools but its due to lack of the Holly Spirit alipo ambiri ndipo ngati salapa the hell is waiting 4 such pple,may God have mercy!!!

  9. From Old Testament to New testament homosexuality is sin.Pastor Kaiya you better resign now as you work under devil

  10. If it is nt asin….y God him self nt create aman or awoman alone?? Tsoka kwa okwanilitsa malemba

  11. comment reserved, chifukwa ndingayambe kulankhula pambali pabwino ndikupawona ndithu.

  12. Ng’oooo!,you have writen in water ng’ooo!,so you satanic pastor,you thought people would agree with your evil views?Why do you want to be a sign of last days by making people realise people will love money than love among themselves.If I may visit your home,won’t l get a wife there?what about children?dont you have?were they born from a man?was God foolish by creating Adam and Eve?If what you have said is right,God would have just created two men in the beggining rather than individuals of different sex!!TAKE NOTE:the Hello is waiting for you,you can never decieve malawians,WE ARE NOW AWAKE,these are not 1940’s!

  13. rude! mr kaiya, my God wat a sin thing, ife sitilora kuti tilangike chifukwa cha munthu mmozi we kip on saying no to homosexual. and knowingly even dogs and goats knows It is a sin according to the Holy Bible and Holy Koran and
    it is a crime according to the laws of our beloved nation.
    In the Holy Bible (ROMANS 1:18-32, 1 CORINTHIANS
    6:9-10, 1TIMOTHY 1:10) it is punishable by death,

  14. Bvuto lili ndi anthu enafe ndi loti timakhulupilira abusa koopsa mwinanso kuposanso bible,,to be honest mulungu atati atilozere axibusa enieni zoti 10 angakwane ndakayikiratu,,,,can u imagine a man who calls himself a pastor nkumati mathanyula si uchimo? which Bible does he use? am not righteous koma dis Fretcher is as bad as devil himself, ,last days inde;indeed

  15. Those are the feck pastor ,that the bible said already sorry to the people prezing god under him .I Jindex never accept a very open sin like stupid guy unless they give birth .vyamthondwee pastor ameneyo

  16. Inetu nchifukwa chake nimasilira ma islamic countries komanso chisilamu sindimafuna kumva zanyasi ngati izii

  17. “There are two sides to this issue. For men who choose to marry other men, that is a sin. However for men who are born attracted to other men, it’s not a sin,” said Kaiya…… By this it is the same with people born with physcal challenges we always accommodate them mosiyana ndi oti wakadulidwa mwendo or kuphuritsidwa maso kokaba. MALAWI24 could clearly present Pastor Kayiya opinion kuti it has 2sides even give the quoted verses in Romans because you were following it…..Its apity that Pastor kayiya has got all the insults resulting to how the article has been headlined

    1. i still see no justification to this bra! homosexuality is never in born, naturally God created a woman for man. its so unfortunate that a man of God would even suggest that other people are attracted to those of same sex by nature.

    2. Blessings with due respect…ziri ngati mmene anthu amabadwa ndi chilema…..all the people who are born with degrees of disability; crippled, blind, death were created by same GOD who created those that are whole! The way we clothe naked mad persons its the way these should be treated! Mmene sitingamulore wamisala kumapha anzake coz ndi wamisala its the same way we should help people who have same inclination to same sex that they should live a normal way not promoting such behaviour. Aliponso amene during sex action with their wives does fellatio and cuningulus (sucking each other private parts) which I just think kut homosexual does the same. Go deep on eunuchs in the Bible– people who choose not to marry. They are also strange people isnt it?

    3. Blessings with due respect…ziri ngati mmene anthu amabadwa ndi chilema…..all the people who are born with degrees of disability; crippled, blind, death were created by same GOD who created those that are whole! The way we clothe naked mad persons its the way these should be treated! Mmene sitingamulore wamisala kumapha anzake coz ndi wamisala its the same way we should help people who have same inclination to same sex that they should live a normal way not promoting such behaviour. Aliponso amene during sex action with their wives does fellatio and cuningulus (sucking each other private parts) which I just think kut homosexual does the same. Go deep on eunuchs in the Bible– people who choose not to marry. They are also strange people isnt it?

  18. YOU MUST BE VERY STUPID FLETCHER KAYIRA NEVER CALL YOURSELF A PASTOR ANY MORE. WE DONT NEED PEOPLE LIKE YOU IN MALAWI & DONT FORCE PEOPLE TO INSULT YOU.

  19. Last days warning izi mbusa akuikira ndemanga anene verse lake baibulo tilione ,Ndipo masiku akudza kwake ayandikira konzeka kale linseli za u gay zinali kuti?

  20. I knew it. That mother fucker was only on air for money. he is not a fuckin man of God. All gays they luck love. How wud one love fellow man up to intimacy? That’s not love its insanity.

  21. Kodi Kaiya ameneyu ngwampingo wanji?Pitala wamugula kuti azinena zimenezi nzina la Devil eati?chabwino takumvani abusa…nde mukathese banja lanulo ndikukufunani ndikukwatireni muzikataya nkhoko payard mwamva..?

  22. let God be God dont do his judging for him …if every sin is equal then gays are no different than liars and adulterers which am sure most of us at one point have been but that doesn’t mean we should be sent to jail. iam not saying its right am just saying no man should imprison another for their short comings

  23. Abusa ophunzitsa zosangalasa munthu osat Mulungu…..adagwa amenewo pa maso pa Mulungu olenga kumwamba ndi dziko lapansi… osawamvera… Dyera ndi dziko lapansi….abusaaaa, mwaiwala nkhan yaSodomu nd Gomola….?

    1. Za sodomu ndi gomora zinanditopetsa. Kambani za lero. Maiko ololeza mchitidwe umenewu alipo ambiri. Tiuzeni limene linaona zonga izi ndi liti? Ine ndikuona ngati Malawi akuona armageddon chifukwa chosowa chilungamo pa nkhani monga imeneyi

  24. Eish Kukalamba ndiubongo omwetu uku waliyiwala bible nthawi yomweyi.Abusa Werenganiko Romans Chapter1 Muyambile Verse27,ndiye Mutiuzenso.Paja Kumudzi Nkuti apastor?kkkkk mufunse Ken Nsonda Irespect Him Though he consetract on politics but he doesn’t forget za m’bible.

  25. Your are the first Pastor since l was born to say that,maybe you are also one of them because none supports something without being part of it,you dont deserve to be a Pastor in Malawi

  26. mmmmmm mabodzatu awa…. i watched the said program on TV sananene kuti homosexuality is not a sin ayi….. He said to be attracted to afellow man as it can be to opposite sex is not a sin but to do the thing is a sin… thats what he said… mabodzawo

  27. kuulutsa mau pa radio sikuti ndi m’busa akagwele adya za ma gay zambiri kufuna kusocheletsa anthu zidalinso chomwechi nthawi ya Lot sodomu ngati adawonongedwa mchitidwe wake omwewu

  28. kuulutsa mau pa radio sikuti ndi m’busa akagwele adya za ma gay zambiri kufuna kusocheletsa anthu zidalinso chomwechi nthawi ya Lot sodomu ngati adawonongedwa mchitidwe wake omwewu

  29. This guy is trying to confuse as with his bad ideas. What he should know is that there will never be reward to those who turn their against JAH. He is not aware that homosexual is satanic ideas, it’s quite evident that he is also a GAY although he has been married to a woman.He thought that AZUNGU will give him a lot of cash for saying this foolish statement. Their thinking capability is below that of a DOG. SHAME ON U BAD PASTOR.

  30. Kodi Mbuye wanga Mwagona??? Nanga Why mukumpatsa satana Danga mpaka chonchi? Plz Do something Papa we are crying to you ndipo tagwada pamapazi anu Papa.

  31. Pali mipingo ina ndiya anthu ina ndiya Mulungu.bcoz Mulungu anatilenga ndicholinga choti tizichita chifunilo cha Mulungu.ndiye ma pastor mukuwanenawa ndiwoti anayambisa mipingo yawo osati ya Mulungu.Pano dziko ladzadza ndi usatana chifukwa cha ma pastor onyenga ngati amenewo.tsoka mtunda ndi nyanja poti oipayo watsikila konko.YESU anapelekedwa chifukwa cha ndalama.Aneneli ose kunalibe mneneli ophuzila koma amangozozedwa ndi mphavu ya namalenga.pamene Aneneli alero akuchita kupitalila ku sukulu ngakhale alibe umulungu mutima mwawo.one of them iz Mr kayiya

  32. Its very sad and worrysome that the highly acquired honour this so called pastor enjoyed had gone this easy way for we had now know his master,LEVITIKO amanena momveka bwino mosafunikira wina kulalikira kuti ichi Mulungu anyansidwa nacho…,who are we to justify this sin!
    AS REVALATION 2:4-5 SAYS THAT “koma ndili nako kotsutsana ndi iwe,kuti unataya chikondi chako choyamba. Potero kumbukira kumene wagwerako nulape nuchite ntchito zoyamba koma ngati sutero ndidzaza kwaiwe ndipo ndidzatunsa choikapo nyali chako kuchichotsa pamalo pache ngati sulapa”. Pastor kaiya lapani

  33. Pastor amene kuyankhula zopusa choncho ine mpaka nditatulukamo church kumapita kuthu ndithu ndipo bola kukapemphela ndekha osati osati kukhala pa mpando church kumamvela ma pastor ngati awa

  34. Itink Fletcher some how goes crazy .He is so stupid .kukanakhala bwanji makola ake akanakwatiwa ndi mwamuna mzake kapena mkazi mzake akanabadwa iyeyo . He iz a real fool

  35. Pastor Uyu Ndi M’dzukulu Wa Satana. Bt Why Dis 2 U Malawi.Ndatsimikiza Kt Umphawi Umacititsa Ucitsiru.Akhala Pang’ono Atiwuuza Kt Ngat Mukufuna Chinthandizo Muziyenda Maliseche.Dziko Langa Malawi Usayiwale Mulungu.Boma And Other NGOs Awavumatitsa Obama M’kamwa Ndicifukwa Chake Akumazembazemba Pa Nkhaniyi.We Say Malawi Ndi Dziko Lowopa Mulungu Nanga Uku Ndikuwopa Mulungu Kapena Satana?Dn’t Late Our Poverty 2 Do Us Apart With Our God.

  36. Sionse ot Ambuye Ambuyd azalowe mufumu wakumwamba.Apa nde zaoneselatu kut dis greedy pastor ‘ll yield notin @ de end.He ‘ll ganishin teeth in de hell.Maonekedwe auMulungu koma mphamvu yake adaikana.

  37. maluz a muswa ameneu,what a sham to 2 u, u so called a paster….PASTER OF A DEVIL!!! paster ochititsa manyaz iwe.chonsecho2 ali ndiana komanso mkaz kunyumba

  38. Nchikhala ndi truck makamaka road master,pastor wa chambayu nakammangilira kumbuyo mkumamkwakwaza,kapena kumuyendesa grinder pamimba.UZAFA NGAT GALU pastor iweeee

  39. أنا حصلت على 3000 طلب صداقة
    احصل انت ايضا على آلاف طلبات الصداقة من بنات و اولاد
    ومن جميع الدول العربية والاجنبية
    الشرح من هنا ==> http://www.talabat.ga

  40. Mulungu analanga mzinda wa Sodomu ndi Gomola chifukwa chani abusa a KAIYA? l wonder if at all this pastor went to bible school. Or he was just appointed by his fellow church members after being the oldest member in the congregation. Open up people this is the clear testimony that we are in the last days. Lord have mercy on us.

  41. If it’s reported by #Malawi24, am 100% sure its twisted. These guys are a disgrace to the media fraternity. They have this tendency of fabricating and twisting stories to gain attention, they are total SHAME!!!

  42. Indeed the devil is showing himself throuhg his chosen ones who once claimed to be gospel gurus but now the devil is even controlling them, I used to admire yu. Mr kayiya but now yu have just shown malawians that yu sold your soul to the devil. don’t let money make yu lose your diginity and morals

  43. Azibusa enawa Eeee , kma ndi wa mpingo wanji ameneyi satanic chani ? Ine zopusa ayi ndngadye deal mwa mamuna nzanga kkkk imeneyi mbuzi ndithu eshhhh so sad

  44. what a public shame dear pastor! kani ubusa wanu unachokera kwa mdierekezi? ha aaa! agalatiya opusa! kwatirani mwamuna mnzanu lero musudzule mkazi wanu uja chifukwa mwaledzera, mwachita chigololo ndi mwamuna inu. sindidzamvereranso programme yanu ngakhale ulaliki wanu wonyengawo! abusa ozungulira mutu ndi umphawi komanso adyera ngati mvimvi!

  45. Abusa ana anu akuwerenga zimenezi? nanga akuti bwanji pa zimenezi? mwadalitsa angati amuna okhaokha chiyambireni ntchito? izizi anakuuzani abambo wanu, ambuye wanu kapena? ndikulangizeni ine mwanamwana ine? sioyenera kukhala apongozi anga inu? shutup musadzaneneso zimenezo.

  46. Ameneyu ytisatayenthawi ndikumutchula kut poster cifukwa sakukwanila ngakhale pa ubusa waziweto ziwandaso zilibwino cifukwa ziwanda zimamudziwa mlungu koma uyu ndiosocheletsa nkhosa a ambuye evil suppoters ana anjoka

  47. Eeesh….. “4 God So Lovd De World & He Gav Hs Only Bgoten Son That Who Eva Blv In Hm Shall Not Perish Bt Av Evalastng Lyf” God 4gv Dem, 4 Dey Not Know Wat They Do. These R Last Dayz Indid, Mpaka A Pastor.

  48. I cannot buy what the so called pastor said, look it is absolutely not true for a person to born attracted to a woman, I can only agree if that person starts to be attracted to a women as he grows. If this happens it means that the person is possessed with evil spirit and he requires total deliverance. God did not create a man to be attracted to his fellow, then god purpose of woman is null and void, I don’t think if god can contradict himself

  49. The pastor says the truth that Homosexuality isn’t a sin but rather a small thing that hen puts together with other devious thing becomes a sin. A sin is combination of many devious thing. However the pastor has justify his status as a man of Gd if he really is!!!

  50. wowww i nvr thot malawian pastors ar lyk ths fr real tht devil z at wrk bt gud pipo out thy let nt ths pipo decive us coz tht son of man z on th way cumin so b careful

  51. If is that so y u didn’t divorce ur wife then ukwatire brother wako 4sek with ur rubbish…………. U deserve to die wava I we chi China pastor including u america

  52. Thats Why Mulungu Watikwiyira Osatipatsa Mvula,bt What Has Come Over You Pastor,ndikakukhulupiliran Kom Aaa Manyaka Enieni Bt You Need To Know That Musocheletsa Ambir, Mulungu Atikhululukire As A National

  53. An2 ngat inu ndiofunika Mulunguo paekha kuzakuchoxan zwanda zanuzo… Cz t xmx ndzazkulu hvy…!! Eh. Mundpaxe verse mu bible. Ymwe inalembedwa nyax zmezo… En muambe mwakwatra anada man lyk u en u guys shud bear chldrn or els u wl danc d muzk pastor. GOD shud purnish uuuu lier.

  54. If dats the case GOD would av never created EVE…..stop cheatin ppo….tiuzen kapena ndi verse it yomwe imaloleza mathanyula!!!zixilu,..kukomedwa ndi ndalama….

  55. ngati tchimo ali kugonana ndi nkazi popanda ukwati nde inu mwati. sodomo its not a sin koma langizo kwa a khirisitu nde mwati muzitsatilabe chi khirisitu coz your pastor and even pope betrayed you so think deeply

  56. Malawi was there long time ago why today we should move on with rubbish things, it’s not everybody is rich, it’s not every country is rich we must stay as we used to stay , Malawi will never be like America, Malawi wil never reach where SouthAfrica has reached accept that our country is poor with their poor leaders n life wil move on, I don’t support the idea homesexual is a sin, even don’t they respect that, even cows they do respect that ,Dog male has got feelings in a female dog to respect what God has created each n everything with their purpose, Ass is for kubibila not for useless things why can’t that pastor go to church with bra or skirt?

  57. Ndithu Akaiya Zavuta Apa Mwawalodza Kut Asinthe Zonena Et?Munthu Wa Mulungu Wapanga Bwanji?Wapenga Ndi Bible Et? Tisiyire Bible Ana Tione Kut Tipange Nalo Bwanji,mot Akaiya Munakwatilana Ndimwamuna Mnzanu?Zotitengela Kokatiyesa Ife Ayi,Takana Ndimwaz Wa Yesu Fire! Fire! Fire!

  58. Bola Chauta Akadalenga Galu Kusiyana Ndi Ndichitselekwechi Tisamale Abale Anga Asatisocheletse Ano Ndi Omalizadi Masiku Anthu Ngati Awa Ndiwo Akubweletsela Ng’amba Namalenga Akukwiya Nao Kwambili.

  59. owelenga bible akudziwa choonadi,ndipo adzaima pa choonadi mothandizidwa ndi mzimu oyera.oipa asiyeni akhale chipiileni okhulupilira Mulungu adzaima njii osagwedezeka

  60. He is after money not truth.The truth sets someone free, although he said that but deep down his heart he knows exactry what is written in the Bible

  61. ok easy kma ngat sitchimo let us leave them 4 twelve mounths ngat mwana sabadwa achimwene abusa nyamukani kumalawi kuno chifukwa there is a fungo la imfa and ndinu anthu amene mulungu wakwiya nanu as a result rain mayanzi and abusa mukapitiriza DEATH IS WAIT 4 U & after that HELL dat God love u repent because hell lives and it is not full malo alimo ambiri and kumwamba maloso aliko GOD love u

  62. i never expected a veteran pastor like fletcher to come out openly and say this,may be he has his own type of bible which does not have the story of sodom and gommorrah,ifeel sorry for him

  63. he is one of them and indeed if he is a real pastor i wonder which and what bible he uses? The scriptures are already there Mr so called Pastor,unless you are misleading us!

  64. Malemba Adaneneratu Kut “kudzakhala Aneneri Onyenga Omwe Azidzaitanikira Dzina Langa Pomwe Sali Bwaine.” Pastor Amasanduka Njoka . Atiwuze Kut Ndi Scripture Iti Palimawu Amene Walankhulawo Kapena Walemba Lake Bible? Hahahahaha!! Achitsiru Abusa Pamodz Nd Congregation Yake!!

  65. Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!

  66. Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!

  67. Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!

  68. Sindikudabwa nazo bible linakamba awadi ndi masiku otsiliza tiyeni tipatuke chabe imeneyo ndi njira ya oyipa wuja ngakhale akutinyengelera ndi dziko lapansi ameneyo ndi one of aneneli aja onyenga!

  69. Iwe flesher pamodzi ndi a homosexualitywo mukafune kwina kokhala nt our beloved malawi,ndipo uyambe ndiwe kukwatira mwamuna nzako

  70. Iwe flesher pamodzi ndi a homosexualitywo mukafune kwina kokhala nt our beloved malawi,ndipo uyambe ndiwe kukwatira mwamuna nzako

  71. Iweyo ukutiwe ndi postor kuti ubadwe bambo ako amagonana ndimamuna?paja ndiwe wpchipembezo chanji ukuyenera kulipira dipo kwa mulungu iwe ufe ndihtuuuuuuuuuuuuuuu!

  72. Iweyo ukutiwe ndi postor kuti ubadwe bambo ako amagonana ndimamuna?paja ndiwe wpchipembezo chanji ukuyenera kulipira dipo kwa mulungu iwe ufe ndihtuuuuuuuuuuuuuuu!

  73. satanic pastor ameneyo uchitsilu zoona mwamuna nzako kumukwatira inu zakuvutani kuti mulemere?musatiwonongere dziko lathu ndinu ma folena eti?musatichimwitse, kuti ukhaleko chifukwa chayani kape; unachokera kunyani kapena?

  74. satanic pastor ameneyo uchitsilu zoona mwamuna nzako kumukwatira inu zakuvutani kuti mulemere?musatiwonongere dziko lathu ndinu ma folena eti?musatichimwitse, kuti ukhaleko chifukwa chayani kape; unachokera kunyani kapena?

  75. guyz musakwiye naye paster kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake

  76. guyz musakwiye naye paster kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake

  77. guyz musakwiye naye pastor kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake

  78. guyz musakwiye naye pastor kaiya izi zinalembedwa kale mu bukhu loyera kuti adzabwera oterewa mmasiku otsiliza koma tsoka kwa iwe kaiya ngati umkagwira ntchito ya mulungu kalero yakwana lero nthawi yanu kuti satana akugwilitseni ntchito yake

  79. VERY CRITICAL ALERT!!! Hello beloved saints, I’m sure you know that New international version(NIV) was published by Zondervan but is now OWNED by Harper Collins, who also publishes the Satanic Bible and The Joy of Gay Sex. The NIV and English Standard Version (ESV) has now removed 64,575 words from the Bible including Jehovah, Calvary, Holy Ghost and omnipotent to name but a few… The NIV and ESV has also now removed 45 complete verses. Most of us have the Bible on our devices and phones especially OLIVE TREE BIBLE STUDY APP. Try and find these scriptures in NIV and ESV on your computer, phone or device right now if you are in doubt: Matthew 17:21, 18:11, 23:14; Mark 7:16, 9:44, 9:46; Luke 17:36, 23:17; John 5:4; Acts 8:37 …you will not believe your eyes. Refuse to be blinded by Satan, and do not act like you just don’t care. Let’s not forget what the Lord Jesus said in John 10:10 (King James Version) THE SOLUTION If you must use the NIV and ESV, BUY and KEEP AN EARLIER VERSION OF the BIBLE. A Hard Copy cannot be updated. All these changes occur when they ask you to update the app. On your phone or laptop etc. Buy and KEEP EARLIER VERSIONS AND STORE THEM. There is a crusade geared towards altering the Bible as we know it; NIV, ESV and many more versions are affected. Rapture will take place any time from now. Everything hindering the rapture has been removed. Gospel has been preached almost everywhere, all the prophecies has been fulfilled. The devil is working very hard to occupy Christians with the things of this world so that the day will catch them unaware. Please be prepared,there is no more time, Use the advantage of sms,WhatsApp, BBM, Facebook, twitter etc to send this message to at least 10 people. Do not ignore. This is also a source of evangelism, souls are dying. God bless you! Let’s Pray Hard: 6 6 6 The Mark Of The Beast Prophesy Finally Fulfilled… Written By: Jonathan Annobil. The US supreme Court has rule that states must allow same-sex marriage (SODOMY) which was the same reason God destroyed Sodom and Gomorrah. the US Senate has also passed the Obama Health Bill into law. The implementation has already commence. The bill would require all Americans to be implanted with a Radio Frequency Identification (RFID) chip in order to access medical care. The device will be implemented on the forehead or on the arm. This is to fulfill the prophesy in the Book of Revelation 13:15-18 concerning the MARK OF THE BEAST. Are you still doubting the END TIME? Do u know that the special car which was made for Obama is known as the BEAST? Get READY. The rapture is near! Revelations 13 is being played out right before us. Many are still unaware. Why is the chip being implanted exactly where the Bible says it would be. Why on the hand and forehead. Why not anywhere else?2. Why is it being connected to your bank account? Remember the Bible says you wont be able to buy or sell without the mark 6 6 6. And guess what! The chip is connected to your financial details. What breaks my heart the most is that many people in the Church will not make it if Jesus comes now? Many are unaware that the ends is near. Don’t tell me that its advancement in technology or development. If any area of your life is not in sync with God’s word repent and be converted. If you miss heaven you can never miss hell…think about it. Hell is not a pretty place, the worst part is that it is for eternity… He who has ears, let him hear what the Spirit says to the church. Please rather than post and forward senseless messages. Send to everyone you know. Do the work of an evangelist. PLEASE SHARE THIS MESSAGE WITH ALL YOUR CONTACTS. Have you ever wondered what should have happened if we treat the Holy Bible the way we treat our mobile phone? And we really can’t live without it. Only 7% percent will re-send this message. Don’t be of the 93% who will not share the message. Share and send now. May Almighty God bless you

  80. VERY CRITICAL ALERT!!! Hello beloved saints, I’m sure you know that New international version(NIV) was published by Zondervan but is now OWNED by Harper Collins, who also publishes the Satanic Bible and The Joy of Gay Sex. The NIV and English Standard Version (ESV) has now removed 64,575 words from the Bible including Jehovah, Calvary, Holy Ghost and omnipotent to name but a few… The NIV and ESV has also now removed 45 complete verses. Most of us have the Bible on our devices and phones especially OLIVE TREE BIBLE STUDY APP. Try and find these scriptures in NIV and ESV on your computer, phone or device right now if you are in doubt: Matthew 17:21, 18:11, 23:14; Mark 7:16, 9:44, 9:46; Luke 17:36, 23:17; John 5:4; Acts 8:37 …you will not believe your eyes. Refuse to be blinded by Satan, and do not act like you just don’t care. Let’s not forget what the Lord Jesus said in John 10:10 (King James Version) THE SOLUTION If you must use the NIV and ESV, BUY and KEEP AN EARLIER VERSION OF the BIBLE. A Hard Copy cannot be updated. All these changes occur when they ask you to update the app. On your phone or laptop etc. Buy and KEEP EARLIER VERSIONS AND STORE THEM. There is a crusade geared towards altering the Bible as we know it; NIV, ESV and many more versions are affected. Rapture will take place any time from now. Everything hindering the rapture has been removed. Gospel has been preached almost everywhere, all the prophecies has been fulfilled. The devil is working very hard to occupy Christians with the things of this world so that the day will catch them unaware. Please be prepared,there is no more time, Use the advantage of sms,WhatsApp, BBM, Facebook, twitter etc to send this message to at least 10 people. Do not ignore. This is also a source of evangelism, souls are dying. God bless you! Let’s Pray Hard: 6 6 6 The Mark Of The Beast Prophesy Finally Fulfilled… Written By: Jonathan Annobil. The US supreme Court has rule that states must allow same-sex marriage (SODOMY) which was the same reason God destroyed Sodom and Gomorrah. the US Senate has also passed the Obama Health Bill into law. The implementation has already commence. The bill would require all Americans to be implanted with a Radio Frequency Identification (RFID) chip in order to access medical care. The device will be implemented on the forehead or on the arm. This is to fulfill the prophesy in the Book of Revelation 13:15-18 concerning the MARK OF THE BEAST. Are you still doubting the END TIME? Do u know that the special car which was made for Obama is known as the BEAST? Get READY. The rapture is near! Revelations 13 is being played out right before us. Many are still unaware. Why is the chip being implanted exactly where the Bible says it would be. Why on the hand and forehead. Why not anywhere else?2. Why is it being connected to your bank account? Remember the Bible says you wont be able to buy or sell without the mark 6 6 6. And guess what! The chip is connected to your financial details. What breaks my heart the most is that many people in the Church will not make it if Jesus comes now? Many are unaware that the ends is near. Don’t tell me that its advancement in technology or development. If any area of your life is not in sync with God’s word repent and be converted. If you miss heaven you can never miss hell…think about it. Hell is not a pretty place, the worst part is that it is for eternity… He who has ears, let him hear what the Spirit says to the church. Please rather than post and forward senseless messages. Send to everyone you know. Do the work of an evangelist. PLEASE SHARE THIS MESSAGE WITH ALL YOUR CONTACTS. Have you ever wondered what should have happened if we treat the Holy Bible the way we treat our mobile phone? And we really can’t live without it. Only 7% percent will re-send this message. Don’t be of the 93% who will not share the message. Share and send now. May Almighty God bless you

  81. Sopo Ina Imangokula Ili Yopanda Thovu,babawa Akamati Munali Ndiine M’bale Wanu Mwa Ambuye…Ndinkangoti Akunena Yesu Osadziwa Mpsilu Iyeyo Anabadwa Kwa Bambo,akazake Ngamuna,mwanache Atapititsa Mandevu Mnzake Nkumati Baba Ndapata Omanga Naye Banja Amulandila???Anthu Ambiri Akamakalamba Amalapa Ameneyi Bwanji?

  82. Sopo Ina Imangokula Ili Yopanda Thovu,babawa Akamati Munali Ndiine M’bale Wanu Mwa Ambuye…Ndinkangoti Akunena Yesu Osadziwa Mpsilu Iyeyo Anabadwa Kwa Bambo,akazake Ngamuna,mwanache Atapititsa Mandevu Mnzake Nkumati Baba Ndapata Omanga Naye Banja Amulandila???Anthu Ambiri Akamakalamba Amalapa Ameneyi Bwanji?

  83. Koma abale dzikoli lathadi zidzindikilo zakwanilitsidwadi mpaka afletcher kaiya koma yehova atipangile chifundo enafe kuti tisayesedwe

  84. Koma abale dzikoli lathadi zidzindikilo zakwanilitsidwadi mpaka afletcher kaiya koma yehova atipangile chifundo enafe kuti tisayesedwe

  85. Pastor Kaira if u says being gay z nt a sin then y dnt u marrie ur brother???? Maganizo opusa atsogoleri anyasi.

  86. huh! alas! do these pastors,prophets read the holy bible or may be they jst greedy for money? Why run away from the truth that mathanyula is a sin? I think these pple are insane?

  87. This is really the right time to turn to Jesus! How can a man claiming to be a pastor Say something as silly as it is on the media! I aint judgin’ but every man with ths kind of life shal be cast in deeper pits of hell!

  88. zidzakhala chonchoso nthawi ya 666 adzizatipeleka kwa adani ndiomwe tikuti azibusa pano chonde tichenjele masiku ano tisakhulupilile munthu

  89. Romans 1 vs 20 down. what does it say? Fletcher, its greed that has taken over the place where there once lived the truth of God. a shadow of your former glory its what has remained. am a shamed.

  90. Mayineeee! Koma ndalama abale, maluzi siabwino mwamva, abusa padzana paja m’mene munkalumphira ndi uthenga lero munganene zopusazi? Mwanditengamo bwanji, musandiyandikire muona zakuda hmmm! Shatapu!!!

  91. siwonse oti Amen amen atakalowe ufumu wakumwamba musaiwale amene adamupereka analinso wophuzira wake naye Satan Ali nawo ake atumiki ngati PASTER FLETCHER KAIYA

  92. siwonse oti Amen amen atakalowe ufumu wakumwamba musaiwale amene adamupereka analinso wophuzira wake naye Satan Ali nawo ake atumiki n

  93. I hope you did not listen to what the Paster said. Why are you dirtening the image of the paster? Please, learn to listen to what other people say.

  94. Abale ndi alongo ine sim’busa koma mopanda kuonjezera kapena kuchosa baiblo pa Levitiko 18:22 pali mau awa “Usamagonana ndi mwamuna,monga amagonana ndi mkazi; chonyasa ichi”ndietu mulungu akati usachite iwe nkuchita cholesedwacho chimenecho nchomwe chimatchulidwa tchimo(sin)

  95. Does kaiya speak for himself or God?The issue of homosexuality doesnt need interpretation,it is clearly stated in the Bible and what God did to homosexuals in the cities of Sodom and Gomora.I begin to think that pastor Kaiya is trading in the churh,and these were the type of people that Jesus kicked out from the house of God

  96. The Bible says “we must respect our pastor’s but this time mmmmmmm i must say!!!!!!!!! u be very very stupid…Ps kaiya…

  97. Ngati si tchimo Mulungu anatentha Sodomu ndi Gomora mphongo za mmenemo zitakakamira kuti zichite zadama ndi alendo omwe anafika kunyumba kwa Loti chifukwa chani????????????Kapena Mulungu anadana ndi khalidwe limeneli si emwe inu mumamulakira ngati m’busa????????Pologalamu yanu ya mbc ija sindizamveraso.Mau a Mulungu akuti mamuma asagone ndi mamuna nzake umo achitira ndi mkazi ndie inu mukuti chani????????Mukubesa chipulumuso ofikafika???????

  98. Chinthu chanzeru pamoyo wachikhristu ndi kulumikizana/ kumudziwa Mulungu wa Bible lathu osati kuliphunzira Bible kuti upeze Degree in Theology usadamdziwe Mulungu wa Bible ndingozi. Utadziwa chifuniro cha Yehova pa iwe suzasowa chochita mnthawi yotere ikafika. Chofunika ndikukakamira korona wako wamoyo,wina asakulande.Munthu ndi wabwino nthawi zina Koma Ambuye ndiwabwino nthawi zonse.

  99. Akufuna banzi Kayiya. No doubt about that. Rember that late Professor, Bingu wa Mutharika once said, ” Malawi is not poor but the people of Malawi are poor”. Kkkkkmkkkk

  100. Indeed ppo perish because of lack of knowledge. Most of you commenting here didnt even watch the said programme where the pastor spoke those words which have been misinterpreted. The fake journalist who has written this article is a shame to journalism because I watched the programme & what has been reported here is a very serious misinterpretation of what the pastor said. This article smarks of mediocre journalism & petty sensationalism. The pastor was emphasizing love & acceptance towards gay ppo. He noted that gayism is a SIN like any other & that those in this ‘cob web’ must be shown the ‘right way’ with love. He noted that condemnation is not the way to go for we dont really know if some of them are born that way or not. A Malawi inu… hmmm

  101. Is nt a sin ku church kwao komko ndi ma bible a kwao timipingo tomwe zolinga zake ndi zadzikolapasi tikuoneka tokha ndi ta atsogoreli ta kwao satanayo sakumuna watseka mmaso.

  102. Is nt a sin ku church kwao komko ndi ma bible a kwao timipingo tomwe zolinga zake ndi zadzikolapasi tikuoneka tokha ndi ta atsogoreli ta kwao satanayo sakumuna watseka mmaso.

  103. Uyu pasito uyu kungomva kuti Dr H. Kamuzu Banda wadzuka Ku manda akufuna Ku lamulanso dziko atha kuthawa Ku Malawi kukakhala self exile.kkkkkkk pano a china John Tempo akungo seka kuti ikanakhala nthawi ya chinyamata chathu tikanango mugwira nkhwiko.

  104. Uyu pasito uyu kungomva kuti Dr H. Kamuzu Banda wadzuka Ku manda akufuna Ku lamulanso dziko atha kuthawa Ku Malawi kukakhala self exile.kkkkkkk pano a china John Tempo akungo seka kuti ikanakhala nthawi ya chinyamata chathu tikanango mugwira nkhwiko.

  105. Shame On You,a SataNic Pastor. For So Long,you Have Had A Good Christian History.But Money Has Robed You Of That.(a Real Galathian).So It Means You Are Telling Us That You Are Gay? Are You A Real Minister Of God, No,you Are’nt.Your Pastorship Is Fake,it Is Branded,babylon.

  106. Shame On You,a SataNic Pastor. For So Long,you Have Had A Good Christian History.But Money Has Robed You Of That.(a Real Galathian).So It Means You Are Telling Us That You Are Gay? Are You A Real Minister Of God, No,you Are’nt.Your Pastorship Is Fake,it Is Branded,babylon.

  107. In de last dys de snake wil try 2 deciv even de selectd.Kod amene mwapanga lyk ndiye kut zomwe wanena munthuyu mwasangalala nazo?

  108. In de last dys de snake wil try 2 deciv even de selectd.Kod amene mwapanga lyk ndiye kut zomwe wanena munthuyu mwasangalala nazo?

  109. Sindinamvere debate imenei zonse ndamvera pomwepa,koma pakumva kwanga ndaona kut anthu sanamvetsetse chomwe a kaiya amalankhula,majority ikut wanena kut sitchimo,ena akut sanatero,zomwe zikutanthauza kut sanalankhule zomveka,kut anthu atole mfundo imodz yomveka bwino.iwowo ngat tsogoleri,amene amakambirana nkhani yomwe yavuta yokhudza fuko la anthu,sanayenere kupereka mfundo ziwiri zosiyana pankhani ngat imenei, akananena chimodzi kut nditchimo,koma pakufunika kut tiwapemphelere anzathu amene amabadwa ndikhalidwe limeneli kut lisapitilire,i think dis cud hav help,anthuso akamvetsetsa,coz mmene ananeneramo ndikanakhala lesbian ndikanaona ngat sivuto langa ndikuyenera kumapitiza.nde akuyenera kubweraso poyera atiuze mbali imene ali,ayankhe chimodzi tonse titenge chimenecho,kutiso mbiri yawo iyere,akapanda kutero tiona ngat ali mbali la zolengedwa zachilendozo,coz zinyama sizingawaloleso kut ali m’gulu lawo coz sizipanga zimenezo

  110. Sindinamvere debate imenei zonse ndamvera pomwepa,koma pakumva kwanga ndaona kut anthu sanamvetsetse chomwe a kaiya amalankhula,majority ikut wanena kut sitchimo,ena akut sanatero,zomwe zikutanthauza kut sanalankhule zomveka,kut anthu atole mfundo imodz yomveka bwino.iwowo ngat tsogoleri,amene amakambirana nkhani yomwe yavuta yokhudza fuko la anthu,sanayenere kupereka mfundo ziwiri zosiyana pankhani ngat imenei, akananena chimodzi kut nditchimo,koma pakufunika kut tiwapemphelere anzathu amene amabadwa ndikhalidwe limeneli kut lisapitilire,i think dis cud hav help,anthuso akamvetsetsa,coz mmene ananeneramo ndikanakhala lesbian ndikanaona ngat sivuto langa ndikuyenera kumapitiza.nde akuyenera kubweraso poyera atiuze mbali imene ali,ayankhe chimodzi tonse titenge chimenecho,kutiso mbiri yawo iyere,akapanda kutero tiona ngat ali mbali la zolengedwa zachilendozo,coz zinyama sizingawaloleso kut ali m’gulu lawo coz sizipanga zimenezo

  111. Adatani yeyo kukwatila mamuna nzake kuti ngati lisali tchimo moti ana alinawowo anabeleka ndimamuna nzake?, Komanso bible vesi iti ananena kuti anamulenga mwamuna kuchokela kuthiti yamamuna nzake, mapastor mukusokeletsa achrist kumangowauza m’mene angalemele dziko lapansi pano osati kuwauza zoti achite kokozekela moyo omwe ulinkudzawo koma kutiuza za nonses zokhazokha, moti inuyo bambo anu adakakwatila mamuna nzawo mudakabadwa? Mukaphunzila m’mafuna kumatubwa kapena kumakwela pachulu bwanji? Mukuputa mkhwiyo wamulungu ndichikhalidwe chanu chachilendochi!

  112. Adatani yeyo kukwatila mamuna nzake kuti ngati lisali tchimo moti ana alinawowo anabeleka ndimamuna nzake?, Komanso bible vesi iti ananena kuti anamulenga mwamuna kuchokela kuthiti yamamuna nzake, mapastor mukusokeletsa achrist kumangowauza m’mene angalemele dziko lapansi pano osati kuwauza zoti achite kokozekela moyo omwe ulinkudzawo koma kutiuza za nonses zokhazokha, moti inuyo bambo anu adakakwatila mamuna nzawo mudakabadwa? Mukaphunzila m’mafuna kumatubwa kapena kumakwela pachulu bwanji? Mukuputa mkhwiyo wamulungu ndichikhalidwe chanu chachilendochi!

  113. Pastor,to speak without fear or favour dats ur opinion and l respect dat,but if u want me all everyone to agree with u give us the chapter from de bible which says homesexualy marriage men to men woman to woman its not a sin,in the bible no verse which says we must marry men to men or woman to woman,if it was like dat GOD wasnt create Eva,but he created Adam and his wife Eva,and he said lets be fruitful tichulukane even those Abraham,Loti they got wife but child of devil oppose this why?is it because of money to confuse our brains

  114. Pastor,to speak without fear or favour dats ur opinion and l respect dat,but if u want me all everyone to agree with u give us the chapter from de bible which says homesexualy marriage men to men woman to woman its not a sin,in the bible no verse which says we must marry men to men or woman to woman,if it was like dat GOD wasnt create Eva,but he created Adam and his wife Eva,and he said lets be fruitful tichulukane even those Abraham,Loti they got wife but child of devil oppose this why?is it because of money to confuse our brains

  115. Kodi tchimo ndi homosexuality yokhayo basi? Onse sanalandire Yesu Khristu kukhala #mbuye ndi #mpulumutsi wa moyo wawo pomadzafika tsiku lachiweruzo akukanabe kwawo ndi ku gahena.

  116. Kufunafuna funding or he has failed to define what is Gay. its not just being attracted to the same sex. what kind of Pastor is this? I used to have respect for him but now I see evil in his eyes!!! hiii

  117. Ofcourse it’s too bad to just be called ‘SIN’ lets call it ‘ABOMINATION’ for such people to understand the gravity of its badness. GOD forbid!

  118. No wonder the Batist church excommunicates members are against such ssues..kkkk Leviticus 20vs 13 tells it all….wow! Laughable….

  119. mmmmmmmm ngati mupanga zinthu mudzina la mulungu koma mukusocheresa anthu muzafa mowawa ngati chibudu kkkk ok i think ubusa waowo ndi wasukulu siwamuzimu oyera

  120. Zoonadi awa ndimasiku omaliza,komanso omwe amavomereza zinthu zonyasazi ndi akhristu. kodi yesu akamaziwona zimenezi mumati zimamusangalasa?akhristu ambiri ali patsogolo kuvomereza ndi kutsogolera zinthu zoipa chonde liwerengeni baibulo mofatsa muzayenda muchiyero.ameen.

  121. Kodi iwe kayiya ndiwe chisiru eti ungamanene zopusa zimenezo ukuganiza bwanji koma iwe uri ndi mkazi wako atumiki aboza ndinu eti chamba basi

  122. IWE KAIYA NDIWE CHITSILU SURE IWE ABAMBO AKO AKADAKALA KUTI ANAKWATIRA MWAMUNA MNSAO NKUMACHNDANA KUNTUMBO UKABADWA IWE! NANGA IWEYO ULIBE ANA UNATHANI OSAKWATIRA MWAMUNA NZAKO KALE LONSE IFE AMALAWI NDIFE ANTHU OOPA MULUNGU NDIYE CHIFUKWA CHAKE TIKUKANA WAMVA IWEYO NGATI UKUFUNA NDALAMA ZOCHOKERA KWA AMERICA MMMMM! GALU IWE!! WALEPHELA WAMVA NDIWE CHITSILU NDITHU

  123. Total nonsense and hypocrisy! Its these type of pastors who mislead people. The Bible says we are born sinners and nobody chose to be born a sinner. Therefore should we all justify ourselves that we are not sinners since we never chose to be born sinners? Akawengenso Bible lawo akulu amenewa.

  124. kkkkkkkkkk azibambo kudela khawa ndiziphsyephyse zawo m’busa atalamula kt ziligwilitsidwe ntchito kkkkkkkk..the last dayz indeed

  125. A pastor polishing a sin,Indeed mr fletchar kaiya z a fake pastor, z serving satan not true living God,shuold no longer air spiritual programs on MBC ,he z a potential threat christianity dscontiinuity

  126. If nt Sin why did God destroyed Sodom & Gomorah 4 they Were Practing the same thing.Think Twice B4 U Speak,osamasewera Ndi Mulungu Wamakamu.

  127. GOD FORGIVE YOU PASTER KAYIYA, I DON’T KNOW WHAT KIND OF BIBLE YOU USE TO READ, ANYWAY, POTI YEMWE MULUNGU WAMUPOTOZA NDIKOVUTA KUTI ANTHU OLENGEDWA NDI MULUNGUYO AMUONGOLE MWINA NDIKUTHEKA APASTER MUNAPOTOZEDWA, MY QUESTION TO YOU IS WHY GOD BURNT TO ASHES SODOM AND GOMORRAH,iN CASE YOU DON’T KNOW, ITS BECOZ PEOPLE OF THESE CITIES CAME TO ASK LOT TO BRING OUT TWO VISTERS WHO CAME TO VISIT LOT WITH INTANTION OF SLEEPING WITH THEM

  128. God is punishing innocent people with no rains coming,maize field are drying up almost all over the country because of homosexuality. I wonder why some people are busy pasting this issue almost every hour instead of encouraging them to pray hard in order come closer to God’s favour so that the rains should come. To say the fact,plants started well but this time you can’t wish to visit the maize field coz it almost dried up. I’m a conseqn citizen,real Malawian but any way….

  129. Sign of spiritual bankrupt, otherwise why should a so called Pastor engage in supporting this notorious behavior? Even Satan never support same sex marriage.

  130. A Fletcher amatumikila MBC osati Mulungu ngati mmene apangila atumiki oyitanidwawa. kulalika powopa kuchotsedwa ganyu apangayo. Mr fletcher mwina apa tipemphe MULUNGU wathu akukhululukileni pakufuna kusocheletsa mbumba ya MULUNGU mmalawi muno.

  131. malawi should be careful and aware that these so called gays or residbians, are not christians at all but they are ministers and agents of the devil and they are on their mission of confusion not only in malawi but the whole world at large. theso human rights groups must know that even monkeys and dogs can not do such kind a thing, this therefore means that, these monkeys and dogs are wiser than these so called gays and resibians.

  132. Mateyu 24 vs 23 Pomwepo munthu akanena kwa inu Onani Kristu ali kuno kapena uko musambvomereze. 24 Chifukwa akristu onama adzauka, Aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikuru ndi zozizwa, Kotero kuti akanyenge anthu ngati kuti nkotheka.

    Mateyu 24 vs 11 Ndipo aneneri onama ambiri adzauka nadzasocheretsa anthu ambiri.

  133. Kkkkkkkkkkkkkkk koma akanati Kamuzu alipo haha haha ulendo wa Bambo Tempo bwana Chakwamba kungoti akulu akulu amenewa mphamvu zao zatha.bwenzi mutakaponda Ku thambani paka mtengo kaja.kapena Chaku Nsanjeko Ku penu.olonso ka life sentence kamene.kaya.

  134. I think Kaiya has lost human sense,he needs special prayer because everyone knows Bible and Quran ,mkulukulu iwe ungamathanyule? tell me which verse yomwe imafotokoza za zomwe ukunenazo? umphawi tangoyamba kuyenda mwa mwenye uzipempha uzinamizira umasikini

  135. i dont see anything wiser kumakamba izizi pamene tose tikudziwa kuti ndi ntchimo ,,anati chifukwa chadama khala nayeni wanu mmodzi sanati mamuna nzako kapena mkaz nzako ayi,,,koma anthu amaliseche osiyana ankhalire limodzi why? kukwatana kutheka ndipo zikhala zokoma.nde iwe kukhala mbusa doesnt matter bible ndili nalo

  136. Which verse in Romans supports your claim? Show us. Don’t force the Bible to speak what we want.

  137. kaiya and chakwela ndimazibusa okonda kobidi,,,,,,, this guys mmmmmmmmm i dnt know; they claim to be pastors BUT……………… Wina amalizitse

  138. osayelekeza mkomwe kuganizirapo kut nduzabwn ungadzafe imfa yowawa kafusen Robert chiwamba kungoyelekeza chabe wapangA b careful uzakukuta mani

  139. Kaiya truly u r misleading the nation,where in de Bible was God pleased with homosexuals.Lets put money aside and tell the truth please men of God.

  140. One thing I like about islamic countries is that this issue of homosexuality is that people can not even waste their time debating about this issue because if found the punishment is death.

  141. Ubwinowache ndioti,zonse zinalembedwa kale kuti kuzabwela aneneli onyenga,azachotsa ziwanda ndi kuudza mapiri kuti achoke ndikukakhgala malo ena mdzina langa koma ali onyenga.

  142. Ubwinowache ndioti,zonse zinalembedwa kale kuti kuzabwela aneneli onyenga,azachotsa ziwanda ndi kuudza mapiri kuti achoke ndikukakhgala malo ena mdzina langa koma ali onyenga.

  143. That one is not a pastor for Almighty God. He is for Satan and he mustn’t make people stupid in the name of God.

  144. Kkk mukungopusisa anthu cholinga mukapsele limodz, ndkanakonda de tym he wz sayn dat akanaika verse nafe tione. Iwe pastor kukanakhala zmenez bwez iwe uliko? Kufufuzanso mwina uli ndmkaz and mungulimbikitsa anzanu kut azkwatilana okha okha iyaaa mxiew. Nonse amene mukuvomeleza ambuye akukanthen ndthu.

  145. Koma Yesu akanati alipobe Ku thupi bwenzi atakukokani makutu azibusa inu.mukuzitenga kuti izi?Tiuzeni zachipulumutso,zinazi mukamati uza tidzakuswani nao mapama muli kati molalikira old mutandiyimika mu mpingo,mpingo wake uti?

  146. faulse pastors who claim to know the word of God but r there misslead multitude, same sex marriage is satanic n devilish! he’s not pastor of Gods pple he is of Luciferian, I have for long been listening to his concocted lies on mbc radio, he’s fake!

  147. Men of God please its better to shut up on homosexuality issue than making comments that will end up denying your integrity and good reputation you have been building over many year please,please men of God

  148. Zamilandu yakubamukukanika ,chuma chaziko chikubedwa mungoyang’ana anthutizivutika ndiwumphawi,pankhani zawusiru chiwewetho.Basi kutha kwamwezi malipiro pwi,muli timagwira ntchito.

  149. Weeeeeh malawi wanga ine there is stll pple who stand n say homosexual is not a sin. Who are u Fletcher? Are u a Vice God? You come with ur new commandments

  150. kuoneka opemphera koma mphamvu Yake mlungu anayikana.and apa zaoneka kuti si onsedi akutchula ambuya,ambuye ati adzalowe ufumu wa mlungu,koma okhawo akuchita chifuniro chake.

  151. Leviticus 20:13: “If a man also lie with mankind, as he lieth with a woman, both of them have committed an abomination: they shall surely be put to death; their blood shall be upon them.”

  152. Mziweruza zinthu zimene mungathe kuweluza,pali sizanu alipo amene angathane nazo osati inu.pamenepa amene amawerenga Bible sangadabwe ndi izi ,chifukwa uku ndikukwanilisidwa kwamalemba.

  153. Munthu akakhala kuti anali wa polisi koma anachosedwa amatha kumaopsezabe anthu ena omwe sakudziwa kut anachosedwa.so may be is kaiya.but Sitingaope dzina chifukwa lilingati chovala sumtimes utha kuvula but it shows who he is.

  154. Kkkkk,tili mnyengo yosiliza,mpaka pamenepa,madalaivala aganyu ndichoncho…gwiritsani chomwe baibulo likunena,mukatengera za munthu,ndithu Malawi azatha ngati Sodomo ndi Gomorah..

  155. Chitsiru cha pastor.malawias pliz dont listen to these so called pastors,just listen to ua Bible.evn ua mother/father wil deciev u but won’t.

  156. Mateyu 24 vs 23 Pomwepo munthu akanena kwa inu Onani Kristu ali kuno kapena uko musambvomereze. 24 Chifukwa akristu onama adzauka, Aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikuru ndi zozizwa, Kotero kuti akanyenge anthu ngati kuti nkotheka.

    Mateyu 24 vs 11 Ndipo aneneri onama ambiri adzauka nadzasocheretsa anthu ambiri Adzauka.

    Mateyu 7 vs 15 Yang’anirani inu mupewe aneneri onyenga amene adza kwa inu ndi zobvala zankhosa, koma m’kati mwao ali Afisi kapena Njoka Zolusa. 16 Mudzawazindikira ndi zipatso zao.

  157. like the story of Esau&jacob,jacob sold his birthright for soup coz he was hungly,if homosexaul is aborminable b4 God,now r we going to sell the right to bcome childlen of God coz we’r poor?.

  158. after all these past years Mr Kaiya ,is this the message you hav decided to preach to the country ?are you sane ?oooooh what ashame ,Idin;t know you are one of them

  159. ma pastor ena…. mukuti bwanji pankhaniyi….. tithandize or munthandiZEni nzanuyi

  160. Pastor ameneu ndi pumbwa ayambe iyeu kukwatra mamuna nza ngat angakave kukoma akakalowesa gadaf wakeyo kumtaya seche.

  161. kodi pastor ameneyo amakhala kutko anthuni,,,,ife anthu monga amenewo tikhoza kuthana nawo pompopompo,,,asatipusisile ana amulungu,,,,adzafa imfa yowawa ameneyo,,,,,ngati kwawoko ndiwosauka en akufuna kulemela sapanga choncho

  162. Angry Malawians arguing without thinking. This is not a foreign act. Why do we have the term “mathanyula”? It’s because it was happening amongst us. While we don’t agree with the practice let’s be wise on how we are handling this. Killing people will serve no purpose. They are our friends relatives.

  163. Shame on you pastor kaiya,when I was listening your preaching at MBC ,I was thought that may be you are a wise man bt 2dy I observe that you r behind stupid gvt

  164. Tikawerenga bible ku Gennises ,timamva kuti ,mulungu adapanga Adamu muchifanizo chake,ndipo poona kuti Adamu adali oungulumwa chifukwa adaliyekha ,adamupangira mkazi ngati ,omuthetsa nkhawA zake ,bwanji mulunguyo sadamupangire mwamuna mnzake?Tiyeni tisamale masiku otsiliza aneneri onama adzayima,nanena ali uko pofuna kusokeretsa nkhosa za mulungu ,Mulungu odziwa kudalidza akudalitseni nonse amene mukutsutsana ndi pastor dev Kayiya@Amen

  165. nanga onse sanavale ma trouser chifukwa chani? mesa anati mwamuna azakhala ndi nkazi wake ngati thupi limodzi nanga uyo ndi nkazi?

  166. Ndiye uchitsiluwo umeneo amawerenga Bible lake liti iye Kayiyayo?Akufuna kusocheletsa anthu basi wakhuta ameneyu etiiiiih

  167. Sindimaembekezera kuti akaiya angayankhule zimenezi, ndakhala ndikumvera ma ulaliki ao pa radio koma mmmmm nyengo zomalizadi izi.

  168. Iyeyo anakwatila mkazi chifukwa chiyani amusiye mkazi wake atenge mphongo ijake kuti ife tisimikizetu nanga akungotelo atatenga chick koma2 Illuminat wafikapo2

  169. Munthu wamkulukulu koma kumaganiza ngati mwana eti,iyitu ndi nkhani yochititsa manyazi komaso yomvetsa chisoni kwambiri,pastoryu akudziulula, kuti iyeyu amapanganawo zamathanyulazi,eti kupepela apastor,shame on you!! UKALALIKILE KU MPINGO KWAKO NGATI ANTHU SAKAKUTHAWAMO MU CHURCH YAKOYO!!

  170. If there z no any sin live ur wife ukwatire mamuna mzako Pastor opanda zelu amakamba zimenezi pagulu kulibwino ubwelele mimba mwa amayi ako kuti ukabadweso kwa mamuna mzako ngat ndiwe wa Business usasokeletse anthu!

  171. Satanic postor ameneyo nanga ngati si mtchimo mulungu analangiranji? Sodomu ndi gomora tsoka busa amene asokeresa nkhosa za mulungu ndipo azakathidwa.

  172. W@ kind of Holy Bible do the preacher lyk this one study,did any prophet in this bible preach abt homesexualitly ,is this love that God wnt dis world 2 share in a hply lyf & bear children generation 2 generation ,descendance 2 descendance eish 2 days Man’s of God i wonder

    1. there z,a big difference in being homosexual and homesexual acts.. to my own view being homosexual its like having a disability and we Can’t curse them if they are born that way instead pray 4them so that they can not engage in homosexual acts. even God himself didn’t punish the people because they were homosexual, b@ he punished them because they were engaging in homosexual acts. disability z not inability, lets pray 4them lyk we do when praying 4people with disabilities and make them stop existing and start living Amen!

  173. Kwa onse omwe ali okhunzidwa ndi nyansi za anthu otelewa, bwanji osangowagwira ndikuwapha?? Paja kunanenedwa, “YENSE ONYAZITSA DZINA LA MULUNGU OYERA APHEDWE”. Mchitidwewu unkanapitilira kaamba kolekelera ndi kuonelera amchitidweu. Kodi alipo adzalekelera mwana wa iye mwini kuzetsa chisoni pamaso pache? Wanzeru awongola mtengo ukadali waung’ono. Tichitepo kanthu

  174. Kwa onse omwe ali okhunzidwa ndi nyansi za anthu otelewa, bwanji osangowagwira ndikuwapha?? Paja kunanenedwa, “YENSE ONYAZITSA DZINA LA MULUNGU OYERA APHEDWE”. Mchitidwewu unkanapitilira kaamba kolekelera ndi kuonelera amchitidweu. Kodi alipo adzalekelera mwana wa iye mwini kuzetsa chisoni pamaso pache? Wanzeru awongola mtengo ukadali waung’ono. Tichitepo kanthu

  175. Choka satana iwe!mneneli onyenga.maluzi akupweteka eti?bola uzingolalika m’ma bus tizikusonkhela limodzi-limodzi.mungoononga mbili ya zibusa anzanu.ndiwe m’busa wankhumba,bakha iwe.

  176. Choka satana iwe!mneneli onyenga.maluzi akupweteka eti?bola uzingolalika m’ma bus tizikusonkhela limodzi-limodzi.mungoononga mbili ya zibusa anzanu.ndiwe m’busa wankhumba,bakha iwe.

  177. Mr kaiya ma verse kuyambira chakale chipangano ndi chapano zammutuzo ai ndipo mokupephani mutule pansi nthito ya ubusa komanso pa radio serious

  178. Mr kaiya ma verse kuyambira chakale chipangano ndi chapano zammutuzo ai ndipo mokupephani mutule pansi nthito ya ubusa komanso pa radio serious

  179. Which Church is he pastoring. The Church of the Lord Jesus Christ or the church of satan. Mr Kaiya please ask God for forgiveness.Read your Bible correctly and be lead by the Holy Spirit not mens’wisdom. Homosexuality is a sin before God. Please preach to your congregation the truth of God.

  180. If this is true,then its very sympathetic,because this subject of homosexual, if even people who have nothing to do with the things of God still dont accept this so what more so called believers?supporting homosexual is ministering the devil directly or indirectly therefore write them off completely in your life such so called Pastors and pray for them because its clear that they are walking in a big darkness either by choice for material gains,identification by a certain category of people or ignorance about the word of God regardless of their tittles.

  181. If this is true,then its very sympathetic,because this subject of homosexual, if even people who have nothing to do with the things of God still dont accept this so what more so called believers?supporting homosexual is ministering the devil directly or indirectly therefore write them off completely in your life such so called Pastors and pray for them because its clear that they are walking in a big darkness either by choice for material gains,identification by a certain category of people or ignorance about the word of God regardless of their tittles.

  182. chonsecho pali iyepo anakwatira mkazi.kodi mufuna chuma chani? Mapastor a fake awa koma dziwani kuti mukuputa sodom ndi gomora

  183. chonsecho pali iyepo anakwatira mkazi.kodi mufuna chuma chani? Mapastor a fake awa koma dziwani kuti mukuputa sodom ndi gomora

  184. Its not asin in in his family& in his church but to the one who created heaven & earth its asin we fear God not kaiya.

  185. Its not asin in in his family& in his church but to the one who created heaven & earth its asin we fear God not kaiya.

  186. pastor,inuyo malo moti muthandize kupemphelela dziko lathu kuchotsa chiwanda choyambitsa mtchitidwe wa mathanyula inu mukulimbikitsa anthu kuti sitchimo?nthawi yonsei ndakhala ndikumamvela uthenga wanu mukamalalika pa radio ndipo mwakhala mukundisuntha,koma pastor,pastor mwakhumudwitsa mtundu wa malawi.

  187. pastor,inuyo malo moti muthandize kupemphelela dziko lathu kuchotsa chiwanda choyambitsa mtchitidwe wa mathanyula inu mukulimbikitsa anthu kuti sitchimo?nthawi yonsei ndakhala ndikumamvela uthenga wanu mukamalalika pa radio ndipo mwakhala mukundisuntha,koma pastor,pastor mwakhumudwitsa mtundu wa malawi.

  188. Kanixo a Kaiya ndi a Chitsilu motere eit…So sad….So Mr let me tell you that from now on wards never waste your time telling people innocent souls that you are a pastor otherwise u don’t qualify to be a man of God…..You are saying that Mathanyula sitchimo?….Ngati kukwatila akazi awiri mkolakwika so what abt kugonana ndi mwamuna mzako wa ndevu ngati iweyo…… May God plz rescue us 4m this sinfull thing done deliberatly..

  189. Kanixo a Kaiya ndi a Chitsilu motere eit…So sad….So Mr let me tell you that from now on wards never waste your time telling people innocent souls that you are a pastor otherwise u don’t qualify to be a man of God…..You are saying that Mathanyula sitchimo?….Ngati kukwatila akazi awiri mkolakwika so what abt kugonana ndi mwamuna mzako wa ndevu ngati iweyo…… May God plz rescue us 4m this sinfull thing done deliberatly..

  190. koma inu mwati ubusa winau nditani? ine koma ndigwizane Ndi Vasco kuti satanaso anaika ake azibusa, ndipo wina ndameneyu kaiyau, aaaaah moti munthu wankulu ngati amenru nkumabwelesa nkhani zopusa ngati zimenezi? mmmmmmm ayi ine ndasiya kumvela programme ija amapangisa akilu amenewai basi kufatsa nkufasa nkhani sake zimenezo? bambo kaya mmmmmm Shame on you, Mulungu akhale opusa kumulenga mwamuna ndi nkazi!? kuti azikwatilana? mukanadamupempha kaye Mulungu kuti lizikalamba thupi lokhalo nzeru zisakalambe nawo koma vuto mubadzidalila nokha osampempha Kaye Mulungu, ndi chifukwa chake kukuiwala udindo wanu apa mwaamba kuoneka mbari yomwe muri, koma konzani zolankhula zanu.

  191. koma inu mwati ubusa winau nditani? ine koma ndigwizane Ndi Vasco kuti satanaso anaika ake azibusa, ndipo wina ndameneyu kaiyau, aaaaah moti munthu wankulu ngati amenru nkumabwelesa nkhani zopusa ngati zimenezi? mmmmmmm ayi ine ndasiya kumvela programme ija amapangisa akilu amenewai basi kufatsa nkufasa nkhani sake zimenezo? bambo kaya mmmmmm Shame on you, Mulungu akhale opusa kumulenga mwamuna ndi nkazi!? kuti azikwatilana? mukanadamupempha kaye Mulungu kuti lizikalamba thupi lokhalo nzeru zisakalambe nawo koma vuto mubadzidalila nokha osampempha Kaye Mulungu, ndi chifukwa chake kukuiwala udindo wanu apa mwaamba kuoneka mbari yomwe muri, koma konzani zolankhula zanu.

  192. Bola ukanangokhala chete pankhani za usatanazi apa zangowonetseratu kuti upastor wanu mwangouvala ngati njekete nkati mwanu mulibemo upastor anyway mukuyenera kupemphereredwa inu kuti mulungu akkhululukireni

  193. Bola ukanangokhala chete pankhani za usatanazi apa zangowonetseratu kuti upastor wanu mwangouvala ngati njekete nkati mwanu mulibemo upastor anyway mukuyenera kupemphereredwa inu kuti mulungu akkhululukireni

  194. I watched the whole debate dzuro and the man of God didn’t say what Is being reported here.trust me.I wonder why journalists always want to twist things to catch peoples attention.that’s not good at all.

  195. a kayia so kumanganiza mwava makolo anu anaka nkhala mahomo bwezi mulipo inu kupanga promot zinthu zopusa bwanj ….koma ndinu a lil pastour inuyo kapena u r after money nt GOD??

  196. a kayia so kumanganiza mwava makolo anu anaka nkhala mahomo bwezi mulipo inu kupanga promot zinthu zopusa bwanj ….koma ndinu a lil pastour inuyo kapena u r after money nt GOD??

  197. Fletcher Kaiya is not the agent of Devil but he is Devil himself. Abusa onyenga Fletcher Kaiya am disappointed with you and our Living God will surely punish you devil!

  198. Fletcher Kaiya is not the agent of Devil but he is Devil himself. Abusa onyenga Fletcher Kaiya am disappointed with you and our Living God will surely punish you devil!

  199. Abale ndi alongo, tiyeni tipemphele molimbika…..bcoz, there is man of god, ndiye pali MAN of GOD…..SIONSE amati ambuye ambuye akalowe koma OKHAWO OCHITA CHIFUNIRO CHAKE

  200. Abale ndi alongo, tiyeni tipemphele molimbika…..bcoz, there is man of god, ndiye pali MAN of GOD…..SIONSE amati ambuye ambuye akalowe koma OKHAWO OCHITA CHIFUNIRO CHAKE

  201. Mbuzi ya mmbusa nthawi yothaitha kugwira chikolopa,kma anat tsoka odzanazo fletcha ali mgulu laodza nazowo coz akuvomeleza such mapractice

  202. Mbuzi ya mmbusa nthawi yothaitha kugwira chikolopa,kma anat tsoka odzanazo fletcha ali mgulu laodza nazowo coz akuvomeleza such mapractice

  203. Masiku alelo akuvesa chisoni pa maso pa Mulungu anayankula kale malemba usachosele kapena kuojezela abusa mukuojezela nayeso azakuojezelani milili yowawisa pomoyo wanu gati muchosela akuchoselani madaliso anu.mulibe manyazi kuchula dzina la Mulungu musakumudziwa musanamizile abuye.chulani yemwe mutumikila kupatula Mulungu wa Yesu wamoyo.umasulidwe!!!!!! iweyo.

  204. Masiku alelo akuvesa chisoni pa maso pa Mulungu anayankula kale malemba usachosele kapena kuojezela abusa mukuojezela nayeso azakuojezelani milili yowawisa pomoyo wanu gati muchosela akuchoselani madaliso anu.mulibe manyazi kuchula dzina la Mulungu musakumudziwa musanamizile abuye.chulani yemwe mutumikila kupatula Mulungu wa Yesu wamoyo.umasulidwe!!!!!! iweyo.

  205. pastor aren’t you glad that your dad wasn’t a gay?coz if he was a gay u wouldn’t exist.no body is born a gay,people are gays because of the choice they made,,,,what a wrong choice though……

  206. pastor aren’t you glad that your dad wasn’t a gay?coz if he was a gay u wouldn’t exist.no body is born a gay,people are gays because of the choice they made,,,,what a wrong choice though……

  207. U r a messenger of the devil mr kaiya & u need to repent for what u’ve said, olo kuti mukufuna kulemera nde money yake ikhale yamagay? pezani njira ina, shame on u

  208. U r a messenger of the devil mr kaiya & u need to repent for what u’ve said, olo kuti mukufuna kulemera nde money yake ikhale yamagay? pezani njira ina, shame on u

    1. Amen brother bt the man of God needs to b specific coz he has followers & they need two need to knw the truth coz what we say is what comes frm our heart so asamangopaza they hv to clarify the meaning of what they say

  209. But Not So Long Ago,He Was Preaching To People That When God Saw That Adam Was Lonely And Not Happy He Created Eve To Make Him Happy.My Question To This Man Z .Why Did God Not Just Creat Another Adam And Put Him In The Garden.What Wud Be The World?.

  210. But Not So Long Ago,He Was Preaching To People That When God Saw That Adam Was Lonely And Not Happy He Created Eve To Make Him Happy.My Question To This Man Z .Why Did God Not Just Creat Another Adam And Put Him In The Garden.What Wud Be The World?.

  211. Whether its asin or not but we malawians we don’t want this 2happen in our beloved country Malawi.Mxiiiiiiiiiiii FOOLISH PASTORS

  212. Whether its asin or not but we malawians we don’t want this 2happen in our beloved country Malawi.Mxiiiiiiiiiiii FOOLISH PASTORS

  213. But Not So Long Ago,He Was Preaching To People That When God Saw That Adam Was Lonely And Not Happy He Created Eve To Make Him Happy.My Question To This Man Z .Why Did God Not Just Creat Another Adam And Put Him In The Garden.What Wud Be The World?.

  214. But Not So Long Ago,He Was Preaching To People That When God Saw That Adam Was Lonely And Not Happy He Created Eve To Make Him Happy.My Question To This Man Z .Why Did God Not Just Creat Another Adam And Put Him In The Garden.What Wud Be The World?.

  215. Leviticus 18 vs22 No man is to have sexua relations with another man; God hates that. Leviticus 20 vs 13 Good news bible. Wokumva amve.

  216. Leviticus 18 vs22 No man is to have sexua relations with another man; God hates that. Leviticus 20 vs 13 Good news bible. Wokumva amve.

  217. maitanidwe ndi ntchito ndi zinthu ziwili zosiyana, Mr Kaiya akugwila ntchito ya ubusa ku mbc iwo sanaitanidwe ndi mulungu koma owalemba ntchito(boma/mbc) ndiyeno ndizosadabwisa kunamizila mulungu/bible kuti anavomeleza zopusazi, chonde azibusa osakomedwa ndi ndalama lalikilani chomwe bible likunena osati kunamiza anthu, shame to mr Kaiya.

  218. maitanidwe ndi ntchito ndi zinthu ziwili zosiyana, Mr Kaiya akugwila ntchito ya ubusa ku mbc iwo sanaitanidwe ndi mulungu koma owalemba ntchito(boma/mbc) ndiyeno ndizosadabwisa kunamizila mulungu/bible kuti anavomeleza zopusazi, chonde azibusa osakomedwa ndi ndalama lalikilani chomwe bible likunena osati kunamiza anthu, shame to mr Kaiya.

  219. Mr Fletcher ur a #Stupid Pastor I av neva seen in my Life n even ur Fmly 2, Umusiye Mkazi wakoyo akwatiwe ndi Mayi wa Mvano ku Chrch kwanuko,Chitsiru cha Mbusa,Galu wachabechabe

  220. Mr Fletcher ur a #Stupid Pastor I av neva seen in my Life n even ur Fmly 2, Umusiye Mkazi wakoyo akwatiwe ndi Mayi wa Mvano ku Chrch kwanuko,Chitsiru cha Mbusa,Galu wachabechabe

  221. ng’weeeee phuuu ndashuta…..mazira ako fretcher kuthako kukukuyabwa et……f#ck off

    1. may the good lord forgive each one of you the program was not what is here atola nkhani ndinu olakwitsa kwambiri muli ndi ufulu two much

  222. Apastor amene ndithu tisawabisire amenewo ndi amithenga asatana, ndipo amene afa imfa yowawa ndithu ngati akufuna moyo alape lero lino

  223. Apastor amene ndithu tisawabisire amenewo ndi amithenga asatana, ndipo amene afa imfa yowawa ndithu ngati akufuna moyo alape lero lino

  224. tingolapa machimo athu tingataye nawo nthawi iz Zonsezi bible linanena ngati sukuwwreng bible uzingolimbana nazo koma nzoti sizingasinth ndipo zuyenera kuter poti nzomwe bible limanena Nthawi yatha akuluakulu check your steps

  225. tingolapa machimo athu tingataye nawo nthawi iz Zonsezi bible linanena ngati sukuwwreng bible uzingolimbana nazo koma nzoti sizingasinth ndipo zuyenera kuter poti nzomwe bible limanena Nthawi yatha akuluakulu check your steps

  226. Eish,Mulungu achite nafe ndithu patokha sitingathe mutumiki wa Mulungu mpakana kumavomeleza zoterezi.Chitani mamanyazi azitumikinu posagwiritsa ntchito dzina lake wamwamba mwambayo pazinthu zoposa ngati zimenezi.Koma poti kunalembe za aneneli onyenga masiku omaliza,ayi abale ndi alongo chonde tisawamvele koma tikhazikike mumawu a Jehova pamene tikumenyana ndinkhondo ya satanayi.

  227. Eish,Mulungu achite nafe ndithu patokha sitingathe mutumiki wa Mulungu mpakana kumavomeleza zoterezi.Chitani mamanyazi azitumikinu posagwiritsa ntchito dzina lake wamwamba mwambayo pazinthu zoposa ngati zimenezi.Koma poti kunalembe za aneneli onyenga masiku omaliza,ayi abale ndi alongo chonde tisawamvele koma tikhazikike mumawu a Jehova pamene tikumenyana ndinkhondo ya satanayi.

  228. so disgusting especially coming from a pastor he too should go to hell and fuck with the devils there for enternity if you can lock phiri and amosi in one room and tell them to produce children can thy? So if we can all follow suit where will the next president will come from kutha kwa dziko I guess

  229. so disgusting especially coming from a pastor he too should go to hell and fuck with the devils there for enternity if you can lock phiri and amosi in one room and tell them to produce children can thy? So if we can all follow suit where will the next president will come from kutha kwa dziko I guess

  230. Zikhala zamveka zomwe anenazo iwowo akakwatiwa ndi mamuna nzawo.

  231. malawi24 dziwani kut pali u pastor wapa radio wosatsatira baibulo koma ntchito ndiensobpali u pastor weniweni wosankhidwa ndi Mlengi wa makamu. inakakhala kuti sitchimo ndiekut Mulungu sakadalanga Sodomu ndi Gomorah . Tsono a Kaiya akufuna mabungwe awakonde adye ndalama ambuye ali nawe tchito mbale Kaiya.

  232. olo ife ma Chinese zimenezi sitikulola ndizosayenela ndipi anthu amenewa tikaapeza aziwotchedwa….a Kaiya inuyo asiyeni akazanu mukwatilane mamuna mzanu tione ngati mungapange,,,, mwangokula mulibe mzelu mxiiiii

  233. Pastor F.Kaiya,I used to hear your good preaching on MBC,words of inspiration, much respect,but this time you have lost it. Taonani mukutukwanidwa ulele

  234. Kayiya need to go to bible school. And study again. This pastor samaganiza kuyambira zaka zam mbuyomu amapanga program ya tikuyankhani koma ndiye kunali kuyankha za m mutu. Anthu ngati awa ndi omwe yesu adalosera Kuti kuzabwera Aneneri onyenga. And that’s dangerous coz it will lead more people to go astray

  235. Vuto ndiloti timadikila munthu kuti atiuze choonadi pomwe BAIBULO tilinalo. Tatiyeni a Khirisitu inu tizidzifunsa kuti “Kodi akadakhala Yesu pankhaniyi adakayankha ngati a Kaiya wa? Basi Choonadi tachipeza. Anthuwa pano akukwaniritsa okha 2Timoteo 3. Pano atengeka nkufunafuna chuma nkumakhotetsa dala choonadi chaYehova chomwe tikumachipeza m’BAIBULO. Anthu atisocheretsa tikapanda kuchenjera.

  236. Holy ghost Fireeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeeee!!!!!!!!!!!!!!!!!

  237. homesexaulity is not a sin is more than a sin if god destroy those peo way back nd who r we plz malaw is country tht bliev in god so plz plz plz ths habit it has to end once nd for all sumthng need to b done or thy must leave the country play sumhwere

  238. Pastor Kaiya ananena kuti “ngati munthu anabadwa mwachibadwidwe chakuti amakopeka ndi anthu ofanana naye ziwalo limenelo sitchimo pakuti pobadwapo anabadwa ali chomwecho chili ngati chilema komano ngati ayamba kutsatira maganizo akewo kumapanga zogonanazo ndi anthu ofanana nawo ziwalo pamenepo munthuyo wachimwa.” akuti chofunika anthuwa ndi kuwakonza kapena nditi kuwalangidza kuti asiye maganizidwe oterewa. Koma sananene kuti homosexual sitchimo ayi.

    1. Thanks #Patricia, Anthu apa akungoyankhula zinthu zakuti sakuzimvetsa ngakhale programm yo sanayimvere. Nayonso Malawi 24 yangolemba nkhaniyi mwachidule ndi cholinga chakuti anthu anyodze munthu wosalakwa.

    2. Thanks #Patricia, Anthu apa akungoyankhula zinthu zakuti sakuzimvetsa ngakhale programm yo sanayimvere. Nayonso Malawi 24 yangolemba nkhaniyi mwachidule ndi cholinga chakuti anthu anyodze munthu wosalakwa.

    3. Anatero koma pastor shawa anati chani? Ndiziwanda mpaka anawafunsa kuti kodi munthu waziwanda akalowa ufumu? Anyankha kuti chani? Akayiyawo? Anayankha nsanga ndi ashawa mpaka ana werenga vrs apa nane ndinadabwa mene amayankhira akayiya dzulo kaya ndi debate kuti wina anene ee kapena ayi? Koma zinali zoona not debate .nane ndaimvela yonse.

    4. Anatero koma pastor shawa anati chani? Ndiziwanda mpaka anawafunsa kuti kodi munthu waziwanda akalowa ufumu? Anyankha kuti chani? Akayiyawo? Anayankha nsanga ndi ashawa mpaka ana werenga vrs apa nane ndinadabwa mene amayankhira akayiya dzulo kaya ndi debate kuti wina anene ee kapena ayi? Koma zinali zoona not debate .nane ndaimvela yonse.

    5. Chidule akuyiyambitsayo awauze tipange referendum anthu aponye maganizo awo kuti tithane nayo bwanji ngati ku zimbabwe commrade mugabe anathana nayo.kunonso tikanathana nayo.

    6. Chidule akuyiyambitsayo awauze tipange referendum anthu aponye maganizo awo kuti tithane nayo bwanji ngati ku zimbabwe commrade mugabe anathana nayo.kunonso tikanathana nayo.

    7. bright umadziwa kuti anthu timachimwa poganiza ,posilira ndi njira zina being apastor sakanagwiritsa zitsanzo zimenezo and kumvrtsera bwino clarification inawakanika to me apastor adavomereza koma mophiphiritsa

    8. bright umadziwa kuti anthu timachimwa poganiza ,posilira ndi njira zina being apastor sakanagwiritsa zitsanzo zimenezo and kumvrtsera bwino clarification inawakanika to me apastor adavomereza koma mophiphiritsa

    9. there z,a big difference in being homosexual and homesexual acts.. to my own view being homosexual its like having a disability and we Can’t curse them if they are born that way instead pray 4them so that they can not engage in homosexual acts. even God himself didn’t punish the people because they were homosexual, b@ he punished them because they were engaging in homosexual acts. disability z not inability, lets pray 4them lyk we do when praying 4people with disabilities and make them stop existing and start living Amen!

    10. there z,a big difference in being homosexual and homesexual acts.. to my own view being homosexual its like having a disability and we Can’t curse them if they are born that way instead pray 4them so that they can not engage in homosexual acts. even God himself didn’t punish the people because they were homosexual, b@ he punished them because they were engaging in homosexual acts. disability z not inability, lets pray 4them lyk we do when praying 4people with disabilities and make them stop existing and start living Amen!

    11. Munthu umachimwa pokuganiza mpaka kulipanga tchimolo nde ngati anabadwa ndikumasilira anzawo ofanana nawo ziwaro ndi tchomo basi,ngakhare sanapange umathanyulawo.

  239. I thought Kaiya was a man of God all along,just to be surprised at his comments yesterday, he was even courting the bible verse half way,failing to unfold the truth, shame to the old man, he is an instrument of the devil,the other pastor younger than him unfolded the bible truth. Shame on you Kaiya,you will perish in hell

  240. Nde taonani anthuni ukwati wamagayz,,,,amangisa apapa nde kumafunsa kut ngati sitchimo nanga “lemba liti” likulora ukwati umeneyu?

    Apapa zangoneseratu kuti ukwati ngati uwu atha kuuvomeleza ndithu!!!

  241. No one can lay any foundation other than the one already laid,which is Jesus.If any man builds on this foundation using gold,Silver,costly stones, hay or straw…..his work will be shown to light,it will be reveaved with fire and the fire will test the quality of each man‘s work – 1Corinthians 3 :11 :Lord Jesus,you are the foundation of our marrage.Help us look to your strength in every way as we build a life together. Amen

  242. what kind of bible does he read…….coz the bible says in Leviticus 20 vs 13 ‘if any man lies with a man as one lies with a woman, both of them have done what is detestable..they must be put to death their blood will be on their heads…..

  243. Inu amene mukumati palibe chimene akudziwa…. Zoona amene mukuti m’busa Kayiya yu sakudziwa kut Amuna ndi amuna kukhalira malo amodzi ngati banja ndi tchimo????

    Ufulu uwu….. Tiona nawo zovuta kwambili kuno ku Malawi..

    Mabvutowa Satha…

  244. Mr kaiya mukufuna kungodya nao chuma chama donors or fame??? koma ma pastor enawa can u divorce ur lovery wife and marry an attractive men? because its not a sin then come on air and tell the citizens of Malawi . try to be real

  245. mzake watson shaba anati zomwe ananena msonda kuti bola Galu ndizoona koma kaiya anati ena amene anabadya ndichilakolako chamamuna akhoza kupanga koma abusa ena kaya ndimaluzi eeeee

    1. Ndipo anaoneka chifukwa cha manyazi anayamba kumavomeleza kuti ndikulakwa ataona kuti ashaba akunenetsa kuti sizoona nditchimo.pamodzi anati kuwapha ndiye tilakwa koma ndiuchimo ndipo amsonda sanayambitse kuti aphedwe,koma okha ma gay ndamene ananena modelera.ndiye nsonda kunalikumuvomereza kuti muyenera kuphedwa kumene.akuti nsonda walakwitsa satan ulindichilungamo?manyazi ulibe? Wekha kuyambitsa ndemanga wina comment walakwa? Nthawidi yakwana anthuwa atulukira poyera.ndipo chidule iwowo osanena kuti tipange referendum akuopa chani?

  246. Ambuy atithandize.Dziko lapansi ladzala ndi uchimo kotero Mulungu wakwiya .YESAYA 29 V 9,,,,KHALANI NDI KUDABWA,SANGALALARANI NDI KUKHALA AKHUNGU,PAKUTI MZIMU WA MULUNGU WASANULIRA INU TULO TOGONETSA *ZIMENE MASO ANU APHIMBIKA; NDIWO ANENERI,MASOMPHENYA ANU APHIMBIKA ;NDIWO ALAULI………..AMEN…AMBUYE THANDIZANI MALAWI…

  247. Mulungu alinafe cholinga,poti kunalembedwa,sitikuyenera kudabwa koma kutsimikizira pazimene baibulo limatiphuzitsa kuti tizikhala wokhulupilira,pakuti Yehova sali ngati munthu amene aphwanya pangano.Likhale phuziro lalikulu kuti tilimbike kupemphera kuti zina ngati zimenezi tisamaziveso kuopa kuchimwa pakuganiza.Mulungu chitanafeni poti maso athu ndi akhungu,ndipo makutu athu,samva,ndi ine ochimwa koma ndikupempha kuti muchisomo chanu,ndizalowe muufumu wanu.Amen

  248. For one thing am sure is that all church leaders can be corrupted on this issue of gays, but not Catholic bishops… ndimomwe maluzi athyoleramu azikana ndalama from state house…

    Nature itself does not support such ideology of gayism….

  249. Kunali bwina akanatenga chimwala kumangirila iye mkuchiponya panyanja kuti tisadzaveso kapena kukuonani aneneri onyenga inu

  250. Izi nde zopusatu, kam’busa kameneka kamawerenga Bible lanji? De bible z clear on 1 corinthians 6:9 dat homosexual offenders wil nt inherit d kngdom of God…nde akut chan ameneyu? Mxiew!!!

  251. Mr kaiya sindikukhulupilira kuti makolo anu ali moyo chifukwa zomwe mwakamba apa zawonetsera2 kuti ndinu munthu opanda uzimu anakhala kuti alipo anakakulangizani ndikukutengeran kwa anthu oziwa mawu AYEHOVA kuti muwamvetse bwino

  252. So y did God punished sodom and gomorah ??? Abusa kodi mumasuta chamba powelenga Bible ? Mukumawelenga chozondotsa buku lopatulika ??? Muwelenge jude 1:7 ife takana machimo.

  253. Pass this on to the Esteemed Reverend

    Leviticus 20:13 NKJV
    If a man lies with a male as he lies with a woman, both of them have committed an abomination. They shall surely be put to death. Their blood shall be upon them.
    :

  254. Finally this man has exchanged his salvation and future glory with money.Be careful men of God out there.You might b the next.Devil wants 2 use u the way he has used this veteran preacher. Late fletcher kayiya.

  255. Enanu chufukwa chosadziwa mwatenga matembelero po nyoza,abusa God is watching you

  256. Pastor! Are u from this planet.Even rapist,murderers,armed robbers and even terrorists were created by God.Should we embrace them.

  257. Wumwanawangawose ndimapelekawulemu kwa Kaiya kuti ndimunthu wowopa mulungu koma pano fokofu,wathantchito,wapanga expire,mwanawanjoka osatiwonongela Malawi wathu wokoma

  258. The fig tree is now showing its newly updated leaves,just to show the man kind that rainy season is at hand!It’s high time people have been proclaiming about this,and now is the hour!Let He who has the ear understand what is happening!JESUS IS COMING AGAIN.Pitirizani kupanga,kwa anthu otembenuka ndichmwemwe chfukwa akuziwa kuti mpulumutsi wayandkra kuzawatenga ku dziko lobvundali.OPUTSA ndi inu muli busy backng up ur constitution kuti spanga legalise homo-sexualy!What u cud do is to prepare for the 2nd coming of the KING!

    1. Thanks,,i recieve the blessing!It’s high time we hav bn down trodening ourselves in speaking the truth.But now is the only last moment GOD has granteed to us that we can speak out what is true and full of life.AZIPANGA MA UKWATI AWOWO,,,kod ngat angelo sanabwere kuzamuuza loti kut athawe sodom ali ndi mkwiyo pamaso pamulungu???

  259. Pastor seriously, Jesus didn’t lie when He said during end times we will see false prophets. Woneka a chipembezo koma mphamvu yake anayikana kale. Pastor supporting Sodom and Gomorrah. Please repent at once other wise you are leading the sheep of God astray. You know the consequences of doing that God will not gonna watch you leading His children astray.

  260. Asogoleli achinyengo muzawaziwa ndi ntchito zao, auzimu ongovala ngati malaya nkati ali afisi kkkkkkkkk mapastor amanthanyula aaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa sangandilalikile ine chifukwa zimu oyera anyasidwa nao. Mulipo ambiri muziulula

  261. Muzipemphera kwambiri mr.Akaiya kuti mulungu asunge mzimu wanu-you must be 70yrs plus koma Zikumvetsa chisoni kuti mzimu wanu udakanyengedwabe…timakana kuti izi sindimazimvetsa bwino!

  262. It’s really funny to see christians go mad on this, these so called god fearing they dont even know anything about God. Big up Mr Kayia!

  263. Kaiya is being sold out his soul to the illuminatic society in America, for his personal gain. What kind of Bible is he reading?

  264. M’busa wonama kupita kukaphunzila za ubusa chifukwa chofuna kupeza ndalama not kulalikila za ufumu wakumwamba,akuyankhula zopusa chifukwa wadyakale ndalama yake.

  265. Amene wamawerenga bible apapa watsimikiza kuti anodi ndimasiku osiliza

    Azakhala nawo maonekedwe achipembedzo koma mphamvu yake ataikana kale!!!
    Ukuku mulungu ndikutionesera ndithu aneneri onyenga ankati azabwera aja uyu ndimmodzi mwaiwo,,,,,,ndamva chisoni ngakhale ndiliochimwa ndithu!!!!

    1. Tsoka ngati sititembenuka mtima ndikudikira mwa tcheru kudza kwa Mwana wa Mulungu. ..
      Chifukwa zizindikiro nde zikukwanilitsika ndipo Satan akunyenga ndi kusocheretsa ingakhale osankhika omwe a Mulungu kuleka njira ya choonadi
      Tiwapempherele abusa amenewa

    2. being homosexual is not wrong coz its an intimate feeling born within a person, b@ engaging in homosexual acts is morally wrong n also a sin.
      guess th@s wh@ he was tryng 2say.

    3. being homosexual is not wrong coz its an intimate feeling born within a person, b@ engaging in homosexual acts is morally wrong n also a sin.
      guess th@s wh@ he was tryng 2say.

    4. there z,a big difference in being homosexual and homesexual acts.. to my own view being homosexual its like having a disability and we Can’t curse them if they are born that way instead pray 4them so that they can not engage in homosexual acts. even God himself didn’t punish the people because they were homosexual, b@ he punished them because they were engaging in homosexual acts. disability z not inability, lets pray 4them lyk we do when praying 4people with disabilities and make them stop existing and start living Amen!

    5. there z,a big difference in being homosexual and homesexual acts.. to my own view being homosexual its like having a disability and we Can’t curse them if they are born that way instead pray 4them so that they can not engage in homosexual acts. even God himself didn’t punish the people because they were homosexual, b@ he punished them because they were engaging in homosexual acts. disability z not inability, lets pray 4them lyk we do when praying 4people with disabilities and make them stop existing and start living Amen!

    6. Lets preach the world of GOD through these social mediaz 2 my own view weather iz disability ths iz wrong ndithembelero lobwelapo coz ov sin we r in the last dayz we as christian we ll b affected also wth these thing coz til mu dziko lasokalo chofunika kupephela kolimba ndithu Yesu akubwela posachedwa

    7. Lets preach the world of GOD through these social mediaz 2 my own view weather iz disability ths iz wrong ndithembelero lobwelapo coz ov sin we r in the last dayz we as christian we ll b affected also wth these thing coz til mu dziko lasokalo chofunika kupephela kolimba ndithu Yesu akubwela posachedwa

    8. Gomezulu Bin Mkakato how do you call someone a footballer, when he has never played football in his entire life? homosexuality and homosexual activities are two things that can’t be separated at all. Because it is the activities that define someone to be Homosexual or not. Nobody is judged on their thoughts but it is the actions accompanied by those thoughts that give a person his or her identity. Therefore Leviticus 18:22 says it is disgusting for a man to have sex with another man. As such the word homosexuality is also a disgust in my ears. No apologies. Let God arise, and His enemies scatter!!!!

    9. And point of correction to all who say one is born a homosexual. No! God cannot say do not sleep with a fellow man as a man sleeps with a woman and vise versa, and He Himself create homosexuals. God does not contradict Himself. He is right and just. Homosexuality is demonic. Evil spirits that enter a man or woman. They need to be cast out with prayer and total surrender and repentance.

  266. Mr Goodfellow Phiri your comment got logic and it makes sense but we can not fix disabled people rather love them who they are ,locking them in jail for whom they are won’t solve the problem becoz that behavior was there and will be there,others say its end of days no its not like that due to the fact that the homosexuality started even before jesus,Bible condemn it but does not mean that they were not there but its a sin really lets treat them as sinners coz we r not perfect, ,thats my opinion.

  267. Tisaiwale kuti satana sali yekha alipo amithenga ake ndipo pastor Kayiya is one of them. shame on u fake pastor who advocates this dog acts

  268. simple its not aba the govt shud legallise, but the owner of malawi who r peaple them selves chose which z right for dem. so its better we shud hv a refferendam on this issue.

  269. One of those MAN MADE men of God. Priests, pastors , Apostles, All this names are titles now . Bible school alone cannot qualify one as pastor.. God is a spirit .

  270. its not aba whether its a sin or not. let Him ‘God’ judge. but lets stand for our diginity. unlike animals who r devoid of dignity n integrity, w r humans with ful dignity. why even those animals nos that this z ov the same sex unlike this one? people lets b realistic

  271. Bambo Kaiya Ndinkawapatsa Ulemu Kuyambira Pomwe Ndinali Mwana.Ndimatsitsimuka Ndi Program Yawo Ya Lemekezani Mulungu.Koma Pomwe Zafikapa,ndakhumudwa Komanso Ndili Wa Manyazi.Ambuye Awakhululukire Chifukwa Palibe Chomwe Akudziwa.

  272. Ndilola mwazi wanga ukhitsidwe kamba kotsutsa zonyasazi,akapezeka pafupi ndi ine ndiwapha inenso mudzandiphe,bwanji a president inu ngati kholo la dziko mupeze mphongo nzanu??Zuma alipo agement wanu pitan kamutengeni akhale nkazi wanu,ife tidzatengela inu ngati kholo lathu,amalawi tikulira kamba ka zoipazi.Mawa adzatilanda dziko kamba ka ndalama akupeleka pano,mawa state house ya malawi idzakhala ku USA inu nkumati united states of sanjika malawi ku america.Ife ayi.Nanu ma paster amatsiku ano tatopa nanu,kusowa sugar tsiku limodzi mwayamba zoti ndinu a pastor ndikunena inu anthu opanda khalidwe ngati inu.Mukandifuna ndikupatsani address yanga mubwele mudzandigwile am ready for any attack.

  273. Okay, if z not a sin now am going to marry u fretcha.. to be good example, maybe we cn bearing child from man to man… inu2 ngati mkufuna ndalama yambani ndale ife za utsiru muno ai

    1. kkkkkk apa nde tikutha kuona pastor achinyengo akuvomverexa zoipa akuti mutha kukwatirana nokha nokha for example frank married to John, or mary to jane… nde kuti agaluwa ali ndi nzeru kuposa ma pastor athuwa coz galu sanapange ximenexo since I ws born,

  274. Pastor thinking like my son prince and even my son is better than him how can well known pastor say like that?if is not a sin why God distroy Sodom anda Gomolah?what was the bible realy mean when it says new marriages?is it trying to mean new weeded?or same sex?my the lord punish u the devil who mislead the Nation.Money makes man to be stupid now is true I can see

  275. Akeeeeee! Watsala Ndi Kaiya Kusanduka, Uyu Nde Asanduka Kambuku2, Mwat Ndi Wa Mpingo Wanji! Akuyenera Awatenge Amathanyula Amzake Apeze Dziko Lawo, Coz Alibe Malo Mmalawi Muno, Holy Gost Fire!

  276. Mulungu amakonda aliyese komasangakodwe ndizoputsazo kod mulungu analakwa kulenga anthu awiri mwamuna ndi mkazi nakha inumukuzitenga kuti zokwatilana amuna okhaokha malaulo amenewo mulungu azakulangani tiyeni tipewe ndi asatanawa

  277. Mulungu bwerani nsanga mudzatiweruze anthu anu tikuwonongeka,kodi anthu woyambitsa khalidwe lamanthanyulanu akanakhala kuti makolo anu xanakwatirane bwenzi mulipo? kodi Mulungu ndiwopunxa kule mkazi ndi mamuna?mudzafa imfa yowawa ngati mulungu wanu ndindalama zomwe mukufuna akupatsenizo mukavomereza,wolenga ife tonxe akutiwona akungondikira nthawi kuti adzatiweruze.

  278. Akayiya monga muthu wamulungu simunakatero mudza ifa yowawa inu mulibe mkazi? Munakwatira mamuna zanu?chinakupangitani mchani kusilira mkazi osati mamuna

  279. Dziko lathapo apa zizindikiro nde nzosanena mkulu osocheretsa uyu. Mr kaiya with small letter k ana anu mungawavomereze zimenezi?

  280. mr kaiya z a poster not a pastor. others r born pastors stil others r artificially made. 1 of de artificial ones z mr kaiya he z tryng 2 coat gold on sin. shame of u & i wish Jah shud strike u b4 de end of de rain season

  281. 1 corinthians 4: 9 Do you not know that the wicked will not inherit the kingdom of God? Do not be deceived: Neither the sexually immoral nor idolaters nor adulterers nor male prostitutes nor homosexual offenders 10. nor thieves nor the greedy nor drunkards nor slanderers nor swindlers will inherit the kingdom of God.

  282. pastor kaiya please I berg u in the name of jesus,don’t mislead pple,ngati mwagwa mmanja mwa Yehova be it for yourself

  283. My malawi!! Wea were u going to?? Is this the way solve all ur ploblems?? Instead to keep on playing aimed at coming out in all ur problems apa malawi akuonjezera nkwiyo wa Mulungu!!! Tizingosaukirabe.. Pastor amenei Mulungu ndi2 amulanga chabwino iyeyo angotipasa verse imene imanena kut sitchimo… Kulankhulaku tilankhule zot Bible adalemba osangoti ndalama yakoma mmmmm Mulungu amukanthe mtumiki wa satana amenei kumangot u pastor?? Pot agogo awo adali apastor??

  284. ANTHU OFUNA ULEMELERO WA DZIKO.
    BIBLE NDI MALEMBA NDI MAWELUZO TELL HIM TO READ AROMA 1:26-36 APEZA KUTI ANTHU OTERE AYENELA …….?

  285. or patavuta bwanji sindingapange mtske imeneyo ndikatenge gadaf wanga akalowe potulukira manyi kutichan.ndata ntchito yake ndichan.mxew mufuna mutiwoningere ana athu .

  286. Chibanzi chiri mkwamwa that’s why…….or wadya vyamba va ku kotakota, wish I could know where he’s basing his argument……

  287. Homosexuality may not be a sin, in fact it is a psychological disability. Certainly a disability cannot be a right, and it’s not a right that requires legalisation. Therefore our work should be to minimise the calamity among us by curing it not to promote it. Do we promote insanity or do we cure it? Which is better?

  288. Asadzalalikenso pa MBC mumuuze kwa amene muli naye pafupinu bwanji iyeyo ali ndi mkazi komaso ndi munthu wankulu samayenera kukamba za umve ngati zimenezi FUCKEN IDIOT GO TO HELL

  289. Mwana Wa Satana Iwe!..coz of ds dats y God z not gvn us rains! May b He z so mad at u fuckn pastors ndakwya nanu kwambri!

  290. Dyera la ma pastors enawa lingotikumbusa atumiki amene anakana Mulungu ndikusatira ndlama kotelo analandira zowaeneleza malinga ndi dyela lawo

  291. Zoonadi ameneyu ci£ungamo akuciziwa kma ndiwadyera akufna kulemera ngat zilizimenezo amusiye mkazi wake akwa£e mamuna nzake anthu atengele paiyeyo

  292. Tell him he knows nothing about the bibble…he is a pastor just to earn a living…….dont mislead pipo……..i hop his mother is a man…not a woman

  293. My questions
    Is this man married?
    If ‘yes’
    is his wife a man?
    if not
    then He must go find himself a man to marry
    cos we need leader who lead by example
    So we belive his words are true

  294. mubusa wamizimu ameneyu muneneri wonyenga wa chi tchayina gahena ikumudkirira kape iwe eti tziti ndiwe mutumiki wa mulungu anangosowa zonena mwana wasatana iwe fake prophet lapa machimo akowo

    1. Eya kwambr,anyway timva, ngat nd zoona then ndikhulupira mkuluwinawake wanena kut many pastorz and prophets and apostles are sent but with devil to lead us astray,however not long wil it take azidziwika okha!

  295. Koma ndipofunika kuti a Kaiya afotokoze chomwe akutanthauza. Mwina sitikuwamvetsetsa bwino. Koma ngati akuikila kumbuyo za mathanyulazi ndiye aaaaaaaaaaaaaaaaa!! Abusa ndi chaninso?

  296. Fletcher Kaiya Ndi Mbuzi, Chidzete, Fisi, Galu, Chitsiru Cha Munthu.
    Asationongere Dziko.Sodom & Gomorrah Adaonongedwa Chifukwa Chani?Wakutumayo Akuphetsa.Ndalama Walandirayo Ikuphetsa Imfa Yowawa.
    #choka_satana..!!

  297. Which Chapter In The Bible Is Supporting His Statement?Which Kind Of The Bible He Uses?Pls Dont Mislead The Pple We Are In De Last Days.U Shall Know De Truth,and De Truth Shall Set U Free Thats Wat De Bible Tells Us.We Dont Want To Live In Bondages.

  298. whether its a sin or not………Gay people should be left alone….God will judge them as he will with us coz we aint perfect either..im not defending anyone ..

  299. kkkkkkkk pali pastor wa mulungu ndiye pali pastor wa devil , mr kaiya ndi pastor wa devil , koma onse ndi ma pastor , pastor uyu ndi wa maluzi akufuna ndalama , ndipo umunthu alibe adzafanso imfa yowawa zedi , mulungu sanamudziwebe mpaka pano ngakhale ali pastor

    1. Koma a Kayiyanso…….. sikudetsa chikhilisitutu kumeneku? Ndizimene zilikumtima kwanu kani? Mwawotcha CV yanu ya Mulungu mutafika kale ….. Shame!!!!

    2. Ino ndi nthawi yongofuna ku bwelera kwa MULUNGU Posiya zoipa zonse,malinga ndi mmene ma pastor wa akuchitira pokonda ndalama

    3. Apa bakha ali ndinzeru kwambiri kuposa anthu,chomvetsa chison nchot anthuwo amakhulipilidwa ndikudalilidwa ndi anzawo (Atsogoleri shame on u mwatanganidwa ndikusonkhanitsa chuma nthawi ikutha kaya mukadyera kut chumacho? Mufa imfa yowawa

  300. Uchtsiru Ndiwo Umenewo If It Isnt A Sin Mulungu Sakadalenga Adam Nd Hava Ndkuwakhazka Pamodz. Peza Atalenga Amuna Awir Then Akaz Awirixo Kt Akaz Okhaokha Akwatrane!May B Atat Atenge Amunawo Akhale Mbanja Kwa Miyez Ten Twone Ngat Wna Atha Kukhala Impregnated! Adzngozuzka Odyera Nd Ena Coz Amuna Azngokufa Chabe Thats Sacrifice {apm Mudzamuvoterexo}

  301. This kind of pastor they just a paster in order to get chopeleka and chakhumi not a messenger of God……as my bible told me already about fek prophets i don’t surprising it’s enjurry time

  302. Shame on u Kaiya did u married to man like u?? U don’t have children at ur home??? Bambo ako akanakwatira mamuna mzawo iwe ukanapedzeka padzikoli? Mau amenena kuti zokhumudwisa sizingalephere kupedzeka pakati pathu,KOMA TSOKA KWA OBWERETSA ZOKHUMUDWISAZO

  303. Zopusa basiiiiii,, Mulungu wake uti ameneyo,,, Mulungu adali opusa kulenga Adam ndI Hava,, bwanji amaleka kulenga amuna okhaokha mmunda muja,,, apa Mulungu bola abwere azatiweruza b4 anthu amenewa asanatipoteze enafe

    1. I was also asking myself that which bible does he use?ofcourse i havent read the whole passage but i dont believe that he z a christian/pastor.many pple are disguising themself nowdays as christians but in true sense they are not.Their acts are testifying whether they are christians or not.

  304. Masiku Otsiriza.Anthu Otumikira Nkhosa Azasanduka Osocheretsa Nkhosa.Ngati Si Tchimo Bwanji Mulungu Adaononga Sodom & Gomorrah?

  305. Pastor Kaiya, do you mean after downloading the whole data you end up flushing into Trapence’s stomach? Kuchimwa ndikwa aliyense koma tsoka kwa iye okhalisa mu uchimowo. As a Pastor your duty nkuzikusa nkhosa zosochelanso kuti zibwelere mkhola. ngati timapemphelera mbava kuti isinthika why not wamathanyula? ndalama za azungu zikuphanitu. MUZAFA INFA YOWAWA PASTOR. I rest my case.

  306. these are last days people. just go back to you Bibles and read about these men of God who will love themselves and money.

    God is still in control and will judge the sinners. turn away from your sinful life and follow the ways of God there you shall know the truth of the matter.

    God protect Malawi!!!!

  307. Mr kaiya, one thing u must know is that people in Malawi respects u kwambiri and kumene mwachoka ndi kutali mukugwira ntchito ya Mulungu. that gray hair mmutumo zikuonetsa kuti mwakula. pali azitumiki ambiri a Mulungu amene akhala chete pa nkhani imeneyi posafuna kusocheletsa anthu. musataye chipulumutso chanu mu last minute chifukwa cha ndalama. u r the one who is heading BAPTIST CHURCH, should we conclude to say that ur church is in support of this act? am sorry for u MR LONG TIME PASTOR. ………

  308. Is he another Gay Pastor? He should help us understand spiritually what the word of God day about Gay relationship? If we had only Gay on earth would mankind not die natural death by now?

  309. I watched that program on tv, and he said, some people were born with both male and female staffs and later on they chose whether to be a man or a woman, and some are born with the desire of same sex or. And to be that is nt a sin bt when you start practising homesexual is when you commit a sin

  310. Being born a homosexual???ndekuti mulungu angalakwitse???a chunga imeneyo psychology or theology??? Homosexual is learned not instinctive. Tatiuzeni zimakhala bwanji kuti mulungu kulakwitsa mpaka nkazi kapena mwamuna kumasilila nzake eish!!!!abomination.

  311. Fletcher Kaiya is a Chamba abuser. Msataye nthawi kumamfunsa zinthu ngati izi. Munthu uyu amakondanso kunyenga ti atsika ta U/10. Mutha kuchita verify this by asking members of Baptist Church. Pliz! Mr Kaiya stop smoking dagga, as i alread told u on zat day becoz most of the times, we, your relatives have noted zat u speak under the influence of dagga.

    1. God will punish you for this why are you saying something you don’t know believe me or not you will never have peace

  312. vuto ndilakuti mukulitenga Baibulo kuti lifanane ndimaprinciples anu.bola zoona zake mukuzidziwa pansi pantima wanu .verse mukunenayi amakamba zaanthu osabeleka kapena kuti opanda chilakolako

  313. Shame on u mr kaiya,look at ur face!satana wenwen.Mudzafa choyima mr.Musamale kwambili ndi Mulungu wamoyo & akuchitilen chifundo mr kaiya.

  314. Eeeeeheeeee mumabisala kuseli kwa Bible pano mwavumbulukako iinvi zili thooo chisilu ukufuna kupezelapo kakhobidi kazizukuluuuu.

    Ndimakupasani ulemu koma mmmmmm nchifukwa chani muli ndi mkazi & being m’busa ngati ana sazibadwa muzikamlalikila ndaniiiii.
    Satana pa ndalama ndiye kuti mulipo kaphava tikuziwa.

    Pasogolo ndi KEN MSONDA pansi tiazibusa tonyenga nchifukwa mukumaoneka mwalemela from no where now we know tizikuopani atumiki asatana inu

  315. Pastor Fletcher Kaiya Opens Another Debate, GOD Created Homosexuals, Kodi Aliponso Winaaaaaa…. Nkhani Yovuta, Pali Anthu Ena Amadzitenga Ngati Odziwa Bible Kwambiri, Iyoyo Akhale Ma Saint, YESU Anabwela Ku Dziko Lapansi Kudzafunafuna Wotaikayo, Sizili Kwa Ife Kuweluza Munthu, Asiyeni Ma Homosexual Asangalare, Pa Malamulo Khumi A MULUNGU Palibe Lamulo Loti Usakhale Homosexual, Big Up Pastor Kaiya.

Comments are closed.