A 23 year old Malawian man in Nkhatabay is in police custody for allegedly abducting and sexually assaulting a 15 year old girl, police say.
Nkhatabay Police confirmed the arrest of the suspect and identified him as Chimwemwe Mlenga.
According to Nkhatabay police spokesperson, Ignatius Esau, the incident happened on October 26 this year in the district.
“He abducted the 15 year old girl and had sex with her until the second day of November, members of the community discovered she was at Mlenga’s house,” said Esau.
Mlenga who hails from Chapema village, Traditional Authority Timbiri in Nkhotakota will soon be brought to book to answer charges of abduction and defilement.
Basi wanyengelatu ameneyou anzanyenganso after 15 years
Kamoyu kalyengi vatimala kali
Did you learn from our leader in Afrique du Sud ?
zausilu
Akazi thandizani abambo kuchipinda mukuona akuvutika basi kuwasiya zoona? Koma inu.
Ndikupempha apolice kuti adziwombela ndi mfuti wogwiririra ana.
Khalidweri ndiloipa winawe ndiye ukutanthauza chani ukati simwana? Kapena zakukondweletsa ndimlongo wako wagwiririlayo?
ana alerowa akunyanya thako ngati wankulu.
Ok Tamvanao
FOOL
This z not rape for sure
Atonga mwaonjeza nyere ngati bulu bwanji..
There’s no good news abt malawi! all what i read is bad news! I Love my country Uganda.
Atoliyapu ngwandu anganyayawa aluwa voachita iwu.
Muchiwotchiwakacho, chatilengeska.
15 yrs swankulu ayi,kma atskana alero sakumakhalangat ana akumapanga zithu zolakwitsa azbambo pamene iwo ali achchepere
some of the comments give me cancer,imagine if she was ur sisiter
Rape ndi ku Northern ku eish! achuluka…..ku South kuno kulibe anthu ogwirira apart from Joe Gwaladi
bodza limenelo.posachedwa pompa agogo ku balaka raped his grand dota.nanga khansala ku mj?uchitsiru uliponseponse & there’s no tribe which is perfect.
Uyu wagwiririra dzulo ku Mulanjeyu
Zaka 15, simwana ameneyo inu mwangovutika kulemba nkhaniyi kuli ana ku dziko kuno azaka 13, 14 …… Komakukwatiwa ndi madala azaka 30. Komanso ndikukumbukila president winawake anakwatila mkazi wazaka 40 iye panthawiyo anali ndizaka 84 bwanji sanakammange.
Banja ndi ngwirizano…sono nkhani ili apa ndi yogwiririla. Ukutanthauza kuti munthu wazaka 15 akagwirilidwa pasakhale mlandu coz u think ndiwankulu?
Mmmmmmmmm man anapangana amenewo inu zangovuta kuti mkaziyo ana virgin basi ndiye paja ukamaziyamba kumene mkazi amatuluka magazi.
Khataby U R Vexing Malawi Wth Ur Fuc*n Tenderncy!
15 years ndichibwezi chimenecho
Awo anali pa chibwenzi, anagwilizana just say mkaziyo was first time kupedzana ndi mamuna if there is some effection!
These issues have become rampant in Nkhata Bay.Offenders must be locked up for long periods to deter others.
They agreed… Koma zinazi ? Thats a perfect match
23-15=8
Aaaa inu wa 15 yrs ndiwamkulu anagwirizana amenewo tangowafufuzani bwinobwino amenewo
ameneyo bax akalow
Ok
Introduce castration law for dirtening an innocent girl
Malawi Why?
kkkkk msiyene adye repuyo anawa nowadays akumawonjeza espeshally mavalidye :…….kakaakkk
Sikugwilira kumene check their ages its a gap of 7 years.it was a set up
Mwati masiku 7 amadya rape? Limenero ndiboza, amenewa anali pa mpiru kkkkkk!
Mtayeni mnyamata. Anawa akuziwana kungoti makolo a mkazi sanafune kukhala ndi mkamwini pakadali pano, ndiye ngati apatsana mimba makolo atani.
amadziwa chomwe amachita ,mtayeni