Oyimba wa kale wa chamba cha hip hop Jolly Bro (JB) akupitirizabe kuthira makala a Malawi a ku South Bend ku Amereka. Pano waonjezera mkwiyo kwa mkulu wa dambwe Tay Grin. Ati kumene akukayimba kumeneko… ...
Articles By Lindiwe Sambalikagwa
…52 miliyoni yanga ya bet yapita Zija ankapanga azimalume kalekale zomakunyengelera chimanga chophika kuti akonze nsewu zamuonekera James Chaola amene anawina bet ya 52 miliyoni. Kusiyana kwake ndi koti iye sanamubwenzere ndi komwe chenje, amuuza… ...
…akushopa pa kaunjika wa kumeneko Kumudzi kuno Lulu ndi namandwa oyimba. Zithunzi zake za makabudula pamene ali ku Amereka zikuoneka za mtengo wa patali. Koma oyimba Jolly Bro kapena kuti JB ati tisatengeke nazo. Ku… ...
Tanzanian combat engineers have left Malawi about two weeks after they were deployed to restore and rehabilitate infrastructure destroyed by Cyclone Freddy. The 59 were sent to the southern region of the country towards the… ...
…Wadzudzula mchitidwe ozithandiza wekha Kudya beti ndi kosangalatsa inde. Kwa ena kupambana mayeso kumene kutha kukhala chinthu cha mtengo wa pamwamba. Koma zonsezi sizingafike pa kugonana. Kugonana ndicho chinthu chokongola kwambiri pa dziko pano, watero… ...
…boma likupanga malamulo atsopano okhaulitsa ma dalaiva a chakumwa Phungu wa dera la pakati mu boma la Mwanza a Nicolas Dausi anachemetsa ku nyumba ya malamulo pamene anadzudzula nduna ya boma kuti imanyogodola anthu omwa… ...
…misonkho ikuthera ma lendi mu Lilongwe…nduna ndi ya nsanje yotenga mkazi ngati kapolo…ana 5, amayi 5 Nkhani ya nduna yoona za masiketi, imene pena imapanganso za chuma, ikupitilira. Mayi amene anabwera kugulu ndi kulengeza kuti… ...
Zoti tiri pa chisoni sizinaoneke. Zoti tate wathu ndi m'busa sizinaonekenso. Pena kumati mwina malaya ofiyira tinavala lero anamusokoneza mmaso Mo Salah kuti amayesa ndi Manchester United. Chifukwa atiswa ndipo atisambitsa chokweza. Olo naye kochi… ...
Chithyola More Malawians working at Mwanza Border will lose their jobs when the One-Stop Border post is launched, government has revealed. The losses are a direct opposite that President Lazarus Chakwera promised during his presidential… ...
...Khoti labwenzeretsa Mayi Chizuma Tsiku lofa nyani mtengo ulionse umatelera. Boma la a Lazarus Chakwera lakumana nazo ku bwalo pamene oweruza ayimitsa kaye chiganizo choti awapumitse pa ntchito. Bungwe la maloya mu dziko lino, Malawi… ...
Legal scholars say Secretary to the President and Cabinet Colleen Zamba has no authority to suspend Malawi Anti-Corruption Bureau (ACB) director general Martha Chizuma. Zamba on 31 January informed Chizuma that she should stop exercising… ...
Villagers in Chitipa have killed a man for not taking part in community work. The man has been identified as identified as Jamu Chizumila. According to Chitipa Police Station Public Relations Officer Gladwell Simwaka, villagers… ...
A nduna oona za chikhalidwe a Michael Usi amene amadziwikanso ngati Manganya ati Mulungu achita ndi a Malawi onse onyoza a Chakwera. Polankhula pa mwambo okumbukira M'busa John Chilembwe ku Chiradzulu, a Usi anadzudzula a… ...
Malawi Music star Driemo has released a video for his new song titled Pano. In the song, a heartbroken person complains after being dumped by their partner It is the third video for the Malawi… ...
Part of the M5 Road has been washed away at Phakwe, 54 kilometres from Kaphantenga, and motorists have been advised to use the Nkhotakota-Kasungu Road. Roads Authority (RA) spokesperson Portia Kajanga says the road has… ...