DPP suffering from Mia fever


Lazarus Chakwera Sidik Mia MCP

Sidik Mia’s decision to return to active politics by joining Malawi Congress Party (MCP) seems to have rattled the ruling Democratic Progressive Party (DPP) which has launched attacks on the new MCP member.

Mia who is taken as a political giant from Shire Valley is noted to have given fever to the ruling DPP as top party officials have started criticising MCP and Mia in particular.

A week after Mia joined MCP, DPP organized a political rally to counter the one that MCP held to welcome Mia.

Sidik Mia
Mia’s joining MCP still a big concern for DPP.

Though DPP spokesperson Francis Kasaila disclosed that they had planned to have a rally at Shire Valley before Mia’s move, speeches at the ruling party’s rally showed that the business tycoon is now a thorn in the fresh of DPP.

Kasaila claimed that MCP has no popularity in the Shire Valley hence the use of influential musician Lucius Banda to have people in large numbers at the rally.

“Anthu anavina, kuvina eeeh mpaka kutopa, ngati mungafuse anthu akuuzani kuti Lucius Banda sanapiteko ku Ngabu, anthu amasatila kuvinako ikazafika nthawi yovota azavotela chitukuko (people danced until they were tired. If you ask people they will tell you that they went to see Lucius Banda since he has never been to Ngabu but during elections they will vote for development [DPP]) ” said Kasaila on local press.

He also branded Mia as a recycled politician who wants to spearhead his ambitions and not the needs of Malawians.

Speakers at the DPP rally in the Shire Valley claimed that Mia influenced MCP using his “money” since he want to become the country’s vice president.

MCP leader Lazarus Chakwera was also not spared from the attacks as the DPP officials faulted him for allowing Mia join the party.

Some officials repeated DPP President, Peter Mutharika’s remarks that Chakwera is “a new Judas Iscariot who has sold MCP for K200 million”.

The tension between the country’s two major parties has begun with just under two years before Malawi goes to polls.

As days go closer for ordinary Malawians to be very important in the eyes of politicians, the verbal wars are expected to intensify.

247 thoughts on “DPP suffering from Mia fever

  1. tisamanamizanepo apa za awa a Mia. Mia has no muscle to wrescle with APM and Chakwera should not raise his shoulders high because of this nonentity screwed politian. MCP nthawi yake inatha ndi kamuzu. palibe angaiwale nkhanza zojse zokwe anapanga agalu amenewa. kudyetsa anthu ng’ona, kuotcha nyumba za anthu mkumati akuwukira kamuzu, kulanda ziweto ndi katundu osiyanasiyanaa. Ask MR Majiahen Gondwe from Rumphi. MCP iinawalanda ma truck ndi zigayo zawo zonse. ma truck 17 plus zigayo 24 kumati akupikisana ndi kamuzundiye iwe lero uziti Kwachakwacha? kunja kunacha kalekale ndi Bakili Muluzi. inu mumawasiya anthu mundima mkumawanamiza kuti kwacha. panopa anthu anayera mmaso ndi Atcheya 1994 ndipo inu mpatanso wanu oti munganamize anthu anyani inu unatha. thanks to Bwana Tcheya powatsekula anthu mmaso. muzathra kotsutsa komweko. enanso ndi awo alandila 11billion yoti apangire campain kumbuyo kwa wina hemwe kachipani kake kakanizidwa kupanga register. ndiye kuti kumpotoko kulinso chipani chomwe chizapikisane ndi MCP pogawana mavoti mufune musafune. pomwe kumwera Mia sangamake ndikwa DPP chipani chokondedwa ndi gulu la ma million a anthu. ask Joice Mtila Banda, anagwetsedwa ali pa chiongolero. chipani kuluza chikulamulira tinaonera pa A Mayi. and chinawina ndi chipani chomwe chinamangidwa atsogoleri ake pomwe chakwerayo ankayenda momasuka koma analuzabe. muziona. ulendo uno chakwera azapanga resign kuti hasi wachisiya chipani chamagazicho

  2. KKKKKKKK ENA AKUTI KWAWO NDI KUDYA NSIMA BASI NDICHIMENE AMAZIWA KKKKKK ALOMWEEEEEEE NDI KUDYA SUNGAWAPOSE HEHEHEHEEEE WANDISEKESA KWABASI IWE MLOMWEEEE NDI NGOLONGOLIWA PAJA MUNAPHUNZILA KWA MFUMU WANU NGOLONGOLIWA KUTI MUNTHU AMAFUNA NSIMA BASI.

  3. munthu aliyense ali ndi mbali yabwuno ndi yoipa, if u critise mias decision, what have you done to this nation which has bring a change to life of Malawian citizens. malawians will remain poor minded if you dont think positive than critising. Ngati akupanga ziganizo zolakwika bwanji inu osapanga za nzeru nafe tioneko luso lanu. Ndi nthawi yawo just watch vote is 2019

  4. Malawians lets start thinking postive enough,yes mcp inali khanza zimene ndimanva not kuona,zimene ndikuona ine ndi ifa ya Rhobert Chasowa, Isaah Jaunju from ACB,21 pple on 20th nully 2011,wina nkumanenabe kuti amalawi akufunabe DPp,are you sure?? kalikondani dziko lanu posatengela chipani,ndizonvetsa chisoni kuti winawe untha kuima poyela nkumati dpp 2019 boma malingana ndimmene amalawi tikunvutikila,kapena mwina pali chimene mukupeza mukamasapota dpp yo,but in normal thinking capability Peter Mutharika with his Government is not helping Malawians.poti ati amalawi ndife zitsilu koma ZITSILU ZEDI ndi pitayo ndi masapmasapota akenu.

  5. fish always rot from head’ For MCP to win 2019 election please change the name

  6. You are a political giant if you are loved by many and you switch from one political party to another if you are losing support the guy is losing support in the lower shire. The guy is losing the support he had in 2008 and i would do the same if i was a politician

  7. I don’t think DPP worries with Mia.Mia has no political influence in Southern region. Besides, MCP has no value in Malawi politics. We can’t go back to Party that killed Malawians like chicken. The party that jailed thousands for no reason at all.We can’t delete history because history helps us choose good direction.

  8. Nonsense APA what will all this take us to we Malawians always vote for candidates who have nothing to offer but something to be offered,its not the leader who got a problem but the system

  9. ZIMANDIDABWITSA NDALE ZA KUNO KU MALAWI TIMATSOGOZA ZOIPA ZA MTSOGOLERI ALI YENSE NDIPO NGAKHALE ADACHITAPO ZABWINO ZANJI TIMAIWALA MUNTHU AKALOWA CHIPANI CHOLAMULA MUKUTI NDI WANZERU KOMA AKALOWA CHOTSUTSA NDIYE KUMANGOLALATA TIKATI TIFUFUZE ATSOGOLERI ONSE OMWE AKHALA AKULAMULIRA MDZIKO LINO NDI OMWEWO OMWE AKATSOGOLERA CHIPANI CHA MCP NDIPO NGATI KUDALI ZABWINO AMAPANGA NDI OMWEWO NGATI KUDALI ZOIPA NDI OMWEWONSO AMATSOGOLERA TIYENI TINGOKHALA OKWEZA DZIKO LATHU OSATI KUMANGOTAYA NTHAWI YONGOMALALATA.

  10. Nonse A Dpp Mungamaope Mun2 Modz Bac This Seemz Kt 2019 Muluza Ugalu Wanu A Dpp Palibe Comwe Mukucta Mu Zko Muno Nchto Matma Bax At Ndinu Ophunzira Zanu Zimenezo Ndie Muone Cpan Caxala Ckuopsa Ndi Mcp Bax, Munyabeee

  11. COMING OF MIA TO MCP DO NOT MEAN THE POWER TO DEFEAT.MEAZUNGULILA MITU?AFTER KAMUZU DIED NDI CHANI CHIKUPHULA MCP STURPTFUL

  12. Dzenje ukaliwonera patali imakhala ngat advantage koma ukalumpha mwachangu imakhala disadvantage as apa nde umakagwelamo mwamphamvu than mumene zikanakhalira poyamba.Iwas a supporter of MCP during 2014 elections but the party seems not to reason about their repeatitive failures.Concetrating in the Northen region is just wastage of time.Does Chakwera think that northeners will still support him if Joyce Banda can return today?,,,He can’t even reason why DPP doesn’t care about his offensive campaign in the north.

  13. Mcp singawine, mwasiya kukamba za R.Msowoya after calling him Lebwedelebwede.yudas Chakwera wagulitsa chipani.

  14. Kkkkkkk mwati nthenda ya disease ikudwalidwadwayo kwa suffering ndi SIDIKMIASIS? Kodi ndi virus ya kachilombo kapena protozoa yakanyongolosi? kkkkkkkkkkkkk nde kodi ilibe medicine yamankhwala?kkkkkkkkkkkkk

  15. They haven’t seen anything yet.
    Come 2019 there will be more DPP supporters, cadets,MP’s and more people from the Southen Region joining MCP.
    Yanyamuka.

  16. IFEYO NDI MCP BASI , A DPP MNAWINA 2014 KAMBA KOBERA MAVOTI M’MWENYE WANA A SAULOS CHILIMA ANAWACHITIRA ZA MASENGA NDI MA COMPUTER, TIZAONA MULUNGU AKALORA, 2019,

  17. Mia hired Lucius banda coz he knew that anthu azabwera kuzavina dance ya ulele not msonkhano,lower states siphweketsa kkkkkkkk

  18. Mia has brought headache in MCP not in DPP if you follow politics already Msowoya, Kaliwo, Kabwila and crew have hinted on procedure of joining a party at their Mzimba rally. Cant you see this crack yourself. All along you have been saying Gustave Kaliwo is a DPP inculcate but its clear now even Msowoya supports the SG in calling for a convention whats that in MCP SIDICMIASIS as one has wrongly diagnosed it in DPP yet its symptoms are clear in MCP as articulated by various speakers at the Mzimba rally.

  19. ndie zakuipa kwanu akunena ndan? chotsan kae hitsotso chanu mmaso mwanu ife timakudzwan koma stkamba zanu coz ifeso tiri ndizovutaso bwanji mkuopa mia coz mukanakhala kut smukunjenjemera simukanatanganidwa kumaipitsa mbiri ya mia. manyaz bwa!!! mulibe?

  20. dpp is a party good for all Malawians.what happened after bingu death.the madam sworn in.she was ill advised.devalued the kwacha, prices of goods skyrocketed. inflation rose to double digits.due to poor policies some people took advantage of loopholes stole money in billions. the international community lost trust and left with every support ceased both financial and technical. the civil service had no direction and service delivery stalled up to the extent that mortuary at central hospital broke.MIA was part of that team.Malawi cant trust that man.he is part of that failure. not all is well now but atleast we have a direction and power is there at sanjika .palibe akuti fwee! ! ndi chaponda yemwe kumangidwa.thats a good record on rule of law or unselective justice. food is available due to good and sound policies. dpp ndi machine.mcp ndi mwana

    1. ubwere kuno kumudzi udzaone mmene mulimi akuvutikira. ukuganiza kut mulimi agulitse 7 bags of maize just for one bag of fertilizer? ndie ma good policy alikut? kumaganiza kaye musanalembe kalikosepse

    2. what if the price of a bag of maize could have been at 12 thousand kwacha? good for a farmer eeeeh but in the other way bad for the country.chakudya chadula.in certain districts people starts dying becoz they could not aford to buy maize.fair prices of agricultural goods always hurts the producer but good for the country .food kirk starts dedevelopment. sankhani commercial agricultural produce yina.soya or tobacco. fertilizer subsidy main core is for country food sufficiency and security especially maize.evance no kupha ndalama on maize.sorry but pitilizani kulima bro.chuma chili mu soil

    3. awuze ben.zina zimaoneka simple .example kamuzu failed to give us identity cards and we ended up absorbing millions of Mozambique people as Malawi ans.a big hand for dpp.what about fertilizer subsidy. cash transfer. miseu and other developments.people have brought cars and buses becoz of dynamic policy strategy of dpp.its not simple. hail dpp

    4. Mmmm ine ndiye cndinayiware or pang’ono pp mene imalowa kunali kulibe chilichonse ku malawi kwathu kuno, Mafuta agalimoto, magetsi, mankhwala just mention afew koma Mzimayi uja anayesetsa zina kumayamikirako posatengera chipani. aon

    5. anayesetsa chiyani ? selling a plane to buy maize ? devaluing the kwacha to please the imf and world bank and later abandoned her due to cash gate.its easy to run a govt on short term the way she did but in the long run you suffer.the prices which went up due to the devaluation are felt so badly bu the people. mafuta was an issue of a secret sanction by a few greedy foreign ers who wanted to rule from behind .za mankhwala iiii you are lying.magetsi its a problem which even now needs massive investment. these to you chimonbo if you understand the political language

    6. Auzeni amenewa sakumudziwa mkaladi ameneyi sangawine 2014 analephera kumpangira kampeni mbare wake timangopita kukalandiramo ndalamazo basi tizidyadi koma dpp ndi boma 2019 basii

    7. Food is not available due to DPP policies but good rains….boma lopanda any real direction/goal misewu ikumangdwa ya substandard funded…zot even private sector z being affected sukuona ayi??? Tpt fares unjustifiably hiked and the fair trading arm kuli zzzzzzzzzzzz ma politicians anu omango2kaaba

  21. Mia is not a threat we know him even when cattle were distributed but pipo bouted them all MCP inclusive due to doublefaces and indecision and easily carried away with Naira

  22. Mia,isn’t a heavy weight in terms of politics at all,i wonder there is alot of noise some are explaining more about what happened in zambia,don’t forget you are here in malawi,we need all of us to be calm enough to see what is going to happen.Mcp it has been out of government for several years,even john tembo himself he has been failing to gain power with his party into government.Nobody wants mcp to rule again this country.Chakwera lost the game last time let’s wait and see if he is going to qualify just because of mia. Mia is just another kid and he can’t do any surprise,completely he’s too young.

    1. I am a fan of MCP, may u please take out that mind ( nobody wants MCP to rule this country again) is that democracy??? Do you know how many millions of Malawians voted for MCP last tripartite election?? A Malawian but u still don’t know that MCP is main opposition party in the house. Who voted MCP to be on that position, if nobody wants MCP again?? Wake-up, if you sleeping and ask those they can teach you something

  23. Bawawatani Pakuti Masiku Akusadziwa Mulungu Analekerera, Chomwe Ndikudziwa Ndichaku Ndi Yesu Khristu Ekha Amene Adzadzetsa Ulamuliro Okomera Anthu Onse.salmo 146 vs 3 -6, akt musamakhulupilire zinduna kapena mwana wamunthu amene mulibe cipulumutso mwaiye…..achakwerawo alinso ndi zofoka zawo mwinanso mudzalira mkumati bora kare. remember chakwera ndi yona walero amene wathawa ntchito ya Mulungu, chenjerani mudzaona ngati wakupatsani ndi Mulungu Ciri Ciwiya Ca Satana

  24. Who in his right senses can vote for DPP again. A party of thieves and gluttons.

  25. Southernerz Are Well Organised Unlike The Centrollerz And The Nothernerz, I Dont Think That The Southernerz Azabetsa Utsogoleri Wa Dziko Kuchigawo Chapakati Or Chakumpoto. Had It Been Apakatife Tili Well Organized Ngati Akumwera MCP Ikanawina Kalekale, Koma Tinagawanika Kalekale. The Coming Of Mia Will Bring Absolutely Nihil To Mcp Politics. Mark My Words!! We Will Hear “ATIBELA REMIX PART 5,” In 2019.

  26. End of Dpp in lowershire ,muone by election tikukhadzuleni kuti mudziwe zoti sitikucheza ask Regional chairman for south akuti ngati mcp sidzapeza ma mp oponsa 30 ku south adzatula pansi udindo .Even kasaila sadzawinanso believe me

    1. Zazii Mia wabwera lero pamene amawina kasaila iye kunalibe sanapange campaign Lower Shire kuli anthu angati ndiye bwanji sanamuwinitse Gwanda? Kadyani nayo chaje ndalama

  27. ife kuno kuno kumzimba sitikufuna munthu wina aziti ndine wa Bpppppp,tizakugwirani Pakhosi.Mesa Mumat Mugula Chimanga Mpaka Lero Kuli Ziii Muma Admarc????? Mwatikwana Mwamva?

  28. ndale zakumalawi kumadzitsata ndibwino,paja aliyese amavotera akwao.za achaponda mukuziwa kale anaotcha CV,chilima sakumfuna amkat mwachipani,aja munapha anthu 20kumpoto aja? chasowa,njauju,yapabingu,anthu inu mavote anu ndi amene munapha aja mwamva eti? atsalawa ndi aife aFORD KKKKKKKK

  29. Every national election we say mcp boma from 1994 up to now. Which boma are you talking about? Lets start thinking positive. Dpp is the only party survive without season

    1. ln Senegal, theŕe was an opposition party which was being led by Abdulai Wade. It was in opposition for more than two decades, and it got into power when people got fed up with the ruling party. The unexpected thing can happen, have an open mind, such is life, things don’t àlways go your way

    2. Yeah who ever win will be officialy our president. Remember DPP was in opposition but manage to demolish PP in government so do u think mcp is gonna make it…..

  30. “u get twisted with someone who has jus has simple scales yet you have simple weapons to defeat..what’s that ? fear of the unknown- Bill Cosby”

    what is driving the DPP crazy lives me less desired than ever… DPP is in power ruling instead of taking advantage of their wisdom in power to facilitate dvpt projects in the country that can other wise help them gain fame nd votes. they are busy attacking someone …..who hasn’t at all twisted their wound …what’s that? by incting such attacks they are jus increasing molale to MCp…..

    I happen to wonder if DPP has wisdom to note that.its fearing the unknown

  31. There’s no suffering in DPP its only MCP fan’s who can see things in a different way he was there supporting PP what happened in 2014 DPP won now just wait this is 2017 come 2019 DPP all the way he’s there to take over from Chakwera because he knows that Chakwera will not carry the day after all its his last term and that will be the end of MCP Mark my words MCP idzaluza ndi ma vote ochepa

  32. chakwela ndi boma 2019, pitala is going to suffer heavy defeat, chakwela will won everything in northern Malawi, in central he going to won also pitala kwanu Ku brantyre ndikomwe akakuvotela not all them, kulibe zobela mavote thawi yino paulendo DPP

    1. KKKKK pitala sazawinaso ai akulephela kunena mau oti DPP woyeee, ndiye wina akuyakhula mwano pano mawu anga akufanana ndi pitala wanuyo

    2. Kodi Anthu Inu Mumafuna Kaye Chachikulu Chichitike Ndipamene Muzizati Bola Akadalowapo Wina Muziganiza Mofatsa Popanga Zithu Musamavote Kuti Poti Ndi Wakwathu Muzalira Nazo Mpaka Liti Ndiposo Mukamati Mcp Ali Ndi Mbiri Yoyipa Ali Amati Let The Past Go Sikuti Aliyese Akalowa Mu Mcp Ndioipa Ayi Anthu Ndi Osiyana Musiyeni Naya Aonese Zake Nanga Zimene Ankapanga Bingu Ndizomwe Akupanga Peter Ayi Aliyese Ali Ndi Ntchito Yake

    3. Stv Mlowoka ine siwapitala koma ndikudana zomaima pachulu mkumati ife akumpoto Pitala ku BT komweko ..kusayenda ndikomwe kuli bvuto

    4. Masamu apa avuta, ngati kulowa MCP Mia akuganiza kuti aonjezera mavoti akunama, MCP + MIA = MCP – 5 NR + 2 SR. The guy will facilitates high deduction of votes in the north as the favourite their is msowoya. mcp will gain popularity in only CK and NE not the whole south. believe me.

    5. Bvutotu apa lagona pa atumbuka akufulumira kuyankhura kuti ku bt kwanu komweko nkuona mulibe chitukuko cholodzeka mumalimbana ndi mitunda yopanda madzi osadzimvera chisoni Mia mukunyadirayo ndi wakummwera chakwerayo ngwapakati inu mukhala choncho atumbuka north Dpp 50% central Dpp 50% and southern Dpp 100% ngati ndikunama ndiudze chigawo chomwe chilibe phungu wa dpp ndiye muone mcp kummwera ili ndi aphungu angati?

    6. DPP wont be affected in the Lower Shire. There was late Gwanda Chakwamba but DPP remained unshaken and won elections from opposition. DPP will make it in 2019.

  33. Zilimbanani Ife tili busy kuchepetsa umphawi wathu ndipo ndi Yesu yekha yemwe adzabwerese kusintha ndi mtendere wamunthu osati andale,

    1. Dikila choncho adaliposo ena ku zambia amanena choncho pano adazindikila otsutsa atapambana chisankho chosecho nthawi imeneyo president Lupia Bwezani Banda sankayembekezela kuti angagonjetsedwe

  34. U must research first if mia is ahevy weight in chikwawa and Nsanje,osamawerengela mbewa ndimichirta yomwe.the low mind ppl wil multiply while the wise men are silent.

    1. It’s very hard to preach MCP in the southern region am telling u . MIA CAN ONLY WIN THE HEARTS OF WEAK PEOPLE FROM HIS NKOMBEZI TERRITORY . not further than that

    2. Jah the bigger judge. muziti mulungu akalora tionana mawa. the future of this country lies in the hands of the most high not chakwera, not mutharika, not atupele and not Mia but chisumphi so stop the grandiosities

    1. For you nothing change kuchoka kwa akuba kubwela kwa abwino koma dziwa kuti ku Zambia Lupia Bwezani Banda adagonjetsedwa ndi achipani chotsutsa udziwe zimenezo

      1. You seems like you work with MCP eeee man akutumani kuti muzilalikira za mcp or mimadya nawo let me remind you it was mcp that lose from opposition in 1994

  35. Omwe musapota mia is bkoz you dont know how bad this man is…watengatenga minda ya wanthu….mkumadyetselamo his cattle.

    who ever sells ng’ombe kwa mia has to wait for 90 days to be paid …..yet in halves.
    Just remember mia ndi mwenye wa ku india.
    M C P .will loose northern region ngati angaganize kuti mia akhale running mate.

    1. Northern region doesn’t belong to one single rapporteur.Nobody should deceive you.We hate politics of idol-worshiping.Had it been so Kamlepo a man who has fought national battles would have carried the day.

    2. #A LIAR!Tell the victims to go to court and have their land back from Mia!Visit #Ndata farm today!You will be surprised with Bingu’s Hectrage.Ndiwe Mfana kayamwe uko!Shame!

    3. ngat Mia ali mmwenye waku india nchifukwa chani boma la dpp linamupatsa unduna m’mbuyomu. apa zingosonyezeratu kut kalulu akakuthawa umamunyoza kut samakoma chonsecho pansi pantima ukudziwa kut ukanamugwira ukanakamwera nsuzi

    4. #A LIAR!Tell the victims to go to court and have their land back from Mia!Visit #Ndata farm today!You will be surprised with Bingu’s Hectrage.Ndiwe Mfana kayamwe uko!Shame!

    5. It means you dont know how the tumbuka oparetes.
      Nsanje and chikwawa ndi maboma ofanana zochita ndi kumpoto.
      Mia is not a heavy wieght.

    6. Akulu lowershire njomvana..
      Since 1994 mcp sidawinepo mpando..
      Kupatulapo nthawi yomwe chakwamba adali ku mcp.

    7. So is Chakwamba’s time before 1994,thats why somebody says you should be too young to understand these issues.People are just weary of this Diphiphi’s maladministration.

    8. Ili ndi bodza la nkunkhuniza. Mia has vast land which he and his family legally acquired. He is in beef business ans buy cattle from small scale business people. Yes he doesn’t immediately but there’s a reason why people still choose to sell ther cattle to Mia.

    9. That’s how all politicians do, go to MJ mulli, the munthalikas and all of them in ruling or opposition go in their areas, you ll find same things

    10. Kayiya ………
      Zikuwonetselatu kuti inuyo siochokela ku lowershire.
      Dziwani kuti chiyambi chopasukilatu chipani cha mcp mkumuyika mia vc president.
      Anthu pano adakalilabe minda yawo.

    11. Apa zikuonetsa kuti ena muli mbali ya akuba pamene ena muli mbali yabwino kwabasi kwa inu amene muli pa mbuyo pa mbava dziwani kuti nthawi yanu yakuba :a Billion yatsala pang’ono kutha kuzambia kudali president Lupia koma adaluza ndiye ena musamanamizidwe kuti boma silimaluza ilo ndi lankunkhuniza bodza

    12. ayi wabodza iwe munthu wa ku india apezeka bwanji ku malawi? zasankho basi,komanso munthu sangalande munthu munda popanda dongosolo la boma amene analandidwa mindawo apite kwa Dc akawafotokozele zimenezo

    13. Mia sanalande malo anthu musamunamizile ndiemwe chikhulupililo chathu chili pa iyer amwene kulowa kwa mia ku mcp dpp misonkhano paluponse aona chani uoooo

    14. Waipa Coz Walowa M C P Muja Anali Ku D P P Simumanena Zonsezi Bwanji Mwayambakale*2 Kunjenjemera Anangomva Mia Abwera Lero Njenjenje Kunjenjemera Kkk Dpp Sidzamva

    15. Zowona dpp ikunjenjemela but pa political floor MCP Ndikhombwani.
      Mdamva dpp mpaka kuyamba hospital project ku makhanga ya 1billion.
      Kkkkkk .

    16. It doesn’t make any sense with ur comment,just know that DPP has now sinking becoz of that good decision for Mia to join us.Simunati apapa zangoyamba hehede uluu.MCP tikubwera komko mwatikwana inu adpp kuba,katangale,kupha.

    17. kodi kupha mukunenako kwa dpp kuli pati kufa kwa mbava kumpoto mukadzidandaule mwina enanu munali ana fusani makolo anufe mmene tinabvutikira ku malawi,kutilimitsa CCAM kodyela ndalama osakuona plot yokupha ma bishop achiloma,kuphedwa kwa ulendo wa gadama mwina bvuto sakuudzani makoli wanu zinali muno ngakhale nditadya njinga sindingavotere mcp ndipo ndikubwera kudza sikita 2019 ino tambala ameneyu

    18. Nanu inu #mcp ndichipani?. Chifeleni #Kamudzu tioneseni kapena tiuzen chitukuko chilichonse chomwe chipanichi chapanga mdziko lino kupatulapo chitukuko chowotcha galimoto ya #Jessie #Kabwila kumenyana okhaokha kumukakamiza #John #Tembo kutula pansi udindo china m”cha?.

    19. Iwe MALUNGA ukuti MCP ndiyakupha wayiwala kuti Dausi adalimkulu wapayaniya ndiye amkatsogolela nkhaza? komaso Bakili adalindi udindo waukulu muMCP gulu limeneli ndilo limagwila ntchito ndiTembo zoyipa.

  36. Mutharika with his Dpp has nothing to offer to Malawians.He is a failure in all sectors of life.A poor planner,bad performer,Corrupt and arrogant!

    1. #Dalitso that is a very good question my brother. Agalu amenewa amangodziwa kunyoza, kususa but akulephela kusamala mabanja awo koma busy kulimbana ndi anthu oti zawo zinayela kale

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading