The Nkhotakota first grade magistrate court has fined a man for encroaching into Nkhotakota Game Reserve and cultivating cannabis Sativa locally known as Chamba.

According to Nkhotakota Police Public Relations Officer Sub Inspector Williams Kaponda, the man, Bernado Mikayele, 32, has been convicted and ordered to pay a fine of K40, 000 or in default to serve two years imprisonment with hard labour for illegal entry into the game reserve.
He has also been sentenced to pay a fine K200, 000 or in default to serve 6 years in prison for cultivating Chamba.
If he fails to pay the fines Mikayele will go to jail and serve the sentences concurrently.
The convict hails from Kapelura village, Traditional Authority Kapichira in Kasungu.
141 thoughts on “Man fined for growing chamba in game reserve”
Comments are closed.

Zopusa
Kod boma limalimbana ndi chamba chifukwa chani?azilimbana ndi zinazo kom mbali yokhayi ndiy ai xiku lina tizaukura ndithu ngati oxazitenga bwino coz tinatopa nanu a boma mukumva!!!
Achamba ndefdilu ndi kunena pano ndapangakale 500.000 odana ndi chamba ali forkolo farken labch
Achamba ndefdilu ndi kunena pano ndapangakale 500.000 odana ndi chamba ali forkolo farken labch
Rasta man food
sanalakwe chamba ndi game ndipo ndindalama iiiiii kusiyana ndikuba aaaaa!!!! Walakwa chani?
sanalakwe chamba ndi game ndipo ndindalama iiiiii kusiyana ndikuba aaaaa!!!! Walakwa chani?
Chamba ndi deal heavy fodya sakuyambapo let us try season ya mawa alimi a fodya asalimeso 4dya insted alime Ganja ucan see dora zomwe Mw ingapeze bt government kukhomerera……… work up just legaliz it Mulugu sanalengepo chinthu chopanda ntchito. muli chuma mu Chamba bt we cm like we r short sighted
nde chamba chokhachokhacho ine ndalima changa mubwere muzaone Kasungu panoso chidayamba mphonje
May be he want to recoved our economy for the next season kkkkkkkk
May be he want to recoved our economy for the next season kkkkkkkk
nde yake
nde yake