Green maize sale banned!

Advertisement
Green Maize Malawi
Green Maize Malawi
Green maize sale banned.
(Photo credit REUTERS/Philimon Bulawayo)

Blantyre City Council (BCC) has banned the sale of green maize in the city effective Thursday February 18. BCC announced the ban through a press release and said the business of selling fresh, cooked or roasted maize has been banned with immediate effect.

The council has since warned residents to strictly observe the ban, saying anyone found selling maize in the city will be prosecuted.

Residents have also been reminded through the statement that the council has laws that need to be followed by individuals in the commercial city.

The constitution of Malawi gives power any council in the country to make by-laws and enforce them.

Early this year the ministry of local government issued a directive banning sale of green maize in gardens, especially this time when the green maize is ready for consumption.

Advertisement

56 Comments

  1. Kuletsako kti tikhoza kutenga matenda anji ngati ku south africa botswana akgulisa inu mutiuza chan? The problem inu andale kuno kmalawikuno athufe mmationelera kwambiri ambiri akdyesa ma banja awo busnes yake yomwey mukango khuta sausange basi kuyakhura zakukhosi kwanu mxiem #simuzaionaso8vote yanga

  2. Kuletsako kti tikhoza kutenga matenda anji ngati ku south africa botswana akgulisa inu mutiuza chan? The problem inu andale kuno kmalawikuno athufe mmationelera kwambiri ambiri akdyesa ma banja awo busnes yake yomwey mukango khuta sausange basi kuyakhura zakukhosi kwanu mxiem #simuzaionaso8vote yanga

  3. Every year amaletsatu mumunda chikakhwima chimanga ndipo zidayamba kalekale monga ine wamu lilongwe city kuva izi sizachilendo ndipo ukangopezeka a city council amalanda,,,

  4. Every year amaletsatu mumunda chikakhwima chimanga ndipo zidayamba kalekale monga ine wamu lilongwe city kuva izi sizachilendo ndipo ukangopezeka a city council amalanda,,,

  5. Inde mwina tikolola ; zimakolezera kuba kwambiri mma 7koloko usiku kupeza munthu akutuluka mkanjira ka kochokera ku Wainela kupita ku Mbayani wasenza chithumba ; sungamfunsenso kuti mwatengacho nchiani mantha. Kukacha eni minda mumva akulira chabedwa

  6. Inde mwina tikolola ; zimakolezera kuba kwambiri mma 7koloko usiku kupeza munthu akutuluka mkanjira ka kochokera ku Wainela kupita ku Mbayani wasenza chithumba ; sungamfunsenso kuti mwatengacho nchiani mantha. Kukacha eni minda mumva akulira chabedwa

  7. Ndizoonadi ineso ndagwilizananazo asiye chifukwa zimabweletsa njala mdziko chifukwa muone kuti ndi matani agati mumadya chimaga chootcho or chompika naga atamati azidikila kuti akolole bwezi anthu avutika chonchi? Ine chaga mchisoni kwaana abadwawa adzaona moto walu lu lu lu!!!

  8. Ndizoonadi ineso ndagwilizananazo asiye chifukwa zimabweletsa njala mdziko chifukwa muone kuti ndi matani agati mumadya chimaga chootcho or chompika naga atamati azidikila kuti akolole bwezi anthu avutika chonchi? Ine chaga mchisoni kwaana abadwawa adzaona moto walu lu lu lu!!!

  9. Apo mwateta njara yiriko ndipo yizankhrako asiyeni anthu agule ndi kugulisa mwa ufulu bola chinkhare chosaba, malawi is democratic country

  10. Apo mwateta njara yiriko ndipo yizankhrako asiyeni anthu agule ndi kugulisa mwa ufulu bola chinkhare chosaba, malawi is democratic country

  11. Mwayamba khuyu eti chimanga chinayamba kuochedwa nthawi ya JOHN CHILEMBWE nde mukanene lero kut faz isiye kuotcha chimanga or kuphika kumagulisa zafodya eti ngakhale dziko lomwe timadalila kopezela ndalamako ku SOUTH AFRICA faz ikuphika ndi kuotcha mela.

  12. Mwayamba khuyu eti chimanga chinayamba kuochedwa nthawi ya JOHN CHILEMBWE nde mukanene lero kut faz isiye kuotcha chimanga or kuphika kumagulisa zafodya eti ngakhale dziko lomwe timadalila kopezela ndalamako ku SOUTH AFRICA faz ikuphika ndi kuotcha mela.

Comments are closed.