Teen murders abusive father in Dowa

Advertisement
Genesis Chigamba
Genesis Chigamba
Lewis Chigamba; Arrested.

An 18 year-old Malawian young man in Dowa district is in police custody for beating his father to death.

The young man, identified as Lewis Kachigamba, beat his father Genesis Kachigamba, 44, who was abusing the young man’s mother.

According to a source, on the day of the incident Genesis was drunk and was insulting his wife.

This angered Lewis who started to beat the father.

The drunken father got unconscious and died on the spot.

A post-mortem conducted at Dowa District Hospital revealed that the man died due to internal bleeding.

Lewis will appear before court soon to answer charges of murder.

Both Lewis and Genesis come from Topaizi village, T/A Msakambewa in Dowa.

Advertisement

104 Comments

  1. I think kundende kulibe facebook sakuwona zomwe mukulembazi ng’ooooooh. komanso ndi nfana ampitisa ku Mikuyu, Kachere, kapena Mpemba. azikagona pa bho kudya chimodzi modzi. mwamulila. nanga mdalayo anakapha sten-yo?. Love for His mum. koma samadziwa kut zifika pamenepo.

  2. mwanayo sanalakwe coz he was fighting for the gender Violence,so Kaliati save him

  3. Kkkkkkk Bamboyo Mwati amachita ‘Abuse’ Mkazi wao? Tanditanthauzireni mawu amenewa mu chichewa,”the Man started abusing his wife.”

  4. Osamapanga chiganizo utapsa mtima zosatira zake amakhara ma regret taona u killed ur only blood shame on u ask God to forgive u

  5. Anthu ena munabadwa bwanji munthu waphedwa mukuchita like tiyeni timve chisoni chifukwa achinyamata alero zachuluka zosuta tiyeni tiziganiza before u mark (LIKE)

  6. [READ MY STORY. ON HOW I GOT MY HIV CURED].
    Truthfully, i was tested HIV + positive for the past 8 years. I keep on managing the drugs i usually purchase from the health care agency to keep me healthy and strengthen, i tried all i can to make this disease leave me alone, but unfortunately, it keep on eating up my life. So last Two Months i came in contact with a lively article on the internet on how this Powerful Herb Healer get her well and healed. So as a patient i knew this will took my life one day, and i need to live with other friends and relatives too. So i copied out the Dr Collins the herbal healer’s contact and I contacted him immediately, in a little while he mail me back that i was welcome to his Herbal Home whereby all what i seek for are granted. I was please at that time. And i continue with him, he took some few details from me and told me that he shall get back to me as soon as he is through with my work. I was very happy as heard that from him, as i was just coming from my friends house, Dr Collins called me to go for checkup in the hospital and see his marvelous work that it is now HIV negative, i was very glad to hear that from him, so quickly rush down to the nearest hospital to found out, only to hear from my hospital doctor called Browning Lewis that i am now HIV NEGATIVE. I jump up at him with the a test note, he ask me how does it happen and i reside to him all i went through with Dr Collins. I am now glad, so i am a gentle type of person that need to share this testimonies to everyone who seek for healing, because once you get calm and quiet, so the disease get to finish your life off. So i will advice you contact him today for your healing at the above details: Email ID: [email protected] or you can also add him up on whataspp +2349036950737. CONTACT HIM NOW TO SAVE YOUR LIFE AND DOCTOR ALSO CURE ALL KIND OF DISEASE AND SICKNESS: [email protected] AS HE IS SO POWERFUL AND HELPFUL TO ALL THAT HAVE THIS SICKNESS..

  7. Let’s not judge him until we hear his side of the story. Am strongly against what he did but it will be better to look at the issue with full knowledge of the whole incident.

  8. Kma abro akanati ena apangezimenezi inumusanabadwe mukuganiza kuti mukanamuona Malawi inu? ndithuilinditsoka ndiyepopeza MWATENGELA LAMULOKUMANJA uzionawakulawatha mbale

  9. Mwanayotu ndikuona kuti amangofuna kumuphunzitsa mdalayo ndi makofi. Analibe cholinga chowapha koma kungoti mowawo wangothandizirapo. Midala inai ikayatsa imathoka bad. Amukhululukire sadzawaphanso.

  10. The boy doesnt deserve custodial sentence, he needs to be acquited, he doesnt posses an danger to the nation. He had no intensions of killing he acted out of provocation, he would nit bear seeing his mum abused always. I pity him. wish you a fair trial boy stay strong. dont let anger overtake you again

  11. Koma ameneyu ali ndi tsoka… Anzako pano tikulira, moyo ukukhala ovuta kukhala opanda bambo… Mmmm Ambuye akuone mwapadera sure

  12. Koma ameneyu ali ndi tsoka… Anzako pano tikulira, moyo ukukhala ovuta kukhala opanda bambo… Mmmm Ambuye akuone mwapadera sure

  13. Mwana otembeledwa bambo ako akulela kuyambila tsiku lomwe anakuika mmimba mwa amayi ako mpaka kufika tsiku lomwe unawapha aaaaa chitsilu chamwana kapike basi chitsilu.

  14. Mwana otembeledwa bambo ako akulela kuyambila tsiku lomwe anakuika mmimba mwa amayi ako mpaka kufika tsiku lomwe unawapha aaaaa chitsilu chamwana kapike basi chitsilu.

  15. ooooh mwana iwe amzako kusilila uli ndi ababa. basi iwe kupha dala. ambuye akukhululukile ndithu kalanga ine umasiye kuwawa.

  16. ooooh mwana iwe amzako kusilila uli ndi ababa. basi iwe kupha dala. ambuye akukhululukile ndithu kalanga ine umasiye kuwawa.

  17. Patricide, pitty! whats was wrong with ur father. Up to the extent of killing em, so bad ameneyo life emprisonment with hard labour . Inject him with parrafin azikatupa

  18. Patricide, pitty! whats was wrong with ur father. Up to the extent of killing em, so bad ameneyo life emprisonment with hard labour . Inject him with parrafin azikatupa

  19. mwana opanda nkhalidwe,kupha atate ake oti aledzela osangokawatsekela nyumba bwanji ngati amavutitsa kuti ukawathela nkuwayankhula mwapadela kuti asinthe.nanga chonchi murder case yaikodola yekha iyi

  20. mwana opanda nkhalidwe,kupha atate ake oti aledzela osangokawatsekela nyumba bwanji ngati amavutitsa kuti ukawathela nkuwayankhula mwapadela kuti asinthe.nanga chonchi murder case yaikodola yekha iyi

  21. Waisova man enafe tikulakalaka abambo anamwalira 1991 sindinawaone mmaso nde iweyo ukamawapha shame on u ngati chilipo anakulakwira osakambirananawo bwinobwino bwa?? Uli ndi soka ndithuu

  22. Waisova man enafe tikulakalaka abambo anamwalira 1991 sindinawaone mmaso nde iweyo ukamawapha shame on u ngati chilipo anakulakwira osakambirananawo bwinobwino bwa?? Uli ndi soka ndithuu

Comments are closed.