Limbe second grade magistrate on Wednesday sentenced Patrick Chapita to two years imprisonment with hard labour for stealing car parts worth K60,000.
According to Southern Region Police assistant public relations officer, Widson Nhlane, the incident happened on 5 January in Kanjedza township where Chapita stole the items in a motor vehicle and was arrested after investigations.
Nhlane said Chapita stole a propeller shaft and a starter motor and was arrested after police investigated the matter.
Chapita was taken to court on 13 January this year and he was sentenced to 24 months imprisonment with hard labour.
He hails from Tayale village, T/A Bvumbwe in Thyolo district.
38 thoughts on “Man to spend 2 years in prison for stealing car parts”
Comments are closed.

Uhummmm! Koma Malawi akumka kuti?
mmmmm nsambi a bale bola akànà vulaźa kapena kuoñonga zinthu ziña iweñso oweŕuźawe uziganizira kuti anzàko ali ndi anthu omwe amadalira iwowo
Mmmm Malawi wataika wa cash gate akupatsidwa 5months wakuba ma car parts 2yrs zakumtuuuuuuu!
wakuba ndi wakuba basi.. zake zimenezo asova.. amaba ma battry agalu amenewa
Kuba ndi kuba basi amchepesa bola zikanakhala 8
Simunabeledweko inu mungonena. There is a dferent btwn stealin 4m govt cofers n stln 4m an individual.
nde bola ukanangoba galimoto yonse
Kandalamako kachepa kwambiri very shame
Most men r dying & others imprisoned or getting mad. This is worrisome cos it is increasing no. of spinsters. No wonder prostitution is on the increase
Another Lhomwe on the prowl
Si mulandu umenewo akanaba galimoto bolaniko koma some parts aa atuluke basi
Mumvereni chisoni ndi umphawi unamutuma pajatu sikadza kokha
bola ameneyo…..sanaphe munthu kumusenda chikopa…….