Man fundraises for purchase of presidential jet

Advertisement
Peter Mutharika
Peter Mutharika
Will not use chattered jet again.

A man in Lilongwe has launched a fundraising project to raise money for the purchase of a private jet for Malawi Government.

The man, Sidney Ndembe, said the project will generate US$20 million for the purchase of a jet for the country.

Speaking to the local press, Ndembe said Malawians must take responsibility by contributing towards the purchase of the jet.

“If the government has failed it is up to citizens to do it to help their government,” said Ndembe.

Ndembe further said the project will have a bank account that will be accountable and transparent.

Ndembe said:  “The records of the money will be published in newspapers for everyone to see how far the contributions are in terms of reaching the target.”

In 2009, late Bingu wa Mutharika bought a 14-passenger Dassault Falcon 900EX presidential jet worth US$13.26 million.

However, his successor, former President Joyce Banda, sold the jet due to numerous challenges that rocked the country.

 

Advertisement

74 Comments

  1. Jet for what reasons? Agule ndi ndalama zake osati za boma. Akumayakhula kuti mene amalowa iye pa mpando anali ndi ndalama. Nanga amafuna chani? Poti dzeru zoyendetsela dziko alibenso.

  2. Ndembe watumidwa sankhapo phuzo lokuyenera plus stupid person

  3. KENDO. Bwana presdent akuyenela agule ndege ikakhala njala yanuyo iye anachita kuyipeza ndipo sangapezeke presdent wothesa njala dziko muno

  4. Vuto lofuna uprezidenti kuti basi muzinjoya ndalama za analawi ndi limenelo. Akungova matako kuyabwa chifukwa choti jet tilibe. Ndiye poti a Malawi ambiri prezident amamuona ngati mulungu

  5. This is too much now.between life and jet which iz more precious? Everytime malawi is losing her people due to medical drug shortage.then a mad man is bringing in rubbish ideas.shoul true malawians buy that? After all never will that jet be used to carry any sick malawian to hospital! Do not acumulate wealth out of poor malawians.

  6. You fail to mobilise people to do fund raising for our fellow malawians who are sturving in our public hospitals,instead u r telling us to buy jet for a billionaire like peter? He said he was already rich when he was elected, agule yekha jet akaza luza azizayendera popita kundata farm

  7. Koma malawi akupia kuti? How can you form this nonsense project while our ship is sinking no hospital drugs no food in hospitals even homes school adjustment no import of goods no money securation then you want to buy jet who is going to pay parking do you know what you are talking because man of God has two jets so is paining you why can’t your professor nil down to Bushiri anf berge for one or borrow if he needs respect dony forget that from his mouth hr sayd is a billionaire be4 he enter government let him buy one which he will take it after retirement

  8. Ndalama mwaba kale mukufuna kubwatika ndani.Kaguleni ndegeyo.Koma onse aja mwawamanga chifukwa cha cashgate atuluke chifukwa iwo analibe phanvu yokuba ndalama za anthu inunso phanvu wazitenga kuti?Oo YEHOVA kumwamba tinvereni chifundo!AGOGO DR H KAMUZU BANDA munatisira nkhondo palibe populumukila,

  9. Ndalama mwaba kale mukufuna kubwatika ndani.Kaguleni ndegeyo.Koma onse aja mwawamanga chifukwa cha cashgate atuluke chifukwa iwo analibe phanvu yokuba ndalama za anthu inunso phanvu wazitenga kuti?Oo YEHOVA kumwamba tinvereni chifundo!AGOGO DR H KAMUZU BANDA munatisira nkhondo palibe populumukila,

  10. Zamkutu. We have more pressing problems in Malawi. Malawians are suffering -no basic necessities. The jet is very very far from being a priority for Malawi. Stupid idea from an idiot who just want to get cheap publicity.

  11. Our country is now becoming a BANANA REPUBLIC whereby its citizens are treated like foreigners and foreigners are treated like citizens. Shame on our country

  12. Why not to fund raise money to buy food for our hospitals where poor patients are dying in the hands of no mercy government.

  13. Kufuna muziti athu anasokha ndalama zandege ngati timalephela kudula ticket ya BB ndiye yogula ndege tikwanitsa bodza limenelo usatiyike phula maso ngati akutuma plz give us some air we are tired of the Muthalikaz the bandaz Muluzis better Kamuzu eis

  14. KUSOWA ZOCHITA ETI BWANJI NDALAMAZO OSAGULIRA MANKHWALA MUZIPATALA OLO KUGULIRA CHIMANGA ANTHU AKUFA NDI NJALA

  15. Munthu wanzeru zake amene sanapengepo,angatenge madzi mu cup kumatira munyanja. Osamapusitsa amalawi anabadwira m’mavuto,anakulira m’mavuto asiyeni apume.PLease give them some fresh air!

  16. A Ndembe kodi mwazungulila mutu eti? kapena wakutumani ndi bwampini yo? inu athu akuvutika ndi njala mankhwala mzipatala muli nde azikasokha ndalama za ndege malo moti muyambitse fund raising yoti mugulile mankhwala mzipatalamu nosense

  17. We wil contribute generously towards this as people are dying of hunger in hospitals, rural areas, prisons and all over, no drugs in hospitals, no ambulances, making women delivering in minibuses. So I really belive that shallow minded ppo like us wil contribute to this. Especially civil servants like me whose salaries are still peanuts dispite promises by our geneious leaders to raise salaries, some going without leave grants until now. And perhaps business people will contribute more, whose goods are heavilly taxed in borders, kwacha depriciating mercilessly against foreign currency. So lets really contribute generously to the president who has millions in dollars in the US. Share us the acount number so we can deposite the hardly earned cash towards the purchase of the jet.

  18. We wil contribute generously towards this as people are dying of hunger in hospitals, rural areas, prisons and all over, no drugs in hospitals, no ambulances, making women delivering in minibuses. So I really belive that shallow minded ppo like us wil contribute to this. Especially civil servants like me whose salaries are still peanuts dispite promises by our geneious leaders to raise salaries, some going without leave grants until now. And perhaps business people will contribute more, whose goods are heavilly taxed in borders, kwacha depriciating mercilessly against foreign currency. So lets really contribute generously to the president who has millions in dollars in the US. Share us the acount number so we can deposite the hardly earned cash towards the purchase of the jet.

  19. Thats bullshit… If the proceeds for the other jet are not yet known, what the hell you so called patriot??? Akutuma ndani? You think Malawians are that stupid to support your mockery ideas????

  20. DPP yaba kale misonkho yathu ndi iwenso ukufuna ubere m’malawi amene ali wefuwefu kusakasaka madzi abwino, kandalama koti apitire kuchipatala, schl fz ya ana atatu, agule 23:21, alipire lent, alipire magetsi and agule ka suger koti mawa aphike kaphala ka wodwala poti muzipatala zaboma sakudya pamwamba pazonse iwe ukuti chani? Mesa apulezitenti ndi achuma kale adatero! tenga zako ndi zawo zambirizo muphatikizane mugule jetyo ife amalawi tidzakuthokozani mpaka kale!

    1. Man, mwayitha coz magetsi,madzi,misokho,feez komamso mzipatala zaboma tinayamba kulipira kenako mwati ayi zachepa koma tiyende m’makomo mwawo tisokhetse ndalama zogula jet.kodi mukufuna mpaka tiyambe kuvala masamba amitengo?ndalamazo mukasokhetse kwa pitala yo ndi nduna zake komanso amphungu ake coz pakali pano ife a malawi we r jst lyk needy pple.go 2 hell nt 2 us.

  21. Mwayambapo a DPP. Another cashgate. We know like Lutepo,u steal and contribute.

Comments are closed.