Chaponda achoka chothawa ku Mulanje

Advertisement
chaponda george chased 1
chaponda george chased 1
Anthu aku Mulanje kuthamangisa galimoto yomwe anakwera a Chaponda.

Nduna ya zamalimidwe dzulo lolemba pa 29 August inaona mbonaona pomwe gulu la anthu mu boma la Mulanje linamulumila mano ndi kumupitikitsa mu bomalo.

Ndunayo, a George Chaponda, yemwenso ndi phungu wa nyumba ya malamulo wa mu dera lina mu boma lomweli la Mulanje anapita mu bomalo kukayendera ntchito ya Blantyre Water Board yofuna kupatutsa madzi kuchoka ku Phiri la Mulanje kuti anthu a ku Blantyre ndi madera ozungulira azipulumukilapo.

Chaponda, yemwe anthu ena akuti chipani cha DPP chikumulinganiza kuti azakhale President kuchoka kwa a Peter Mutharika, anapita ku deralo zitamveka kuti anthu ena a ku Mulanje akukana zoti achotse madzi mu Phiri lawo.

George-Chaponda
A Chaponda anayenda wa uyo-uyo.

Iye analimbitsana mtima ndi mlembi wamkulu wa mu unduna wa zamalimidwe, a Erica Maganga, pamodzi ndi phungu wa ku Mulanje Pasani, a Angie Kaliati, kuti akamveledwa akapita ku deralo.

Zodabwitsa zinali zoti anthu atamva kuti kukubwela akuluakuluwo, iwo anathamangila ndi kutseka mseu ndi miyala ndi mitengo kuti galimoto za wofowofo za akuluakulu abomawo zisadutse.

Atafika a Chaponda ndi anzawo anatutumuka anthu atawapitikitsa ndi kuwauza kuti ngati akufuna kupatutsa madzi mu Phiri lawo, ayambe kaye adzala mitengo mu phirilo komanso awapatutsile ena kuti iwo azimwa.

Zitafika povuta, galimoto za a Chaponda ndi anzawo zinatembenuka, kubanduka ulendo wa komwe anachokera.

Advertisement

104 Comments

  1. Hello my name is john I want to give a testimony about my HIV virus that was cured by a great spell caster. Since last 4years I have being a HIV AID patient. I never think I will live long again and am so grateful to Dr sule who help me cured my HIV AIDS last 3 weeks. I was in a great pain so I told one of my best friends; he told me that there is a great spell caster that can cure my VIRUS. I asked him if he had his contact, he gave me his contactl, I contacted him he talked to me and he perform the necessary things and sent it to me through corrier delivery company and deliverd to me at my place and he told me that after two weeks I should go for a test. Which I did, when the doctor told me that am now a HIV negative I couldn’t believe myself I went to see another doctor the result was still the same, I was human on planet earth, so I emailed him and thanked him. Please if you are having a similar problem please visit him/contact him via whatsapp +2348162447651

  2. Ine ndimaganiza KUTI alomwe ndi atulo koma apamwatha a thamangisidwe batsi galuamenewa atikwana mzimonokwambiri AmalawiTiyeni TiyeniTipangechimozi pothane ndi AGaluWa

  3. Dzuka malawi Dzuka amona ngati amalawi tikugonabe hahahahaha heheeeeee mpaka duna kumaziphwisila ikuthawa kkkkkk mbava zimenezi tizazinyelele wasala mulongo wake uja wa khope ngati gule wamkulu timamunchula kuti maliya azazionenaye

  4. Amutham angitsa mwina analibe passport yolowe ra m’dziko limene li, tisaiwale kuti Thyolo $ Mulanje akuti ndi dziko loima palokha. Ulendo wina asa dzaiwale kutenga passport.

  5. Loko ikukwaneni tilankhulabe basi Kaya ndimalume anu muya nayo basi Tsopano wasala peter muthalika yayonso wagijimeko pang’ono wanyanya kudelera ameneyu, Mwava guyz tipange zimenezooooo

  6. Kumeneko ndiye kubwela osamunyengelera galu ameneyo kwamake akanene wasala iwe uti mphuno bii! Pamenepo bokosi takhoma kale paulendo.

  7. mwaonesa chisanzo chabwino inu anzathu akumulanje kwanu komwe chode amalawi anthuwa atidyera mokwanira zimenezi chonde zipitilire mpaka zikafike kwa che mtalika wo abweze zathu basi nthawi yakwana paulendo onse basi

  8. My name is Samuel Tapologo and this a testimony of how i became HIV NEGATIVE, i never thought i will be totally cured from HIV/AIDS, i have been suffering from HIV for some years, i have spend a lot of money finding cure for HIV/AIDS until i found this true man who cured me completely with his powerful herbal medicine, i have tried different means to get this virus out of my body, all the possible ways i tried did not work out for me, i came across doctor olumo through some amazing testimonies concerning how Dr Olumo has cured different people from various kind of sickness most especially HIV/AIDS with the help of his powerful Herbal Medicine, so i was encourage and i contacted Dr Olumo i told him about my Sickness, He told me not to worry that he was going to prepare some Herbal Medicine for me, after some time in communication with Dr Olumo he finally prepared the herbal medicine which he sent to me through courier service and he also gave me prescriptions on how to use it, after taking the Herbal medicine for some days, i went for test to confirm and the result was totally negative ,i went for test again in a different hospital still the same negative , Today i am fit and healthy to live life again, I am so happy for the good work of Dr Olumo in my life, if you are having a simillar problem kindly email HIM on { [email protected]} OR CONTACT HIM WITH HIS NUMBER OR CHAT WITH HIM ON (WHATSAPP) (+2348138956767) Dr Olumo can also cure, HERPES, CANCER, HEPATITIS.

  9. DPP ikuyenera kuganiza bwino ngati anthu Chaponda akunthangitsa ali nduna yet mufuna akhale president Izagwira ? Mmmm ndakaika

  10. Boma la peter nde mbola kukhalira kuba tu iya tatopa nanu ukabweraso iweyo nyapapi nde uzasiya nsapato tu

  11. If this is a true story it means the lhomwe of Mulanje are pure mihavani or munyamwero. These were the type of lhomwe who could kill their own leader for money. Today they are found in in some parts of Mozambique mainly in Nampula Provience. How can you chase one of your own? And what was the reason behind? Is it not through jealousy ndi umbuli ?

    1. Pipe ya madzi singadutse mmunda mwako mkumapita Ku Blantyre iwe ukumwa zithaphwi,the demand is simple give them water first. Bravo guys

    2. I come from Namphungo , the constiuence once owned by P Kaliat . I cannot blame Honourable Kaliati for not bringing water in our area .I would rather put the blame to all the legislators who had been there from the time of the late Benson Nathava, The late Ray Chimenya Severe. The living Robson Makuwira other than putting the whole blame on Kaliati. This is just an example. Chaponda is a new kid on the block.Can you tell me what the other MP s had done in this area before Chaponda came into the lime light. Why treating him like this? The blame should not go to Chaponda alone .

  12. Posted in: Corruption. 4 Comments

    We as Malawians, we ask President Peter Mutharika to send on force leave the seven cashgate concerned cabinet ministers. Recently Malawi Electoral Commission has suspended its top bosses to pave way for justice and this must apply to civil service and cabinet ministers or else Mutharika must resign as well.

    On 29th August 2016, George Chaponda minister of Agriculture and Irrigation was chased and stoned in Mulanje by angry citizens. People started Stoning him and the function was disrupted and Chaponda had to run into his vehicle to save his dear life. People of Mulanje have rejected their own son in his homeland as they consider him to be a betrayer and a cashgate thief. Let us learn hold hands and learn from our brothers and sisters in Mulanje for unity and say ENOUGH IS ENOUGH.

    These people are political thugs, they are politically corrupt to finish every little resource Malawi ever had.

    Political corruption is the use of powers by government officials for illegitimate private gain. This corruption include bribery, extortion, nepotism, influence of murder, robbery of public funds etc. This government of DPP facilitate criminal enterprise such as drug trafficking, money laundering, and misuse of government power for other purposes, such as repression of political opponents and general police brutality.

    Above all DPP and Mutharika are influencing bad politics, threat to elections process e.g (Mchinji elections undermined), bribing MPs to pass bills, bribing Judges and authorities in defending them over corruption (Cashgate), favouring them e,g(20 May 2014 Elections), diverting funds for food, health, development and delaying salaries for civil servants.

    In politics, corruption undermines democracy and good governance . Corruption in elections and in the legislature reduces accountability and distorts representation in policy making; corruption in the judiciary compromises the rule of law; and corruption in public administration results in the inefficient provision of services

    https://dzukamalawi.wordpress.com/2016/08/29/mutharika-and-dpp-are-politically-corrupt-they-must-resign-of-face-mob-justice-soon-as-possible-asap/

Comments are closed.