Reports reaching Malawi24 show that seven prisoners have today escaped from Mangochi Prison.
According to Mangochi prison officer in charge Jonas Chimoto, the prisoners escaped between wee hours of one to two o’clock on Sunday using a channel that they had dug at the toilet.
Chimoto added that the channel led a way out of the prison and they dug it using an old axe and knife.
The seven escapees are believed to have been led by two notorious criminals who are answering murder charges.
The remaining prisoners said they were afraid to to alert the warders on duty since the escapees threatened to kill the remaining prisoners if they dared to shout.
Meanwhile, the police have launched a manhunt for the inmates.
(MORE TO FOLLOW)
123 thoughts on “Prisoners escape from Mangochi prison”
Comments are closed.

kkkkkk muzmanga ndende zolimba!!!
UDzanu idzo ife tinamangidwapo ku zmb
Zoona kupezamwai kuthabasi achina makuluni pachirili amavuta kwambiri
Grace Chinga Coffin
gd move
kukhwima anthu a ku Mangochi
kukhwima anthu a ku Mangochi
Achita bwino athawa akapume nawonso ndi anthu
Gus luck guy’s mulowenso chakumzuzu atijoine kumenyana ndi boma
Good timing,tidyere limodzi MONDOKWA!koma be reformed MWAMVA!kkkkkk.
Shaa zigawenga zovuta azitulusa camma 2am? Tisamale mmacottage plz.
So we have our own Michael Scofield in Mangochi!
So we have our own Michael Scofield in Mangochi!
Prison break
Kmso ziphuphu ndi zomwe za tchuluka
apolice akumalawi ndakutulukila ndinu makape kukuyimbilani 4ni kuno akumba muva kulibe driver kodi simumatha galimoto eeeeti
Koma akayidi athawawa ndiwoti adapha anthu pogwilitsa ntchito zikwanje, m’mawa lino ali kwanuko, ngakhale mukuti achita bwino
Andende amasulidweee!!!,amudima awone kuwala,kundende sikofela,ngati akufa munthu amene ali kunja akuyesayesa kugwila ntchito koma mavuto pwilikiti even njala,ndiye wakundende atani?alimbako?ndiye ngati mpata wapezeka atani?kuthawa kaaaa
Mangachi police anthu ogona mpaka kwathawa anthu oti amakhala nawo limodzi.