Mwawi Kumwenda hits 15 thousand votes


Mwawi Kumwenda
Mwawi Kumwenda
Mwawi Kumwenda

The 26 year old netball star is on the verge of being named as the 2015 International World Games Association (IWGA) athlete of the year award after taking a massive lead over her competitors.

She has now reached 15 thousand votes whilst her strongest opponent is yet to reach 5 thousand votes. Kumwenda is the only African athlete competing in the New Zealand, the World’s best netball league.

According to statistics for the World Cup netball tournament where she was named the player of the tournament, she had a shot success rate of 91 percent and netted 321 goals in eight games for Malawi Nation Netball team (the Queens).

If she she is succesful, she will become the first Malawian athlete to be honoured with such an award.

The former Escom United shooter is the only African represantative competing for the award.

The voting session will be clossed on 31 January.

Malawians have been supportive in the on-going voting period and from the look of things, she will get the award.

157 thoughts on “Mwawi Kumwenda hits 15 thousand votes

  1. Munthu akati mpoto woyeee!!! pali vuto? Ndi chifukwa chake sukulu imakuvutani anthu inu

  2. Ndakhala ndikuzuzika mumtima kamba ka anthu ena ofumira kumpoto ndikhalidwe lanu lodzikonda koma ndakumvetsani ambirinu ndinu ophunzira koma mulibe kuzindikira mwachidule tinene kuti usavage. Oteronu pepani ndipo kwainu amalawi akumpoto pitiliza ndikhalidwe lanu la umalawi, enanu khalani ndi umpoto wanuwo. Dziwani kuti zamwaizi ndi za dziko la malawi osati mpoto,mwera kapena pakati ayi kkkkkk

    1. Iweyo Francis ndi mtundu wako ndinu anthu osaphunzira (Osakonda sukulu), anthu opanda vision (osawona patali), okonda kuchinda basi (your entertainment is chigololo), mbava (mukulephela kumaliza even project imodzi yadziko, Anthu ansanje (Mmalawi nzanu asatukuke koma amwenye ndi ma foreigner). learn a thing or two from anthu akumpoto. inunso osayamba kuzikonda bwanji mmalo momangosusa chilichonse chotukula dziko ngati federal system bwanji?

  3. Mulinawo kwanuko bwanjisanawoneke? U r failures,,,,, No racism in sports,,,, Mwawi for Malawi,,,,, aakeeeee!,,,mungatinyanyiska ise!!!!akweee!

  4. akanakhala anali kumpoto kwanuko akanamuona ndani ndimayesa anabwela ku commercial city ndiye kuti aziwonedwa kunja kupepela

    1. Kodi ka blantyre ndi ka “commercial city”? kuganiza kwa umphawitu uku

    1. awuze ras denie bola zimenezi. ifenso tikufewa pa zowona atipase mphoto aaaa

  5. ma guys ..mukulemba zoti mpoto woyee..simunagwirise bohh ufulu wakaganizidwe..infact am moved to say ur stupid. .inenso ndiwaku mpoto..but I just dont rally behind bullshit..ur spoiling mwawi s luck..this is a national pride thing as we are all malawians and are proud of her..I for one voted..did you..?..so don’t just come on her page chit chating..bullshit..cause true patriots of the north mukuyinenayo..think befot speaking. .#bene_mpoto_arest my case

  6. When someone says mpoto woyee! You are just stupid .do you think ndi anthu a ku mpoto omwe amvota ..malawi nsankho suzatha….

  7. Tidakakusiyirani ma northerners(kukaya kwanuko) akanafika 15 sauzande?..sibwenzi ali pa 23 ameneyu.tamaganizani plz.

  8. 4rget about bullshit talks. Even those in England who like Mwawi do vote. We, other northerners, are silent bt u pig-helded pipo busy throughing words at each other. WHEN ARE U GOIN 2 GROW? Thats why we will top among poorest countries. Polish ur lips!!

  9. Anthu akumpoto thats why upresedent umakuptilirani ine ndavota times times ndiye umvekere mpoto oyeee. Where were you? Muzakhala choncho mpaka kalekale i hate you mxw fool!

    1. iwe ndiye ife u president inde umatikanika koma inu ma president zisilu ndy mumakondwera ndi ma prezident mumasankhaw ma bullshit…. We are on top only that inuyo mumaziwa overpopulation that’s the area you beat us..

    2. Shut up my friend kuzimva utumbuka muchepese,you mean the whole malawi mwavotera mwawi ndinu basi? Atumbuka musamazimve uchitumbuwa mxw!

    3. Kondwani panyapako if u notherners u can manage to vote for someone into the particular position then y dont u vote for the presidential possition mxw

    4. John Sylvester….galu iwe!!! kodi Mwawi ndi waku Mangochi? vuto lako ndi chani. Mpoto woyeeeeee!!!!!

    1. iwe man ndiye kukhala opanda President zikusiyana pati ndi zisilu za ma prezident mumaziyikazi answer me….We a lead only that we are few get that clear..

  10. atumbuka ndinu anthu opepera kwambiri. ndunena ndiwe “matembo khunene tchongwe” kaye chidzina kunyasa. nzimaiyu ndimmalawi zats y timavota.

  11. atumbuka ndinu anthu opepera kwambiri. ndunena ndiwe “matembo khunene tchongwe” kaye chidzina kunyasa. nzimaiyu ndimmalawi zats y timavota.

  12. iwe amene walemba kut mpoto woyee!! ndi iwe amene walemba kut kumpoto kuliluso mukuwonongaso zinthu2. ife timavota timawona ngat mwawi ndi mmalawi2. mumapanga sankho y? zats y atumbuka anthu akummwela ndi apakat samakupasan boma. kupusa!!!

  13. iwe amene walemba kut mpoto woyee!! ndi iwe amene walemba kut kumpoto kuliluso mukuwonongaso zinthu2. ife timavota timawona ngat mwawi ndi mmalawi2. mumapanga sankho y? zats y atumbuka anthu akummwela ndi apakat samakupasan boma. kupusa!!!

    1. I am Kumwenda from mpoto, Ine ndabwera poyera kutsutsa anthu o mnthu akunena zot mpoto woyyyeee. Chifukwa mwawi agwirizira flag ya Malawi & Africa. b together no matter ur area,dstrict o region.

  14. A very Good example to all Malawians.
    We can achieve anything, lets keep dreaming in Colour.
    #Go Mwawi! Go Malawi!! Go Africa.

  15. Now we have two thngs for us to be recognizd world-wide; 1 Mwawi Kumwenda’s vctry. 2 Being the poorest country world wide. Thumbs up Mwawi!!

  16. zabwino zonse mwai u r the best queen among all the queenz!!!

  17. Here we have shown how together we can go beyond,thank you Malawians.God remember Malawi.

    1. umbuli c wabwino,,,,,she’s there as a Malawian,,,,,mumatitukwanisa other northerners like us coz of that illiterate thinking

    2. vuto losayenda anthu oti mwakhala moyo wanu onse malo amodzi mumaganiza mopusa. ifeso ndi atumbuka bt tababwa ndi kukula pakati pa anthu apakati ndi ku mmwera despite our parents being typical tumbukas. mwawi ndi mmalawi first b4 being a tumbuka

    3. vuto losayenda anthu oti mwakhala moyo wanu onse malo amodzi mumaganiza mopusa. ifeso ndi atumbuka bt tababwa ndi kukula pakati pa anthu apakati ndi ku mmwera despite our parents being typical tumbukas. mwawi ndi mmalawi first b4 being a tumbuka

  18. mene tamuchitira support mwau as our fellow malawian and african,let also support peter to bring the economy up..Together we stand,Divided we fall.thanks

    1. i think vuto sindiwe koma kusunganizira omwe akuvutika ndi ziganizo zake peter. bt sindikudzikudziwa ngati mulungu akukodwa naye mwina tagokhala odanana naye chabe.

  19. A MALAWI NEWS mwayamba kulemba zanzeru osamangotichedwesa ndi nkhani zomangotisaukisa dzulo za Magay, zana President, lero Cashgate. Ndichifukwa chake ndimasapota Tim ya Atsikana osati ochuka ndi chambawa ati National footbal team iya! Kumangoononga ndalama za boma basi. Game ndi Mwayi both national and international level

  20. U are right my brother Joseph, we(Malawians) seem like we are sophiscated at taking our own country down. Shame on us!

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading