Parents in the area of Traditional Authority Chituli in Malawi’s Mangochi district have blamed chiefs in the area for authorizing initiation ceremonies of girls as young as 5 years-old.
The issue has been raised after Youth Net and Counselling (YONECO) conducted a gender based violence sensitization campaign in the area.
According to a parent who opted for anonymity, the girls who were sent to initiation camps are becoming rude to the parents due to the advice they are given at the camps.

“They challenged us whenever we advise them saying they know anything that any woman does in marriage, that is how a woman handles a man in bed,” she said.
She added that the act is becoming more serious as the parents fear that the children will contract HIV. On his part, Group Village Headman Nterera said that the issue is not new in the area.
He added that they will discuss the matter with fellow chiefs on how best to curb the situation.
34 thoughts on “Initiation ceremonies ignite conflicts in Mangochi”
Comments are closed.










Namachendeyo wayenjeza sopano akufuna anthu akasangalale ndi chikhalidwe chanji. Koma abakili munatilakwila posankha galu osowa ulemuyi.
they lost their mind.
Kuyambila kale ntundu uliwonse umadziwika ndi chikhalidwe kapena gule wa kwao.
Patsogolo ndi UDF, patsogolo ndi Bakili , patsogolo and Chiyaoooooooooo!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Hahahahahahaha!!!!!! Five yea………………… #what??????????????????
Ukufuna ukhale ngati ndani
Abakili mwawonatu munapasa mpata alomwe koma achepa wachiyawo wangalusa akuyambisa kulesayo amai ake ambuyake amakewo anazipeza achita ndemvu ngati chisilu kodi iwe piter tikuwope nanuso amuluzi ngati linali dyela kusakha ntundu umenewu mwawonatu aleseso manganje kodi amuluzi munakumana kukachaso ndi agalu amenewa eti bayasinyanyisa manje sikhathele namasimba akapoloma gwilani ntchito mumulodze mandemvuyo
Ayao ali ndichikhalidwe chao musawasokoneze nanga bwanji alomwe simukuwanena poti ali ndizao
koma mwasowa zochita bwanj paja kumuz kut mukufuna kuthesa chikhalidwe cha ayao bwino nayo kupali kuwa mwasanga
ndamo sya ayao atuleche
boma lililonse lili ndi chikhalidwe chake tisunge mwambo basi
iyiii awonjezadi m’paka a5yrz. anawatu mukuwawononga ndi Awaa akumakhala ndi m’phanga opasa Matha akangokulapo pang’ono kufika pa 14yrs.kkkkkk pepani ngati ndalawula.
Kkkk Let Mi Have A Sip.