Sitinaukile – atelo mabishopu a Katolika ku Malawi
Ma bishopu a mpingo wa Katolika pansi pa bungwe la Episcopal Conference of Malawi (ECM), ati zomwe alamula kuti a nsembe asamapeleke mdalitso uli onse kwa anthu okwatilana amuna kapena akazi okhaokha, sizikutanthauza kuti iwo… ...