Gwaladi watembenuka mtima

‘Zangondipatsa minyama’: Ngati Saulo panjira ya ku Damasiko, m’modzi mwa anamatetule pa nyimbo za lokolo, Joe Gwaladi yemwe ali m’manja mwa apolisi, akuti watembenuka mtima ndipo pano akuti ayamba kuyimba nyimbo zauzimu. Gwaladi wayankhula izi… ...