Apolisi amanga okuba nthambo za magetsi
A polisi ku Mulanje amanga bambo George Naphazi a zaka 48 powaganizira kuti akhala akuba nthambo zamagetsi ndi katundu osiyanasiyana. Bamboyu wamangidwa anthu akufuna kwabwino atakamuneneza kuti wakhala akuba nthambo za magetsi komanso katundu osiyanasiyana.… ...