Mwamva kulira kwa a Malawi bwana – HRDC yayamikira Chakwera
Bungwe lomenyera ufulu la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) layamikira mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera poyankhula zomwe akuti zikusonyeza kumva kulira kwa a Malawi, ndipo HRDC yati uwu ndi utsogoleri omwe a Malawi… ...