The 11th edition Conference on Sexual and Reproductive Health and Rights (SRHR) has started in Morocco where Malawi is being represented by UNESCO Ambassador Caroline Mkandawire who is among young people calling for capacity building… ...
Articles By Raphael Likaka
Catholic Development Commission in Malawi (CADECOM) in the Zomba Diocese has introduced a project called Food Crisis Response which will provide cash amounting to K100,000 to each of 607 households at Sub Traditional Authority ldana.… ...
Chipatala cha mpingo wakatolika cha Pirimiti mu Boma la Zomba achitseka potsatira kusamvetsetsana komwe kulipo pakati pa ogwira ntchito ndi akuluakulu atatu woona ntchito zapachipatalachi. Malinga ndichikalata chomwe Malawi24 yawona ndipo chasayinidwa ndi wapampando wa… ...
In a bid to prevent road accidents in South West Region, South West Region Police Headquarters has embarked on sensitising primary school learners on road safety tips. Speaking at Chichiri Primary School in the City… ...
Phungu wa mdera la Chikwawa West a Susan Dossi athokoza boma la a Lazarus Chakwera chifukwa chofuna kumanga nsewu wa Chapananga omwe wakhala nthawi yayitali utawonongeka. A Dossi awuza Malawi24 potsatira zomwe adayankhula mtsogoleri wadziko… ...
Mfumu Makungula a mdera la T/A Nkagula Boma la Zomba akuyimba lokoma pakhomo pawo chifukwa akupha makwacha ndi ng'ombe za mkaka komanso nkhuku za mazira zomwe amaweta. Poyankhula ndi Malawi24, GVH Makungula adati alindi ng'ombe… ...
Yemwe akufuna kudzayimira chipani cha Democratic Progressive m'dera la Zomba Thondwe pachisankho chakunyumba yamalamulo mi chaka cha 2025 a Dumisani Lindani ati mosakayika konse iwo akudzapambana chisankhocho. A Lindani awuza Malawi24 kuti pakali pano anthu… ...
A 22-year-old young innovator, Stuart Nankhumwa, has made a device capable of tracking vehicles which he says will make it easy to track stolen vehicles. During the launch of the device in Zomba City, Nankhumwa… ...
The Catholic Commission for Justice and Peace (CCPJ) in Zomba Diocese says it would like to woo many women to contest in the 2025 general elections. The commission also wants to see many women parliamentarians… ...
District Social Welfare Office in Zomba has condemned child marriages in the district and called on traditional leaders never to allow such marriages in their respective areas. District Social Welfare Officer in Zomba, Christopher Ndaona… ...
Chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) chati Peter Mutharika ndiye yankho la a Malawi ndipo ngati mtsogoleri wachipanichi ndiwokonzeka kudzapikisana nawo pachisankho cha 2025. Gavanala wachipani cha DPP mchigawo chakum'mawa a Imran Ntenje ndi womwe… ...
The Mbomba First Grade Magistrate's Court in Ntchisi has sentenced Lemekezani Wilisi, 19, for raping a 74-year-old granny. Public Relations Officer for Ntchisi Police Station, Sub Inspector Salomy Zgambo has confirmed to Malawi24 about the… ...
Advancing Girls Education in Africa (Age Africa) has donated assorted items to 10 girls at Masongola Secondary School in Zomba who are under its education support programme as a way of keeping needy girls in… ...
Bungwe la mabishopu achikatolika la Episcopal Conference of Malawi (ECM) lasankha katswiri pankhani ya zamalamulo Professor Ngeyi Kanyongolo kukhala wachiwiri kwa wamkulu wa Catholic University. Bungwe la ECM lalengeza zakusankhidwa kwa a Kanyongolo kudzera muchikalata… ...
Bwalo la milandu ku Zomba lapeza olakwa bambo wina Chimwemwe Zololo yemwe amafuna kugulitsa mwana omupeza kwa bambo wina ochita malonda ndipo lati lidzapereka chigamulo chake pa 14 February. Wa Police oyimila Boma pa milandu… ...