Government of Malawi has increased the minimum wage for workers in the country. This came to light on Friday when the minister of finance, economic planning and development Goodall Gondwe presented the 2017/18 national budget… ...
Articles By Mphatso Khutcha Richard
Nzika za ku Malawi zokwana 300 zomwe zimakhala m’dziko la South Africa koma opanda zikalata zokwanira azitumiza kuno kumudzi. Potsimikiza za nkhaniyi, wachiwiri kwa m’neneli wa nthambi ya boma yowona zotuluka ndi kulowa a Wellington… ...
Osewera mpira wa miyendo yemwe ndi m'modzi mwa a chiyamba-kale m’dziko muno, Joseph Kamwendo wati iye akukula koma mu maseweredwe ake a mpira ma timu adziwaphera nzeru. Kamwendo yemwe pakali pano akusewera mpira wake mu… ...
As the health sector in the country continues to encounter drug pilferage, Machinga police are keeping behind bars two Health Surveillance Assistants (HSAs) for stealing drugs. Machinga police spokesperson Davie Sulumba identified the suspects as… ...
Be Forward Wanderers have warned their fellow Airtel Top 8 chasers that they should not count on the injuries of Lucky Malata and Francis Mlimbika as a chance for them to easily pass through. Nomads… ...
A 40-year-old man who raped his 16-year-old daughter in Machinga district has been sentenced to 12 years in jail. The rapist, Kanyenga Damson, was found guilty of defilement which is in conflict with section 138… ...
Munthu wa umunthu amakhala ndi chisoni, mantha, ulemu mwa zina koma izi sizili choncho m'dziko muno pamene mchitidwe ophana ukupitilira. Izi zikutsimikizika pamene bambo wina wa zaka 67 ku Nkhatabay wapezeka ataphedwa ndikudulidwa mutu komanso… ...
Pamene masewera a chikho cha ma timu asanu ndi atatu mu chikho cha Airtel chomwe chifumbire kuyambira lowelukali, anthu ena otsata za masewera a mpira wa miyendo ati chikhochi chikhalangati ngati kukumba madzi pa thathwe… ...
One of the well-known gospels artists in Malawi Steve Muliya over the weekend organised a music party to celebrate reaching 10 years in ministry. Muliya held his Zisomo gospel celebration on Sunday 7th of May… ...
UKAid and UN Women have donated bicycles to people with albinism and community policing structures in Machinga. A total of over 32 bicycles as well as umbrellas and sunhats were given to people with albinism… ...
Despite government ordering Illovo Sugar Limited to end the sugar crisis, the commodity is still not available in some parts of Malawi. Earlier this week, the ministry of industry, trade and tourism gave a 7… ...
A court in Machinga has sentenced a 62-year-old man to 12 years in prison for raping a 17-year-old girl. According to Machinga police publicist Davie Sulumba, the convict sexually abused the girl who is a… ...
A 21-year-old man has been arrested in Machinga for killing his sister in-law’s boyfriend. Police in the district confirmed the development with Malawi24 and identified the suspected murderer as Elias Jalasi and the deceased as… ...
Bugwe loyang'anira masewera a mpira wa myendo muno m'malawi la Football Association of Malawi(FAM) lasefa ma bwalo osewerera mpira wa super league chaka chino. Bungweli lomwe lalamulanso kuti bwalo la zamasewera lalikulu la Kamuzu ku… ...
Kufuna kuonedwa ndi kukondedwa ndi aliyense pa masamba a mchezo ndi khumbo la wa chinyamata aliyense pa dziko malinga ndi zifukwa zake koma ku Malawi zafika pa mlingo wachilendo pamene achinyamata ayamba kulowa mpaka m'manda.… ...