Kwa nthawi yoyamba tsopano kuchokera mchaka cha 2017, banki yayikulu pa dziko lonse ya World Bank yalengeza kuti ipeleka thandizo…
Zina ukamva kamba anga mwala, zina zikamachitika nkumati kodi ndiku Malawi komkuno? Inu anthu am'mudzi mwa Chimombo mdera la mfumu…
A Bon Kalindo akhala akusungidwabe mchitokosi cha apolisi uku akudikira chigamulo kuchokera kwa woweruza milandu a Muhammad Maxwell Chande lachisanu…
A polisi mu mzinda wa Lilongwe ku Area 3, anjata a Jonathan Nkhosa yemwe ndi mphunzitsi wa kupulayimale wa zaka…
Akaidi pa ndende ya Kasungu lero pa 5 December anali pa mwambo okumbukira ufulu wa chibadwidwe pa mutu woti "Ulemu,…
Sukulu ya ukachenjede ya Kamuzu University of Health Sciences yalengeza kukwera kwa sukulu fizi kuchoka pa K400,000 komanso K550,000 kufika…
Kutsatira mavuto omwe alipo kamba ka namondwe wa Freddy yemwe adaononga mbewu ndikuyika a Malawi ochuluka munjala yadzaoneni, tsopano boma…