Despite President Lazarus Chakwera’s claiming that he is committed to fighting corruption, his administration is still doing business with companies linked to corruption suspect, Zuneth Sattar, the latest being payment of 8.4 billion kwacha in… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Private Schools Association of Malawi (PRISAM) has over the weekend elected new office bearers who have vowed to complement government's efforts towards improving the country’s education sector. On Sunday, January 28, 2024, PRISAM held an… ...
Pomwe masiku akusenderabe kuchitseko kuti dziko lino lichititse chisankho chaka cha mawa chino, chipani cha Democratic Progressive (DPP) chataya ena mwa mavoti ophaipha, kamba koti anthu ena otsatira a Kondwani Nankhumwa, ati nawoso atuluka nchipani… ...
Pelekani molowa manja: Sinodi ya Blantyre pansi pa mpingo wa Church of Central Africa Presbyterian (CCAP) yakhazikitsa ntchito yobweza ngongole ya ndalama zokwana 2 biliyoni kwacha ndipo yagwada kupempha akhilisitu ake kupeleka 10,000 kwacha aliyese.… ...
…Lombwe akuti nzakeyo anakhomera ku dowa “Lu-Lo my vote”: Kuli kusambwadzana za mkabudula uku pomwe mtsutso wa ubwino wokhala ndi digili kapena kungokhala ndi chilembwe basi, wafika pa mwana wakana phala pakati pa oyimba Dan… ...
Malawian celebrated guitar virtuoso, Erik Paliani, is set to host unforgettable ‘The Ultimate Guitar Workshop' in Lilongwe this weekend. The renowned Jazz maestro Paliani, will host the guitar workshop at Flood Church in Lilongwe on… ...
The Ministry of Natural Resources and Climate Change through the Department of Climate Change and Meteorological Services says most parts of the country will experience dry weather conditions in the next seven days. This is… ...
The Malawi Police Service (MPS), has warned all its officers against the increasing cases of sharing internal and sensitive information with the public. This is contained in another leaked internal memo, dated Thursday, 25 January,… ...
Agenda ku polisi chamba chili mthumba: Abambo awiri a m’boma la Mwanza athilidwa zingwe powaganizira kuti ndi omwe anakadawira galimoto ya boma ikuyenda ndikuba tenti komaso chinsalu chofiyira chija amayendapo mtsogoleri wa dziko m'misonkhano chija.… ...
Anthu ena omwe sakudziwika mpaka pano akuti usiku wapitawu anakadawira galimoto ya boma ndikuba katundu wina wakunyumba yachifumu koma kwa pano akuti chinsalu chofiyira chija amayendapo mtsogoleri wa dziko m'misonkhano chija, chapezeka kutchile lina. Usiku… ...
Private schools owners and managers under the umbrella body Private Schools Association of Malawi (PRISAM), will be in Dowa this weekend for an Annual General Meeting where they will also launch private schools SACCO. Confirming… ...
The First Grade Magistrate Court in Lilongwe has sent two street connected children to Chirwa Reformatory Centre in Zomba after they robbed a man of a laptop bag, smartphone and K20,000 cash while armed with… ...
Police at Kanengo in Lilongwe have arrested four people for stealing assorted beer manufacturing materials at their workplace while four other people have been arrested for buying the stolen materials.According to Kanengo Police Station Public… ...
Mneneri Shepherd Bushiri yemwe ndi mtsogoleri wa mpingo wa ECG - Jesus Nation Church walengeza kuti akufuna kugula ndege yonyamula anthu obwera ku mapemphero ake kuchokera m’mayiko ena. Izi ndi malingana ndi zomwe mneneriyu walemba… ...
“Hallo, ndapatsidwa ndalama yokwana K500,000 ndi m’bale wanu kuti ndikutumizileni, nde kuti ikufikeni munditumizile kaye K50,000”: Amayi awiri ochanuka m'maso adzikapatsilidwa nsima pa zenera ku polisi ya Zomba chifukwa chofuna kulowetsa ma simu kadi okwana… ...