Youths in Mulanje district have expressed optimism about improved quality youth-friendly reproductive health services delivery as Network of Journalists Living with HIV (JONEHA) has started collecting qualitative and quantitative data under its Community-Led Monitoring (CLM)… ...
Articles By Archangel Nzangaya
President Lazarus Chakwera is receiving praise for instructing the National Council for Higher Education to revise university student loans to help cushion students amidst the rise in cost of living due to rising inflation and… ...
Unduna Woona za Madzi ndi Ukhondo wati kuyambira pa 7 mpaka pa 14 mwezi uno, madera ambiri kumpoto kwa dziko lino komanso m’mbali mwa nyanja, akhalabe akulandira mvula yamphamvu, zomwe zikupeleka chiopsezo choti kumaderawa kutha… ...
Leader of ECG - Jesus Nation Church, Prophet Shepherd Bushiri has reached out to over 6000 people who have been depending on wild tubers as their main meal in Nsanje district. Nsanje is one of… ...
Concerned youths in Mchinji district have threatened to hold demonstrations over what they are describing as unfair recruitment process for health positions within the Ministry of Health, as they accuse authorities of recruiting 15 people… ...
Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre, akusunga m’chitokosi mzimayi wina wa zaka 21 chifukwa choononga paipi ya madzi a Blantyre Water Board mwadala ndicholinga choti atunge madzi aulele. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa polisi… ...
Malawian poet Tendai M Shaba has been featured in the Commonwealth Poetry Podcast which celebrates poetry in the 56 Commonwealth countries. Commonwealth Poetry Podcast releases poetry episodes in which they talk with someone from one… ...
Lachisanu lino chidwi cha anthu chikhala ku Mangochi ku nyumba ya Page komwe mtsogoleli wa chipani cha Democratic Progressive (DPP), Professor Peter Mutharika, akhale akuyankhula ku mtundu wa a Malawi kudzera pa msonkhano wa atolankhani… ...
In readiness for the 2025 tripartite election, a new political party, National Development Party (NDP) which has expressed commitment to advancing the interests of Malawians through inclusive governance, has officially been registered. According to a… ...
Apolisi m’boma la Mangochi, amanga mayi wa zaka 25 pomuganizira kuti wakhala akubera anthu ndalama pomawagulitsa mankhwala omwe amanama kuti amachiza matenda a HIV/AIDS. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi a Amina Tepani… ...
Private Schools Association of Malawi (PRISAM) has launched its Mzuzu chapter with Mayor Thomas Chirwa being elected chairperson for the region. After successfully launching the Blantyre and Lilongwe Chapters, the association, launched the Mzuzu Chapter… ...
Nthambi yowona za anthu olowa ndi otuluka m'dziko muno ya DICS, yati ntchito yobwezeretsa sisitimu yake yomwe inasokonezedwa ndi akathyali ena ikubala zipatso ndipo akuti pali chiyembekezo chokwanilitsa ntchitoyi asanathe masiku 21 omwe anapeleka mtsogoleri… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera, lero akhala akutsekulira chipatala cha nthenda ya khansa mu nzinda wa Blantyre chomwe wamanga ndi mpondamatiki Thom Mpinganjira. Izi ndi malingana ndi kalata yomwe boma latulutsa Lolemba yomwe… ...
Illovo Sugar (Malawi) plc together with two other partners, have handed over a 19.5 hectare solar-powered irrigation scheme to people from 13 villages at Nchalo in Chikwawa district. The irrigation scheme which is being implemented… ...
Malawi’s Afrobeat sensation Onesmus, continues to raise the Malawian flag on the international scene as his ‘Green Light, Red Light' song has been featured on the new Season 4 of Netflix series ‘Blood & Water'.… ...