Police at Kanengo in Lilongwe have hailed the support they receive from stakeholders towards security and have since launched this year's festive season joint patrols. The launch of the 2023 festive season joint patrols, took… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Akuluakulu a mpingo wa God's Chapel alengeza kuti zigawenga zomwe zinasowetsa mtsogoleri wawo Hastings Salanje masiku angapo apitawa, zamulavura tsopano ndipo ali bwino bwino. Pa 1 December chaka chino, akuluakulu a mpingo wa God's Chapel… ...
Mighty Mukuru Wanderers are planning to lodge a complaint against Football Association of Malawi’ Secretary Alfred Gunda and members of the Competition Committee for scheduling their Airtel Cup quarterfinal second leg match against Silver Strikers… ...
Kuli kanthu kokanthula nchala mchipani cha Democratic Progressive (DPP) pomwe mtsogoleri wake a Peter Mutharika achotsa a Kondwani Nankhumwa pa udindo wa wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipanichi mchigawo chakum'mwera. Izi ndimalinga ndi kalata yomwe chipani… ...
M’modzi mwa anthu otchuka pa fesibuku, Pemphero Mphande wauza anthu onse omwe akunena kuti mzilazembe pa maimbidwe a Giddes Chalamanda akula asamakaimbe ku ma “show”, kuti ayambe kupeleka ndalama zothandizira umoyo wa tsiku ndi tsiku… ...
Timu ya Mighty Mukuru Wanderers yauza bungwe la Football Association of Malawi kuti liyimitse kaye masewero onse a mpikisano wa Airtel Top 8 pofuna kudikira chigamulo pa apilu yomwe ikufuna ipange ndipo yati apo bii,… ...
Days after Democratic Progressive Party (DPP) Secretary General Grezelder Jeffrey organised a National Governing Council (NGC) meeting, leader of the party Peter Mutharika has replaced her with Clement Mwale. This is according to a press… ...
The Ministry of Natural Resources and Climate Change through the Department of Climate Change and Meteorological Services says the dry spell which has hit most parts of Malawi, will extend to Tuesday next week, December… ...
Authorities at the multi-billion kwacha International Blantyre Cancer Centre (IBCC), which is being funded by business guru Thomson Mpinganjira, have disclosed that the facility will be ready for cancer patients in January, 2024. This was… ...
Leader of the Democratic Progressive Party (DPP), Peter Mutharika, has commended some National Governing Council (NGC) members for not attending the controversial National Governing Council meeting which he has labeled as illegal. DPP Secretary General… ...
…akuti samapanga chibwezi ndi azibambo obowoka mthumba Pomwe amayi oyendayenda ena akumatchaja ma K1000 komanso ma K2000 m’makwalalamu, oyimba wankazi otchuka m’dziko muno Zani Michelle Chiumia yemwe amatchuka ndi dzina loti Zani Challe, watutumutsa abambo… ...
Africa’s entertainment services provider, Multichoice Africa Holdings (MAH), has announced the resumption of DStv services in Malawi, after months of battling with the Malawi Communications Regulatory Authority (Macra) over price adjustments. In a press statement… ...
Khanda la miyezi isanu ndi iwiri, lafa pomwe nyumba yomwe linagonekedwamo usiku lokhalokha inayaka moto pa nthawi yomwe mai ake anapita kokachita zadama ku nyumba kwa njonda ina. Watsimikiza za nkhaniyi ndi wofalitsa nkhani pa… ...
Timu ya Mighty Mukuru Wanderers yanenetsa kuti ngati bungwe la Football Association of Malawi (FAM) siliyimitsa masewero ake ndi timu ya Silver Strikers lero, iyo siyikapezeka pa masewerowa kufikira chilungamo chidziwike. Dzulo lachiwiri, timu ya… ...
Players in the insurance industry, have been challenged to become more innovative in raising awareness about the Importance of insurance and how it contributes to national development so as to raise the insurance penetration rate… ...