Khuda Myaba yemwe pano alibe timu yomwe akuonetsera ukatswiri wake, watutumutsa gulu pomwe wanena kuti alibe ganizo losewera mu ma timu a Mighty Mukuru Wanderers komanso FCB Nyasa Big Bullets ponena kuti matimu onsewa sangakwanitse… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Dowa police station is keeping in custody a 24-year-old tailor identified as Brian Banda for putting on a nursing officer’s uniform. Confirming the development to the local media was Mponela Police Station Public Relations Officer,… ...
…ati wofesa amayembekezera kukolora …ati BBC ikuwawidwa ndi kukula kwa mpingo ngakhale TB Joshua anamwalira Akuluakulu a mpingo wa Synagogue Church of All Nations (SCOAN) ku Nigeria, ati anthu asatekeseke ndi nkhani yomwe wayilesi ya… ...
Ngati njira imodzi yofuna kupewera matenda a chimanga omwe agwa mdziko la Tanzania kuyambukira mdziko muno, boma la Malawi lati likagayitsa chimanga chomwe linalanda anthu ena omwe amafuna achilowetse mdziko muno. Izi zikudza pomwe boma… ...
Timu ya Mighty Mukuru Wanderers yapulumukira dzenje lokumbakumba pomwe bungwe loyendetsa mpira mdziko muno la FAM lauza timuyi kuti isachimwenso kwa chaka chimodzi kuti isalandile chilango chomwe bungweli linapeleka choti Wanderers isatenge nawo gawo pa… ...
The just released documentary by the British Broadcasting Corporation (BBC) explaining how late prophet Temitope Balogun Joshua commonly known as TB Joshua, allegedly committed sexual crimes, life of abuse, harassment, manipulation and staged miracles, has… ...
Following an impressive performance of their reserve side in the 2023 season, officials at Mighty Wanderers say they are reverting to their culture of relying more on players from the club's reserve side with five… ...
Patadutsa zaka ziwiri ndi miyezi ingapo chimwalilireni mneneri TB Joshua ku Nigeria, wayilesi ya British Broadcasting Corporation (BBC) yabweletsa poyera zotsatira za kafukufuku yemwe inapanga pa zoipa zomwe a Joshua amapanga monga kugwililira amayi ndi… ...
Boma kudzera kwa mlangizi wake pa za malamulo lati likukonza zoti likasume kutsutsana ndi chigamulo choti lipeleke ndalama yokwana K103 miliyoni kwa a Brian Banda ngati chipepeso powachotsa ntchito ya mneneri wa mtsogoleri wa dziko… ...
Clyton Thomas also known as Akila who won actor of the year 2023 and entertainer of entertainers awards at the Malawi Broadcasting Corporation's (MBC) Entertainers of the Year Award ceremony last week, has finally received… ...
The Democratic Progressive Party (DPP) has labelled the Human Rights Defenders Coalition (HRDC) as hysterical and selective in activism and has strongly urged it to refrain from poking its nose into the affairs of the… ...
Potsatira zionetsero zomwe mtsikana wina Hendrina Kamenya anachita ku maofesi aboma munzinda wa Lilongwe Lachinayi zokhudza ndalama za chipukuta misozi za malemu bambo lake, lero Lachisanu boma lapeleka ndalamazi. Mtsikanayu yemwe ndiwochokera m’boma la Mwanza,… ...
The Lilongwe Resident's Magistrate Court has on Wednesday, 4 January 2024, sentenced a man who is in his 30s to three years imprisonment with hard labour for forging a Malawi passport to continue his stay… ...
Adindo awapempha kuchita machawi kuthetsa kusamvana pankhani ya malire a dziko lino ndi dziko la Mozambique ku Mangochi pomwe akuti apolisi ndi anthu a m'dziko la Mozambique atchetcha chimanga cha a Malawi ku midzi ina… ...
Pena munthu ukaganiza kwambiri ukumati mwina bolaso kuweta agalu athu omwewa achikudawa. Komabe kuganiza izi ndi kamba kamkwiyo nde tiyeni tizisiye naye zimenezo, koma funso nkumati alira bwanji makolo ake a Miracle omwe amawona tsogolo… ...