Madonna says David Banda is future Malawi president

Advertisement
Madonna-David

United States pop star Madonna has said her Malawian adopted son is a future leader of Malawi.

Madonna-David
David and Madonna

Madonna said this on Twitter as she praised 12 year-old David.

“On President Day I celebrate the future president of Malawi, the warm heart of Africa, Banda,” Madonna said in a tweet.

David Banda is the first child the American pop star adopted from Malawi.

The 59 year old also has three other children adopted from Malawi namely Mercy James and twins Stella and Estere.

Presidents’ Day is an American holiday celebrated on the third Monday of February in America.

Originally established in 1885 in recognition of President George Washington, it is still officially called “Washington’s Birthday” by the federal government.

Advertisement

199 Comments

  1. Madonna umapasidwa ulemu ku malawi koma ngati ukufuna kutukwanidwa zamuike mwana wakoyo u president wo

  2. when almighty God says yes…. who knows akhalapo u President wa akaziwa ndani lets wait & c sogolo lamunthu amaliziwa ndimwiniwake Mulungu.

  3. it’s ok,let him come to be the president of football association of Malawi,awawa atitopetsa mwina akalamba!!

  4. Zaziiii, anthu otchona kunjawa nd amene akutionongela dzikoli, ameneyu olo khwanya angamudzwe?? Tizilamulirana tokha kuno mavuto athu timawadzwa tokha, no need for someone from US to come and tell us

  5. There are a lot of Malawians abroad who are doing good without adoption parents. And they can rule Malawi without being a puppet of anyone. David Madonna is far more to be called president because he is Madonna, s puppet

  6. Only B.Muluzi & Joyce Banda r true Malawians..not bingu. peter..
    O chakwera..they all half Malawians..new York boyz ma niggaz awa

  7. he will not cope up with a malawian politics.Will he managetm to lie to convince people because malawian doesnt trust truth but lies.How will he manage to define the terms like cashgate?how will he know where to lay foundation stones?how will survive oppositon crooks who critisize govt when it deliver promised productive services?how will he hold accountable those who steal poor peoples taxes and run to foreign countries and just hear that he/she was delivering a speech in university hall or such such meeting?how will he manage to run a govt with grand ministers,lustful mps and wea minded councellors?will he manage to persevere the land full of anamapopa,rain blockers?will you manage to give your civil servants meager salaries whe they complain you challenge that working in govt its a calling or else go anywhere to look for green pasture?will be patient when you hear that there is blackout,run out of water of water,hospitals run out of drugs,the country run out fuel at the same period?WAAH GWAAN SISTER?BUN!!!

  8. Is presidency, the only career David and his white mother see as lucrative? Let him concentrate on football and become George Weah of Malawi. And I don’t think Madonna can sink so low as to insinuate such sentiments.

  9. Ndizotheka!Ziribwino Poti Alikutali Akanakhala Kuno Chakwera Akanamusowetsa Kunena Zoona Mr Chakwera Udindo Akuwufuna Kwambiri.

  10. I’ll be the one to to compete with him don’t worry guys and for sure i will evade/conquer this young man kkkkkkkk(tayendapo bare ife primary level school)

  11. Ma politicians okalambawa akamva nkhani ngati imeneyi amanyansidwa maningi. And mwalakwa kuulula chifukwa ayamba kumukhomerera akabwera kumudzi kuno.

  12. MALAWI YANGOSANDUKA BEEN ALIYESE KUFUNA KUILAMULILA. SATAN AKUFUNA KULANDA MALAWI BASI, KULEPHELA KUMUTCHINGA TCHINGA SATAN WALIMBA.

  13. Let people understand. She means David is a Malawian son and can become anyone as a Malawian. Why being angry with anything. Let us get his point of view.

  14. I think we shud give Banda a chance, after a proper scruitney, i have realised that people who once lived in America and educated there, become good presidents.

  15. a Malawi kutokota zopanda pake nanga zogona ndinjala,kapena kuyenda wapasi zikugwirizana bwanji,,,,,, ngati mulungu analemba basi zizatelo

  16. Chikondi cha munthu wa kuda chidabweretsa Hastings ndani ndani kwaoko Ku ghanako ndikumusitha dzina avekele kamuzu Banda chonsecho kamuzu weniweni adalibe chala cha kuphanzi chimodzi and amathanso kuyakhura chichewa not kama litchowa uja

  17. Iwe maddona why choosing president position for that young man. Kwa ine ndimaganiza kut adzakhale “Tobacco control commissioner” apo ndiye tigwirizana koma na mfundo iyi asaa na pepe maddona udzawaziwa amalawi kut amagangalama. Maka pa makofi a ma votes

  18. hahaa kamuzu Banda, Joyce Banda, and now David Banda?? We have had enough with the Bandas let’s try the phiri’s now!!

  19. Madonayu akufuna kuzalamulira back door eti? Mayesa amati mwanayo akufuna kuzakhala wosewera mpira, nde pano zasinthanso? As long as sakuchokera uku Ku ujeni uku, no problem. Chifukwa pano nde atikwana.

  20. Mavuto alikuno akuwaziwa ameneyo…azakhale president wakonko..kutionelera chani koma yah zuka malawi…..maloto onama ameneo

  21. Kkkkkkkkkkkkkkkkkk…..Malawian leaders come from sourthen region, he will be the leader of opposition!

    1. The mentality that some people have, it raises questions which have no answers…..@Mdeza next time bring in a comment that promote UNITY not regeonalism!! za

    2. Dpp Boma!Anthu Achigawo Chapakatife Kudzikonda Maka Awa Achakwerawa Ikanakhala Kamuzu Alipobe Vote Yanga Ikanapita Kwaiye Koma Awa Akutsogolera Mcp Panopawa Akuoneka Ndiomva Zawo Zokha.

  22. Both the First President HKB and current President APM stayed in USA for over 40 years.
    Let’s wait and see

  23. every bulding was at first a picture; not drawn on the paper but insides someones mind.it takes man’s efforts to make it visible to the whole society and not excluding madona’s dream of caring for leader of this nation. good development!

  24. Azibambo a ndevu zawo ndi azimayi azima bele kuno kuma kwiya ndi nkhani yoti madona akumu funila zabwino mwana wake…shame….ku sawukako nde vuto u always think negative

    1. David is still young, by the time he reaches 35 yrs of age to contest I suppose Maddona will be laying in peace in Grave then/

    2. True that ….but since most Malawians are too blind to see what this pop star trying to achieve in the name of David banda.

  25. That will be in hands of the voters, if he will have a good manifesto, why not giving him a chance, otherwise we need people who knows how if feels kugona ndi njala komaso walking 6 km to xul during rain session crossing rivers.

  26. i thnk bolaso Daved becous ola mwana atha kuloza chipatala chomwe anabadwila komaso ndikomo lomwe wachokera nanga enawa mungatiuze chulu chomwe idali nyumba ya amai awo? ene way Daved ndi wathu wathu mmalawi sikuzakhala kusokera ai.

  27. everyone from America but a Malawian born is qualifying for de that highly appreciated position let mi go in USA then i’ll come bak to rule kkkkkk

  28. In Malawi everything is possible kkkk or mukane even munthalika family yakulira ķunja pano akulamula with blocken chichewa so zothekaso ndi David mai Malawi

  29. Ndizotheka ngati kuli koyenela kutero
    ena tili kuwaonawa akulamula bwanji?
    Chichewa satha kulankhula zokha zokha zima blocken

  30. what does he know about Malawi if I may ask?. He has grown up in America silver spoon life . We need people who has grown up on this soil and they know how it feels to be called a Malawian.

    1. yeah we need real Malawian who have suffered from birth up now and they are living here. No normadic pple are needed in malawi

    2. Pajatu amalawi amafuna anthu ngati amenewa okulira kunja
      osati okulira kuno ngati
      Joyce Banda
      Atupele Muluzi
      chakwela
      amenewa ayi akukanidwa kulamula Malawi

    3. He doesn’t seem to love politics than football……..to be a Malawian coach one day I would agree to that but not president.

  31. I understand that adopted son shall always be an asset of that country why should he be future leader of Malawi, I doubt that very much.

  32. Sinanga anawona kale kuti manyasa ndi anthu oti amayembekezera kuti munthu amene wakulira kunja ndiye woyenera kuwatsogolora

    1. KKKKKKKK Iwe usandiseketse m’mesa akudzala miyala yamaziko ati ndizomwe anakaphuzira kumangalande k………….kaya imela liti bolani Dausi azikayithira ingawume paja ng’amba yabvutaso kunyasa

Comments are closed.