Money stress: Nomads pull out of CAF tourney

Advertisement
Be Forward Wanderers

Be Forward Wanderers FC have announced they are withdrawing from the CAF champions league.

Malawi24 understands that this is due to what is being described by Nomads officials as worrisome financial constraints.

Be Forward
Nomads pull out of CAF tourney.

The TNM Super League champions were slated to head to the Democratic Republic of Congo to face AS Vita.

Initial reports had suggested that the Nomads also had hiccups to register players let alone to gather funds that they would have to spend to take part in the continental showpiece.

They had set up accounts where supporters were making contributions but the funds collected are reported to be lower against the estimated expenditure.

The Nomads were along with Masters Security FC representing Malawi in continental club competitions.

In cases of this nature teams get fined but as it is CAF is yet to make a statement.

Advertisement

44 Comments

  1. Mmadana ndi Noma chifukwa chani inu a Malawi 24? A simple investigative journalism you can’t do. You suck. Not worth to be an online publication

  2. Masapota a Noma mumazipopa eeee ife olemera iiiii inu mulibe kanthuuu or ku akaunti kwanu matama thooooooo Mulungu wafuna kuti musiye Matama kularata a Bullets osauka inu iiiiiiiiii lero ndiizi

  3. Hahahhhahahaha
    Nooooo!!!! Beforward Wanderers,dont Start What You Can’t Finish! Mwashosha! Kudambwe…Tiye Nazoni…
    Munaputa Dala Nkhondo Ya Azibambo…

    What About Masters Fc?!

  4. Hahahaaaaaaaaaaaaa…………..!!!!!!!

    Basi Malawi yonse nganganga pambuyo pa Masters Security… heheheeeeeeeeeeeeeeee……….!!!!!!!
    osamasaka chomwe simungachiphe//
    Zinthu zina osamayetsa ngati simungazithe//

    heheeeeeee koma I cant stop laughing ndiiiiiiiithu, mesa munkati club yandalama inu? mesa mumati ulendowu mudziyenda pa ndege not za Bullets zija zoti popita ku Comoros Ireland kukwera bus? hahahaaaaaaaaaaaa ulendo wa ku CAF wakanika dikilani chibhalo basi.

    Ndimadabwatu ine, ka Team kopanga draw ndi Mangochi Select, chigolinso chochita kubweza pa penalty, nkumati ulendo wa ku CAF mukalimba?

    Nkhani sindalama zokha zavuta ayi, komanso manthaaaaa kkkkkkkkkkkkkkk kuopa kubesa hohohooooo

  5. FAM yakana pempho la Wanderers kuti awauze a CAF zoti sakwanitsa kupitiliza ndi lingaliro lawo losewera CAF

    FAM yati wanderers ione yokha zochita cz inakana kupereka 15 mita yomwe FAM imayenera kulipira zoterezi zikachitika

    Tsono iwo ati izi sizikuwakhudza awauze okha a CAF

    More to come

  6. Phuma ndi nyere sizimagwirizana. Munanyanya kuberekedwa ndi kupeza ma player mwachinyengo. Hehede wasows2 okutolani apa. Muisovenge.

  7. Team yoyalusa iyi how can you start preparing for CAF without sound financial?.Wait a minute! what are you going to to do with funds that we’ll wishers deposited in your account?.
    Nanga a BULLETS mutithandiza bwanji coz we’ve started training earlier than we planned?. Neba you must be serious this withdrawing will put you in much trouble fwethu.

Comments are closed.