DPP losing? That’s a dream of a barren woman- Jeffrey

Advertisement

The ruling Democratic Progressive Party (DPP) has claimed that the party will win the general elections in 2019 saying those who think DPP will lose are dreaming like a barren woman.

DPP’s Secretary General Greselder wa Jeffrey disclosed that the five year term that the party has had is for developmental foundation.

Wa Jeffrey: The party is to rule again.

Wa Jeffrey added that the ruling DPP will defeat opposition parties in Malawi with votes in 2019 to have a second five year rule.

“Kuluza? maloto achumba bwa, boma sitilikutuluka, ndipo sitikutekeseka (DPP losing? That’s a dream of a barren woman, the party is to rule again and we are not afraid),” said wa Jeffrey.

She further urged Malawians to vote for DPP during the forthcoming tripartite elections next year.

“A Malawi okuona kuti zinthu zikuyenda, omwe akudandaula ndi a opposition chifukwa cha nsanje, akufuna mpandowu (Malawians know that all is well, opposition parties are the ones complaining because of jealousy),” she added.

Meanwhile, the DPP has disclosed that it is to hold a convention to elect its presidential candidate for the 2019 elections.

President Peter Mutharika who says he will seek reelection in 2019 is expected to stand on the party’s ticket.

 

Advertisement

157 Comments

  1. U floosh woman do u think dat de malawian are stil driming about ur crazy profesor?4get abt dat gangstr wil win 2019.

  2. Nonse makape plus opposition ovota Ali pheeeeeeee vote sitipanga pa fb ndipo wina sadziwa m’komwe zoti kuli fb nde uli busy kulimbana apa zaziiiiiiii

  3. Mzimayi walankhula mau onyazisa azimayi anzake amene akusowa ana pamene akufunisitsa atakhala ndi ana. Azimai mwawalandira bwanji mau achipongwe kuchokera kwa mai muzanu?

  4. Mzimayi walankhula mau onyazisa azimayi anzake amene akusowa ana pamene akufunisitsa atakhala ndi ana. Azimai mwawalandira bwanji mau achipongwe kuchokera kwa mai muzanu?

  5. Mai ndinu opusa do u think we are happy ndi Dpp? chaponda anaba koma ali ku? achina Namkumwa milaandu yao ija anamangidwa? 72hrs blackouts? Blood sukers? apa tungodikira nthawi! No one will vote for. Dpp and its thugs mai! MCP ndie Boma likubwela!

  6. Munthu Wa Chuma Kumulalikira Kt Adzafa, Eeee! Mutha Kudana Naye. The Same Applies To Dpp, Kuwauza Zoluza 2019, Sangakuvomelezeni. Kma Akuluza Ndithu, Cme 2019.

  7. Ine olo atandipopera doom mkamwa, at my Youthful age sindingovotere nkhalamba ya zaka 81regardless any political affiliation. Izapanga chani chopindulira moyo wa achinyamatafe? Maganizo opepera ngati awa ndi omwe awononga Zimbabwe mma 2000. Ma fresh brain atha Ku DPP ko?? ZOMBWABWANA BASI!!!

  8. This woman has a foul and stinking mouth,she he thinks she is the only one who will vote,and she has forgotten that’s how exactly she was saying during the by elections period and alas!her might party lost miserably,and ndi you are repeating the same words!we shall meet again on the battle field next year.And u will regret wat you are saying now.

  9. Michael Ussi aka Manganya akusiya ntchito ku ADRA ndipo akufuna kuyamba ndale.
    Iye watsanzika kale mabwana Ake.
    Ussi wapangitsa kale print ma t-shirts ndi zipewa komanso nsaru.

  10. In 2019 a day after elections we will hear that a certain professor has collapsed after hearing that he is trailing a certain DR by over half a million votes. The professor will collapse bcoz he knows has looted alot. He stole with his brother and is still stealing now. He is shielding corrupt party officials bcoz they share the looted money.

  11. Ineyo Plus Akazi Anga Azibale Anga Sitingavotele DPP Inu Ofunika Mupakile Mukakonzekenso Chifukwa 2019 Mukabela Kuipa Sure!!!

  12. Ngati waJeffley akhalabe s.g.Ku DPP idzakhala disaster yoopsya 2019. DPP idzaluza koopsya kuja. hule silitha kuyankhula ili. Asayiwale kkuti pa 17/10/17 amayankhula chimodzo modzi koma zinatha bwaa? A Malawi atopa ndi chipani cha nyansi ichi.

  13. Stupid useless woman who always trying to appease her boss mark my words MCP is going to celebrate after an emphatic victory

  14. Who is going to vote. And if you know that you will win why busy sticking nose in opposition. Instead of putting development in action you are busy campaigning since into power. Mulungu simunthu ngati John ndi Mary. Unless they is something that you know and we don’t know. Don’t take Malawians as fools. I see these same people talking today after loosing they will blame one man and join the party which will win. Remember Mugabe was top of game ndinkhuku zokuntha kuntha and other came in and cook it.

  15. All barren women in the Bible after praying they gave birth to powerful men of God.Samson and Samuel are good examples.In 2019 the barren woman will bear a great baby who will deliver Malawi from the bondage of poverty.

  16. Sarah and Hannah were barren yet they dreamed kids. Read the story of Hannah in the book of Samuel or the story of Elizabeth and Zacheria. Keep mocking, Malawi will decide.

  17. But why make a reference to a barren woman? Is a barren woman not a woman? This is an insult from a rotten mouth once again. A barren person also carries a vote which Dpp badly want. Wise up Jef. This is 2018.

  18. DPP losing its like a dream of a barren woman?….remember, when people saw a barren woman in Sarah, God saw a Mother of many Nations. So you must think twice before speak!

  19. Mwakonza bodza lantundu wanji mu manifesto anu adpp loti muwapusitse nalo amalawi kachikena???? Gileseda sindimadabwa nawe paja kwanu ndi ku nkhotakota komwe kunalimidwa chamba choncho umati ukasutasuta mkumawona ngati tonse timasutaso

  20. MMAI YU AKUNENA ZOWONA DPP SIINGALUZE AI. IKUWINASO 2019. VUTO CHITINI CHOPANDA MADZI PHOKOSO. CHIPANI CHOGWETSA DPP NDIYE SINDIKUCHIWONA AI.

    1. Mr phozongo u will never stop to amaze, si inu mmati kumwera kulibe mcp nde mukutchula bwanji blantyre. Vomerezani kuti mcp in unstopable this time.

    1. Poichotsa mcp inakukwanani pochotsa udf inakukwani, kuchotsa dpp ya late bingu inakukwanani. kuchotsa pp inakukwanani. ndiye mupange chanu chipani chomwe sichidzakukwaneni ngati chingawine.

    1. Iwe analankhulapo zanzeru ameneyo?.kwake nkunyoza ndi chifukwa timamuti ndi hule mkazi wanzeru sangamalankhule ngati momwe amalankhulila ameneyo

  21. Ooh mukamanga mpumulo wabata wina??ukufuna kunena chani??.Ayi wanena bwino,utsogoleri waziko lino muziutenga choncho apo ayi MWANYERATU.Chodabwitsa munakamanga mpululo wabatawo koma kulephelanso kuwina pachitsankho.General election si by election tu.Palibe chipani chochosa Dpp pampandotu pokha pokha chitayambika china apo zingatheke kuchosa Dpp kapena mupange ufiti wanu munenawo wa mpululo wabatawo nanga sinu amene mumaziwa kutenga zinthu mwachidule apo bii muzaziona.

  22. Uzawina mobera momotu other wise ndamenyesa khwangwa pamwala ukuwona ngati amalawi ndi mwamunawako kuti wapanga uhule ukonkunena kuti tikambilane ndi banja amalawi mwawaliza kwakwana mwatiswera masukupamutu kuyambila bingu weniweni ukachita masewera tikamanga wina mpumulo wabata

  23. Was she not saying the same prior to the 5-1 crashing iin the by elections! She talks like this to save her post and bluff her master!

  24. Ndale Za Pamalawi Zidasintha Nkhanga Zawona. Ife Odalira Ulimi Mwatigwetsa Kokwana Ndimitengo Yanu Yotibera Mphechepeche Mwa Njobvu Sitingalole Tipitemo Kawiri Asiyeni Anzanu Anzeru Za Ku Mmawa Awongolere Mwina Nkusimba Mwayi.

    1. 2019 sikuzakhala kubera, tinakutulukirani njira zimene mmabera zonsezo zizatsekedwa. Mcp ya chakwera ndi ija ya Tembo ndi zosiyana kwambiri. Chakwera ali ndi team yochangamuka dpp inayesera kuti ibele pama byelections koma zinakanika zizakhalanso chimozimozi 2019 we will be very vigirante.

    2. dpp dont rig elections but has a winning formula. it instills hope to local Malawi. assures people of food security. it promises development and implement what it says.it chooses nice words to speak Malawi. it avoids anger in its politbro ranks.it has mature leaders in its ranks which people from chitipa to nsanje who are trusted by the people. Malawians cant trust somebody who threw the bible down and start politics. impossible

    3. But the same dpp has failed to fulfill its promises thats why it will be voted out. The only strategy dpp has is to rig elections nothing else. Strategy iliyonse akuipanga pano will lead them to lose. Streategy ya mcp nkuwauza anthu ma weaknesses a dpp like corruption, nepotism, kulephera etc. 2014 anthu anavotera dpp chifukwa ankaona ngati izipanga zija inkapanga dpp ya bingu koma ayi ndithu ndi chifukwa chake muzalunzeso. Anthu pano aseguka kumaso adziwa kuti peter mutharika ngolephera he talks alot but fulfills nothing.

    4. dpp promised food security. it promised donor confidence and a return of donors on budget and development funding. it promised single digit inflation .it promised of long term plans like liwonde barrage overhall.it promised Malawians of our oneness thus national ID and inclusion of all people across Malawi in party and government positions.dpp cant fullfill mcp promises.no.it does what its manufesto says

    5. Kkkkk, koma na mcp imandimvetsa chisoni bwanji. masapoter wawo munthu akalowa dpp chimsinamu, kukwiya wagulidwa. munthu akalowa mkachipani kawoko ndiye kakakaka yakeyo. akadzaluza mudzaimvele atibela. iwowo anawina ti aphungu kaya tingati palibe aliyese wa dpp analunkhula zoti mcp mwatibela ai. koma aphungu amene aja adakakhala wa dpp mukanamva phokoso lakelo losaneneka. koma na 2019 ndiye muliladi mpweeee. itakugayani dpp.

    6. DPP won’t win this coming tripatite election no matter how the tricks they may play… anthu adazindikira pano… mumodzi wa anthu omwe adazindikirawo ndineyo… i was voting for dpp in previous elections .. but now i cant vote for these clueless leaders who lack the will to develop Malawi koma busy kutibela ndi kudzilemeretsa okha

Comments are closed.