No civilians in military Super League teams

Advertisement
Nomads vs Silver

Malawi Defence Force (MDF) has told all its Super League teams not to accommodate civilians in their teams.

Nomads vs Silver
No civilians in military.(File)

According to an inside source, a letter about the new policy has been sent to all Super League military teams.

“The letter says all teams should look for players from different barracks and camps in order to beef up their teams,” he said.

Malawi Defence Force has four teams in the elite league of Malawi namely Moyale Barracks, Red Lions, Kamuzu Barracks and Mafco.

 

Advertisement

56 Comments

  1. How Can The Be Civilians Ithought Acivilian Is Signed To Play Amillitary Teanm That Player Undergoes Amillitary Training As Well So After Undergoing That Training Do They Still Remain Civilian???

  2. vuto asilikali amafuna kuti aziwina game yina yiliyose koma ndimakalanyani akaluza avekele we r tranined to kill zikugwilizana pati ndi mpira kkkkkkkkkkkkkkk

  3. Say what???…are killing me u make stupid decisions

  4. But mr spoon better your solders to make their league not to mix with civilians one day will be big problem what happened 19s I hope that you still young or before you to come this world kkkkk

  5. Koma zosewera mu league asilikali ndikuonera kuno KuMalawi basi Maiko Ena kulibe zimenezi amene namva olo kuona Maiko Ena asilikali akulowa mu league chondr andiziwise ,ndipo ngati mwaila zomww zinachithika mmbuyomu muma19s pa Lilongwe Community Ground asilikali a Red lions anayambisa ndeu athabwisidwa njomba ndi Zex Lajabu anthu kuthupha mpanda

    1. 3/4 ya ma team a league yaikulu ku Botswana ndi Achisilikali, ndiyesa kut ku malawi kuno mkumene anawonera zimenexi…….

  6. I totally support this idea. I because the reason of establishing football teams is to make their soldiers physically fit. So why include civilians

  7. koma zabwera ndi namafoloko kaya mukuti supuni zitikumbutsa anthu abwino oupeza achimbayo ndi azawo…anali nawo malamulo izi zapyoza sure….yambitsanidi league yanu muzikapondana ndimajombojombo opanda ma dhindo kuphaziwo…zantiiiii

  8. Good news, but please we are not seeing any help to the national team, we have many Army teams, which are supposed to have strong players, but its the opposite.

  9. Nanga kuthamangitsa ref pa Chitowe chonchija?mukanampeza basitu bwenzi ali kuli chete.Mukhonza kupanga league yanu asilikali

  10. Redlions, Mafco, Kb, Moyale, Chilumba Garrison, Changalume Barracks, Blue Eagles.The Police can form a team from South and North and apply to FAM to form a soldiers league.Mumatiponda inu inde

  11. Chomwe chimandikhumudwitsa kwambiri dziko la Malawi chaka ndi chaka limalemba ntchito asitikali kuti adzisewera mpira mkumawonga ndalama kumawalipira chonsecho m’maboda olowera ndi kutulukira mu dziko lathu mulibe olondera ndiye funso mkumati kodi ntchito ya asitikali ndi kusewera mpira????????

  12. Then Military teams should also have their own military league, Blue Eaglez, Moyale Barracks FC, Cobe Barracks Fc, MDF Marine, Airbon Fc, Mafco Fc etc you must compete on that Military league!

    1. military team must be stoped to play soccer in our country is now time to go and guard our boarder because mozambique soldeirs are busy killing our brothers in mangochi what type of soldeirs wegot there in malawi why soldeirs are busy playing soccer whiles boarders are open for police from mozambique its now time to show this boys their job send them to our boarders for guarding

Comments are closed.