Fifa pats Wanderers on the back

Advertisement
Be Forward Wanderers

Football governing body Fifa has extended congratulatory messages to Be Forward Wanderers for winning the Tnm super league in the 2017/18 season.

Infantino: Has congratulated Wanderers.

In a statement which Malawi24 has seen, Fifa President Gianni Infantino says the Nomads win in 11 years deserves a pat on the back.

‘’This title is the result of the determination of everyone involved and my congratulations to the players, the coach, the administration, the entire technical and medical staff as well as the fans for this great achievement,” says the statement.

The Nomads knew their fate last weekend after a 4-1win over Masters Security.

Advertisement

43 Comments

  1. Adakadziwa afifawo kt ndalama yake nd 15 mita bwenz akugomva chson kmaso adakadzwa kt yathera kwa sing’anga bwenz akuonjenzeran pang’ono cz mutsala ndichikho chabe ndilama mutapatsa Ayaya, Okodza pa Nbs ndi anyamata omenya Amzuni

  2. sha!!!!! koma chi team ichi???? chayamba kale kudziwika ku FIFA? ku likulu lampira, nangano kuli m’mene timenyere CAF? kudziwikako ndie kukafika kumwambatu, ku heaven!!!!!! ha ha ha!

  3. Team yotchuka dziko lonse,nanga uyu watengako lig koma zotelezi kudalibeko,I mean we’re the best in Malawi and no wonder Fifa has recognized us,bullets ilibe club house,maplayer ake amakhalira kugona ndi njala akapitanso ku training amayenda wapansi,how do you expect anything good from such manyaka team

  4. Kkkkk mpaka fifa? Koma team iyi ndi yodziwika ine sindinamvepo kuti kampopi yayamikilidwa ndi fifa itatenga league amadziwa kuti imagula maref

Comments are closed.