Man arrested for rape

Advertisement
Rape Malawi

Nkhatabay Police Station is keeping in custody 29-year-old Gift Mbale for raping a 6-year-old girl.

According to Public Relations Officer for Nkhatabay police Cecilia Mfune, the suspect and the girl’s parents stay at Nkondezi within the district.
On Saturday the rapist found the girl alone at home and he raped her.

Rape Malawi“When the victim’s parents noticed the girl was having difficulties in walking, she revealed the whole incident to them.

“The matter was reported to police and suspect was arrested on Sunday,” said Mfune.
The victim was referred to the hospital where results showed she was raped.

Mbale hails from Mwaluweyu Village, T/A Mwelang’ombe in Karonga District.

He will appear before court to answer the charge of defilement.

Advertisement

57 Comments

  1. Koma zimandivuta kumvesa pankhani yogwilira anayi kodi akazi atichulukirawa ndie kuti simukuwaona??????? Akazi kunjakuno amisinkhu yawo akusowa amuna ndie inu mukusiya amenewo nkumalimbana ndi wanache chichi??????

  2. Kodi kumakhala kuti mumapititsa ngati mkazi kapena pali zina zomwe mumatenga ine sindivetsa please guys tandiuzeni kodi mukuti mwana wa zaka 6 pamachitika chani ,kukhala mwana wanga ngati a police mungadzampeze munthu ameneyo alimoyo ndukaika nditakwirira nthumbirayo kudzalapo nthochi

    1. Aise fra mulungu amapulumusa anthu mwana uja akulira ife timaona ngati wangodwala tinamuuza sister kuti apite naye kuchipatala zonsezo zimachitika ada omwe adamugwililira ali pompo ine ndi mzanga yemwe ndi bambo wa mwanayo tinatalikila titabwelera sister ija inatibitsa inangoti ati mwanayo tipite nayo tonkha mzanga uja atangofika ndi mwanayo achipatala adangoti mwanayi tanena kale kuti amgwililira atangova choncho adamfusa mwanayo ndipomwe amanena kuti gift wamlowesa chinthu kumaliseche kwake atamupasa 50kwacha pompo adatenga mpeni kuyamba kumusakasaka mwamwayi apolice adamgwila tikadali kumyang’anabe ndipomwe adapulumukila

    2. @niko koma zooona ?
      Chomwe ndikunena ndichoti munthuyo ochita zimenezozo amati akugona ndimkazi kapena amakhala akutenga zizimba ,tiyeni tinene zoona mwanayo osatha msinkhu koma kukakamiza kuti alowe

    1. Amwale vani izi kuchoka pomwe zachitikila izi ndi pa bala yoti ili ndi mahule ambirimbiri pali mtunda wa20metres khulupiliani man komanso ada ogwililirao amakonda kucheza ndi mahuleo

  3. Komanso guyz sindine wa chipatala koma kungomuona munthuyo guyz zake zinada kale kale ndikhulupileni timagona nyumba imodzi nthawi zina pamodzi ndi dala yake ya kafanako

  4. AMENEYO NDIYE TIMATI WAGWILILIRA NDIPO I JUDGE HIM PERSONAL HE IS SUPPOSED TO BE IN JAIL FOR 34YEAR’S. NEXT TIME A MALAWI24 MUZALEMBESO ZOLINGANA NDI MISIKHU YA MUNTHU NDISAZAVE KUTI MUKUTI A MAN WAGWILILIRA MWANA WA ZAKA 17 NDIPO AMUPASA MIMBA MWAMUNAYO ALI NDI ZAKA 21 ZOMATIMANGA CHIFUKWA CHOSAVESESANA ZICHEPE

  5. Guyz nkhani imeneyi ndiyoona mwana anagwililidwayo ndiwamzanga chawanagwa phiri ndipo titapita ku police ndi mwanayo gift anavomeladi komanso adao zaka abisa he is 34 or above. Mutha kundifunsa ndikuyankhani

Comments are closed.