Thieves steal Escom cables in Mzuzu

Advertisement
Malawi

Thieves have stolen cables at a transformer in Zolozolo location in Mzuzu.

The incident happened on Sunday night.

According to nearby residents, they saw two vehicles and people in Escom uniforms at the transformer on the night.

Malawi“It was around midnight when we saw two vehicles with people in uniforms, we thought they are Escom officials who come and give us power since the area had no electricity, but surprisingly there was no electricity till morning when we discovered that some things are missing at the transformer,” he said.

Escom officials failed to comment saying the matter is in police hands for investigation.
People are taking advantage of load shedding to vandalize transformers and steal cables.

Two years ago, thieves also stole some copper cables at the same transformer forcing residents to have no power for almost two weeks.

Advertisement

172 Comments

  1. OKUBAWO NAWO ALI PA FB CHONDE MUKAIONA COMMENT MUPITENSO KU MKULA FALLS MUKABE ZOMWE KUNGAKWANISE KUBA ,IFE ZATIKWANA ZOMWE AKUPANGA ANYANI AMENEWA ,

  2. kkkkkk koma nde action yabhotu.
    Kufunika kwberanso mapolo ndi ma wire basi tatopa nazo. Ma powerbank alowe m’bwalo.
    koma kodi kumalawinso kuli escom??? kkkkkk

  3. Vima black out mulengesesa navu My MALAWI lekaso ayamba kukubiyani vipangizo asani monsi mwa EDUCATION chalucho chakutodani kwendesa andipaseni ine ndamthu wabura school ndeyedesepu waka 2 years muwonivo wadichitiyege YESU pawutsongolere wangu nokubayana nochimoloko noblack out love One another like JESUS

  4. I think most of Malawian we are educated savages why comenting well done , good Job to criminals?. Whose tax has been stoled ? When Escom will be purchasing other cable which where do you thing it will come from? Learn to be patriotic and love your country .i cry for my country

  5. Mmmm,,,,not stealing but “taking.”In fact,they r of no public use.Had t bn dat they r of any use,hopefully there couldn’t b blak-outs!! Thumbs up Mzuzu men!!

  6. Zisiru inu anthu obwezeresa chitukuko mmbuyo mnaba ndinu? Ife timavutika ndi mdima anamaliwongwe inu bwanji azakubereni inu kunyumba kwanu ,osati zonse mzitengera ntabwara

  7. achita bwino aba mwina ndalama zamisonkho yathuyo mkumagwira ntchito yoyenerera kumagula ma cable ena kusiyana ndikuti zidzingolowa mmatumba awo abomawo

  8. BT,LL,Zomba and other area please wake up steal more cables of ESCOM so that they must have real excuse for black out

  9. Achita bwino paja kundende masiku ano ndi ku Gelli zowopa kundende ndizakale!!! keep it up! kundende masiku ano ndi konjoyetsa malamulo anakalamba.

  10. Good Idea! Dats Wat We Need For De Sereous Cetzens Nt Escomshit, Let Dem Come Here 2continue Deir Tramendas Work. Proud Of U Thivies

  11. Achita bwino paja kundende masiku ano ndi ku Gelli zowopa kundende ndizakale!!! keep it up! kundende masiku ano ndi konjoyetsa malamulo anakalamba.

  12. Since there no electricity their is no use.sell them to scrap yard.people from north they don’t deserve electricity.

  13. Hahahaha!! I was revisit all the comments posted here but No one is behind Escom so I don’t think Police will take any action! rather than support these thieves!!

  14. Kaili de cables av no live power.there are useless so let them b used by serious citizens. Actually, they are not thieves but rightful owners .unless gotten by foreigners..

  15. since we are the only country without electricity they have seen that its a waste of resources for the cables to be there for nothing. They should even steal the whole mkula……n we are not going to report them.

  16. Ngat muli ndi nambala za mbavazo plix share.,azabeso kuno ku lilongwe ku chilinde A21. Sangayatse magetsi 12:58pm ndikuzimitsa 01:30pm. Just fo 30min. Fon osalowa or ndi 20% yomwe.

    1. And chodabwitsa ine mchoti akungoyendera dzimagalimoto dzabwino a Escom…pamene anthu tikuvutika. Abe ndithu dzimakhebodzo.

  17. kkkkkkkkkkkk achita bwino…akusule makasu ndizidebe…mesa sizikugwila ntchito….thats what i call recycling of product’s

    1. pa nthawi yomwe timakhala tikukoza zina zinthu zina zimaonongekanso. so abawo akukakonzera magetsi ena nde a ESCOM asadandaule kwambiri sinanga zipangizo zimangokhala osagwira ntchito.

Comments are closed.