Mzuni students to join PAC demonstrations

Advertisement
unima fees demos

Students from Mzuzu University (Mzuni) have disclosed that they are to join Public Affairs Committee’s (PAC) peaceful march to show anger over the delayed electoral reforms bills.

Confirming the development, Mzuni students leader Wazamazama Katatu said the students are to march in solidarity with PAC on the electoral reforms bills.

Wazamazama Katatu
Katatu: Has confirmed the development.

Wazamaza said the electoral reforms bills are a lifetime opportunity for citizens of Malawi hence the decision to join PAC.

PAC has set December 13 for nationwide demonstrations on the delay to table the electoral reforms bills.

Churches in Malawi have since mobilized their members to take part in the demonstrations.

Among the electoral reforms advocated by PAC include the controversial 50+1 voting system.

Advertisement

173 Comments

  1. Ana a sukulu nawons ndi nzika za dzulo LA Malawi,amanva kupweteka chimodzimodzi mmene wina aliyense anganvere ngati zinthu sizikuyenda bwino.Thumb up to Mzuni students for making it,you are showing that,you are bonified Malawians who feel pain.You are there to learn so as to understand things deeper and also to have a potential of differentiating Good from bad,go ahead that coming!!!!!!!!

  2. Mzuni has overtaken other universities in malawi. It is now one of the best. Go ahead my school you can contribute to a better change for my country go go go ahead my Mzuni

  3. za ziii izi.andale adzakugwilitsani nchito yopanda malipilo ana inu.aphungu nanuso mupanga boycolt zokambilana mubwelele mumakwanu musamathe allowance ndalama misonkho ya anthu.moti mudzikambilana zamagetsi.mudzidya bill.anthu akukanika kudya zigayo sidzikuyenda.bill yanuyo anthu akumidzi sakuyidziwa so akayambe kuwaphunzitsa Kaye.APA town nawo ndiwochepa. akuziwapo za chinthu ichi.

  4. Idiots inform of students.. fools!. graduates my foot…

    Atleast political science students from chanco or Public administration students….

    Nosense,, demo or no demo nothing will change. If iwere APM onthat day, will tune to live coverage of those demos and the following day hold amass rally just to show them hw foolish the participants of the demos are…

    Kwanyezerera, kumilonde, kunenekude, milale, sakudziwatu kuti 50+1 ndi chani..

    Imet some catholic members of one rural church kkk.. after reading of the nosense paper… amvekere” akuti kaya 50 yatani akuti kaya kuli chani kaya,, ndiye akapanga okha zimenezo” imagine mpingowu uli pa trading center nanga kurural kwenikweni kk.

    Basi kungomva kuti, mcp singawine pawokha mwati koma ma demo… kaye kupanda manyazii

    1. And u think participating in demos its intelligent, let me revisit my dictionery,
      U attend the demos and tell me in 2019 who is mbuli….
      Educated savages.
      Malawi is not in acivil war not are we in any political crisis that can attract the contents of that bill…
      Ambirinu mamina ali lendelende, without reading the contents of the bill. Kkk chikundisekesa ine mchakuti ati pulezidenti azikhala ndi Degree as aminimum… and Iwas looking at graduates of this era, mmmmmm, very few deserve this but the rest mmmm iresponsible ones…

  5. Ana Asukulu Musalowelere Ndale.Ena Muli Kumeneko Ndipo Mumalandira Thandizo Kuchoka Kwa Anthu Ena Akufuna Kwabwino Koma Mwaiwala Zonsezo Mwakwera Pa Nsana Wa Njobvu.NB:Nzanga wina adali mu chaka chachiwiri kupanga maphunziro pa polytechnic.makolo ake ndiosauka ndipo amathandizidwa ndi anthu ena akufuna kwabwino.kukuchitika ma demo pa poly anachita nawo kuiwala komwe akuchokera as aresult adachotsedwa sukulu ndiye inu mwaiwala mudapitira kumeneko

  6. Way to go Mzuni! Chanco students anali kale kuli achina Mwakhwawa.

  7. Hehee mnkokenkoke, 50+1 inkhazikisidwe basi, inu amene mukumati siyambwino, for your own selfish, but for the Nation of Malawi it is good, you have been cheating us for so long tili mu Democracy tiyenera kulankhula, mukunamizila Ndalama for Election, ndipo if need arise for rerun Mind u it’s Government of Malawi Programs and Budgets osati zachipani so u need to see the two Different things, Every political party must be ready to go through the process if things didn’t work in first voting,

  8. Zikafani… Nde bwino ifenso tikumafuna ku univesity ko..zitsiru za ana..akukuphani kumeneko dnt blame government makolo anuwo strait ku pact kwanu konko.. kkkk!!! ka muti Pac ..

  9. How some people are viewing the electoral reform bill is as if it will automatically put Chakwera in power and remove Peter come 2019. Imagine if Chakwera wins the 2019 presidential elections by 50% and Peter gets 35% of the vote and 15% other, a re-run will have to be conducted between Chakwera and Peter thereby making Chakwera and MCP staying out of power longer and providing room for Peter and the DPP to re-organise themselves to overturn the tables. It would take a minimum of 90days to do the re-run not including court injunctions and that would have a major negative impact on the economy as well.

    1. Ine mayesa uchitsiru umachoka ndi mau a aMulingu..koma yayi te..ndaona atsogoleri enawa ndi ntchito chabe..simaitanidwe nkuna utsiru wawowo sukutha kkk

    2. Uwu ndi uchitsiru chabe kwa ine phindu leni leni palibe izi zizangothandiza kuika atsogoleri osayenera mmaudindo “Ziwani ichi 2019 Chakwera sangazapambane ndi 50 + votes and malamulo omwe alipowa akanazamuthandiza iyeyo!

    3. Sense. The electoral policies which are in place now are advantageous to Chakwera. I see mcp members hanging their leader by supporting 50+1

    4. Nkhan siyot chakwera akhale pa udindo ai koma anthu oposa theka adzakhale kut asakha mtsogoleri mmodzi so izi zomat 33%president 67enao kugawana to me its not good

    5. who told you kuti a PAC akuthandiza Chakwera? if this bill is passed it will be there beyond Chakwera and Peturo’s time.

    6. Hey #Abel and #Donton I am only expressing my view. Am not specifically taking sides on the bill but before the bill is passed there must be through consultations and reviews of possible scenarios after an election has happened. Otherwise if this bill is hurried it shall at one point cause serious legal implications in the future. We have so many bills that are being amended now because they were hurried and people were politically emotionally high when pushing for those bills. There is still one full year before the May 2019 elections to thoroughly consult and review the bill.

    7. The issue has more advantages issue of development should not be of bias and other things.The matter is president should be of everybodys choice not 1/4 of the whole Malawi.

    8. It is an important bill for the nation at large but all possible outcomes of an election with such bill in place must be looked into carefully. Imagine in 2019 a presidential candidate gets 45% and the second one gets 39% and for the first time in the history of voting in Malawi you are told you haven’t won the election until you get the 50 + 1%. There is need for more civic education to the masses so they understand the bill so that everybody is mentally prepared to accept the outcome of the elections and being willing to wait for a re-run and being able to accept the results. Political party supporters are usually over zealous and can cause havoc if they don’t understand what the law says in specific situations

    9. It will only take a sensible person to see sense in my argument. I am not against the passing of the bill but it must not be hurried. Even for Chakwera himself the bill might work against him in the 2019 general elections.

  10. Yeah Endeed Aliense Ali Ndi Ufulu Otengapo Gawo Pachilichonse Kma Onsewa Ndiolephera Ndipo Pa 13 Mupite Mukapange Zioneserozo Pa 14 Muzandiuza Kut Mwapindula Chan

  11. Even without mentioning but the truth is that students are also Christians or Muslims. Automatically, they are there on 13th.

  12. So You Want To Join Them, Do You Really Understand Their Intent,Ana Asukulu Musalowelele NdaleMungayambe Kuwona Zokhoma

    1. Remember fanikiso phiri,everson matafale ndi chasowa,pangani za xul guyz ndale xxapangeni patsogolo,mukaphatikiza andale ngoopsya aphwanga mukafa nkhani yanu tidzidzangoivera panyuzi pepala ndithu

  13. Big “why” to MZUNI students; why these students do not learn from the past, it is the north which suffered most during the July 20 demos and other such events in the past? By the way what is in the so called 50+1 that outweighs the problems rocking the country that would be solved by the august house during this sitting? I think they deserve not to be called students, they must be called savages!!!

    1. The problems are available because wina osaziwa tchito yake anabela pa chisankho potengelapo mwayi chifukwa cha kufooka kwa system yomwe ilipo panoyi kuti atizuze amalawi. So we want change now not tomorrow.

  14. 1 of comments that hurts me is when some1 talk bad with northern. Kodi mwayiwala kuti any change of gud starts from north.

  15. ndipo tisawasiyesiye amenewa,akumationela munkodi.Tiyeni tonse tigwirane manja pa 13 pano

  16. Tikamakhala ndi matha palibe chomwe chidzasithe dziko lathu, ufulu omwe tikuupedza lelowu ndi xoti ena anamenyela khondo ndipo anafa, chovuta ndi cani ifeso kupanga chimodzi modzi kusiyana ndi kuti dziko lathu lionengeke,tiyeni tichose matha gyz tipange umodzi usaopa boma ndi athu timatelo tili komko

    1. Lolani mwanzi wanga ukhale fuel osendesela dzikoli Sindizalola kuti ndikhale chete kuli bwino kumwalila kusiya ndi kukhala moyo wautali wauchisilu opanda mphindu

  17. Ana opusa mukakafako zanu. Winawe makolo ako akukupasa feez movutikira ndikumapanganso nyasi zakozo, uzawabwezera chani, mmalo mopanga tsogolo lako

    1. It’s not that they have forgotten what they went for but they are being patriotic and exercising their democratic right

    2. A Stan sukulankhula bwino….atleast they are concerned about the future of this country which they must stay and work after their varsity

    3. @ Stanzio you are a pathetic lot! Is that coming from a patriotic Malawian? The problem of supporting parties without seeing and understanding is that!

    1. ana othawa mkondomu awa ongobadwa mwangozi zolemba zawonso zimakhala zangozi…akanadziwa makolowo akanangonyengana puleni ukanabadwa wa nzeru

    2. Abraham Bandah ngopepera uyu osalimbana naye.

      Mtati muone ma photo ake mutha kudziwa kuti munthuyu ngosokonekera.

      Munthu zoona nkhope kunyezimira ngati wadzola Covo or brake fluid

    1. yr government shame on you, mpaka someone can stand and say my government hahahahahha mbava zokhazokha olo manyazi mulibe just imagine kukaba ndalama za makhwala, chimanga, za escom, zama water board eish

    1. Amwene Kumalikonda Dziko Lanu Osamngoti Chilichonse Kutengeka Ayi Kapena Kuthamangira Kuphwanya Zinthu,chifukwa Mukaononga Zinthu Za Anthu Ovutika Ndi Anthu Komanso President Malo Mokonza Mavuto Athu Akhala Akukonza Zinthu Za Anthu Zomwe Zaonongeka Komanso Kumakhala Kubwezeretsa Chitukuko Mmbuyo Kwa Anthu Opanga Malonda Chifukwa Kuti Business Kuti Ikule Ndiye Kuti Panali Ndalama

    1. So you are trying to tell me that ku Chancellor college, polytechnic, bunda college have the students from the southern region and central region respectively

    2. People dont know why these are public institutions.The fact that its in the northern region doesnt mean its for the Tumbukas. It is for all Malawians

    3. Somebody is trying to misunderstand my question.This is in response to a comment by a certain man whose thought is that students at Mzuni are all Tumbukas.Iam so sorry iam not a cadet and never shall I be.Search me please

    4. Mkuzingwa Yohane you can tell the intelligence of someone by their failure to grasp the meaning behind such an easy comment you have posted above haha

    1. Why are you saying afera za eni? Malawi is a democratic country and our constitution clearly states that we have a right to hold peaceful demonstrations this premitive mind of the one party rule where people are killed for no reason we won’t accept it

Comments are closed.